A Gadama ndi anzawo analowa mmanda lero pa 21 May. Kodi analakwanji kuti aphedwe?

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 18 сен 2024

Комментарии • 166

  • @georgemsangu
    @georgemsangu Год назад +11

    Ine ine Ngati George Msangu from Mzimba centre.ndizaferamo sindingavoter McP.okhao ana osadziwa kanthu ndiomwe mavotera zopuzmsa. Reporting from South Africa

    • @RiteRoderick
      @RiteRoderick 2 месяца назад

      True big inenso i won't vote for chipani chokuphachi ndiine mwana wa Adad mpakana kale

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 Год назад +2

    Here we go! Thanks bakili muluzi RUclips channel!! We need some more teachings kuti tidziwe za anthu oyipa amenewa a mcp, agalu amenewa!! Akupha onyasa and opanda chikondi !!

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Год назад +3

    Brother timakunyadila kwambila mumalakhula chilongamo mulungu apitilize kukutetezani chifukwatu tikuziwakuti pali anthu ena samafuna chilungamo kutichiziwike mwainuyo taziwachilungamo and we still upgrading muma stories anuwa may all mighty allah bless you and protect u as you stand for the truth

  • @patrickbonongwe8569
    @patrickbonongwe8569 Год назад +2

    Mulungu azipitiliza kumupasa chilango Kamuzu ankawona ngati sazafa wasala Tembo ndi Kazamila anthu oyipa mitima

    • @yusuffatch4146
      @yusuffatch4146 11 месяцев назад

      Tembo mumanena uja wapita tu. Watsalandi wina uja

  • @charlesmpiyama-js4gy
    @charlesmpiyama-js4gy Год назад +5

    Awa ndi makina keep it up, I personally appreciate
    for the work tirelessly done,

  • @luciascharles4345
    @luciascharles4345 Год назад +7

    A mcp kuyambila kale ndiya galu awa

  • @Razarusmbavachakwera
    @Razarusmbavachakwera Год назад +9

    Awa ndimachine opangila machine azake pankhani yazofuvuzafuvuza

  • @fefa2050
    @fefa2050 Год назад +5

    Nice Job Brother GOD bless you

    • @jomochirwa
      @jomochirwa Год назад

      Oooh nchifukwa chake adad adatsekeledwa account yawo etiiii

  • @Ndinenjani
    @Ndinenjani Год назад +3

    Very sad Malawi where murderers are hero’s and victims are villains. The truth must be told.

  • @chiyenangomba3330
    @chiyenangomba3330 Год назад +8

    Innocent blood was shed, malawi silizatukuka chifukw Cha mwazi wa athu osalakwa koma I know the judgement day is coming soon

  • @innocentliyawo3943
    @innocentliyawo3943 Год назад +2

    He was a freemason sent to our country for sacrifices. He was not a Malawian as well.

  • @Bushiriderick811
    @Bushiriderick811 Год назад +9

    I wish Malawi as republic we could hournering these hero's in the name of heroes day not kamuzu day

  • @farookousmane715
    @farookousmane715 Год назад +8

    Keep it up..may almighty grant you more years of blessings for your daily endeavors

  • @charlesmpiyama-js4gy
    @charlesmpiyama-js4gy Год назад +3

    Komadi 21 may chaka chilichonse boma likanaika nthawi yokumbukira anthu amenewa, instead timapereka ulemu kwa mbava yotchedwa kamuzu, shame!!!!

  • @rodwellmwenekitete8974
    @rodwellmwenekitete8974 Год назад +4

    Abakili muluzi anali nawo limodzi chifukwa thawi yimeneyo anali wankulu wa yangi payaniya,,,bakili ndiwakupha asabitsale

  • @charliepoulaliecky1893
    @charliepoulaliecky1893 Год назад +3

    Nchifukwa chiyani ndalama zathu za ku Malawi amayika nkhophe ya mfiti imeneyi???

  • @georgethole3813
    @georgethole3813 Год назад +2

    This is so nice we are learning alot

  • @amisichiphiri8227
    @amisichiphiri8227 Год назад +2

    Zachisoni ife a Malawi 🇲🇼 kwambiri pokumbukila kamuzu day ,munthu amene adapha anthu osalakwa,ndi chifukwa chake sititukuka mulungu anatifulatila

  • @marychipofya4945
    @marychipofya4945 Год назад +3

    koma zinthu zake please..nkhani zomvetsa chisoni kwabasi ndipo zopweteketsa mitima. Amapha anzao ngati iwo ndi amuyaya. Lero naonso ndi mbiri chabe. Anthu awa anawamvetsa anzao zowawa kwabasi. So sad. May their souls rest in peace.

