Kodi ntchito yofufuza anthu opanga chipongwe ndi ndani kodi anthu anagenda galimoto ya president kunapita president kukaloza anthu omwe anamugenda koma mfundo zinazi
Wabodza uyu awa a mcp zinthu amayakhura okha, koma nso. pamawa nkhani yomweyi za amanthanso kukana awa alibe chilungamo or pangono kay amapemphera kay za malemu chilima bwanji. anapha okha koma amakana
Nanga why galimoto yomwe anagwiritsa ntchito mwini wake ndi WA MCP?
Awa amayamkhla izi akakhala pa camera kom kumbaliko amatuma anyamata azikasokoneza, sangakaneso ai ma audio tilinao
Iwe ndwe munthu wabodza chimwedo Banda unazolowera mabodza galu iwe
Mutu ngati papaya
Chimwendo iweyo ngati sumatamba chilipo chilipo paja mwatchuka ndi kunamiza a malawi ndiye utulutse umboni osonyeza kuti chisale adakuimbira phone kmso iyeyo akudziwa za pa mbowe galimoto inali ya member wa mcp imene anakwera okhapa anthu mwangoyaluka za chilima sitinaiwale .
Achimwendo ndinu chitsiru kwambiri lwe mesa ndamene ukumatuma anyamata kut azimenya anthu
KOMA NDE ZAFIKA POTOPESA BWANJI,ZAKWANA.TIKHALIRA ZIMENEZI BASI MOTI TIZIMVA MFUNDO ZENIZENI
Kodi iwe Chimwendo kupanda nzeru bwanji, olo atakhala kut amapanga a DPP okhaokha ndie police ngat Boma bwanji sakuagwira omwe amapangawo popeza ndi ntchito yawo.
Ndipo ndangoononga data yanga kumvera fundo zopeperazi
Iweyo ndie oyipa kwambiri chimwedo banda umatuma anthu kupweteka anthu azikwanje galu iwe
Nanga zikwanje za a dpp zija?
Norman chisale ndi wa bwino?
Mmmm akuru mulungu akukhululukireni
Chimwendo wabodza iwe muyaluka inuu
Nthawi yatha chimwendo
Ife tikufuna report la ndege osati zanuzo mukuziwana Dpp mboma bas
Iwe ndi chitsilu kwambili chimwendo banda dikila a Norman akuyankha
Tikufuna report ife musanamizile chisale apa
Kalembeni
Bwanji a police sanagwile athuwo kape iwe
Ife tikufuna za report nkhondo inayamba kale kuno kumalawi
Nanga achipani Cha Afford nawonso anachitidwa chipongwe ndi a DPP?
Inuyo nkukhala kwanu kukana pa zinthu zachionekere.
Mmesa munankanso Chilima zokhudza mgwirizano kuti palibepo mgwirizano wina ulionse omwe mudasainirana
Koma ndi Po Inuyo afiti awa
Mawu amapita kwa IG oyankha akuyankha a Chimwendo.
Chipani cha nkhanza
Anthu mupwetekana inu chilungamo Kwaaliyese ngt Mungokanirana simuphana😅
Mutuwu wangokula mzeru alibe
Eeeeeish achimwendo ngati ufiti alibe ndakayika
Cha Richard Banda chopusa kwambili
Kodi lwe wamkulu mutu lwe ndi I G
😂😂😂😂
Ndakamba zoveka bwlno ukunamatu zakozo
Chimwendo mapwalako ndithu iwe
Koma iyiiiii ndi mbuli machende amako
Anthu mukungoti ndichisiru komanso ndiwabodza chosecho munthu wanena kuti bweretsani mayina aanthu..Munthu opanda mfundo komanso wabodza amathamangira kutukwana kapena kulira chifukwa amakhala kuti alibe chonena...come up with ur point not kutukwana....
