MCP yatengesedwa ndi nyamata wa ku Ntheu. Chakwera alibe mtendere wamtima

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 14 окт 2024

Комментарии • 146

  • @austenbushiri-cx1kh
    @austenbushiri-cx1kh 2 месяца назад +14

    Mawu! mawu! 🎉 big man

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 2 месяца назад +18

    Zoona zake Zenizeni koma osadera nkhawa chaka chamawa kuvuta am from Ntcheu kwataine village koma mlungu adzatiyakha osaopa osafooka osatopa❤

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 2 месяца назад

      @@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba

    • @FrankSimfukwe-w1s
      @FrankSimfukwe-w1s 2 месяца назад

      Ndipo sitikuopa izisitikungokamba chabe km sitikuopa ife tikufuna chilima wathu chomuphela ndichani atiuze chomwe anawalakwila iwowo

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 2 месяца назад +4

    100%facts brother mcp ndi zigawenga mbiri safuta lero taziona yalembedwaso ina apa.

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 2 месяца назад +21

    Amalawi tonse timadziwa kut Chakwera anapha chilima mosogozedwa ndi Michael usi

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 2 месяца назад +2

      @@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 2 месяца назад

      @@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe
      Chikhulupiliro sagula
      Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu
      Mark 14:48
      (Yesu sanamugwire )
      Mark 15:21
      (Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo)
      Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka

    • @EdwinHowardmkandawire
      @EdwinHowardmkandawire 2 месяца назад

      Iweso kapolo ndege ija ankayendesa ndi chakwera?

    • @EdwinHowardmkandawire
      @EdwinHowardmkandawire 2 месяца назад

      ​@@yowasschitsosa5348kuswa zonene anthuwa

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 2 месяца назад

      @@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 2 месяца назад +10

    Komanso kufatsakwina ndikopweteketsa ,
    Kufatsakwina ndikopusanako ,
    Amalawi ndife anthu ofatsa mopusa

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os 2 месяца назад

      Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.

  • @MeriaMasinga
    @MeriaMasinga 2 месяца назад +4

    Olo Monica akuziwa kt amunanga apha chilima

  • @PIYASSFKGCHIWAYA
    @PIYASSFKGCHIWAYA 2 месяца назад +11

    Ulemu wanu brother

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 2 месяца назад

    Osatopa osafooka osawopa 💪💪💪 chakwera machende Ako aise

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 2 месяца назад +1

    Brother More Fire 🔥....Auza Amenewo....Nthawi zonse chilungamo chimamphweteka muona mufa nd ma BP. MCP yakumpha

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc 2 месяца назад +9

    Mukunena dzona brather m c p kwake kuba ndi kupha

  • @AjibuTwalibu
    @AjibuTwalibu 2 месяца назад +8

    Mmmm man mwalankhura zoona ok

  • @Lingstone-r3z
    @Lingstone-r3z 2 месяца назад

    To stand on the bright side with truth and faith for all Malawian ❤

  • @LouisAndrew-jr1yj
    @LouisAndrew-jr1yj 2 месяца назад

    Ukavomereza kuti Yesu ndi Ambuye, udzapulumuka🙏🙏

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 2 месяца назад

    Well spoken my brother ❤❤❤

  • @TriciaMalikebu
    @TriciaMalikebu 2 месяца назад

    Well said bro

  • @esaMoha-dm4kj
    @esaMoha-dm4kj 2 месяца назад +6

    Bg ulemu wanuw mulungu adalise inuyyo nkwamasinku osse tiutseni soona sandege bg mn ashankwela angompedwa nawosso sikut wawaw kobas skc anashita nkumupha ndi ashankwela yemwyyo mfiti yyamundu😮😢

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 2 месяца назад +2

    mcp tidakwilira limodzi ndi chilima zimu uwakwatha Wina ayelekeze kuyimila ku ntcheu mcp timpha timuyatsira nyumba osatiseweletsa😢

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 2 месяца назад +2

    Ndi chipani chakupha chimenecho Cha MCP ndikukuba ndiye chitukuko chawo cha MCP basi

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 2 месяца назад +1

    Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.