  • @petermitambo9257
    @petermitambo9257 Год назад +6

    Ndikamava, izi zimandikwezeletsa kidzakhala chigawenga chowukila boma. Or kudzajoina magulu amtopola. Zimandiwawa. Andale ndi wanthu oyipa😭😭🤞🤞🤞

    • @AllanBanda-t3u
      @AllanBanda-t3u Месяц назад

      ineso ndimaganiza chomcho anthuwa amadziva ngati mulungu zopusa zazii

  • @abdllahalie2633
    @abdllahalie2633 Год назад +1

    Thanks brother mumayiyimilila koma tipasileni nkhani za nkhondo ya Russia ndi Ukraine tinve mene zayendela ku bankhmutu chifukwa pano mwati ziiii kutipasila

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 11 месяцев назад +1

    Inu mcp was and is the bad party because some of you youngsters you don't know it that's why you are following and to say fact there were many people who were killed well MAN KEEP ON GIVING US THE TRUTH thanks may God bless you and their souls must REST IN PEACE

  • @Bushiriderick811
    @Bushiriderick811 Год назад +3

    Am wondering why up to date the state gvn called mcp still praising kamuzu and hournering that kamuz while he was foreign, killer and destroyed on top of that he didn't do anything for Malawi as development but just to brainwash our parents

    • @tingo3155
      @tingo3155 Год назад

      Nkhanza it means good to them, MCP is rotten to the core

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 Год назад +4

    I'll never praise KAMUZU and if I've done it before it was because of not knowing the truth about him but honestly he was a wicked man and thief in fact MCP wasn't supposed to be ruling today,Rest in hell KAMUZU
    😡😡

  • @HakeemSilaji
    @HakeemSilaji Год назад +3

    Inshaallah 24 years sopano ndikukula guy's holiday anthu gati awa idzakhalampo inshaallah 😭😭😭😭

  • @IanAllstal
    @IanAllstal 2 месяца назад

    MCP ndiyamwazi heavy mpakana panotu Komatu nchipululu simofera bwanji Anthu ofunikira Amathera mchipululu ?? Lero Ina simenei ndunena iyiyiiiyi

  • @petermanMitambo
    @petermanMitambo 3 месяца назад

    ❤ history is the best teacher long live BMTV ♥️

  • @yusufualidan238
    @yusufualidan238 Год назад +3

    Can you take us to mangochi mudzi omwe udawotchedwa uja

  • @daviemafunga
    @daviemafunga Год назад +2

    Inuyo ndikuchikweza brother palibenso angazafane ndiinu pankhani ngt izi kmw

  • @edsonjohnbakaimani
    @edsonjohnbakaimani Год назад +2

    Would you kindly write a book on these four government officials who suffered under Kamuzu administration

  • @chifundoKaluvi-ey5uw
    @chifundoKaluvi-ey5uw Месяц назад

    Ngat tizawinaso Ife adpp tizathesa kukumbukila kamuzi niwakut gana

  • @yusufualidan238
    @yusufualidan238 Год назад +1

    I learn more from this channel

  • @haneefmuyaya7472
    @haneefmuyaya7472 8 месяцев назад

    Bakili Muluzi TV channel:
    We proud of you guys, keep it up updating the hidden information,
    Mumatisekula mmaso, ndi inu vumbuluso ndithu, okwiya nanu
    Ndi Mfiti, Satan, Devil
    We follow you guys

  • @lyiemax
    @lyiemax 11 месяцев назад

    A brilliant research, keep us updated, proud of you always 🔥🔥🔥🔥

  • @johnman4619
    @johnman4619 Год назад +1

    Timafuns mufufuze za karonga stambuli komanso fanikiso phiri .at bakili muluzi ruled

  • @lestermaide-yy4xy
    @lestermaide-yy4xy Год назад +1

    MCP nyasi ya chipan to me I can't vote for it

  • @molicieeosama8877
    @molicieeosama8877 Год назад +1

    You r very important man 🤝🤝💪

  • @georgemsangu
    @georgemsangu Год назад +1

    Am a Malawian watching from sa but kamuzu Mmmmm AI no comments

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 2 месяца назад

    MCP kwawo ndikupha basi afiti okhaokha 😢😢😢

  • @JacoboManeno-uc3lb
    @JacoboManeno-uc3lb 11 месяцев назад +1

    Born and living em😮 northern Mozambique, I noticed the language spoken is of origin 😅BANTU being a BANTU myself (makon😅de by tribe) I was able to understand what NG😅WAZI did to others in his times

  • @ishakatimbe7341
    @ishakatimbe7341 11 месяцев назад

    Kuli mulungu kunja kuno ndamene asunge moyo was big man Peter. Iweyo ndaimika manja🤗

