Asilikaliwo amene akufalitsa bodzawo ndi a bodza ngati enanu bwanji sakupita ku court kukanena umboni wawo anthu mwazolowera ku pachika mayina a anthu apa cholinga wina ayipe inu mukome mukolola zomwezo bwanji osatchulako makolo anu mukunena anthu ena muferatu momwemo mu bodzamo ndiye pali phindu lanji zikuwoneka kuti ena 8 aja si anthu koma chilima basi kudafatu anthu enieni kunja kuno alikuti kili ziiii amapita kumanda nanga inu ndi ine mudzapita kuti kwa anthu andale kapena kumanda kumaganiza 😅😅😅😅😅 awa
Apite ku khoti for what? Timapereka umboni popanda mulandu? Ku khothi siku polisi tu tizidziwa zimenezo! Pakuyenera pakhale mulandu ndiye iyeyo nkukakhala mboni
@@user-qb4pj5yy5b ndiye siyani kulankhula zopanda umboni akutumani a ndale eti mukhalila yomweyio munthu anafa basi mwatsala inu ndi ine dzimvereni chisoni nanga bwanji asakatsegula mulanduwo mukungubwebweta pasi ngozi ya ndege mumayidziwa inu paja mkuyamba ku Malawi kuno eti ndiye ngoziyi yangokumaba ndi mbuli zomwe
Tathokodza potiudza koma usanapite machende ako bwanji unalolera kuti chilima afe chotelo iwe pokhala nsilikari nyini yamako and u chakwera nyini yamako😢😢😢😢 RIP Chilima
Simunati mutuluka mizimu ya anthu amene Aja ikudzuzani zedi ndipo muulurana wat is 10 million after all ndalama malo moyendesera dziko mukupangira uchigawenga inu agalu kwambiri.
Mulungu wanthu sazagona tulo mpaka mwazi wa anthu omwe anafa pa ndegeyi utaonesa Chilungamo Romand Catholic Les prayers so hard mpaka Mulungu atationesa choona
1. Utchule dzina lakoo osati komwe uli.... Chifukwa komwe ulikoo ndikoti akafika sampeza munthu koma dzina lo akhoza kulipeza mosavutaaa 2. Bweraani poyela bwino bwino kuti anthu ayitsate nkhani yi mwatsatanetsatane.... 3. Osamabwera ndi nkhani zabhoza apa where your facts are not straight!!
Ambuye landilani mizimu ya abalewa amene mwawayitana kubwera Kwa Inu chitilani chifundo midzimu Yao pamozi ndi vice president Chilima Mulungu wamphamvuzonse landilani mizimu
Boza ili, paja nvula ikagwa kuchuluka zoliralira, nanga ndege inachita kutela kapena kuphulisidwa? Mesa inagwa kusowa choyakhura eti amalawi tili ndi khwiyo pa ifa ya anthu amene aja ndiye osamatiuza boza ngati limeneri.
MA CADET MULI PA CHINTCHITO CHA SATANA MDYEREKEZI KWAMBIRI KOMA DPP CAN'T WIN BECAUSE OF PLANET CRASH OF VP. WE ARE STILL RECALL WHAT EVIL WORKS DPP HAS DONE TO INNOCENT BLOOD OF ALBINISM. GOVERNMENT VEHICLES WERE MISUSED TO AS POLITICAL PROPERTIES TO KILL THE OPPONENTS. SHAME ON YOU CADETS.
Bwanji wangotchula kuti ukupezekera ku zomba Barack while ku zomba kuli air wing kuli cobbe kulinso changalume and rank number Yako sunatiuze and why sunanene early because iweyo izizi ndekuti unazidziwa zisanachitike nde utha kuwauza anthu za Zina zimenene zikufuna zitadziwidwa kuti zili pati and zinaenda bwanji anatenga ndi ndani mafuso ngati amenewa utha kuyankha?
