Kuyakhula mosaopa Chakwera wamupha Chilima. Chifukwa cha udindo

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 23 июн 2024

Комментарии • 184

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i 6 дней назад +10

    Akulu eeee apa pa kanakhala kuti Pali anthu 10 ngati inu ayi dziko bwenzi likuyenda bwino. I like your style brother ❤

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 14 дней назад +16

    Manganya ndi mfiti yotheratu ndagwilizana nazo

  • @VeronicaChirwa-ct4os
    @VeronicaChirwa-ct4os 14 дней назад +14

    Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.

    • @manfredzalirabetha2440
      @manfredzalirabetha2440 5 дней назад +1

      Ma radio osathandiza a mmalawi muno bola limpopo basi iyaa

    • @user-be5fc3ed1i
      @user-be5fc3ed1i День назад

      Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 6 дней назад +6

    Mizimu ya wonse omwe adawapha pa ngozi ya ndege ija iwanzunzedi anthu amenewa

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 14 дней назад +11

    Posatengera CHIPANI chilima adachita kuphedwa kumene achakwerawo akudziwa Koma pot CHOIPA chimakanidwa sangamvomere Koma MULUNGU akudziwa

  • @MercyKachenje
    @MercyKachenje 14 дней назад +10

    Mau amphavu awa vuto anthufe nsanje too
    Mulungu apitilize kitiululira zinsisi

  • @LamieTiger
    @LamieTiger 14 дней назад +10

    Vuto ndilot athu ena akuikira kumbuyo athu afitiwa athu ot akudalira mitsokho yathu Kut antchedwe olemera mipando akupheranayo nditimisokho tathu toja deleri kuzolowela Moyo osagwira ntchito Moyo opatsidwa zaulele chakwera wayetsa Kuno Ku church Kut udzilandila chakhumi mabatile ako

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 14 дней назад +8

    But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry

  • @ThomasKaphwiti
    @ThomasKaphwiti 11 дней назад +6

    Ndipo manganya siwakuno mayi ake ndi aku Zimbabwe muzikaona kuchenjera ngt akuba nkhuku😅😅

    • @samueljuma4452
      @samueljuma4452 5 дней назад

      Kkkkkkk ngati akuba nkhuku???koma ndaseka

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju 3 дня назад +1

    I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected

  • @OsmanBakali-s5x
    @OsmanBakali-s5x 6 дней назад +2

    💔💔💔💔mpaka pano ineyo ndmangoona ngati a CHILIMA alipo sanamwalire ai.. I will still missing him in my heart ❤️ forever 😭😭😭

  • @PaulMinofu
    @PaulMinofu 14 дней назад +8

    On point❤❤❤❤

  • @InnocentMlowoka-ew4lo
    @InnocentMlowoka-ew4lo 14 дней назад +8

    Chilungamo kuwawa

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 13 дней назад +3

    Voice ya nzeru❤

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 6 дней назад +4

    Amene anapha chilima panya pake 😢😢😢

  • @user-yo9rw8tr4s
    @user-yo9rw8tr4s 14 дней назад +7

    Dosanama munthu Uyo walankhula mau wogwilika kwambile

  • @BensonChilundu
    @BensonChilundu 6 дней назад +2

    Micheal Usi ndi munthu ozikonda kwambiri.zoona zake zaoneka zokha chifukwa iyeyu sakadalolera kukhala Vice President.Koma abale ndalama zovuta ndithu

  • @YusufuKaifa-fr4wt
    @YusufuKaifa-fr4wt 6 дней назад +2

    ❤❤❤❤❤❤my point president chakwera out

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 2 дня назад

    Well spoken my brother we can't keep Quite on what happened in our National, we are still mourning all who died on that day ,it SAD.