  • @enerstmwitha392
    @enerstmwitha392 Год назад

    Thanks my brother and we thanks all the time

  • @rodwellmwenekitete8974
    @rodwellmwenekitete8974 Год назад +2

    Funso lina,,,,kodi eveson matafale adafelanji

  • @MaxwellMustafa-ec8fc
    @MaxwellMustafa-ec8fc Год назад +1

    Zikomo abraz zosezi zikunena za MCP guys MCP sichipani

  • @elishamael-shadai
    @elishamael-shadai 2 месяца назад +1

    May these heroes rest in peace

  • @ruthtimothy9583
    @ruthtimothy9583 Год назад +1

    I like this channel ❤❤

  • @BenissoneErnesto-eh6zs
    @BenissoneErnesto-eh6zs 9 месяцев назад

    Mcp sichipani watching from Mozambique never give up bg brother

  • @honourablemcgregorysc97tv
    @honourablemcgregorysc97tv Год назад +1

    Am watching it

  • @EmmanuelThom2-xf6ij
    @EmmanuelThom2-xf6ij Год назад +1

    We like u ...keep moving bro

  • @YusufAbdull-w6p
    @YusufAbdull-w6p 11 месяцев назад +1

    BIG. 🙏🙏🙏🙏

  • @KalongaKachipi
    @KalongaKachipi 3 месяца назад

    I will tell this story my child .don't celebrate kamuzu day ,don't vote for mcp

  • @emmanuelchilongo2171
    @emmanuelchilongo2171 Год назад

    Loud and clear from Zambia

  • @ibrahimtutini5862
    @ibrahimtutini5862 Год назад +1

    Koditu ena amati MCP inaliyabwino chifukwa chauchisilu mcp inali yoopsa kwambiri ndipo olo munthu nyumba yokhala yako sumagona ngati ndiyako unali ukuopa kuphuzira komweku kungoti ukuziwa bwino zinazake kuposa ena zinalitu zoopsa makolo amadandaula kuti uphedwa lusotu anthu amalibitsa kuopa kuphedwa olo ena akamati bola KAMUZU umakala ugalu kwambiri ngati munali ang'ono amukonda kumakala pasi ndi makolo akuluakulu kumawafusa mene zimakalila. Olo oluka Mikeka omwewa akalukatu okongola amalanda akuti akapeleke kwa KAMUZU ndiye mukamasewela uziziwa kuti olo elo mavuto aliko koma mtendele uliko phone, TV, kukala ndizimenezo unali mulandu kale 😢😢😢😢😢

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Год назад

    I regret casting vote for MCP. Chilima, Mulungu akuone pondinamiza mpaka ine kuvotera MCP:Chipani choipitsitsa.

    • @ShaffTwaha
      @ShaffTwaha Год назад

      Malawian yathu bwanji kodi?

  • @anthonynkhoma4265
    @anthonynkhoma4265 3 месяца назад

    Mudzatiuzenso za mmene anafera a Njaunju komanso banja la a Tambala ku Lilongwe.

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Год назад +2

    Kulakwa kwambiri! These things are not mentioned on Kazumu Day

    • @Roseta0629
      @Roseta0629 Год назад

      Sangatchule😢 apepuke ☹

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Год назад +1

    Makina amenewa

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Год назад +1

    Kale eish kunali Cruelty osati masewera

  • @molicieeosama8877
    @molicieeosama8877 Год назад +1

    Padafunika pakhale filimu Ngati adachitila za yida Amin

  • @GodfreyWhayo-hh1dm
    @GodfreyWhayo-hh1dm Год назад +1

    Katangaleyu adachokera patali ndi chifukwa maboma onse abwerawa akumakhala akatamgale .

  • @SmithMwangulu
    @SmithMwangulu 2 месяца назад

    Best tv

  • @zotsatirabanda4438
    @zotsatirabanda4438 3 месяца назад

    Mukatha mukambenso za imfa ya MacDonald Masambuka tidziwenso zoooona

  • @ishmaelmkuluma2013
    @ishmaelmkuluma2013 Год назад

    Ndichifukwa sikoli silikuyenda bwino coz muli magaz ambir

  • @marychipofya4945
    @marychipofya4945 Год назад +1

    Mpaka kuwaphwanya anthu maubongo awo...mpaka chinsomali kunkhongo mmmmmh zoopsa😫

  • @Abigail-w5d
    @Abigail-w5d 11 месяцев назад

    Kamudzu akaziwa Kuti sanali mumalawi ndichifukwa chake akapha aMalawi

  • @David-y9i6h
    @David-y9i6h Год назад +1

    Koma zibwana tikupanga lerozi ena analimvera kuwawa dzikoli

  • @AllanBanda-t3u
    @AllanBanda-t3u Месяц назад

    MCP Mmmm 😭😭😭😭 ine ayiii or pan'gono

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 Год назад +1

    Uyu ndi katswiri pa zofufuza

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 10 месяцев назад

    Shem story I cry for this story very bad

  • @roychiwaya
    @roychiwaya 10 месяцев назад

    Very ssd

  • @mordecaikachale2497
    @mordecaikachale2497 Год назад +2

    Ndimafunisisa nditamuziwa mkulu ameneyu ...umatimasula kwambiri... ndipo likadakhala dziko la Malawi limamvera munthu uyu bwezi MCP itachoka m'boma

