Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.
Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry
I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected
As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya
Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law
Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
Akulu eeee apa pa kanakhala kuti Pali anthu 10 ngati inu ayi dziko bwenzi likuyenda bwino. I like your style brother ❤
Manganya ndi mfiti yotheratu ndagwilizana nazo
Mwandiyankhulira bwino kwambiri. Ama radio onse sakuthandiza a Malawi. Kulephera kunena chilungamo zoona??? Amalawi muzichangamuka please!!! Ku Church ko mumapemphera chani? Ama Wailesi simunathandize or pang'ono, ndipo tataya nanu chikhulupiliro ma Radio 📻 oyipa panokha.
Ma radio osathandiza a mmalawi muno bola limpopo basi iyaa
Bora Limpopo FM yoha basi komanso ndi imene inasegula maso amalawi kuti ndege yagwera kuchikanga komaso anthu amwalira shame mawayiesi oyima panokha Lero ndimasiya kalekae kunvera hot current.yanga ndi Limpopo FM, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
Mizimu ya wonse omwe adawapha pa ngozi ya ndege ija iwanzunzedi anthu amenewa
Posatengera CHIPANI chilima adachita kuphedwa kumene achakwerawo akudziwa Koma pot CHOIPA chimakanidwa sangamvomere Koma MULUNGU akudziwa
Zoona
Mau amphavu awa vuto anthufe nsanje too
Mulungu apitilize kitiululira zinsisi
Vuto ndilot athu ena akuikira kumbuyo athu afitiwa athu ot akudalira mitsokho yathu Kut antchedwe olemera mipando akupheranayo nditimisokho tathu toja deleri kuzolowela Moyo osagwira ntchito Moyo opatsidwa zaulele chakwera wayetsa Kuno Ku church Kut udzilandila chakhumi mabatile ako
But how manganya did this? he looks like a sheep but he is a bad person, here Boni Kalindo is being punished because of this man eish that's very sorry
Ndipo manganya siwakuno mayi ake ndi aku Zimbabwe muzikaona kuchenjera ngt akuba nkhuku😅😅
Kkkkkkk ngati akuba nkhuku???koma ndaseka
I was wondering how mr michael usi allow to bi a vice president as he was a vice president to late chilima😢😢 we was all.shocked to bi honest usi sanaganize bwino ...indeed they need to comfess ngati amakhulupiliradi Mulungu ....i salute you my brother n may u always bi protected
💔💔💔💔mpaka pano ineyo ndmangoona ngati a CHILIMA alipo sanamwalire ai.. I will still missing him in my heart ❤️ forever 😭😭😭
On point❤❤❤❤
Chilungamo kuwawa
Voice ya nzeru❤
Amene anapha chilima panya pake 😢😢😢
Dosanama munthu Uyo walankhula mau wogwilika kwambile
Micheal Usi ndi munthu ozikonda kwambiri.zoona zake zaoneka zokha chifukwa iyeyu sakadalolera kukhala Vice President.Koma abale ndalama zovuta ndithu
❤❤❤❤❤❤my point president chakwera out
Well spoken my brother we can't keep Quite on what happened in our National, we are still mourning all who died on that day ,it SAD.
