TAMVANI ZA IMFA YA CHILIMA IJA

Поделиться
HTML-код

Комментарии • 214

  • @Sammy-vb1ed
    @Sammy-vb1ed 8 дней назад +11

    This is true and he was warrior and may his saul rest in peace 😢😢😢😢😢😢😢. Chakwera akutinyasa. Chakwera ndiopa kwambiri ndipo akulitenga dzikori ngat ndilamake.

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 7 дней назад +3

    Rest well SKC, thanks for the information

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 8 дней назад +4

    Well spoken Mr Man,, tikufuna anthu olimba mtima ngati inuyo Mr,, Mmene mukuyankhula chonchi ma Members a MCP akusakani bwana.

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb 8 дней назад +10

    Mzimu wachilima mmmm ndi waukali

  • @Kilocssreaction
    @Kilocssreaction 8 дней назад +29

    Amene akudana ndi voice iyi machende ake ndichakwera manyi ake

  • @thomasmfune5150
    @thomasmfune5150 2 дня назад +1

    UTM ndi Malawi Tapya kusogolo ndi pansanapomwe. MHSRIP 😭😭😭

  • @CHAKAKACHAKA-MANMW
    @CHAKAKACHAKA-MANMW 4 дня назад +4

    MUSIYENI CHAKWERA ABALE AKUZIWA NDI MULUNGU, R.I.P BOSS MAN CHILIMA

  • @CambioJumanjih
    @CambioJumanjih 5 дней назад +1

    Incompetent leader Malawi ever hard........ Lazarus chakwera

  • @GracePhiri-ox8wr
    @GracePhiri-ox8wr 8 дней назад +1

    True bigman live and direct

  • @user-ek9dj9qk4v
    @user-ek9dj9qk4v 8 дней назад +10

    Muziika zinthuzi zizipanga slide, zimapangitsa munthu kuonjezela chidwi pomvetsera.
    Thanks for the information

  • @cosmasnkanda8193
    @cosmasnkanda8193 8 дней назад +5

    imfa yapweteka iyi eeeh!

    • @nancynkumbira1466
      @nancynkumbira1466 6 дней назад

      Ndipo yowawa eee sinazionepo ,,i feel for the family

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d 8 дней назад +5

    Chilungamo chomveka bwino kwambiri 😢😢😢

  • @user-xt2gu9yt9q
    @user-xt2gu9yt9q 8 дней назад +5

    Koma eeeeeeee chîungamo kuwawa or kuli agule Pena mudzivesa chilungamu

  • @StevenLazaro-nm9pk
    @StevenLazaro-nm9pk День назад

    Nice massage

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 8 дней назад +2

    Dziko tengani ili achakwela ndi anthu anu, anthu opanda chisoni, Now Mukufuna Kupha APM ndi Born Kalindo, Zonsezo tikuzidziwa

  • @BlessingsNjanji-dj7oq
    @BlessingsNjanji-dj7oq 8 дней назад +16

    Chilima rest well ,until we meet u again

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 8 дней назад +4

    Chimenetu amaiwala, Technology,ili ponseponse,si nthawi imene anaphedwa nduna,4 zija kunalibe, technology.lero.kutelo,ungoonekela, poyela.si,izi.mabvutotu, awayamba,okha.