  • @timothyngulube545
    @timothyngulube545 Год назад +1

    MCP inali yakupha

  • @janenkhoma6447
    @janenkhoma6447 Год назад +2

    Kumwamba tukalowa by favor

  • @charliepoulaliecky1893
    @charliepoulaliecky1893 Год назад +1

    Umakwana boss

  • @DoYouKnow3838
    @DoYouKnow3838 Год назад +2

    the man called Kamuzu(Richard Armstrong) Banda was a ruthless murder....

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Год назад +1

    BIG 👍

  • @user-un8yq1gg2i
    @user-un8yq1gg2i Месяц назад

    Mcp ikangoluza ulendo uno, tingoyithetsa isadzapezekenso komanso kamuzu day ija ichokeretu tisadzayimvenso

  • @LouisAndrew-jr1yj
    @LouisAndrew-jr1yj 4 месяца назад

    The best TV ever

  • @robertchikaonda-mu1bg
    @robertchikaonda-mu1bg Год назад +1

    Kamuzu akuyankha milandu imeneyi munthu oipa.zedi

  • @petermitambo9257
    @petermitambo9257 Год назад +1

    Koma kamuzu ameneyu ikhala masiku wano eehe wallah wenafe tikadavala ma bomba la tinke nawe ehe

  • @cassimmeleka40
    @cassimmeleka40 11 месяцев назад

    Mulungu sangawasiye An2 oipawa

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Год назад +2

    Kom abale anthu ambili adaphedwa mu nthawi yoipayi

  • @user-cv7zg2gl3r
    @user-cv7zg2gl3r 7 месяцев назад

    Nanga Matafale? Komaso chasowa? Best tv

  • @evancedzungu
    @evancedzungu 5 месяцев назад

    Chilungamo pa dziko pano plb so siyani kudandaula

  • @LesterSimon-k2t
    @LesterSimon-k2t 7 месяцев назад

    nice

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Месяц назад

    Naye kamuzu akanakhala dolo sakanafa,atsalawa azidziwa Kut wakupha nayenso adzafa

  • @chrissygama8678
    @chrissygama8678 Год назад +1

    Inali nthaw yowawitsa ndithu may their soul rest in peace

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 11 месяцев назад

    Kunalibe kamuzu kalero ameneyu anali Richard wa ku Ghana chibwenzi Cha Cicilia ndi John Tembo, okupha anzao amoyo hiiii 😭😭😭

  • @cassimmeleka40
    @cassimmeleka40 11 месяцев назад

    Mumatisegula mmaso enafe sitimaziwa kuti tembo kamudzi cicilia adalipangira zotani malawi

  • @isaacmussa2942
    @isaacmussa2942 Год назад +1

    Kamuzu anari mfiti kwambiri ngat lyeyo sadzafa

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 Год назад +1

    Zachisoni

  • @mrsmoseskita9180
    @mrsmoseskita9180 4 месяца назад

    14 may timakumbukira chigawenga chotchedwa kamuzu Ghana

  • @Lizzie-h1k
    @Lizzie-h1k Год назад +1

    Nsogoleri wa mtima ngati mvuu😂😂😂

  • @leyydavido-qd9gv
    @leyydavido-qd9gv Год назад

    Big up malume

  • @user-iv3do9vk3u
    @user-iv3do9vk3u 11 месяцев назад

    Bakili muluzi ndiye mbava yayikulu, wakupha wankulu. Anatiphera matafale. Anàpha anthu ochuluka kwabasi mbava ya chiyao nsilamu

  • @amisichiphiri8227
    @amisichiphiri8227 Год назад +1

    Ilibe sound bwanji kapena vuto ndi phone yanga

  • @AfiyakazembeKazembe
    @AfiyakazembeKazembe Год назад +1

    Mumatimasula mithu

  • @blandinabonaventure
    @blandinabonaventure 11 месяцев назад

    Kulibe wamuyaya kamuzu ndi mzako tembo mulungu akuoneni

  • @EmmieEmmie-y2f
    @EmmieEmmie-y2f 11 месяцев назад

    Alipanjra kamunzu sanafike ayi

  • @bayview4554
    @bayview4554 Год назад +2

    Kumuzu was not Malawian that's why he was doing whatever to Malawian people and God he's angry with Malawi country until forever

    • @irenechirwa9710
      @irenechirwa9710 Год назад

      Neso ndinanenapo kale kut kamuzu amapanga nkhanza chonchija chifukwa choti sanali m'malawi.