Inu uyu ndi ndiwaboza mukumva akuti analandila ma 10 mita ndie ngati analandila avutikiranji kunena kuti amusake,koma munthu uyu ndiomvesa chisoni ndipo ndi kapunthabuye alibe chomwe akuziwa even malongosoledwe anta ongooneseratu kuti Ali blank,nkhani zongotolera kuti ena amakamba pena pake sizimasowa.Ukuona ngati akukondwa ndi angati ?ase samala ufera zaweni ngakhale ulibe gawo koma chokhacho chongobwelesa pa social media ukutitaisa time.
Asilikaliwo amene akufalitsa bodzawo ndi a bodza ngati enanu bwanji sakupita ku court kukanena umboni wawo anthu mwazolowera ku pachika mayina a anthu apa cholinga wina ayipe inu mukome mukolola zomwezo bwanji osatchulako makolo anu mukunena anthu ena muferatu momwemo mu bodzamo ndiye pali phindu lanji zikuwoneka kuti ena 8 aja si anthu koma chilima basi kudafatu anthu enieni kunja kuno alikuti kili ziiii amapita kumanda nanga inu ndi ine mudzapita kuti kwa anthu andale kapena kumanda kumaganiza 😅😅😅😅😅 awa
Apite ku khoti for what? Timapereka umboni popanda mulandu? Ku khothi siku polisi tu tizidziwa zimenezo! Pakuyenera pakhale mulandu ndiye iyeyo nkukakhala mboni
@@user-qb4pj5yy5b ndiye siyani kulankhula zopanda umboni akutumani a ndale eti mukhalila yomweyio munthu anafa basi mwatsala inu ndi ine dzimvereni chisoni nanga bwanji asakatsegula mulanduwo mukungubwebweta pasi ngozi ya ndege mumayidziwa inu paja mkuyamba ku Malawi kuno eti ndiye ngoziyi yangokumaba ndi mbuli zomwe
ndipo apite akamange palibe zoti akunama ndizoona zinachitikadi
Uyu akuyenera kutengedwa ndi akubanja akalongosole bwino ...chifukwa ali nawo mu gulu lakupha
Tell us where is blackbox?
Mulungu amakanda munthu onena chilungamo iwe msilikali mulungu akukhululukile pazimenezi koma tikuthokoza ponena chilungamo usasiye pitabe chitsogolo oipa aoneke pa mbalambanda 😂😂😂😂😂
Only JAH knows....everyone shall get paid according to works he has done🔥
Limenelo ndi bodza lochita kupeka. Iweyo bewanji upite ku Police nkukaperekela umboni umenewo. Chimene ukuopa nchani? Wasowa chonena!
Olo zimakhala zoona sangamusiyesiye atanena komano ndioipa yekha atinanalandira ndalama
Uchitsilu mukananena anthu asanafe ndinu m'Modzi mwakuphawo
Stop taking weed +Ambuye ntengeni Bro
Udye ndalamayo usaope usachite matha nyani iwe unatani kuulura zisanachitike mwana wanjoka iwe
Iwe tiye uko vyaboza
Fake news
Thanks for providing us you service
MUZIDZIWA MULUNGU.. ZITICHEDWERSA IZO. MUBWERETSE UMBONI MWACHANGU... TIMVE # YANUYO. YA ZOMBA. PRAISE GOD
Ndaika muzimu wa malemu Chilima manja wa Mai maria. Proud katorika / Lusaka Zambia
Nzelu mulibe Mai maria atan
Eshiiii mulungu amakondwera ndi munthu ovomera tchimo lake inutu mwayamba bwino ingomalizani Kuti anthu tidziwe chowonadi
Example kenya , anthu aku kenya anasiya kupembeza boma lakuba ,
Ife amalaw wachuluka ndi umbuli .