Manganya ndi fiti panya pamake plus chakwera 😢😢
Muli speech yamphavu ndipo boma ili Mulungu achite nanu
Ndipo zoona tatiyeni a Malawi tionetse mkwiyo wathu Maliro ndiye tinayika kwa tsalano tithane ndizigawengazi😢😢😢😢
And is true chakwera akukhunzidwadi and i have more questions
As for radio and tv extension I can agree I was expecting too for them kupangitsa conference yofusa mafuso representing people mafuso amene akufusa. Koma zinazo kaya
Ndipo kukumangan inuyo. Ndizakhala numbar one kusonkha ndalama yokuombolelan mmmmmmm
Kkkk km support iyi
@@user-jn2oc3cn3qkkkkkkk kwachema
Chilungamo chiyende ngati madzi 😂😂😂
Iponden fadah 🎉
The power of massage and the power of prayer indeed
Inu mwayakhula mawu ife tikuwopa kuyakhulapo mwatilakhulira mulungu awakanthe kopotsa
Sanayankhuleponso amangophwisa mkhutu wa udindo usi
Not all days are Sundays
God is watching and may there souls rest in peace 🙏
Mulungu akuona zonse,,, ndipo samagona tulo. 😭😭😭😭😭
Deotoronomy 29 ; 29 verse the secret things belong unto the Lord our God: but those things which are revealed belong unto Us and to our children ever, that we we may do all the words of this law
Manganya mpando kumeneko sanjoya akachita chibwana mkwiyo wa Mulungu umukantha koopsa tikupempheratu magazi a Chilima aja ayankhula usazione ngati wachenjera
Powerful message Duuu may their souls rest in peace ✌️
Inu ndiye mwanena zoona brother mmmmmh ulemu wanu Inuyo shaaaa Ndamva nanu kukoma zedi❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Koma izizi tu we are praying kuti Mulungu alange aliyense amene anatenga gao lokupha chilima pompano asadikile chiweluzo
Mau amphamvu
U are talking sense
So heartly broken dear
Yesu anapelekedwa chifukwa cha ndalama yochepa,God have mercy
Nawoso mayiko usi mbusi yamunthu kukonda ndalama kumeneko mpaka kulolela Kuti munthu ampedwe ndalama abale God bless you mukutidzegula mithu
Chi Michael usi manganya that why amuika pa mpando iyeyo kuthamanga kukakwera pa mpando pakamaso gwaaaaa manganya
It's true my brother that's sad
Yes may God perform wonders that the truth must prevail
Zoona ❤❤❤❤❤❤❤
Osaopa osafooka tizafera mbendera yathu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Bakili muluzi tv yekha akalowa kumwamba bro kuyankhula mowonatu
You will pay for it, what's wrong did our SKC do to you😭😭😭😭😭 the day will come 😢😢😢
Osaopa osafooka tiime pa chilungmo dziko lino nditose ndopo mbendera yake ndiii🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼situkukuopami😢😢😢😢
Basi poti kulibe mulandu okupha ndimphezi ...mudiyeni chakwelayo azasowa omusumila
manganiso anu ameneyo okay alibwino
Enanu mudakangosiya kucommenter Ngati sizikukumvekelani bwino Ife nde tikumva kusekemela chipepeso chathu timachipeza kuzela kwaanthu amenewa chilima wathuuuu tizamfela
Zoonadi manganya ndi munthu oipa sanayakhulapo za imfa ya chilima
Ndi Ana omwe akudziwa
Zoona awa ndiye mau bro end I love you so much brother ❤🎉🎉
Ambuye tipheleni Chakwera 😂😂😂😅😅😅
AMEN 🙏
Zoonadi brother ife tikulira ndithu esh infa ya chilima mmmm😢😢😢😢 mulungu 😢😢😢😢
Ameni amen misonzi ya wanthu osalakwa simapita pachabe
Ndpo mabala akutiwaw
Komad manganya anatidabwitsatu palibe chimene anayankhula pa za imfa ya Chilima an angokhala pheeee ngt sizikunkhudza zombvetsa chisoni kwabasi Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse
That’s true brother if it was khozi ya ndeka suit no trousers no shoes my
Zoonadi inenso ndikusiwa cho cho
Ndipoh zoonadi mwalakhula bwino ndithu broz man
Atola khani afikapodi apasidwat ndalama kut akhale chete ndipo mulungu agwesere mulili mkabudura mwawo Kuti zokozera zawo zinyenyeke kuti AZIWE phamvu ndiukulu WANU mulungu wanga chilimat sadakwake ,osalakwq kwambili ndiuyu chakwerayi
Ndipo inu ka pangolin kamakhala chikwama mpaka kumugwira ndege ikulu ikulu osayipeza😂😂😂
Manganya umuziwe yesu ndiukachenjede wakoyo kupusa kwako Michael usi Mzimu wa chilima ukusate ndikukantha kwambiri
Unali bho koyamba kuja koma zalowa nsanje kwinako
Mudziwa bwanji chilungamoa Malawi ambili ndi osaphuzila ndipovuta
Ndava chisoni
Eyadi ndemweyooooo
Pokhapo pokakamila u president next term, munawonesa kuti chilima simumamufunila zabwino.mukayakha kwa jahjah.
