Kod abwana bwanji osapanga press conference anthu tikuziwine you are like professor lumumba 'you talk 👄 reality without fear 😨 and favor your words are full of wisdom
Mr. Ur number one, vuto anthu ena amangofuna kusokoneza zinthu so ngati akufuna kuti peter azigwilisa ndalama zake nanga mau oti sichipani chake akubwelera pati. chifukwa akudalira ndalama yake Dausi ndinamumva pa Times koma zomwe ankalankhulazo mmmmm zaudani basi
Your are saying the truth brother we need to change the party should be for all 😢 member who are at nec to contribute and surpot The party because they are one of the benefits res okay
Koma kunena zoona interview ya Dausi ndi Brian Dausi ananena kuti APM asayime komano ananena kuti dongosolo lake silinayende ngati mmene chipani chimayenela kuchita ndipo kumapeto ananena kuti alibe vuto ndi APM koma ngati ndi Democracy aperekenso mwayi kwathu ena kaya adzaina APM iye adza support kodi ku DPP kulibeko anthu ena ofuna kupikisana nawo sindikusapota ndausi koma ndimmene ndinamvela pa interview yake
Very interesting Namkhumwa is failing to stand firm in the Parliament as leader of Opposition but he wants to be reader of Opposition in his own party. Koma ndizidabwitsa bwanji he can win
Komanso adausi akuziwa zambiri zakuphedwa kwamalubinho ndioo adausi ndi nankhumwa komanso Ben botolo anapha alubino uja waku nkhatabay Mr makwenda phiri ndioo adausi ndi tim ya apm yomweyo mulamulilo wao akuziwa adausi kuti zao zidada ku dpp alibe chance
Bola munthalikayo.Awo asatiputsitse ndimbava zosakhutitsika ayi.Kulibe zimenezo.Iwe tokota osawopa ife umatitokotela history mopeleka chidwi and umakhala ndi maumboni okwanila.
Ubwino wake ife Sitikufuna APM Atibekekere Mwana 😅 Tikufuna Ntchito Zake zibwelere, Osat Wakura Wakura Wakalamba Ngat Akapanga chinkhoswe Ndi Mwana wa 2000
Dausi asapangetu zachibwana ife tili pa mbuyo pa APM ❤❤
Enanu ngati mukuona kuti zimene akukamba sizikukusangalatsani bas siyan kuvera zokamba zake mukasiya mmalo mwainu apezeka athu 10+ okonda chanel imeneyi
nice answer man
Yes eti MUNTHU OKUTI sizimakusangalatsa koma osadiya kumangolankhulabe haaaaa umbuli CHANI???
Kod abwana bwanji osapanga press conference anthu tikuziwine you are like professor lumumba 'you talk 👄 reality without fear 😨 and favor your words are full of wisdom
Ndipo we need to know him mweee😂😂 I can't stop liking this guy
This guy always says only the truth keep it brother
Apa zanveka bwino tsopano inuyo mumatithandizatu.. ndipo piter ndiwanzeru kwambili
Exactly BG. On point you never disappointed us respect to you bro
y_
Good job and well articulated❤
Zomveka mvemvemve ndithu.
Adad woyeeee
Ife tikufuna apm bas ❤❤❤
Great mind.May God bless you bro
Zoti mcp imadalira chuma cha Kamuzu wanama mkulu iwe
Akunamadi, nkuluyi ndi wa DPP
Nkhani yabwino koma adad ayimeso basi nde zomwe tikufuna
Apapa tadziwa chilungamo chifukwa dausi amaoneka ngat ali pa chilungamo chifukwa chakudziwa kuyakhula
Mmatisegula maso bro..keep it up
APM akuyenera kuyima basi enawa apeze zochita Dausi Nd zizingu zake zija akakhale pansi anthu osafunira zabwino dziko anthu oyipa
Mr. Ur number one, vuto anthu ena amangofuna kusokoneza zinthu so ngati akufuna kuti peter azigwilisa ndalama zake nanga mau oti sichipani chake akubwelera pati. chifukwa akudalira ndalama yake Dausi ndinamumva pa Times koma zomwe ankalankhulazo mmmmm zaudani basi
This guy is agreat guy i
Mwini Channel iyi amatha kutambasula nkhani please ndilankhuleni pa Email yangayo ndizikupanga Support uli Ndi Luso kwambiri kumayamika ndibwino
Ndipo live
Big man inuyo🎉🎉
Its the narrators voice for me mawu a ndiiiiii😅😅
Chikamati "Eeeeeh! Mkudziwa inu"😂 ine kumtima myaa
Kuswa kuswa bro
HRDC ikuopa ndipo anyani ameneo azaziona
Thanks for the video a good one boss
Your are saying the truth brother we need to change the party should be for all 😢 member who are at nec to contribute and surpot The party because they are one of the benefits res okay
Akumuwopa APM komaso achina nankhumwa alembedwa ganyu
No fear no fever straight to point ❤
Koma kunena zoona interview ya Dausi ndi Brian Dausi ananena kuti APM asayime komano ananena kuti dongosolo lake silinayende ngati mmene chipani chimayenela kuchita ndipo kumapeto ananena kuti alibe vuto ndi APM koma ngati ndi Democracy aperekenso mwayi kwathu ena kaya adzaina APM iye adza support kodi ku DPP kulibeko anthu ena ofuna kupikisana nawo sindikusapota ndausi koma ndimmene ndinamvela pa interview yake
2010 bwanji sanapereke mwayi kwa Joyce Banda? 2018 sanapereke mwayi kwa Chilima. Lero chifukwa apanga endorse ndi anzake basi kuyamba kulira?
