Ine ine Ngati George Msangu from Mzimba centre.ndizaferamo sindingavoter McP.okhao ana osadziwa kanthu ndiomwe mavotera zopuzmsa. Reporting from South Africa
Here we go! Thanks bakili muluzi RUclips channel!! We need some more teachings kuti tidziwe za anthu oyipa amenewa a mcp, agalu amenewa!! Akupha onyasa and opanda chikondi !!
Brother timakunyadila kwambila mumalakhula chilongamo mulungu apitilize kukutetezani chifukwatu tikuziwakuti pali anthu ena samafuna chilungamo kutichiziwike mwainuyo taziwachilungamo and we still upgrading muma stories anuwa may all mighty allah bless you and protect u as you stand for the truth
koma zinthu zake please..nkhani zomvetsa chisoni kwabasi ndipo zopweteketsa mitima. Amapha anzao ngati iwo ndi amuyaya. Lero naonso ndi mbiri chabe. Anthu awa anawamvetsa anzao zowawa kwabasi. So sad. May their souls rest in peace.
Thanks brother mumayiyimilila koma tipasileni nkhani za nkhondo ya Russia ndi Ukraine tinve mene zayendela ku bankhmutu chifukwa pano mwati ziiii kutipasila
Inu mcp was and is the bad party because some of you youngsters you don't know it that's why you are following and to say fact there were many people who were killed well MAN KEEP ON GIVING US THE TRUTH thanks may God bless you and their souls must REST IN PEACE
Am wondering why up to date the state gvn called mcp still praising kamuzu and hournering that kamuz while he was foreign, killer and destroyed on top of that he didn't do anything for Malawi as development but just to brainwash our parents
I'll never praise KAMUZU and if I've done it before it was because of not knowing the truth about him but honestly he was a wicked man and thief in fact MCP wasn't supposed to be ruling today,Rest in hell KAMUZU 😡😡
Bakili Muluzi TV channel: We proud of you guys, keep it up updating the hidden information, Mumatisekula mmaso, ndi inu vumbuluso ndithu, okwiya nanu Ndi Mfiti, Satan, Devil We follow you guys
Born and living em😮 northern Mozambique, I noticed the language spoken is of origin 😅BANTU being a BANTU myself (makon😅de by tribe) I was able to understand what NG😅WAZI did to others in his times
Ine ine Ngati George Msangu from Mzimba centre.ndizaferamo sindingavoter McP.okhao ana osadziwa kanthu ndiomwe mavotera zopuzmsa. Reporting from South Africa
True big inenso i won't vote for chipani chokuphachi ndiine mwana wa Adad mpakana kale
Here we go! Thanks bakili muluzi RUclips channel!! We need some more teachings kuti tidziwe za anthu oyipa amenewa a mcp, agalu amenewa!! Akupha onyasa and opanda chikondi !!
Brother timakunyadila kwambila mumalakhula chilongamo mulungu apitilize kukutetezani chifukwatu tikuziwakuti pali anthu ena samafuna chilungamo kutichiziwike mwainuyo taziwachilungamo and we still upgrading muma stories anuwa may all mighty allah bless you and protect u as you stand for the truth
Mulungu azipitiliza kumupasa chilango Kamuzu ankawona ngati sazafa wasala Tembo ndi Kazamila anthu oyipa mitima
Tembo mumanena uja wapita tu. Watsalandi wina uja
Awa ndi makina keep it up, I personally appreciate
for the work tirelessly done,
A mcp kuyambila kale ndiya galu awa
Awa ndimachine opangila machine azake pankhani yazofuvuzafuvuza
Amakamba zabodza uyu
@@GorgeMachelani segula channel chako uzikamba zowonazo
Nice Job Brother GOD bless you
Oooh nchifukwa chake adad adatsekeledwa account yawo etiiii
Very sad Malawi where murderers are hero’s and victims are villains. The truth must be told.
Innocent blood was shed, malawi silizatukuka chifukw Cha mwazi wa athu osalakwa koma I know the judgement day is coming soon
He was a freemason sent to our country for sacrifices. He was not a Malawian as well.
I second you on this Kamuzu was imposter
I wish Malawi as republic we could hournering these hero's in the name of heroes day not kamuzu day
💯
Why should we honour them?
I second u
Keep it up..may almighty grant you more years of blessings for your daily endeavors
The
Komadi 21 may chaka chilichonse boma likanaika nthawi yokumbukira anthu amenewa, instead timapereka ulemu kwa mbava yotchedwa kamuzu, shame!!!!