Bambo inuo ambuye akutetezeni mwayankhura mau amphamvu kwambili ndipo mizimu yanthu amene anamwalira pangozi imeneija iwazuze achakwera komaso onse amene anatenga po gawo ambuye muchite nawo
Kkkkk mimba zilikhutchu Ngati ogulitsa tomato oola kkk Koma big man
Inu ndiye mwandilizaaaaa ineeeeeeeeee maliro awa ,A chilimaaaaaa inuuuuuuu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Chichakwera chakupa galu wacha be chabe kupa andu osa lakwa chaka chamawa ndipa fup mtikumana mbusi simenesi achakwera 😢😢
Ndipo Inu eee ziko ili likupita kuti ndipo ine zundiwawa ndisaname ngati ndikufa ndife koma kumalawi anthu tili ndi mantha kwambiri
Amalawi ndi amantha size😢😢😢
Yes ambuye atithandize abale eesh💔💔so sad
Tiyeni tisiye kumvera ma wayilesi akumalawi chifukwa wonse anaguidwa kale
Bora Limpopo FM radio, Bakili muluzi tv ndi Boooorn kalindo ndi okha amene akutiuza chiungamo
Zimenezi amalawi onse akuziwa zimenezi koma akuopa kuyankhula chilungamo monga chimenecho Mulungu akuteteze kuti upitilize kutiya khulila ku Mtundu wathu..
Iwe ndiye munthu, Malawi tulo anthu kutipusitsa chonchi,tingoyang'anila ngat nkhuku mkhola ikaphedwa imodzi zina zimangoyang'ana. Mmmmm
Koma nde zoonadi ndithu watsala iyeo akuwona ngt sadzafa
Kulankhula chilungamo mopanda kuopa
❤❤
Zoona anthu oyipa kwambiri magazi alimanji mwawo 😅😅😅
Bambo ndithu mwapeleka mitu akanakhala kuti amawelenga kapena kumvela ma media mwina akanaphuzira zina
Nkhani ya Straight 200%
❤
Ili ndi pemphero la Ana a Mulungu,, ndipo akuona ndi kumva msozi wa aliyense... Mudzalira nonse munatenga gawo pa imfa Ya anthu amenewa 😭😭😭😭
Iwe ndiye walasa!
Ndifiti Manganya mwana oyipa kwambiri chisilu chamunthu ichi galu kwabasi nkhankhankha uyuuuuuuuuuuu ndimapulani awo opusawo abvutika okha mitima mwawomo
Ufulu umeneu wa anthu a misala
Akuti pangolini imakhala chikwama koma mumayigwila kukanika kuyipeza ndege koma yayikulu ngati imeme ija eshiii malawi walila ndithu
Mwatilankhulila father 😢😢😢
Akuopa kumangidwa
Osawopa osatopa osafooka 💪🔥🔥🔥
🔥🔥🔥
Mpakana kumupha mzunu kamba ka mpando wa u president ngati kuti malawiyu ngwa amanu mukuona ngati mupitilizabe kulamulako?? Anyani agalu inu anthu oipa
Nkhaniyo ndiyonaaa kapena 😂
Aaaaa ndinu ophwasula ingopitani ku police mukanene umboni wanuwo