10 mita kupha munthu za Bodza ngat izi 😂😂
Zopanda ntchito tonse timaziwa kuti tidzafa koma sitikuziwa mmene tingazafere
Tathokodza potiudza koma usanapite machende ako bwanji unalolera kuti chilima afe chotelo iwe pokhala nsilikari nyini yamako and u chakwera nyini yamako😢😢😢😢 RIP Chilima
Eeeee bosss
Zaboza ngat nkazi wako ndiwopemphera uma chitiranji zimenezo
Koma munalakwa kwambili munapha muthu ofunika kusiya zitsilu komaso ndale zophana zinatha kale kale kupusa kumeneko adzakuvoteleni ndi Amanu😢😢
Kabwezeni ndalama zo pemphelani pemphero lolapa lonsweka tima mulungu akukhululukirani mupite poyela kukabweza ndalamazo 😂😂😂😂😂
Eyaaa.apangedizomwezo
Malankhulidwe anu zikuonetsa kuti ngakhale 8 simunafike, mumagwira ngati ndani ku airport?
Ndiwe chitsilu kwabas bwanji sukwatchula anzakowo nanga
Simunati mutuluka mizimu ya anthu amene Aja ikudzuzani zedi ndipo muulurana wat is 10 million after all ndalama malo moyendesera dziko mukupangira uchigawenga inu agalu kwambiri.
Zikundimvekela ngati zaboza mukufuna kungotipusisapo
mukusowa zochita mmene mumvekeramu mungakhale ten million kulira ndi umphawi
Ngati mukufuna kutchuka muneneee
iweyotu ukunama ndipo palibepo chikumveka panfundo zakozo usanamize ndipo usasokoneze anthu ndi bodza lakolo
Akulu zopanda nzeru izi.
Koma zovesa chisoni kwambiri kumpha anthu wosalakwa chifukwa chandalama Koma ndi zoonadi Kuti pamene pamphedwa munthu osalakwa mulungu amaulula zitsitsi. Zobisika 🙆🙆🙆🙆💔💔💔😭😭😭😭
Alakhulayo panyepake
Pitani ku TIMES TV on live interview ndi Brian Banda amwene
Three mukanene
We wish you well🙏
Waboza kulankhula ngati wakurundi bwerani poyera kuti mumangidwe munthu oyipa iwe kumakapanga chiwembu
Ngati ukufuna kukhululukilidwa,bwerani poyera.
Vuto Kodi president ngati sakupanga zabwino osapanga Kuti achoke bwanji pa mpando
Looking for 1M viewers
Eish desperation is real
Wow
Chomwe mukuopa kut umbon ngat umenewu kukapereka poyera mukuopa andare coz aliyese Ali ndi mantha
😂😂😂 mulungu awakathe ndithu
Kkkkk eeiiiiish koma yaaah. Zabodza izi akukamba uyuyuzi.
Explain everything
Keep it up
Why is the government busy ku anga a Kaluw kusiya athu ngati a wawa why
AM PASTOR CHRIS PLEASE BROTHER GIVE THEM BACK THEIR MONEY,
Exactly esh
Mulungu salephela tidziwa zonse pompano mu ukulu wake alibe othandizana naye
God is great and the justice will be to an open❤
Kupusa kwako galu iwe mxiiiii😢
Mulungu wanthu sazagona tulo mpaka mwazi wa anthu omwe anafa pa ndegeyi utaonesa Chilungamo Romand Catholic Les prayers so hard mpaka Mulungu atationesa choona
Ambuye akutezereni achimwene ,azikumangirani linga tsiku ndi tsiku
Nde iweso uli mugulu lokuphalo
Youuu!
Nde osangozitchula dzina ngat mukunena zoona bwanj. Ndege yoti inaphulitsidwa ingawoneke chonchija? Komaso ndege yoti inatela inganyenyeka chonchija? Campaign yabwanj kod tiyiwone chaka chinoyi mwati
Azikatenga iwe ku zomba all the way upto Chikangawa.....Pezani boza lina sir.
Anatenga bwanji ma pilot a ku zomba nanga ?? Kumenwko kuyesela kuti muphuphe basi.