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 6 дней назад +3

    Manganya ndi fiti panya pamake plus chakwera 😢😢

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s 12 дней назад +4

    Muli speech yamphavu ndipo boma ili Mulungu achite nanu

  • @ThomasKaphwiti
    @ThomasKaphwiti 11 дней назад +3

    Ndipo zoona tatiyeni a Malawi tionetse mkwiyo wathu Maliro ndiye tinayika kwa tsalano tithane ndizigawengazi😢😢😢😢

  • @MtokomaYohane
    @MtokomaYohane 5 дней назад +2

    And is true chakwera akukhunzidwadi and i have more questions

  • @paulinekayuni1621
    @paulinekayuni1621 6 дней назад +2

    As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya

  • @HameedahMasambuka
    @HameedahMasambuka 14 дней назад +8

    Ndipo kukumangan inuyo. Ndizakhala numbar one kusonkha ndalama yokuombolelan mmmmmmm

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds 6 дней назад +2

    Iponden fadah 🎉

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 13 дней назад +1

    The power of massage and the power of prayer indeed

  • @LoveHawabwa
    @LoveHawabwa 4 дня назад +1

    Inu mwayakhula mawu ife tikuwopa kuyakhulapo mwatilakhulira mulungu awakanthe kopotsa

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 6 дней назад +2

    Sanayankhuleponso amangophwisa mkhutu wa udindo usi

  • @AmandaConstance-fx8cr
    @AmandaConstance-fx8cr 14 дней назад +2

    Not all days are Sundays
    God is watching and may there souls rest in peace 🙏

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 12 дней назад +2

    Mulungu akuona zonse,,, ndipo samagona tulo. 😭😭😭😭😭

  • @FelisterNgwira-op7rr
    @FelisterNgwira-op7rr 12 дней назад +3

    Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 6 дней назад +2

    Manganya mpando kumeneko sanjoya akachita chibwana mkwiyo wa Mulungu umukantha koopsa tikupempheratu magazi a Chilima aja ayankhula usazione ngati wachenjera

  • @MichaelWilliamsNyirenda
    @MichaelWilliamsNyirenda 6 часов назад

    Powerful message Duuu may their souls rest in peace ✌️

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 14 дней назад +2

    Inu ndiye mwanena zoona brother mmmmmh ulemu wanu Inuyo shaaaa Ndamva nanu kukoma zedi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 6 дней назад +2

    Koma izizi tu we are praying kuti Mulungu alange aliyense amene anatenga gao lokupha chilima pompano asadikile chiweluzo

  • @LovelyBlini-cu3iu
    @LovelyBlini-cu3iu 14 дней назад +6

    Mau amphamvu

  • @ackimChiumia
    @ackimChiumia 8 дней назад +2

    U are talking sense

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b 14 дней назад +2

    So heartly broken dear

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe7448 10 дней назад +1

    Yesu anapelekedwa chifukwa cha ndalama yochepa,God have mercy

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 6 дней назад +1

    Nawoso mayiko usi mbusi yamunthu kukonda ndalama kumeneko mpaka kulolela Kuti munthu ampedwe ndalama abale God bless you mukutidzegula mithu

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 6 дней назад +2

    Chi Michael usi manganya that why amuika pa mpando iyeyo kuthamanga kukakwera pa mpando pakamaso gwaaaaa manganya

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b 14 дней назад +3

    It's true my brother that's sad

  • @user-ml8lk9dr7t
    @user-ml8lk9dr7t День назад

    Yes may God perform wonders that the truth must prevail

  • @GodisoneNoel
    @GodisoneNoel 14 дней назад +4

    Zoona ❤❤❤❤❤❤❤

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 5 дней назад +1

    Osaopa osafooka tizafera mbendera yathu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @MichaelWilliamsNyirenda
    @MichaelWilliamsNyirenda 6 часов назад

    Bakili muluzi tv yekha akalowa kumwamba bro kuyankhula mowonatu

  • @georgejere2922
    @georgejere2922 14 дней назад +2

    You will pay for it, what's wrong did our SKC do to you😭😭😭😭😭 the day will come 😢😢😢

  • @user-er7ub4ug7y
    @user-er7ub4ug7y 13 дней назад +1

    Osaopa osafooka tiime pa chilungmo dziko lino nditose ndopo mbendera yake ndiii🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼situkukuopami😢😢😢😢

