Onse mapulezidenti opuma Ali nkhwinthi ngati akumetetsa kwa kaondo ku 36, akupweteketsadi mtima chifukwa palibe akumveka kupatula inu akalindo. Ma radio ndi ma TV pa Malawi kulibe ife tikudalira inu akalindo, amtanyiwa ndi Wa bakili muluzi.
Koma abambo inuyo mukuyesesa kunja kukacha mulungu apitilize kukusungani ndi moyo koma ndimati ndi pephe inuyo simungambise chipani chani ndi achina m,tanyiwa bakili TV tikuvitelanitu chifukwa mumaoneka ndinu amaso m,phenya
Kungotiphera bon kalindo muzakhala nkhondo mmalawi
Bwana kalindo mugwirane mana ndi comrade mtambo chifukwa iwowo alibe tulo komaso ngati Malawi first itafuna kuima pa zisankho Malawi ambiri tikondwa inu bwana kalindo tikuona usogoleri mwa inu chifukwa kumuyankhulira mphawi yemwe alibe mawu sikophweka koma kuyankhulira olemera omwe pamapeto pake munthu amalipidwa choncho inu bwana timakupemphererani mulungu agwirise ntchito inu kuti satana achite manyazi kuno kumangichi makanjira
Bon kalindo and antanyuwa bolaso munakangoimila u president that anthu amenewa angokhala chete akusekelela zomwe chakwelayu akuchitazi😢😢😢
Our president komaso mukudziwa kuti kulilongwe kuno kukuyenda anthu akuitanisa chiphaso chauzika,kumat akuchita kalembera oti pakamachitika zitukuko zaboma asamavutike kupita kwamfumu azingotenga mukaundula?Tifufuzileni mutiuze zoona.
UTM, AFORD, DPP and UDF must make an alliance and win government, Chakwera out, useless government.
Koma otsutsa akewa makape
You are right
Km za alliance zikumabweresa udani mmmm better aliyese azpangile yekha
@@JinishgiftMbalaka vuto payekha payekha sangafike 50+1 yomwe yikufunika.
Maganizo abhoo
Bon kalindo machine,, koma Aford, UDF, Aford komaso DPP khalan maso
president wanga wanga vote yanga
Zoona Mr DC president wa Anthu osauka
UTM PDP AFORD CFT PP and UDF must make alliance
Keep it up mr DC
Best DC
Loud and clear
Fantastic DC
The dc❤
Keep up DC
ndipo Pena gati useke president mpaka kuligawa dziko ai zikomo kuphandoko mulungu akudalitseni
Onse mapulezidenti opuma Ali nkhwinthi ngati akumetetsa kwa kaondo ku 36, akupweteketsadi mtima chifukwa palibe akumveka kupatula inu akalindo. Ma radio ndi ma TV pa Malawi kulibe ife tikudalira inu akalindo, amtanyiwa ndi Wa bakili muluzi.
Mnthuyi ambuye amdalise akumenyadi ufulu
The DC
Keep it up the dc
Ine koma opposition yi.....imamunamizila kut akusokoneza ndi anankhumwa,nankhumwa anakuchokeraniko ife timayesa ziyamba kubebano koma manyaka okhaokha
This government must go out we don't need this mcp
Kodi mesa a UTM anachita kuchokera ku zipani opositionizo? Akukolola zimene anafesa amenewo.
Thus our DC 🔥
Koma azipani zotsutsa tapanganipo kanthu inuuuuuu Bon Kalindo ndiye akuyesetsa kukutsinani khutu ndipo CHAKWERA ndinduna zake akufuna kupitiliza kuba mubomali😢😢
Eiish!!
Powerful the DC❤❤❤
Matiimilila DC Landilani ulemu wanu
Bwana DC, ipatseni moto tili nanu, akapangaso chibwana zodzabera chisakhocho tidzangomenyanapo mmalawi muno, ndi mbuzi za anthu
Ulemu wanu mr Kalindo tulutsani ndondo nthawi yakwana bwana
Machine athu The DC
Mr dc dziwani Izi... Zipani Izi DPP UDF AFORD ADD onsewo a kupanga zinthu zoti ayimile mu 2025 Ndipo inuyo musakayikenso ai
Awawa achoke a MCP
Ubwino wake achewawo ali m'boma
Machine ❤❤❤DC
The DC ❤❤❤❤
Munthu uyi mulungu azimutetedza until mcp out of power,,,,Dpp ,,Afford,,udf,,,,why are you not listen to kalindo
Abale a dpp mukutani
DC 💪💪
🙏🙏🙏🙏🙏
Mmm
The DC 🔥💗🔥
The DC🔥🔥🔥
Ineyo ndkunena pano ,dzulo laliwisi moti akazanga achita kukana kuti mwina akufuna kubwera zisankho
Komadi afasa kwambiri azuzeni
Ife UTM tsitiwelengela kuti chipani chotsusa ayi ichi ndi chipani cholamula boma ndi MCP itsewo alephelela lidzodzi kuyendetsa dziko NSONO A MCP KAYA APATSA NDALAMA KAYA TSAPATSA NDALAMA IDZO ZAWO AKUDZIWANI koma munthu wadzelu nsangasalale ndi munthu amene wapha bambo ako ndikumakuwudza kuti ndikutsamalilani bwino ana inu pomwe bombo wawoyo mumalephela kumutsamalila loko anawo bambo wawo ali moyo msimawathandidza UTM mistake yanu ndiyimene umalidze chipani chanu ndanena kuti kumalidza off course ifa ya CHILIMA yachepetsa mphamvu zanu mwina nsimukudziwa NDE MCP AMALAWI YAKWANO NDE OTSUNSA BOMA CHIHANA MUTHALIKA MAYI PATELO ATUPELE KALWUWA NDI ENA OTSE MUTSAKHELE CHETEEEEE KHALANI PAMODZI NDIKUPANGA CHIGANIDZO KUTI UKAMBELE MBELE AKUPANGANI A MCP NDI ARP muchita bwanji chifukwa kungopatsa pata kawili MCP kukhalatso boma amalawi OCHULUKA TiKUFA KOMATSO ULAMULILO UWU WACHIPANI CHIMODZI UDZAKHADZIKIKANO NDE MAMVUTO AKULU KU MALAWI
Dc ❤❤wi love you
From njedza village
Boooooooooooorn kalindoooooooooooooo
Pita iweyo ku khothi ko Mesa umati ndiwe president
Kape ukuti chani
Koma abambo inuyo mukuyesesa kunja kukacha mulungu apitilize kukusungani ndi moyo koma ndimati ndi pephe inuyo simungambise chipani chani ndi achina m,tanyiwa bakili TV tikuvitelanitu chifukwa mumaoneka ndinu amaso m,phenya
KING
Nkhani yonveka bwino
Nanga a Mwananveka muli kwanikiii? Monga inu.
Azibambooooo
Akufuna udindo uyu aaaaaa
Popeza adamumana udindo. ndiye akuona kut aDPP azamupatsa?
@@FranksonKatundulu ndiye ukuganiza kuti what way followard if akalindo akufuna udindo iwe iwe tanena chabwino mchiti?
Dccccc
❤❤❤❤
Mulindimfundo zabwino
Tokotani akolo
Fadah
ACHALUME KUTI CHUBWIIII
Best DC
The DC
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
The DC
The DC