@@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba
@@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,
@@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe Chikhulupiliro sagula Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu Mark 14:48 (Yesu sanamugwire ) Mark 15:21 (Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo) Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka
@@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools
Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.
Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.
Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi
Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi
That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .
Mawu! mawu! 🎉 big man
Zoona zake Zenizeni koma osadera nkhawa chaka chamawa kuvuta am from Ntcheu kwataine village koma mlungu adzatiyakha osaopa osafooka osatopa❤
@@GanizaniKamvazaana mukuenela osatopa kmaso osafooka nanga si moyo umaenda chifukwa cha vice president a chilima, moti ndimadandaula Kwambiri kut malova ngat inu tsopano muyamba kuba
Ndipo sitikuopa izisitikungokamba chabe km sitikuopa ife tikufuna chilima wathu chomuphela ndichani atiuze chomwe anawalakwila iwowo
100%facts brother mcp ndi zigawenga mbiri safuta lero taziona yalembedwaso ina apa.
Amalawi tonse timadziwa kut Chakwera anapha chilima mosogozedwa ndi Michael usi
@@Extratremendouszeus amalawi ake a ku nsipe komaso owelengeka palibe munthu ali ndi mphavu yakupha or yotembelera munthu mzake paja yesu anagonjetsa infa pokha-pokha mulungu akachivomeleza infa imabwela pamoyo wa munthu,
@@yowasschitsosa5348 Izo ndizikhulipiliro za iwe
Chikhulupiliro sagula
Werenga ma verses awa ngat mumaopadi Mulungu
Mark 14:48
(Yesu sanamugwire )
Mark 15:21
(Akukamupachika munthu ochokera kumunda osati yesu wanuyo)
Kms mwa amalawi 100 aliwonse 99 akudziwa kut Chakwera killed chilima together with usi.ndipo Bakili Muluzi tv ananeneratu kut usi salankhula kanthu chifukwa amulonjeza u vice...nde lero azikalankhula ...zopusa basi..dziko loyendetsedwa ndi a ma dramma lingakhle dziko kapena manyaka
Iweso kapolo ndege ija ankayendesa ndi chakwera?
@@yowasschitsosa5348kuswa zonene anthuwa
@@EdwinHowardmkandawire sindilimbana ndi zifwamba za MCP...pano mwaluza mipando yonse ku Balaka,mangochi,Blantyre nd zomba..olo mmodzi owina....mesa anawatuma a Israel kuti akole ndege..pano report latulika koma sakunena,akukonza ulendonso opita kut German konko komwe kuli ofufuza...nde akukatani...iwe ndi chikangawa wakoyo are fools
Komanso kufatsakwina ndikopweteketsa ,
Kufatsakwina ndikopusanako ,
Amalawi ndife anthu ofatsa mopusa
Zoonadi a Malawi ambiri ndi ofatsa koma kufatsa kwake kopusa. Koma ena alipo ochenjera koma chifukwa choti opusa 97% ochenjera amakanizidwa ndi opusawo kuchitapo kanthu. Mantha too much.
Olo Monica akuziwa kt amunanga apha chilima
Ulemu wanu brother
Osatopa osafooka osawopa 💪💪💪 chakwera machende Ako aise
Brother More Fire 🔥....Auza Amenewo....Nthawi zonse chilungamo chimamphweteka muona mufa nd ma BP. MCP yakumpha
Mukunena dzona brather m c p kwake kuba ndi kupha
Mmmm man mwalankhura zoona ok
To stand on the bright side with truth and faith for all Malawian ❤
Ukavomereza kuti Yesu ndi Ambuye, udzapulumuka🙏🙏
Well spoken my brother ❤❤❤
Well said bro
Bg ulemu wanuw mulungu adalise inuyyo nkwamasinku osse tiutseni soona sandege bg mn ashankwela angompedwa nawosso sikut wawaw kobas skc anashita nkumupha ndi ashankwela yemwyyo mfiti yyamundu😮😢
mcp tidakwilira limodzi ndi chilima zimu uwakwatha Wina ayelekeze kuyimila ku ntcheu mcp timpha timuyatsira nyumba osatiseweletsa😢
Ndi chipani chakupha chimenecho Cha MCP ndikukuba ndiye chitukuko chawo cha MCP basi
Zoona auzeni Amalawi wokomedwa Chiliungamo chimawawa A words without aparch mau Mau Mau Mau, anthu ena akumayakhula choncho chifukwa anatisiyawo sa abale awo.