  • @WellingtonHowahowa
    @WellingtonHowahowa 6 дней назад +1

    Basi poti kulibe mulandu okupha ndimphezi ...mudiyeni chakwelayo azasowa omusumila

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g 14 дней назад +3

    manganiso anu ameneyo okay alibwino

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 11 дней назад +1

    Enanu mudakangosiya kucommenter Ngati sizikukumvekelani bwino Ife nde tikumva kusekemela chipepeso chathu timachipeza kuzela kwaanthu amenewa chilima wathuuuu tizamfela

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 14 дней назад +2

    Zoonadi manganya ndi munthu oipa sanayakhulapo za imfa ya chilima

  • @Sabina-hw4js
    @Sabina-hw4js 14 дней назад +2

    Ndi Ana omwe akudziwa

  • @user-fm8ed7eo3i
    @user-fm8ed7eo3i 6 дней назад

    Zoona awa ndiye mau bro end I love you so much brother ❤🎉🎉

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 10 дней назад +1

    Ambuye tipheleni Chakwera 😂😂😂😅😅😅

  • @MirajiYusuf-vx5ux
    @MirajiYusuf-vx5ux 13 дней назад +1

    Zoonadi brother ife tikulira ndithu esh infa ya chilima mmmm😢😢😢😢 mulungu 😢😢😢😢

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 3 дня назад

    Ameni amen misonzi ya wanthu osalakwa simapita pachabe

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwa 10 дней назад +2

    Ndpo mabala akutiwaw

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 6 дней назад +1

    Komad manganya anatidabwitsatu palibe chimene anayankhula pa za imfa ya Chilima an angokhala pheeee ngt sizikunkhudza zombvetsa chisoni kwabasi Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse

  • @Marymahendra
    @Marymahendra День назад

    That’s true brother if it was khozi ya ndeka suit no trousers no shoes my

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 14 дней назад +3

    Zoonadi inenso ndikusiwa cho cho

  • @NoelLangwani
    @NoelLangwani 6 дней назад +1

    Ndipoh zoonadi mwalakhula bwino ndithu broz man

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 14 дней назад +2

    Atola khani afikapodi apasidwat ndalama kut akhale chete ndipo mulungu agwesere mulili mkabudura mwawo Kuti zokozera zawo zinyenyeke kuti AZIWE phamvu ndiukulu WANU mulungu wanga chilimat sadakwake ,osalakwq kwambili ndiuyu chakwerayi

  • @samsonpadiwa9185
    @samsonpadiwa9185 2 дня назад

    Ndipo inu ka pangolin kamakhala chikwama mpaka kumugwira ndege ikulu ikulu osayipeza😂😂😂

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i День назад

    Manganya umuziwe yesu ndiukachenjede wakoyo kupusa kwako Michael usi Mzimu wa chilima ukusate ndikukantha kwambiri

  • @PraiseCedar
    @PraiseCedar 14 дней назад +2

    Unali bho koyamba kuja koma zalowa nsanje kwinako

  • @AjudantFombe
    @AjudantFombe 10 дней назад +1

    Mudziwa bwanji chilungamoa Malawi ambili ndi osaphuzila ndipovuta

  • @NaomieBanda-t6g
    @NaomieBanda-t6g 6 дней назад +2

    Ndava chisoni

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 6 дней назад +1

    Eyadi ndemweyooooo

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z 5 дней назад

    Pokhapo pokakamila u president next term, munawonesa kuti chilima simumamufunila zabwino.mukayakha kwa jahjah.

