Thanks bosses stay safe and warm continue with the good analysis of data collection I hope the these videos reaches the president so that they can become a turning point into practical mind set change on actual development Continue with these
koma nkhani yolimbana ndi obwelayo sinkhani yabwino,tiyeni tikondane ngati tonse tili ndi red blood cells ngati achakwela muli ndi connection yopangila nkhaza obwela from Ruanda please khalidwe limwnwli silothandiza mukanasintha
Chakwela mmutu mopanda nzelu south Africa ikupita pa sogolo chifukwa cha anthu obwela muzapite ku bellvell ku capetown amalawi azazako kugulisa tomato kuotcha nyama ndi zina za mbili munangotengela boma msanje mmutu mopanda nzelu
Kagame walitola dziko lathu ndi boma la chakwela mpaka kulowa asilikali achilendo kumanda malawi inazolowela kupempheza mafano esh amalawi made mistakes to voted congress party chipani chanyazi
Our main challenge is Bakili muluzi here .. akungolekelera anamupanga bribe ..tikuvutika freedom that he gave to us akungoyang'anira wina wake akutizuza
Brother don't worry, the spirit of God show me a vision that chakwera and chilima their leadership is over! Dk is coming in next election he will change Malawi for better.
azikhale alindivuto ngati zinthu zikutelo nanga anthu athawila kuti sibwino kungopanga zokomela munthu modzi bwanji akanakhala ndi iwo ali kumozambiki ndiye anthu aziwatelo so sad. zipani zinazi ndiye ayi bola dzana lija timadandaula za kudala kwa zinthu ndi mafuta osati zopusa zoika moyo wa anthu ena pachiswe ayi.
Ndikuganiza kut emission imeneyi sichotsedwanso pa youtube. Pali emission yinayake pa nkhaniyi yamalefujizi imene inachotsedwa. Sikupezekanso ndithu!! Fortunately, anthu anaipanga kale download before being removed!!
Malefujizi anakhana kuaphatsa ndalama makadete aKagame chifukwa ndalamayo ndi imene boma la Kagame limagwilitsa nchito kubwelanso kuzunza malefujizi. Refugees think that by giving money to the government of Rwanda, they are financing themselves actions of destabilizing refugees!! That is why they always refuse these acts!!
😭😭😭😭...ife monga a malawi tonsefe ndife athu opusa kwambili ndipo tilibe nzeru or pang'ono athu inu munkampanga mademo ku DPP 2019 mpaka kutseka misewu kuti peter muthalika asaduse kulibwanji mademo omwe aja mutawabwelezaso kuti satano-yo achoke pampandopo kapena tinene kuti ulamuliro wake wa satana-yu ukukusangalasani bwanji mwangoti ziiiii or mademo ayiii tawonani satana-yi mene akumawaphera athu osalakwa sizama refugees okha ayii even a malawi akufu simasewe tawonani njala zithu mene zikukwelera tsiku ndi tsiku koma iyee sizikumukhudza aliduuu basi chimutu thasalala kuma office-ko😢😢😢.. sindikudziwa ngati kuti ma video's Anu ndi ma comment awathu amawafikila koma ngati nkutelo ine ndikuti iwe chakwera panya pako pamodzi ndi nduna zako zonse,,ndipo ine ndine muthu modzi amene sindimakufunira zabwino pa moyo wanga ayiii ndipo sindimafuna even nditava dzina lako likutchulidwa near by me ndipo ndimangolaka laka kuti mulungu atangobwela ngati tsiku la lero kuti adzachitenge chitsilu chukula mutu ngati matako a mayi ake atangochiponyera pakati pa moto kuti chipyi chi nfiti ngati chimenechi fuck you chakwera....😭😭😭😭😭
Thanks bosses stay safe and warm continue with the good analysis of data collection I hope the these videos reaches the president so that they can become a turning point into practical mind set change on actual development
Continue with these
Thank you very much bro 🙏🙏👊👊!! Umakwana ndithu!! Umafufuza kwambiri!!
koma nkhani yolimbana ndi obwelayo sinkhani yabwino,tiyeni tikondane ngati tonse tili ndi red blood cells
ngati achakwela muli ndi connection yopangila nkhaza obwela from Ruanda please khalidwe limwnwli silothandiza mukanasintha
Give them citizenship cz they need to stay in peace thank u
Ur de 1 👌big boss💥💥
Thank you bg mn respect ndawi zonse appreciate your intelligent sir
Live live 🔥🔥🔥
Reality exposure
Mmatimvetsa kukoma but mumatisiya mmalere....mmangosiya kulakhula osasazika
I need to see you face face brother u r the best guy
Bakili tv u r a legend
Ndalama ikuononga dziko lathu
Tiwapemphelere ma refugees
Keep up brother manyazi amugwila chakwela
Who burned Quran in Sweden 🇸🇪 give us updates
God provide this channel Aman.
