nanga imfa ya chasowa,issa njauju,imfa za ma alubino,imfa ya banja la anthu angapo aja anafa nyumba yawo itayatsidwa itathiridwa petulo,anamapopa ku Mulanje,anthu anawomberedwa ku mzuzu,adzaulula liti apm wanuyo?papita zaka zingati chichitikireni zonsezi ,nawo abale awo a anthuwa akufuna adziwe.namagwelu ndi chipikuman wonse anjatidwe for crimes against humanity.same same basi
Aaaaa Mary sanapemphe Boma lilionse wapempha a Malawi okhuzidwa bwanji kodi utm my vot❤❤❤
Aaaaaa zipan mwatikwana kod simugamakapembe za mene mudzayenderetsere mboma
Ndipo zowona chilungamo chizaziwika ndipo tizafinya
Namu bwana chikangawa azafele kundende
Kodi imfa ya chilima yasanduka compain. Kodi DPP IDZAwina ndikudzangofufuza ndege . Palibe chilipo apa mwanama. Pangani ina..😂😂😂
Apita oyeeeeeeeeeeeeeeeee ❤
APM 🔥🔥🔥🔥🔥💙 2025 Kuli ntchito
Àpm my vote 💙
APM my vote
My vote ❤❤❤
My vote❤
Zoona
Mbuzi za wanthu izi akakuvotelan ni agogo ako pakhos panu ni muthalika emweyo
❤❤🧘🧘
Kamba mfundo zogwilika kwa Malawi
Video yi kumapetoku siyikumvekatu mau
Isaa Njaunju ifayawo Inu a Dpp simudanene mpakana pano. Boma ndilomweli
Iwe panya pabambo ako
Mcp chipani cha tinteen
A DPP si anthunso abwino ndipo ali ngt a MCP omwewo
Chilungamo chake chiti
Nyekhwe ilipo ku mcp
Za issah njaunju bwanji
My vote peter
Wayamba liti ?
Uko
nanga imfa ya chasowa,issa njauju,imfa za ma alubino,imfa ya banja la anthu angapo aja anafa nyumba yawo itayatsidwa itathiridwa petulo,anamapopa ku Mulanje,anthu anawomberedwa ku mzuzu,adzaulula liti apm wanuyo?papita zaka zingati chichitikireni zonsezi ,nawo abale awo a anthuwa akufuna adziwe.namagwelu ndi chipikuman wonse anjatidwe for crimes against humanity.same same basi