  • @user-so7wg6ii5m
    @user-so7wg6ii5m День назад

    Bambo inuo ambuye akutetezeni mwayankhura mau amphamvu kwambili ndipo mizimu yanthu amene anamwalira pangozi imeneija iwazuze achakwera komaso onse amene anatenga po gawo ambuye muchite nawo

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 11 дней назад

    Kkkkk mimba zilikhutchu Ngati ogulitsa tomato oola kkk Koma big man

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 5 дней назад

    Inu ndiye mwandilizaaaaa ineeeeeeeeee maliro awa ,A chilimaaaaaa inuuuuuuu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 5 дней назад

    Chichakwera chakupa galu wacha be chabe kupa andu osa lakwa chaka chamawa ndipa fup mtikumana mbusi simenesi achakwera 😢😢

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk 14 дней назад +1

    Ndipo Inu eee ziko ili likupita kuti ndipo ine zundiwawa ndisaname ngati ndikufa ndife koma kumalawi anthu tili ndi mantha kwambiri

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du 6 дней назад +1

    Amalawi ndi amantha size😢😢😢

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 14 дней назад

    Yes ambuye atithandize abale eesh💔💔so sad

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i День назад

    Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale
    Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 3 дня назад

    Zimenezi amalawi onse akuziwa zimenezi koma akuopa kuyankhula chilungamo monga chimenecho Mulungu akuteteze kuti upitilize kutiya khulila ku Mtundu wathu..

  • @jamessheki4293
    @jamessheki4293 5 дней назад

    Iwe ndiye munthu, Malawi tulo anthu kutipusitsa chonchi,tingoyang'anila ngat nkhuku mkhola ikaphedwa imodzi zina zimangoyang'ana. Mmmmm

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 6 дней назад +1

    Koma nde zoonadi ndithu watsala iyeo akuwona ngt sadzafa

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 дней назад +1

    Kulankhula chilungamo mopanda kuopa

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 14 дней назад

    ❤❤

  • @user-gi1gh9ry6h
    @user-gi1gh9ry6h 13 дней назад +1

    Zoona anthu oyipa kwambiri magazi alimanji mwawo 😅😅😅

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 12 дней назад +1

    Bambo ndithu mwapeleka mitu akanakhala kuti amawelenga kapena kumvela ma media mwina akanaphuzira zina

  • @AbnormalMk
    @AbnormalMk День назад

    Nkhani ya Straight 200%

  • @ChilangoNdalama
    @ChilangoNdalama 11 дней назад

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 12 дней назад

    Ili ndi pemphero la Ana a Mulungu,, ndipo akuona ndi kumva msozi wa aliyense... Mudzalira nonse munatenga gawo pa imfa Ya anthu amenewa 😭😭😭😭

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z 5 дней назад +1

    Iwe ndiye walasa!

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 14 дней назад +1

    Ndifiti Manganya mwana oyipa kwambiri chisilu chamunthu ichi galu kwabasi nkhankhankha uyuuuuuuuuuuu ndimapulani awo opusawo abvutika okha mitima mwawomo

  • @RaymondKaumba
    @RaymondKaumba 6 дней назад +1

    Ufulu umeneu wa anthu a misala

  • @HamidavioletYassin
    @HamidavioletYassin 5 дней назад

    Akuti pangolini imakhala chikwama koma mumayigwila kukanika kuyipeza ndege koma yayikulu ngati imeme ija eshiii malawi walila ndithu

  • @HopeSaka
    @HopeSaka 13 дней назад

    Mwatilankhulila father 😢😢😢

  • @SebastianSauwa
    @SebastianSauwa 9 дней назад +1

    Akuopa kumangidwa

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 6 дней назад

    Osawopa osatopa osafooka 💪🔥🔥🔥

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 14 дней назад

    🔥🔥🔥

  • @manfredzalirabetha2440
    @manfredzalirabetha2440 5 дней назад

    Mpakana kumupha mzunu kamba ka mpando wa u president ngati kuti malawiyu ngwa amanu mukuona ngati mupitilizabe kulamulako?? Anyani agalu inu anthu oipa

  • @TressLuka
    @TressLuka 13 дней назад

    Nkhaniyo ndiyonaaa kapena 😂

  • @GRACEKUMWEMBE-rv2se
    @GRACEKUMWEMBE-rv2se 4 дня назад

    Aaaaa ndinu ophwasula ingopitani ku police mukanene umboni wanuwo