Malawi ife ndife amantha ausilu , big mwalankhula ngamo Amen
Ndithu iwe wa ku ntcheu ukunena zoona inenso ndine wa ku ntcheu ndithu MCP ndiyakupha kuyambira kale mtima umatiwawa koma mulungu akudziwa zonse ndithu patenge nthawi bwanji koma adzatiyankha amalawi
Iye uja mpaka azafa akuzuzika
@@bamusmajawa1619 munamatu simulungu ameneo and palibe munthu ali ndi mphavu yotembelera mzake,
Zowonadi ndi zowawadi chakwera ndi Muthu oyipa
Chilungamo aise Chakwera ndiyemwe anapha Chilima chifukwa cha udindo
Straight talk eeeee anthu munatipweteka kwabasi imfa iyiyiyi
Ndipo mabala akupweteka
Ndipo asabweredi
Zoona mcpbinapha chilima zoona chakwera akuziwa ndipo ife ku mwera tizailowerela amaona ngati amalawi ndiopusa
Kwambliii Mr your talking the truethhh
Ngakhale Mulungu Kumwambako akuwona Lingatalike bwanji Tsiku Lina Oyipayo Adzagonja Ndithu Mulungu Wathu Ndiwam'kulu Ali ndi NTHAWI YAKEEE AYANKHA M'mapemphero Athu
Komaso kuyakhula chilungamo MCP sikanawina kapanda chilima olo akamayakhula mwamatama akhala dzaka zingati osawina
Ndipo zowonadi zake. Ulemu umasowa.
Zoonad brother umakwana
Wa Bakili Muluzi VT amanena zoona😊
Catholic bishops are very sharp amaima pa chilungamo Mcp ndi yokupha
Mau amenewo mulungu akudalisa mcp ndi yakupha auzeni ndi mbusi za anthu awa
Chakwera ndiwakupha vuto anzathu achewa kuberekana nde chimene chikumlimbisani mtima mumadya naye
Walankhula bwino brother
Inuyo mwalankhuladiii boss ulemu wanu
Osaopa man chakwela anapha chilima sibodzatso ayi
Zoona bro,ndipo anthu awawa ndi oyipa ndiposo ineyo amandinyasa heavy ndipo moyo wanga sindifuna kumawona,ndimava kuphweteka ndipo ineyo ndikanakha nfiti tikanaphweteka ndithu
Kuyakhula kwachilungamo chakwera anapha chilima
Chakwela Tu wapanga chitukuko tisaname Ayi Koma chitukuko chake ndi cha kumaliseche Kwa azikazi ayeni osati chitukuko cha amalawi Ayi mu andiloko chakwela pamodzi ndi uyu wakuzimbabweyu usi
Chakwela achoke and ngati Pali munthu woti akuyenela kumangidwa ndi chakwela ndi nduna zake
Zoonadi dzake, more fire,the truth will prevail 😂😂😂😂😂😂.
Zoona big palibenso munthu oganiza bwino angazavotere Chikangawa mcp anthu panopa ndiokwiya
😂😂😂😂 amati wina ludo kkkkkkk😅😅😅😅
Auze aise,
Zitsiru zimenezo zimene zikuti zalowawa ndale,mbole zawo kwambiri
Fotseki chikwera sangasowe ntendele ndipo mutaya nthawi
Thanks brother
Ulemu waanu brother. Osawanyengelela a MCP ndi makape opanda ntchito.