1. Utchule dzina lakoo osati komwe uli.... Chifukwa komwe ulikoo ndikoti akafika sampeza munthu koma dzina lo akhoza kulipeza mosavutaaa
2. Bweraani poyela bwino bwino kuti anthu ayitsate nkhani yi mwatsatanetsatane....
3. Osamabwera ndi nkhani zabhoza apa where your facts are not straight!!
Wabodza uyu, palibe chilungamo pamenepi
Sunanene dzina lako bwanji kodi maliro mukuona ngati chithu choseweretsa kod atakhala bambo ako ungakambe zopusa kumanama ngati ukudziwa kathu uli jufuna kusikoneza athu iwe ngati unapha ndiwe osapita ku police kukadzipereka uzilakhula zophwisa apa malilo mukuyesa zoseweretsa kod
Ambuye akuyendere mwapaderadera kuti unene zoona zokhazokha.
Mudatani kumuthawitsa osamupha inu asilikali zovetsa chisoni😂😂😂😂
Ambuye landilani mizimu ya abalewa amene mwawayitana kubwera Kwa Inu chitilani chifundo midzimu Yao pamozi ndi vice president Chilima Mulungu wamphamvuzonse landilani mizimu
10million mungagule moyo wa munthu mulungu akukanthen nonse asasiyeko or modzi
Tiutseni soona sandege live in the sauth Africa estan 😢😢
Thank you so much for replying me your welcome
Tell me all story from you soon side please I am Malawian
Koma Razalo Chakwalayo samachita manyazi konse akamaona ndi kumva zimenezi,
komatu mzimu wa munthu ndi oopsya, lero zili bwino koma mawa kaya
Ndikuzimva mwabodza
Inusotu ndinu abodza Inu, msilikali wake wakuti? Dzitchuleni dzina ndi unit yanu, msilikali ophunzitsidwa bwino angapange zimenezo ukukamba mlayiya iwe, umawudziwa uskali iwe?
Ali bado,akuyesa kwambirii
Boza ili, paja nvula ikagwa kuchuluka zoliralira, nanga ndege inachita kutela kapena kuphulisidwa? Mesa inagwa kusowa choyakhura eti amalawi tili ndi khwiyo pa ifa ya anthu amene aja ndiye osamatiuza boza ngati limeneri.
Zowona ndiye ndiziti malume?
@mishecksipolo71 mukavele yomwe watumiza lero mukhulupilila kuti ndiwaboza apa anati ndimusilikali anali kuchikangawa lero akuti anajambula dege ndiyeyo ku airport amalawi tiyeni tiseguke chonde anthu azikusewelesani chochi koma ambuye amukhululukile sakuziwa chomwe akupanga
MA CADET MULI PA CHINTCHITO CHA SATANA MDYEREKEZI KWAMBIRI KOMA DPP CAN'T WIN BECAUSE OF PLANET CRASH OF VP.
WE ARE STILL RECALL WHAT EVIL WORKS DPP HAS DONE TO INNOCENT BLOOD OF ALBINISM.
GOVERNMENT VEHICLES WERE MISUSED TO AS POLITICAL PROPERTIES TO KILL THE OPPONENTS.
SHAME ON YOU CADETS.
Koma2 anthu inu mwasowa cholakhula 10 million ndi ndalama? 😂😂😂
Once a snack always a snack. Sitinaiwale chipani ichi.
Wa Dpp iwe
Rest in peace SKC
Ukalapa mulungu amakukhululukila zoyipa zako bola ukayima muchowonadi ndipo mulungu amakhala kumbali yako mulungu ndiwazatheka bwanji pitilizani kuwulula kt satana achite manyazi
Eish aaa
Following 🙏
Inu muli ndbodza Inu iwey sindwe msilikali ayi wangodzeramo ukufuna kungoypitsa munthu bas nde cholinga chako ife tikudzwa kut nd ngoz and ikanakhala fut anthu akanava kut akuombera nde pita nazo uko zamkutu zakozo usatiwawitse mutu apa
Galu wachabe chabe uyu iwe umakatani kuchikangawa kuchoka ku Zomba? Bwanji osanena nthawi yomwe ija anthu tikusowa Mtengo ogwira? Ukamanama chonchi ukupempha tsoka kwa mulungu
God is great
Aaa 10 mita kandalama kochepachepa, kupha president kumafunika ma 50 mita
😮
Munalakwisa kupha ose komanso ndiwe chisilu
Anthu adyera awa oyiwara mwachangu,nawonso adzafa..