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim 8 дней назад +1

    Munthu wanyau chakwera .my br chakwera akudziwa imfa yachilima

  • @AllieGeorge-ec2cl
    @AllieGeorge-ec2cl 6 дней назад +1

    Chonde chonde tibweretsereni poyera zigawengazi ziyaluke

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 8 дней назад +6

    Good Messnge Chakwela you mast go

  • @user-gg6uh2wo4x
    @user-gg6uh2wo4x 8 дней назад +3

    We are to gether brother

  • @giftttsukuluza4264
    @giftttsukuluza4264 8 дней назад +2

    I salute u for good update only God knows, mmm malawi

  • @user-ju1hw9po8u
    @user-ju1hw9po8u 5 дней назад

    Thanks my lady 😊😊

  • @McneverMauwa
    @McneverMauwa 5 дней назад +1

    MCP chawo palibe azakawinila kumwamba chakwerayo

  • @HaroldBonface
    @HaroldBonface 8 дней назад +4

    Utsi sufuka popanda moto

  • @Tenjklvtcy
    @Tenjklvtcy 8 дней назад +2

    Kumalawi kulibe fiti iyaaah 😂😂 amalakwa chani chakwera

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 8 дней назад +9

    MCP yatipweteka kwambili

    • @user-qf7jw4ho3h
      @user-qf7jw4ho3h 8 дней назад +1

      Only God knows the truth

    • @princedetbozsmallboy1749
      @princedetbozsmallboy1749 8 дней назад +2

      @@user-qf7jw4ho3h to know about now because it's obvious chakwera killed Chilima umbuli kapena ufiti inuso nanu aaaaaa

    • @SolomonNjolomole
      @SolomonNjolomole 8 дней назад +1

      Criminal party mcp.

    • @JamesNgwaya-vz1ox
      @JamesNgwaya-vz1ox 8 дней назад +1

      Wapha ndi chakwera akutsutsawo ndani mbolo yake yosadulayo foolish

  • @ChaletsMukona
    @ChaletsMukona 8 часов назад

    Ziyankhule zitsilu zozala ndimagazi kuyambila kale mpakav kale

  • @user-bc3tx3wp1i
    @user-bc3tx3wp1i 8 дней назад +1

    This is reality big man

  • @janemshanga5349
    @janemshanga5349 3 дня назад

    Like my dad also ananena choncho kuti kumukhulukira uku inali nyambo

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 8 дней назад +1

    💯 %true brother 😢

  • @andrewchirwa2193
    @andrewchirwa2193 6 дней назад +1

    Amuphela Dala chilima sazawinaso 2025

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll 8 дней назад +1

    Winayo masoti ngati mphaka , mr kilimora

  • @CharlesBande-yr1yb
    @CharlesBande-yr1yb 8 дней назад +1

    Tienazoni,angotsola kunjira,ndipo njira sadatseke aí,inunso mutero basi sinu Mulungu aí.

  • @kalimawandale7161
    @kalimawandale7161 2 дня назад

    Komatu Chakwerayu atafuna kukubwezelani mutha kuona zosaona

  • @user-wb5ym2qm6y
    @user-wb5ym2qm6y 3 дня назад

    Komaditu a Huwa Mkaka adalankhula kuti ndale za kuMalawi timapanga ndi usiku.

  • @user-dn3gp6yi4y
    @user-dn3gp6yi4y 3 дня назад

    Chilungamo ndi mwano amene ikumukhuza nkhani imeneyi audio iyi sakupuma nawo bwino akuwona ngati awanyoza koma ayi wayankhula chilungamo
    Zimveka bs any time chilungamo chizatuluka

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 8 дней назад +2

    Idalidi nyambo pama plan athuwadi😢😢

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 8 дней назад +3

    😢😢😢😭😭😭 mcp ndi yakumpa

  • @nephitalychitedze2118
    @nephitalychitedze2118 8 дней назад

    Kusokosera pano sikuthandiza china chilichonse nkhani ndiyakuti. Ngati muli ndi umboni pitani ku Court. Sizomangosokosera zotibweretsera misozi ayi... RIP my Veep SKC

  • @OFG-th3st
    @OFG-th3st 8 дней назад +2

    Chippewa chija
    Ndichoopsa😢

  • @Hong_sing
    @Hong_sing 8 дней назад +1

    Excellent 😭😭😭😭😭

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 8 дней назад +10

    We are together big man!!

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam 6 дней назад

    Cakwela ndiwosalakwa anavomeleza kt cilima zayimila koma nduna xakezi ndizimene zikumuzocelesa kt azipanga zoipa koma mcp must go akazizi achabecabe afiti osekelera

  • @KelvinPhiri750
    @KelvinPhiri750 8 дней назад +1

    zosakhala bwino...i do know when we will change a s a country 😭

  • @CharlesBanda-kv8bh
    @CharlesBanda-kv8bh 8 дней назад

    Ndiwe chitsiru amene ukutukwanawe udikire uwone cho me mulungu amanita ndizitsiru ngati iwe

  • @KelvinJpchimphepo-sh6nc
    @KelvinJpchimphepo-sh6nc 2 дня назад

    Umbuli wakudanawo osaziwa chimene akuchita

  • @SaidiMdoka-pn3zm
    @SaidiMdoka-pn3zm 8 дней назад +8

    Mfiti yayikulu ndi Chakwela m'busa wonyenga

  • @FortuneAndrew-nb2im
    @FortuneAndrew-nb2im 8 дней назад +1

    Respected may his soul rest in peace

  • @reymondpetermaster5697
    @reymondpetermaster5697 3 дня назад

    Skc rest in peace, only God knows about your early departure.