Zoona bro
Sindikuona chifukwa chopangidwira remove nkhani aliense akuona yekha Mene zinaendera Kodi chilungamo mukufuna chotani kuchita kuoneka zokha kuti anamupha mukufunanso chani Chakwera ngoipa anatiphera mngoni wathu Rip skc
Mawu oveka chakwela dzelu alive mamuna ndi wabakili muluzi tv ameneuja amaganiza hsve
Ukuteta yayi àuze zowona
Inuyo chikhala mmaziwa kusaka ndege munkalekelanji kupita kusaka ndege a kapolo a anthu
Ntcheu ndimaiziwa ndiimeneyi
Chilungamo chimawawa
Sindinu nokha akuntchewu ai even boma lakhotakota ndife okwita big pafupi ziko lose nyani chakwela mbuzi akupha
Zoona chakwera anamupha chilima
Zoona anthu a mcp okumpha
Ndimwana yemwe akuziwa kuti chakwela anampha VP wake basi
Ndipo live zoona zake tikuziwa bwino lomwe
This is the truth
Usawope muphwanga chilungamo chake nchakuti chilima anachita kupha a mcp ndichakwera
Thanksyou big
Lero mutenthedwa ndi message yoti inaperekedwa kale kale mukanakhala ozindikila a MCP bwenzi siku lomwe uthengawu inaperekedwa mutaumva
Chakwera Mutu Ngati machende amkango
Kkkkkkkkkk km
Chakwera ndi munthu yemwe anapha chilima ....kuyipa mtima
Zoona zokhazoka ndithu. Mulungu Ali pampando
Tiphe zinyau zinayi kuti tibwenze zomwe chipani cha nyau chimachita.
Mau amphavu bro MCP ndiyakupha idapha anthu ambiri
Ndukugwirizana nazo mbale zoonadi zimenezo mcp chipani chongokhalira kupha
Ife tikudziwa bwino kt anapha chilima
Koma nkulu uyu wayankhula za nzeru kwambiri
Komanso ndege inagwera poyeratu eehh
Chilima adakwera mundenge ndi dzigawenga ndi chifukwa a mcp adakana kukweranao
amenewa akufunika azasinjidwe kumene komas kunena zona palibe wa mcp angapite ku ntcheu azikalakhula mbwelera
Zowonadi brother
Auzeni chilungamo afitiwo
Ndipo kumeneko ndiye kuyankhula
Chakwera wakupha tonse tikuzwa
Zaphabvu brother
Izi nde zoona ine okhara mchewa km imfa iyi yokha idandipweteka😭😭😭😭💔💔💔
😭😭😭😭😭😭😭
Osaopa osatopa osafooka mcp yakupha ndizoona
Koma olo zitalowa ndale palibe vuto chifukwa anthu adafawa ndi andale ndie sindikuona vuto
Zoona zoona mb'ale
Zimawawa kwambiri ighowa ngati anali amai ake or achimwene mhu akhoza kumva motani akaona muthu akangwa pamseu anthu mosachendwa akufika pamalo ngati anali pafupi koma mmmm za chisoni
Kunoso ku mzimba ndife okwiya kwambiri
Mwakhwana brother uko ndiko kukamba
Mau ndiwo mweo ayakhula munthu.
That’s true chakwara killed Chilima for president and is everywhere in world know that Mcp party is not good people and l love Chilima behaviour than chakwara is to man .
Zowona sikunama ai mcp ndi akupha anthu zisiru za mcp mafiti
Mudzayese ngat inuso elazi mudzayipomde
Fire
Tizamusinja amweneo big ngamo
Asakuopyeze mchimwene auzeni chilungamo
Kodi muli joz
Zoona big
Ndizowawa kwabasi munthu kupita wamoyo