Zomvesa chisoni kwambiri mmm
Mmene umalandira umaona ngati mukukapha ziwala? Lero udziti ukulephera kudya ndalama 😢
NDIWE MUNTHU OPANDA CHIKONDI BWANJI SUNADZIWITSE NTHAWI YOMWEYO KUTI ANTHU APULUMUTSE MIYOYO YA ANTHU? KOMANSO IWEYO ULI NDI UMBONI OKWANIRA BWANJI OSAYITANA MABANJA OFEDWA NDIKUWAUZAKUTI TIYENI KU COURT NDIRI NDI UMBONI? MUNAPHANAWO CHIRIMA NDI ANZAKE,BAMBO MLANDU MULINAWO
Mbuli yimeneyi yikupusitsa ndani APA.
Anapha munthu ofunika kwambili,,ndipo the truth will come out soon
Chikhala ndiwe oyima pa chilungamodi ukanadzutchula dzina
Mmmmmm kaya God knows ife kunalibeko
Bwanji wangotchula kuti ukupezekera ku zomba Barack while ku zomba kuli air wing kuli cobbe kulinso changalume and rank number Yako sunatiuze and why sunanene early because iweyo izizi ndekuti unazidziwa zisanachitike nde utha kuwauza anthu za Zina zimenene zikufuna zitadziwidwa kuti zili pati and zinaenda bwanji anatenga ndi ndani mafuso ngati amenewa utha kuyankha?
Chakwera munthu wakupha uyo izi zayenera kuyamba ndinu bomwe asilikali.Mukusekelera zinthu zopusa kupha anthu amtundu wanu womwe mkwiyo wa Mulungu ukukanthani ndithu,Muuzane inuyo asilikali muyambe kukantha Lazaroyo ndi akubanja ake onse
Atakumangani madzinvetsa chisoni Aaaaaa opusa iwe
Nawe camba chakukwana, tinzakhulupilira ukapita ku khoti kukasuma mlandu wakupha, udye ndalama yo, ukananena time yomwe amakokedwayo😂 ndie kut iweso akanakupha, ndie ndipamene tikananziwa kut wafa bwanji pomwe ndege munakwela athu 9, iweo kukhala WA ten, zaziiiii
Inu uyu ndi ndiwaboza mukumva akuti analandila ma 10 mita ndie ngati analandila avutikiranji kunena kuti amusake,koma munthu uyu ndiomvesa chisoni ndipo ndi kapunthabuye alibe chomwe akuziwa even malongosoledwe anta ongooneseratu kuti Ali blank,nkhani zongotolera kuti ena amakamba pena pake sizimasowa.Ukuona ngati akukondwa ndi angati ?ase samala ufera zaweni ngakhale ulibe gawo koma chokhacho chongobwelesa pa social media ukutitaisa time.
Adanenakare achakwera Kuti alorela kukhetsa mwaz
Zoona izi ndithu
Is this real?
Audikira kufuza kwabomakaye akakanama bodza abomao ndipamene akapite kukhot
Kkkk msilikalli opusa wapha nawo
Iweso Sono ndwe wakupha ndye usawoneke ngt dolo ai chfukwa iweyo ngt umafuna kukhala Muthu wabwino ukanaulula pomwe amakupasa ndalamapo osati zithu zachitika kale ndikumaulula kungofuna kumuipisa Muthu bas ulibe umuthu iwe bwera poyera ngt ukukamba zazeru ukubisala bwaj
Asilikali ake ambwiyako amene anakuphumzitsa kuuluka aja..
Koma Chakwera why? Achewa ndithu ndinu oipa ndawonela Chakwera koma mulungu akukantheni tikuona ndithu