Inu ndiye number one basi kwa history
Makwana
Chakwela Ndi mbuziiiii yomwa Madzi ometela NDEVU,iye akuti waipeza nzake nkunena Kagame.That's why akumawapatsa ndalama ma Bulutuuuuuuuu ena kuti azisokoneza DPP Bwantasaaaa Nyawu Gule wankulu kwawooooo.Agalu inu muziwanso pa 2025
Kaaya🤔
Musaiwale kut ndi MCP olomutaiwuza mutavula pant singamve ndipo ndiyosamva
Respect brother man❤❤❤❤
Ulamuliro umenewu ukapitirira ndiye kuti kuMalawi kudzabwera revolution and Iwill be one of them. We are tired of this nonsense now.
That's true
Timakunyadilani big man
Kulankhula momveka bwino bro big up keep it up be safe
Vuto la Malawi timatengeka ndizirizonse zimenezi tikuvutika ndiife osati a president Thanks for your information
You are doing grt job Mr man, keep it up
Ngakhale Ku South Africa ma foreigners ndi omwe akupanga zitukuko
You are saying Truth brother 👍👍🇲🇼 🇲🇼
Koma kanyoni analakwanji guys 😢🥺😭
Chanel No 01 here in Malawi
Salute to our own explorer yool
A best analyst
Chakwela mmutu mopanda nzelu south Africa ikupita pa sogolo chifukwa cha anthu obwela muzapite ku bellvell ku capetown amalawi azazako kugulisa tomato kuotcha nyama ndi zina za mbili munangotengela boma msanje mmutu mopanda nzelu
Kagame walitola dziko lathu ndi boma la chakwela mpaka kulowa asilikali achilendo kumanda malawi inazolowela kupempheza mafano esh amalawi made mistakes to voted congress party chipani chanyazi
Thanks bro
Never give up bro
I learn a lot from you broh.keep it up
Mulungu azikutetezani brother
👏👍2much jzy MW wa2.Brah taday you most am appreciate 2.
BIG 👍
You are doing great job
Mulungu achite nawo azikhale ng'oma pamodzi ndi chakwera
Ayi bakili tv palibenso😮😮Ingwileni ntchito bwana
Anthuwa ndichimodzi mozi Ife muyisiye free
Nduna imeneyi ikufunika imangidwe chilungamo chiwoneke ndi chigawenga chachikulu
Chakwala usatinyatse
Ine ndimafuna anthu angati inuyo muzilowa ndale mukhoza kutithandiza E.g Manganya akugwila ntchito kuposa chilima nd chakwela pano.
Thanks to give us history God bless you
Am agree with u y bakili muluzi is quiet ? He is the one who bring democracy but he is quiet y
Well articulated sir.
Mumakwana big man !!
Idi amin criterion all the time, for example raising texes
Chakwera needs God to deliver him from evil spirit
Our main challenge is Bakili muluzi here .. akungolekelera anamupanga bribe ..tikuvutika freedom that he gave to us akungoyang'anira wina wake akutizuza
Following
Yonse madala madala keep it up 💕💕💕
Nkhaniyo ndiyowona bro munthu wakuda kuzuzika mu thaka ya mu Africa
Awesome bro
Ambuye atithandize akanyoni komwe Aliko awoneni Maka chitetezo chamoyo
Komaso mutiuzereko kwa Chakwerayo kuti kampeni si yopangira ku msikiti
mumakwana big man from here Dubai
Chakwera ndi Zikhale ng'oma ndiwanthu osafunika m'dziko lamalawi anthu achabechabe
Kkkkm😂 indeed chakwera nd nd young brother of id amin 😂😂
Ndinu mbambande brother
Ndunayanu ulibe zeru akupangisa kuti bomayambeso kumatingeira kuno akuwona zimene mukuchita kumeneko
Brother don't worry, the spirit of God show me a vision that chakwera and chilima their leadership is over! Dk is coming in next election he will change Malawi for better.
I like you bro ndipo a Malawi ife nde tili dallow koopsa
First to comment
Well spoken, wokuda ndi wokuda ma burundi akuzuzika mu nthaka yawo fukwa cha zoba uyu opembeza azungu he doesn't deserve to be called a brother
azikhale alindivuto ngati zinthu zikutelo nanga anthu athawila kuti sibwino kungopanga zokomela munthu modzi bwanji akanakhala ndi iwo ali kumozambiki ndiye anthu aziwatelo so sad. zipani zinazi ndiye ayi bola dzana lija timadandaula za kudala kwa zinthu ndi mafuta osati zopusa zoika moyo wa anthu ena pachiswe ayi.