  • @peterlowole7841
    @peterlowole7841 2 месяца назад +4

    Malawi ife ndife amantha ausilu , big mwalankhula ngamo Amen

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona 2 месяца назад +4

    Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 2 месяца назад +12

    Iye uja mpaka azafa akuzuzika

    • @yowasschitsosa5348
      @yowasschitsosa5348 2 месяца назад

      @@bamusmajawa1619 munamatu simulungu ameneo and palibe munthu ali ndi mphavu yotembelera mzake,

  • @LinesiKanzota-fw7sj
    @LinesiKanzota-fw7sj 2 месяца назад +1

    Zowonadi ndi zowawadi chakwera ndi Muthu oyipa

  • @StevenGJohn
    @StevenGJohn 2 месяца назад

    Chilungamo aise Chakwera ndiyemwe anapha Chilima chifukwa cha udindo

  • @ElphinaChirwa-qk3cy
    @ElphinaChirwa-qk3cy 2 месяца назад

    Straight talk eeeee anthu munatipweteka kwabasi imfa iyiyiyi
    Ndipo mabala akupweteka

  • @LilianMbaisa
    @LilianMbaisa 2 месяца назад +1

    Ndipo asabweredi

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 2 месяца назад +2

    Zoona mcpbinapha chilima zoona chakwera akuziwa ndipo ife ku mwera tizailowerela amaona ngati amalawi ndiopusa

  • @GiftMlinde
    @GiftMlinde 2 месяца назад +1

    Kwambliii Mr your talking the truethhh

  • @JosephChikabadwa
    @JosephChikabadwa 2 месяца назад +1

    Ngakhale Mulungu Kumwambako akuwona Lingatalike bwanji Tsiku Lina Oyipayo Adzagonja Ndithu Mulungu Wathu Ndiwam'kulu Ali ndi NTHAWI YAKEEE AYANKHA M'mapemphero Athu

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 месяца назад +2

    Komaso kuyakhula chilungamo MCP sikanawina kapanda chilima olo akamayakhula mwamatama akhala dzaka zingati osawina

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 2 месяца назад +6

    Ndipo zowonadi zake. Ulemu umasowa.

  • @MarcosDjussa
    @MarcosDjussa 2 месяца назад

    Zoonad brother umakwana

  • @StevoZimba
    @StevoZimba 2 месяца назад +1

    Wa Bakili Muluzi VT amanena zoona😊

  • @JosephNambazo
    @JosephNambazo 2 месяца назад +1

    Catholic bishops are very sharp amaima pa chilungamo Mcp ndi yokupha

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 2 месяца назад +6

    Mau amenewo mulungu akudalisa mcp ndi yakupha auzeni ndi mbusi za anthu awa

  • @KaungaYawaka
    @KaungaYawaka 2 месяца назад +3

    Chakwera ndiwakupha vuto anzathu achewa kuberekana nde chimene chikumlimbisani mtima mumadya naye

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 2 месяца назад +2

    Walankhula bwino brother

  • @RafiqueChibwana
    @RafiqueChibwana 2 месяца назад +5

    Inuyo mwalankhuladiii boss ulemu wanu

  • @JosephGeorgeJonathan
    @JosephGeorgeJonathan 2 месяца назад +4

    Osaopa man chakwela anapha chilima sibodzatso ayi

  • @BlessingsTembenu
    @BlessingsTembenu 2 месяца назад

    Zoona bro,ndipo anthu awawa ndi oyipa ndiposo ineyo amandinyasa heavy ndipo moyo wanga sindifuna kumawona,ndimava kuphweteka ndipo ineyo ndikanakha nfiti tikanaphweteka ndithu

  • @JoyceBanda-k8t
    @JoyceBanda-k8t 2 месяца назад +3

    Kuyakhula kwachilungamo chakwera anapha chilima

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 2 месяца назад

    Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 2 месяца назад

    Chakwela achoke and ngati Pali munthu woti akuyenela kumangidwa ndi chakwela ndi nduna zake

  • @WilliamLimwalwo
    @WilliamLimwalwo 2 месяца назад +3

    Zoonadi dzake, more fire,the truth will prevail 😂😂😂😂😂😂.