Abakili muluzi anali nawo limodzi chifukwa thawi yimeneyo anali wankulu wa yangi payaniya,,,bakili ndiwakupha asabitsale
Nchifukwa chiyani ndalama zathu za ku Malawi amayika nkhophe ya mfiti imeneyi???
MCP singathe
This is so nice we are learning alot
Zachisoni ife a Malawi 🇲🇼 kwambiri pokumbukila kamuzu day ,munthu amene adapha anthu osalakwa,ndi chifukwa chake sititukuka mulungu anatifulatila
koma zinthu zake please..nkhani zomvetsa chisoni kwabasi ndipo zopweteketsa mitima. Amapha anzao ngati iwo ndi amuyaya. Lero naonso ndi mbiri chabe. Anthu awa anawamvetsa anzao zowawa kwabasi. So sad. May their souls rest in peace.
Ndikamava, izi zimandikwezeletsa kidzakhala chigawenga chowukila boma. Or kudzajoina magulu amtopola. Zimandiwawa. Andale ndi wanthu oyipa😭😭🤞🤞🤞
ineso ndimaganiza chomcho anthuwa amadziva ngati mulungu zopusa zazii
Thanks brother mumayiyimilila koma tipasileni nkhani za nkhondo ya Russia ndi Ukraine tinve mene zayendela ku bankhmutu chifukwa pano mwati ziiii kutipasila
Inu mcp was and is the bad party because some of you youngsters you don't know it that's why you are following and to say fact there were many people who were killed well MAN KEEP ON GIVING US THE TRUTH thanks may God bless you and their souls must REST IN PEACE
Am wondering why up to date the state gvn called mcp still praising kamuzu and hournering that kamuz while he was foreign, killer and destroyed on top of that he didn't do anything for Malawi as development but just to brainwash our parents
Nkhanza it means good to them, MCP is rotten to the core
I'll never praise KAMUZU and if I've done it before it was because of not knowing the truth about him but honestly he was a wicked man and thief in fact MCP wasn't supposed to be ruling today,Rest in hell KAMUZU
😡😡
100%
Inshaallah 24 years sopano ndikukula guy's holiday anthu gati awa idzakhalampo inshaallah 😭😭😭😭
MCP ndiyamwazi heavy mpakana panotu Komatu nchipululu simofera bwanji Anthu ofunikira Amathera mchipululu ?? Lero Ina simenei ndunena iyiyiiiyi
❤ history is the best teacher long live BMTV ♥️
Can you take us to mangochi mudzi omwe udawotchedwa uja
Inuyo ndikuchikweza brother palibenso angazafane ndiinu pankhani ngt izi kmw
Would you kindly write a book on these four government officials who suffered under Kamuzu administration
Ngat tizawinaso Ife adpp tizathesa kukumbukila kamuzi niwakut gana
I learn more from this channel
Bakili Muluzi TV channel:
We proud of you guys, keep it up updating the hidden information,
Mumatisekula mmaso, ndi inu vumbuluso ndithu, okwiya nanu
Ndi Mfiti, Satan, Devil
We follow you guys
A brilliant research, keep us updated, proud of you always 🔥🔥🔥🔥
Timafuns mufufuze za karonga stambuli komanso fanikiso phiri .at bakili muluzi ruled
MCP nyasi ya chipan to me I can't vote for it
You r very important man 🤝🤝💪
Am a Malawian watching from sa but kamuzu Mmmmm AI no comments
MCP kwawo ndikupha basi afiti okhaokha 😢😢😢
Born and living em😮 northern Mozambique, I noticed the language spoken is of origin 😅BANTU being a BANTU myself (makon😅de by tribe) I was able to understand what NG😅WAZI did to others in his times
Kuli mulungu kunja kuno ndamene asunge moyo was big man Peter. Iweyo ndaimika manja🤗
Thanks my brother and we thanks all the time
Funso lina,,,,kodi eveson matafale adafelanji
Uyang'ane Kuma oudio akale adaponya kale imeneyo
Simunayivele kd pangani search
Search ilipo kale
Zikomo abraz zosezi zikunena za MCP guys MCP sichipani
May these heroes rest in peace
I like this channel ❤❤
Mcp sichipani watching from Mozambique never give up bg brother
Am watching it
We like u ...keep moving bro
BIG. 🙏🙏🙏🙏
I will tell this story my child .don't celebrate kamuzu day ,don't vote for mcp
Loud and clear from Zambia
Koditu ena amati MCP inaliyabwino chifukwa chauchisilu mcp inali yoopsa kwambiri ndipo olo munthu nyumba yokhala yako sumagona ngati ndiyako unali ukuopa kuphuzira komweku kungoti ukuziwa bwino zinazake kuposa ena zinalitu zoopsa makolo amadandaula kuti uphedwa lusotu anthu amalibitsa kuopa kuphedwa olo ena akamati bola KAMUZU umakala ugalu kwambiri ngati munali ang'ono amukonda kumakala pasi ndi makolo akuluakulu kumawafusa mene zimakalila. Olo oluka Mikeka omwewa akalukatu okongola amalanda akuti akapeleke kwa KAMUZU ndiye mukamasewela uziziwa kuti olo elo mavuto aliko koma mtendele uliko phone, TV, kukala ndizimenezo unali mulandu kale 😢😢😢😢😢
I regret casting vote for MCP. Chilima, Mulungu akuone pondinamiza mpaka ine kuvotera MCP:Chipani choipitsitsa.