Mbale zikhale ngoma, please siyani kudzudza anthu otsalakwa, mwabera ndalama yokwana 6milion, lero mukuwadzudza is it fair, mulungu akuone pamodzi ndi chakwera anthu oipa inu, mulozedwe mudzakapangitse mnsokhano kwa goliati mudzaonanso ndalama zonse zomwe mwaba mudzadzitsandza, chakwera munthu woipa iwe
malawi is now lankin as a 3rd poor country in the world. poor governance, jelousy, oppression are indeed some of the factors that are killling malawi
Bakiri muluzi ndi number one
Kodi Mr Michael Sauka yemwe anapeka Nyimbo yafukolathu,kwao kudalikuti???..ai ndithu Big timadziwa zambiri kwainu ndi fire!!!!!
Komanso nkhanza (nkhanza ndi katangale)
Achakwela alephela kusunga dziko alichaba pa business yakumba ndala za amalawi
Umphawi pamodzi ndi nsanje ndizomwe za manga bomali kotero bomali silikufunikanso term inayo.
Only God knows 🙏
Ati kungopita kunja kukapanga za umasikini😂😂
Nakha bwanji ndi takhala ine/inuyo mungave bwanji kuti ndinu refugees
Akaka naneso kandiseketsa nde anachita kutsindikiza 🤣🤣🤣🤣
Keep on updating bro mumatiimirira tikuchapika mmutu bro a Malawi these pple they are propagandas the (tonse).
Uyu chakwera atipwetekesa
chilungamo ndichimene mukuyqngula ulemu wanu bro
Chilungamo chake
Ndikuganiza kut emission imeneyi sichotsedwanso pa youtube. Pali emission yinayake pa nkhaniyi yamalefujizi imene inachotsedwa. Sikupezekanso ndithu!! Fortunately, anthu anaipanga kale download before being removed!!
Zikomo kwambiri big man
Azikhale matama komanso kuipa mtima
Munachita mademo omuchotsa presdent yemwe amapangitsa zinthu kuti zizitchipa. Lero mukulira koma mukulephera kumuchotsa.
Akulu inu muyenera kukhala president ndithu
Mulungu akudaliseni amwene
Koma ku malawi eeeeee ndilibe nako mau
Only God have mercy on us
Inu ndawakulu ndipo Chanel yanu ndi 1
Kom ziko lanthu ndilomvesa chisoni kwambili, akupanga nsanje ndi ma frica azawo osati anthu a pink wa eshiiii so sad 😏😏😏☺☺
Continue kutipatsira nkhani❤
Boma ili latitopetsa lizipita laononga dziko lathu,tonse alliance boma la nkhaza
Zikomo kwambiri Big,
Koma titani kuti zithu mukunenazi zitheke kwathu kuno
Pokha pot tili amphawi kamba ka jealous ndi zoona100%
Malefujizi anakhana kuaphatsa ndalama makadete aKagame chifukwa ndalamayo ndi imene boma la Kagame limagwilitsa nchito kubwelanso kuzunza malefujizi. Refugees think that by giving money to the government of Rwanda, they are financing themselves actions of destabilizing refugees!! That is why they always refuse these acts!!
😭😭😭😭...ife monga a malawi tonsefe ndife athu opusa kwambili ndipo tilibe nzeru or pang'ono athu inu munkampanga mademo ku DPP 2019 mpaka kutseka misewu kuti peter muthalika asaduse kulibwanji mademo omwe aja mutawabwelezaso kuti satano-yo achoke pampandopo kapena tinene kuti ulamuliro wake wa satana-yu ukukusangalasani bwanji mwangoti ziiiii or mademo ayiii tawonani satana-yi mene akumawaphera athu osalakwa sizama refugees okha ayii even a malawi akufu simasewe tawonani njala zithu mene zikukwelera tsiku ndi tsiku koma iyee sizikumukhudza aliduuu basi chimutu thasalala kuma office-ko😢😢😢.. sindikudziwa ngati kuti ma video's Anu ndi ma comment awathu amawafikila koma ngati nkutelo ine ndikuti iwe chakwera panya pako pamodzi ndi nduna zako zonse,,ndipo ine ndine muthu modzi amene sindimakufunira zabwino pa moyo wanga ayiii ndipo sindimafuna even nditava dzina lako likutchulidwa near by me ndipo ndimangolaka laka kuti mulungu atangobwela ngati tsiku la lero kuti adzachitenge chitsilu chukula mutu ngati matako a mayi ake atangochiponyera pakati pa moto kuti chipyi chi nfiti ngati chimenechi fuck you chakwera....😭😭😭😭😭
eti amalawi angoti ziii or mademo
man ukafuna kuziwa kut ndiwo izi mlisabola timalawa
Pipo timuoempherere kanyon zazikulu zichitika
MCP kwawo kapande 2025
Kagameyu muzandtsmkzra tsku lina kt azamuukle kagameyu nd asilikali ake omwe. Kunali omar al bashir
Koma ine ndikamamva izi mtima kupweteka zedi kodi zimachende zaku mpandozi bwanji nkhaza chonchi ambuye chonde zulani mitima yawo