  • @louismagongwa
    @louismagongwa 8 дней назад

    ndakulakwila chani fuko langa lokondeka , mtima ukuwawa bwanji😢😢😢

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 6 дней назад

    Mawu onse amayankhura a mcp aphelezera anthuwa ngakupha basi ngakhale zi siru za anthu ena zikubakira as if they don’t see wat is happening n it’s just only few people amene akumusokoneza president.

  • @paurosi123
    @paurosi123 8 дней назад +2

    Bwandeeeeeeeeee!!!!!!

  • @francis12fombe54
    @francis12fombe54 8 дней назад +1

    Kkkkkkkk koma ya 2025 tidzawone kuti ndolo ndani

  • @user-os7qt6lw2c
    @user-os7qt6lw2c 4 дня назад

    Wayakhula momveka bwino2 uyu..muciyakhulo cathu

  • @ModesterThomas
    @ModesterThomas 8 дней назад +1

    Chooona chimamasula❤❤❤❤❤

  • @NOKIAMalawi
    @NOKIAMalawi 2 дня назад

    Zoona

  • @user-lw9su5om5z
    @user-lw9su5om5z 8 дней назад +1

    Sizingatheke kut achakwera osaidziwa opanga nde chakwerayo

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 4 дня назад

    Chilima R I P

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 8 дней назад +1

    Achewa ndinu oipa kwambili

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 8 дней назад +1

    Zomvetsa chisoni dziko lapita ili💔💔

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 8 дней назад

    Chipani choipa ichi ever in Malawi
    Kma thaw yawathera next year onse amangidwa after kuluza

  • @charlesmartin6990
    @charlesmartin6990 8 дней назад +1

    Komaa!eeee dzikoli

  • @user-sr6fb3dw2y
    @user-sr6fb3dw2y 7 дней назад

    Mukadakhala anzeru sibwenzi mukungolalata pamene Malawi ali pa moto.osatenga bomalo kuti amalawi tisiye kuvutika bwanji? Tatopa inu chilungamo mukuchidziwa koma mwabisala

  • @user-mm5mn9fc6e
    @user-mm5mn9fc6e 8 дней назад +1

    True

  • @martinnyirongo2892
    @martinnyirongo2892 8 дней назад

    Anthu awa amalawi zigewenga zikuluzikulu, dziko lino kulisiya mumanja mwa anthu amenewa ndiye kuti tiluza anthu ambiri ofunikira mdziko muno komaso amalawife titengelepo phunziro kuti sibwino kuvotera zigewenga kapena azibusa