Malawian yathu bwanji kodi?
Mudzatiuzenso za mmene anafera a Njaunju komanso banja la a Tambala ku Lilongwe.
Kulakwa kwambiri! These things are not mentioned on Kazumu Day
Sangatchule😢 apepuke ☹
Makina amenewa
Kale eish kunali Cruelty osati masewera
Padafunika pakhale filimu Ngati adachitila za yida Amin
Katangaleyu adachokera patali ndi chifukwa maboma onse abwerawa akumakhala akatamgale .
Best tv
Mukatha mukambenso za imfa ya MacDonald Masambuka tidziwenso zoooona
Ndichifukwa sikoli silikuyenda bwino coz muli magaz ambir
Mpaka kuwaphwanya anthu maubongo awo...mpaka chinsomali kunkhongo mmmmmh zoopsa😫
Kamudzu akaziwa Kuti sanali mumalawi ndichifukwa chake akapha aMalawi
Koma zibwana tikupanga lerozi ena analimvera kuwawa dzikoli
MCP Mmmm 😭😭😭😭 ine ayiii or pan'gono
Uyu ndi katswiri pa zofufuza
Shem story I cry for this story very bad
Very ssd
Ndimafunisisa nditamuziwa mkulu ameneyu ...umatimasula kwambiri... ndipo likadakhala dziko la Malawi limamvera munthu uyu bwezi MCP itachoka m'boma
MCP inali yakupha
Kumwamba tukalowa by favor
Umakwana boss
the man called Kamuzu(Richard Armstrong) Banda was a ruthless murder....
BIG 👍
Mcp ikangoluza ulendo uno, tingoyithetsa isadzapezekenso komanso kamuzu day ija ichokeretu tisadzayimvenso
The best TV ever
Kamuzu akuyankha milandu imeneyi munthu oipa.zedi
Koma kamuzu ameneyu ikhala masiku wano eehe wallah wenafe tikadavala ma bomba la tinke nawe ehe
Mulungu sangawasiye An2 oipawa
Kom abale anthu ambili adaphedwa mu nthawi yoipayi
Nanga Matafale? Komaso chasowa? Best tv
Chilungamo pa dziko pano plb so siyani kudandaula
nice
Naye kamuzu akanakhala dolo sakanafa,atsalawa azidziwa Kut wakupha nayenso adzafa
Inali nthaw yowawitsa ndithu may their soul rest in peace
Kunalibe kamuzu kalero ameneyu anali Richard wa ku Ghana chibwenzi Cha Cicilia ndi John Tembo, okupha anzao amoyo hiiii 😭😭😭
Mumatisegula mmaso enafe sitimaziwa kuti tembo kamudzi cicilia adalipangira zotani malawi
Kamuzu anari mfiti kwambiri ngat lyeyo sadzafa
Zachisoni
14 may timakumbukira chigawenga chotchedwa kamuzu Ghana
Nsogoleri wa mtima ngati mvuu😂😂😂
Big up malume
Bakili muluzi ndiye mbava yayikulu, wakupha wankulu. Anatiphera matafale. Anàpha anthu ochuluka kwabasi mbava ya chiyao nsilamu
Ilibe sound bwanji kapena vuto ndi phone yanga
😂 vuto ndi4n yanu
I guess it's your phone
Mumatimasula mithu
Kulibe wamuyaya kamuzu ndi mzako tembo mulungu akuoneni
Alipanjra kamunzu sanafike ayi
Kumuzu was not Malawian that's why he was doing whatever to Malawian people and God he's angry with Malawi country until forever
Neso ndinanenapo kale kut kamuzu amapanga nkhanza chonchija chifukwa choti sanali m'malawi.