  • @StevenGJohn
    @StevenGJohn 2 месяца назад

    Zoona big palibenso munthu oganiza bwino angazavotere Chikangawa mcp anthu panopa ndiokwiya

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon 2 месяца назад

    😂😂😂😂 amati wina ludo kkkkkkk😅😅😅😅

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 2 месяца назад +3

    Auze aise,

  • @MrBone-zj1wq
    @MrBone-zj1wq 2 месяца назад +2

    Zitsiru zimenezo zimene zikuti zalowawa ndale,mbole zawo kwambiri

  • @EdwinHowardmkandawire
    @EdwinHowardmkandawire 2 месяца назад

    Fotseki chikwera sangasowe ntendele ndipo mutaya nthawi

  • @Paul-q2p
    @Paul-q2p 2 месяца назад +1

    Thanks brother

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt 2 месяца назад

    Ulemu waanu brother. Osawanyengelela a MCP ndi makape opanda ntchito.

  • @AlexPhiri-in1re
    @AlexPhiri-in1re 2 месяца назад

    Zoona bro

  • @misoMoyo
    @misoMoyo 2 месяца назад

    Sindikuona chifukwa chopangidwira remove nkhani aliense akuona yekha Mene zinaendera Kodi chilungamo mukufuna chotani kuchita kuoneka zokha kuti anamupha mukufunanso chani Chakwera ngoipa anatiphera mngoni wathu Rip skc

  • @JamesChiphazi
    @JamesChiphazi 2 месяца назад

    Mawu oveka chakwela dzelu alive mamuna ndi wabakili muluzi tv ameneuja amaganiza hsve

  • @kondwamlungu8384
    @kondwamlungu8384 2 месяца назад +1

    Ukuteta yayi àuze zowona

  • @EdwinHowardmkandawire
    @EdwinHowardmkandawire 2 месяца назад

    Inuyo chikhala mmaziwa kusaka ndege munkalekelanji kupita kusaka ndege a kapolo a anthu

  • @lysonkaselema7321
    @lysonkaselema7321 2 месяца назад +1

    Ntcheu ndimaiziwa ndiimeneyi

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb 2 месяца назад +1

    Chilungamo chimawawa

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa 2 месяца назад +1

    Sindinu nokha akuntchewu ai even boma lakhotakota ndife okwita big pafupi ziko lose nyani chakwela mbuzi akupha

  • @HendrickBanda
    @HendrickBanda 2 месяца назад +2

    Zoona chakwera anamupha chilima

  • @AndrewMagombo
    @AndrewMagombo 2 месяца назад +1

    Zoona anthu a mcp okumpha

  • @ElizabethMajiga
    @ElizabethMajiga 2 месяца назад

    Ndimwana yemwe akuziwa kuti chakwela anampha VP wake basi

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 2 месяца назад +1

    Ndipo live zoona zake tikuziwa bwino lomwe

  • @shadreckphiri1799
    @shadreckphiri1799 2 месяца назад

    This is the truth

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 2 месяца назад +1

    Usawope muphwanga chilungamo chake nchakuti chilima anachita kupha a mcp ndichakwera

  • @Patricklichakala
    @Patricklichakala 2 месяца назад +3

    Thanksyou big

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j 2 месяца назад +1

    Lero mutenthedwa ndi message yoti inaperekedwa kale kale mukanakhala ozindikila a MCP bwenzi siku lomwe uthengawu inaperekedwa mutaumva

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 2 месяца назад +3

    Chakwera Mutu Ngati machende amkango

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 2 месяца назад

    Chakwera ndi munthu yemwe anapha chilima ....kuyipa mtima

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 2 месяца назад +3

    Zoona zokhazoka ndithu. Mulungu Ali pampando

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 месяца назад

    Tiphe zinyau zinayi kuti tibwenze zomwe chipani cha nyau chimachita.