Ngati unamvera interview ananena kuti membership card isakhalepo kusonyeza kuti anthu asamasonkhe chipani chizithandizidwabe ndi Mutharika
Daus ndiamzake akufuna kusokoneza chipani, adad omweo
Dausi ndi Nankhumwa ndi anthu osokoneza kwambiri, we are tired with them
Best chanel pa dziko lapansi pano
Dausi sakulakwisa
Never give up ❤
Apa mwayankhula zoona Bro ,,, Nankhumwa ndi Dausi kunena chilungamo akusokoneza chipani
Good message Bakili Tv ❤
APM emweyo
Let Peter Munthalika to stand l support him forever
Very interesting Namkhumwa is failing to stand firm in the Parliament as leader of Opposition but he wants to be reader of Opposition in his own party. Koma ndizidabwitsa bwanji he can win
Mumakwana Mr BM tv
I will never disappoint you sir
Powerful as well
Paja awa nga dpp
Anankumwa nd Dausi ngati akuzimva ndalama angotuluka bas ayambise chipani chawo vuto palibe ife zatikwana☹️☹️☹️
Komanso adausi akuziwa zambiri zakuphedwa kwamalubinho ndioo adausi ndi nankhumwa komanso Ben botolo anapha alubino uja waku nkhatabay Mr makwenda phiri ndioo adausi ndi tim ya apm yomweyo mulamulilo wao akuziwa adausi kuti zao zidada ku dpp alibe chance
Vuto lake Chilungamo Chinayandikana Ndi Mabi😮 Dausi Ayambitse Chake Basi
Jealous nde vuto lalikulu mmalawi 😂😂😂
Analysis yanu ya nkhani za Ku Malawi kuno mumakhala ndi mbali....
100% agree with you man
You are always right bro, dpp for life ndipo nankhumwa, botman ndi dausi ndi osokonedxa we know
Dausi ndi mbuli yazinthu sadziwa ntchito ndipongasanje safuna anzao kuti azimveka Ali .ngati Symon vuwa Kaunda komanso khumbo kachali Sanji twoo much
HRDC instead of fighting problems that are making Malawians poor you're busy with APM. This is stupid.
Thanks: kusonka kwabwino chipani sichingagwe .
Zoona bg mn respect ndawi zonse
Zikomo Braz izizi ndinkhondo yomwe akuisaka satidzalora zimenezo
Lumumba ndi patali abwana just appreciate him not compare with lumumba
Dausi wagulidwa ndi MCP uyu asatinyase azipita ku MCP ndipo DPP ikuyenera kuchosa mbava ngati zimenezo
U r my hero
Talking true bro
HRDC very useless asowa zochita mmalo mopanga zachitukuko akulowelela za ndale. failed organisation!!!
Anthu onsewa akunenedwawa ndi oumira nakhumwa Dausi botoman palibe anapasapo ndarama munthu ndikwaziwa amenewa
Nankhumwa akulandira ndalama ku chokera ku Mcp kwa Simbi phiri ndi kwa Chilima kuti Asokoneze DPP
Mumatiimilila Bg
BIG 👍
Cadet kulira mokweza dpp sidzalowaso mboma brother
Kodi inuyo mmene zinthu zililmu mukuti dziko likuyenda bwino? Anthu akuvutka mmizimutu
You mad
DPP is for the Mutharikas family, Why can't u, the Dausis form ur own Party? Go a head APM .