Kodi ukutchatchalika bwanjii
Bwanjii osachita zimenezo pa lmfa ya President wathu Chilima
aChisale akupempha Apolisi kuti agwile anchito, Spokesperson waPolisi asanduka Chimwendo
Kalikonse tikawona
Zandale osagwilitsa dzelu zachibadwidwe ukhoza kuzitengela ndale ndi game 🎮 yauchikape kt uzitengele ukhoza kuzelezekapo chabe
Chimwendo osagodwala kenako kufapo tipume kupusisa kwakeko anayenera kufa Mulungu akanayankha malawi Ali pamavuto chifukwa chameneyuyu
Iwe chimwendo nthawi yonse ija sumanena bwanji waona kuti zafika povuta nde wayamba mabodza, zikusalira uona plus chikangawa uko zikudikila iwe
Aaaa MCP uchisilu uyi
Kodi ntchito yofufuza anthu opanga chipongwe ndi ndani kodi anthu anagenda galimoto ya president kunapita president kukaloza anthu omwe anamugenda koma mfundo zinazi
Kodi aChimwendo mwayiwala kuti munamugenda APM kuNdirande??
Waonekera poyera wa Inkata coz ngakhale 2019 unali owotcha matayala mmisewu
Galu chimutu
Iwe chimwendo panyero pako anthu amene akakhape anzawo pambowe anali a MCP iwe chitsiru chodzadzamamina nkati
Chimwendo wangokula chimutu chakocho koma mzeru ulibe anankhumwa achani galu iwe
Koma Ngati Boma sitikuyenela kulekelela Kuti anthu okha adzimenyana police imayenela Ku chita kathu
Uyu mumati chimwendo amawoneka kuti ndiwochenjera
Koma anyamata anu adzawona maloza
ine ngat mmalawi ndikuona mbali zose kulibeko fundo akungonyozana bas amalawi tili pa vuto mwina kubwele a nyuwani osat kumene tadusaku ndi izi lelo
Wabodza uyu awa a mcp zinthu amayakhura okha, koma nso. pamawa nkhani yomweyi za amanthanso kukana awa alibe chilungamo or pangono kay amapemphera kay za malemu chilima bwanji. anapha okha koma amakana
Mmmmmmmmm Mesa munatchingira panjira and zinatengera chisare kuonesa ukadauro .
Tikufuna report la ndenge ife osati za Achisalezo ife
Kodi iwe umaziona ngati ndani muziko La Malawi umaona ngati dziko ndi LA amai Ako umadabwisa ikubwela nthawi uziona chimwendo
Muthu opusa kwambili chimuthu ngat pwala ranjovu
Chimwendo Banda boza chimutu kukula🤣
Uyu asamulidwe ponena kuti DPP idaotcha a Tambala
Apa nde kuyakha kma za ifa ya chilima osayakha. Chisilu cha muthu.
Ndiye ngati anali onkhaonkha amene anayambisawo osawagwila bwanji olo ali a DPP
Chimutu eti kuyakhula moputsa chifamba chachikulu iwe
Park and go your time is over chimwendo
Koma nkhani ndiyoti anakuuzani kuti yadzadza ndindani ndiye zimene tikufuna kumva apapa
Umboni okuti achisale anakukumburani phone urikuti?
Achimwendo kumeneko sikuchenjela ndikupusa
Umazitenga Ngati ndi iwe dolotu komano one day is one day
Youre very fair in this channel
Nanga anachepa uja bwanji anthu anawatchura police inachitapo chani
Atu awaw ND oipa kd mulung osawalang buanj
Koma achimwendo mukamayakhula muziziwa kut kuli mawa
Chimwendo Banda ulibe humanity
Ma cadet ma cadet kkkkkk ndinu osekesa mukufuna ndeu
Apa obanda mwayankhurako zabwinoko🙏🙏
Ambuye bwerani muweludze dziko lanuli
Kodi anthu akavulazana okhaokha samangidwa
Boza ili ,, iwe Chimwendo panyopako
Ndewu imayamba chocho ife o vota tili pheee
Ngati anakhapana wokha wokha agwireni anthuwo
Ngati anali a DPP bwanji osawamanga?
Taona macomment Chimwendo Banda
Chmwando ndi munthu wamboza
Ndege inagwa chifukwa chani 😢?
His time is near chileg
Chimwendo panyelo pako
Apanika awa.ayankhe za ndege awa..
Mayoopp data yanga ine😢
😂😂😂😂 koma dziko ili eeeee
Chimwendo wa boza iwe ,,,
😂😂😂😂 ndilibe lawyer
Alani witika
Kuyankhula ngat munthutu
Mwapha bwanji chilima
Mutu ngati vembe
Kodi mukuopana
Adah wa nzeru alibe
Mfiti
Milomo yonyasayo
Ndalee anakonzaa
Bodza
Mayina achoka kuti Mesa anyamata anu anathawa