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm 2 месяца назад +2

    Mau amphavu bro MCP ndiyakupha idapha anthu ambiri

  • @FrankAdonis-zl6qc
    @FrankAdonis-zl6qc 2 месяца назад +1

    Ndukugwirizana nazo mbale zoonadi zimenezo mcp chipani chongokhalira kupha

  • @FrankSimfukwe-w1s
    @FrankSimfukwe-w1s 2 месяца назад

    Ife tikudziwa bwino kt anapha chilima

  • @ChisomoMsiska-oi2vg
    @ChisomoMsiska-oi2vg 2 месяца назад +2

    Koma nkulu uyu wayankhula za nzeru kwambiri

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 2 месяца назад

    Komanso ndege inagwera poyeratu eehh

  • @TimexKaufa
    @TimexKaufa 2 месяца назад

    Chilima adakwera mundenge ndi dzigawenga ndi chifukwa a mcp adakana kukweranao

  • @MaritaBanda-p4z
    @MaritaBanda-p4z 2 месяца назад

    amenewa akufunika azasinjidwe kumene komas kunena zona palibe wa mcp angapite ku ntcheu azikalakhula mbwelera

  • @ChifundoJohn-w3t
    @ChifundoJohn-w3t 2 месяца назад +1

    Zowonadi brother

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 месяца назад

    Auzeni chilungamo afitiwo

  • @JumaJuma-i9t
    @JumaJuma-i9t 2 месяца назад +3

    Ndipo kumeneko ndiye kuyankhula

  • @DesireMphatsogama
    @DesireMphatsogama 2 месяца назад +1

    Chakwera wakupha tonse tikuzwa

  • @UsenLashid
    @UsenLashid 2 месяца назад

    Zaphabvu brother

  • @LukaAfromad
    @LukaAfromad 2 месяца назад +1

    Izi nde zoona ine okhara mchewa km imfa iyi yokha idandipweteka😭😭😭😭💔💔💔

    • @spargomw
      @spargomw 2 месяца назад

      😭😭😭😭😭😭😭

  • @chipiesato-ut7hx
    @chipiesato-ut7hx 2 месяца назад

    Osaopa osatopa osafooka mcp yakupha ndizoona

  • @patassonelucaszovuta3431
    @patassonelucaszovuta3431 2 месяца назад

    Koma olo zitalowa ndale palibe vuto chifukwa anthu adafawa ndi andale ndie sindikuona vuto

  • @HarriePearson
    @HarriePearson 2 месяца назад +1

    Zoona zoona mb'ale

  • @ELLENKANJERE
    @ELLENKANJERE 2 месяца назад

    Zimawawa kwambiri ighowa ngati anali amai ake or achimwene mhu akhoza kumva motani akaona muthu akangwa pamseu anthu mosachendwa akufika pamalo ngati anali pafupi koma mmmm za chisoni

  • @CHIWSABINYAMBOSE
    @CHIWSABINYAMBOSE 2 месяца назад +1

    Kunoso ku mzimba ndife okwiya kwambiri

  • @DanielZitande-y1d
    @DanielZitande-y1d 2 месяца назад +4

    Mwakhwana brother uko ndiko kukamba

  • @SandlessWakhuluma-ns1io
    @SandlessWakhuluma-ns1io 2 месяца назад +1

    Mau ndiwo mweo ayakhula munthu.

  • @Marymahendra
    @Marymahendra 2 месяца назад

    That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa 2 месяца назад +1

    Zowona sikunama ai mcp ndi akupha anthu zisiru za mcp mafiti

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 2 месяца назад

    Mudzayese ngat inuso elazi mudzayipomde

  • @PartsonKamkuzi
    @PartsonKamkuzi 2 месяца назад +2

    Fire

  • @NASP-g7h
    @NASP-g7h 2 месяца назад +4

    Tizamusinja amweneo big ngamo

  • @LaynaAdam
    @LaynaAdam 2 месяца назад +1

    Asakuopyeze mchimwene auzeni chilungamo

  • @moseskapelekeza8849
    @moseskapelekeza8849 2 месяца назад +2

    Kodi muli joz

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 2 месяца назад

    Zoona big

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 2 месяца назад +1

    Ndizowawa kwabasi munthu kupita wamoyo