  • @worldfamous_23
    @worldfamous_23 8 дней назад +1

    Akutha thobwa akuluwa

  • @user-un6mw5wm3x
    @user-un6mw5wm3x 8 дней назад

    True story brother

  • @Moses51
    @Moses51 8 дней назад +2

    Chakwela achoke

  • @jeffngwira1987
    @jeffngwira1987 5 дней назад

    This is Deus Sandram's voice

  • @BesterSengeledo
    @BesterSengeledo 8 дней назад +1

    For sure biggman

  • @YohanePatrick-lc2lq
    @YohanePatrick-lc2lq 8 дней назад

    Chilima dzathu wa chinyamata 80s 90s 2000

  • @user-nq9bg8zo4v
    @user-nq9bg8zo4v 8 дней назад +1

    MCP should go

  • @promisemenge
    @promisemenge 8 дней назад +1

    Or azipha nayenso kukumusidikila

  • @PaulKalambo
    @PaulKalambo День назад

    Rest in peace legend

  • @JamesMwangolera
    @JamesMwangolera 4 дня назад

    Chilungamo chimapweteka😢

  • @user-qf7jw4ho3h
    @user-qf7jw4ho3h 8 дней назад +1

    Only God knows the truth

  • @ChristinaMALENGA
    @ChristinaMALENGA 4 дня назад

    Rip acle😢😢

  • @PettyMadondo
    @PettyMadondo 6 дней назад

    Ndipo khaniyi ndiyoona ndinthu koma mulungu alipo

  • @AndrewChiponga
    @AndrewChiponga 8 дней назад +1

    Zomvesa chison + urem akurandira ndi mutharika

  • @LupakishoMwenisongole
    @LupakishoMwenisongole 7 дней назад

    Go ahead brother

  • @user-yj5xv4cy8x
    @user-yj5xv4cy8x 7 дней назад

    Mudziwa chani chakwera khaniyi ampaka mmodzi mwa ndunazake kenako iye aziyeretse basi kuteroko muona

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 8 дней назад +2

    Gule kwao please

  • @user-rq2qb9ql1i
    @user-rq2qb9ql1i 8 дней назад +1

    Tisaweluze timusiye Mulungu akhale yekhayo aweluza pansipompano Koma tikhale manso kwawo kwantha kwasala Kwa ine ndi inu

  • @RAFIKIZULIAN
    @RAFIKIZULIAN 8 дней назад

    Watsala ndiwe kufa ndiwe galu 😂😂😂

  • @MelvinVanRooyen
    @MelvinVanRooyen 8 дней назад +1

    Koma gayz m'dziko likuchita dzinthu yhoo

  • @RanitaMbalule
    @RanitaMbalule 5 дней назад

    Rest in peace skc

  • @AfricanKingdom-uv1qb
    @AfricanKingdom-uv1qb 8 дней назад +3

    Mcp ndiyakupha

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 8 дней назад

    No way chakwera ali momwemo

  • @KabilaKabuka
    @KabilaKabuka 4 дня назад

    Mlahu.akibaru

  • @user-qb2lt6qj1p
    @user-qb2lt6qj1p 7 дней назад

    Chilichose chomwe anachita anthu amenewa chiululika nzimu wachilima ndiwoophsa

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y 8 дней назад

    Ulemu wanu Malume osaopa kunena chilungamo

  • @rosamwenelupembe6856
    @rosamwenelupembe6856 8 дней назад

    Mulungu achitile chifundo dziko lathu la Malawi.

  • @promisegregory8397
    @promisegregory8397 8 дней назад +8

    Vuto lanu a Malawi 🇲🇼 Kusankha kwanu kuti mumulande Boma Peter Mthalika.....wakwiya mzimu wa Bingu,Munya muzingophana shupiti....

    • @andrewmaluwa2713
      @andrewmaluwa2713 8 дней назад +1

      aaa uja adationjeza kwambili APM, nkhaza zomwe ma cadet amachita zija muona ngati tayiwala? aliyense adzafatu including APM yo, osamalakhula motumbwa, dzikoli si la amuthalika, chakwela naye 2025 akadzaluza ndekuti amalawi samufuna osati adzidzati andilanda boma

    • @PRECIOUSMKUTE
      @PRECIOUSMKUTE 8 дней назад

      Lero akutifuna okhatu. Ankatinyoza

    • @sokojane4015
      @sokojane4015 8 дней назад

      Zinthu zimayenda bwino only with Bingu. Munthu uja aaaa anathesa njala ndipo zinthu zambiri zimaoneka ndi maso. Bingu wa Mthalika miss him always​@@PRECIOUSMKUTE

  • @PociahMack
    @PociahMack 8 дней назад +2

    Dikilan wosat kumayakhula ngat wokhoza apa. Kuyakhula maganizo anu anthu ndikumakuwombelan m'manja

  • @user-tb3my4wb1k
    @user-tb3my4wb1k 8 дней назад

    Big up sir

  • @MarthaMartha-rw4zz
    @MarthaMartha-rw4zz 8 дней назад

    Chakwera ndi satana amachita kuoneka pakhope mbudzi imene ija atipweteka fitsi imeneyi asazafe garu amneyi

  • @mgarachimsybwoy9239
    @mgarachimsybwoy9239 8 дней назад

    Only God knows 🙏🙏

  • @grinesskuyere
    @grinesskuyere 5 дней назад

    Sad

  • @FrodrickAwadu
    @FrodrickAwadu 3 дня назад

    RIP skc