Dausi ndi mfiti
DPP yonseyo ndi yakatangale not only Dausi
Akulakwitsa kutero amusiye anytime piter yemweyo
Dausi ndiwozungulila mutu kumalawi kuno kuli zitsilu
Daus ndi Nankhumwa ndimbuzi zawanthu...ngati ayambitse chipani chawo Adad bas
Dausi Ali ndichibwana kwambiri
Ayambitse chawo amenewa Dausi ndi nakhumwa yambani chanu please
Sometimes mtolakhani uyu, amaometsa mbali, khani ija yasokomekeranso…
Inenso ndimaona choncho awa azingonena ma history omwewa onsati za ndale
Uyu amanena fact. HRDC inasapota MCP, ndi chifukwa chani akufuna kulowelera zochitika ku DPP amenenso ali adani awo? Ndimawerenga nyuzipepala ina yake HRDC chairperson kumpoto akufuna kupita ku khothi kuti akamuletse APM asayime. Mtolankhani uyu amanena chilungamo chokhachokha man. MCP yapanga endorse Chakwera palibe wanena kuti si democracy. Ena apanga endorse APM akuti si democracy. Mtolankhani uyu ndi 1
Amene mukumasutsana Nayenu NDI mbuziso zawanthu...uyu amalankhula zogwila mtima..zoona zokhazokha
Iwe ndi bg MN
Ulemu wanu brother
Ngani ijaa ndayivesesa sopano APM YEMWEYO
Ife timaziwa kale kuti Dausi ndiwosokoneza
Kumenek ndiye kulangula tisangomenyana basi anthuwa akutenga machasi
Akuwopa chiyani amusiye peter azayime , dausi ndiwosokoneza malawi atapoa ndi ulamuliro wa chakwera
Adha awawa ulemu wanu
Munthu onena chilungamo chothirako bodza ndi wowopsa kuposa yemwe amanena bodza lopanda chilungamo.
Dausi ndi galu wadyera
Yes ndi zoona kuli gulu Lina likukakamiza APM kt ayime iwe ukumbukile APM 2021 anane yekha kt sazayimeso koma pano anthu awo akumusokoneza APM kt ayimeso ndi zoona izo ???
Muli bho
APM yemweyo watikwanila
Bola munthalikayo.Awo asatiputsitse ndimbava zosakhutitsika ayi.Kulibe zimenezo.Iwe tokota osawopa ife umatitokotela history mopeleka chidwi and umakhala ndi maumboni okwanila.
Dausi ndiopa kuyambira kale atuluke mchipan akayambise chake akapume waba zambiri galu amenei
Bg mumatha kulongosola zinthu
Angochoka muchipamo basi amusiye Apm
Akumuopa Apm
Big ulemu wanu Big ndi makunyadilani
Peter azawina basi ngati palibe kubera
Zitsilu zitatu zimenezi zisokoneza DPP maka uyo wonenepa ngati nkhuku ya vertinary.
Ngati akuti Muthalika family azipanga yekha ndiye ali ndi ufulu wambiri even wochotsa anthutu.DPP inaluza coz of Nankhumwa ndi Dausi dyera.HRDC pamsana pano nonse ndinu mwawononga zikoli ndipo ndinu zitsilu musamalowelele za zipani agalu inu
Dausi bottman ndi nankhumwa ayabise chipani chawaoo
Peter sangathe
Pita ayime basi
Kungoti dausi ndiwamanyi ndipo akuyenera achoke akayambise chipani chake shatapuiiiii
Anafufuma Masaya kkkk iwetu iwe
Ubwino wake ife Sitikufuna APM Atibekekere Mwana 😅 Tikufuna Ntchito Zake zibwelere, Osat Wakura Wakura Wakalamba Ngat Akapanga chinkhoswe Ndi Mwana wa 2000
ntchito zake ziti zimenezo?
😢😢😢😢 god bless you brother
osanyengerera chilungamo chiyende ngati madzi popanda inu sitingadziwe kanthu
Izidi zikudabwisa kuti HRDC ikulowa Pati agulu awa ndiyamene ationongela zikoli ,,,inu a HRDC mukapitiliza zomalimbana ndi DPP tikuochelani mmanyumba mwanu Momo
HRDC all of them they are stupid, ndiwanthu omwe anatipatsitsa mavuto ife a malawi, ife a malawi tiyeni tikavotele APM tatopa ndimavuto