Zomwe wayankhula Bon Kalindo lero pa 10 July atamupeza osalakwa pa Milandu yomwe amamuzenga

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 26 июл 2024

Комментарии • 114

  • @InnocentHerrera
    @InnocentHerrera 17 дней назад +16

    Concerned malawians let's gather here apule anu alakhula mbali yakuno

  • @duliaustin7179
    @duliaustin7179 17 дней назад +5

    Power to people malawi

  • @yuzzykamwendo3937
    @yuzzykamwendo3937 16 дней назад +2

    This guys, is a strong man, he hasn't any fear and all time he fights for Malawians.Lets fight hand on hand guys Dzikoli ndilathu ndithu tisaope.

  • @lualuaboyartist8868
    @lualuaboyartist8868 16 дней назад +1

    Kalindo I lv u I'm in studio now do your special song u de best fada 🔥🔥💪🔥💪🔥💪🔥💪💪💪

  • @Misiyusuf
    @Misiyusuf 17 дней назад +2

    Proud to be Mangochi❤Welcome to Mangochi bon

  • @Legends.For.Life861
    @Legends.For.Life861 16 дней назад +2

    Izo padela Koma Ife tungofuna Kuti utipelekeze Kwa sing'anga amene iwe unapita fukwa ameneyo ndikatundu ndisaname

    • @GreyJecky
      @GreyJecky 16 дней назад

      😅😅😅😅

  • @user-ji2cu9xn7j
    @user-ji2cu9xn7j 17 дней назад +2

    Kkk awa akuiputanso mlandi ina kķkk komabe akunena chilungamo sure inuyo soja WA mphawi mwatenga dzina la lucius

  • @elvisnjoka8428
    @elvisnjoka8428 17 дней назад +3

    Si zachilendo izi azanu a Mntambo ankatelonso tinakutulukani

    • @KimJime-d9k
      @KimJime-d9k 16 дней назад

      Mtambo sanamangidweko sanamveko zowawa

    • @elvisnjoka8428
      @elvisnjoka8428 16 дней назад

      @@KimJime-d9k kumangidwa ndikumeneko koma ndi anthu aja ongofuna zikawayendela basi kwinako ziiii

  • @OliviaFour-rk9ir
    @OliviaFour-rk9ir 16 дней назад

    Umakwana ukufunka kuno kalindo uzachangamuse Ntcheu ❤

  • @Machemba-b7s
    @Machemba-b7s 15 дней назад

    Born kalindo is my eff

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 16 дней назад +1

    Adzafera mbendera iyi kuti?
    Sakugina mizimu ikumusaka.. ndndende Macbeth

  • @THE_BLESSED_SON
    @THE_BLESSED_SON 17 дней назад +6

    Hahaha Kodi muputanso ina bigy milandu 😂😂😂

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk 17 дней назад +1

    That's our beloved president, president for the poor always guided and protected by the living God, long live our president, we poor citizens loves you more, the Dddddd Cccccc!!!!, the senior pangolin 🔥🔥🔥🔥

    • @KimJime-d9k
      @KimJime-d9k 16 дней назад +1

      Zoonadi ine ndi mboni kundende kuli anthu osalakwa

  • @williamdyton7498
    @williamdyton7498 17 дней назад

    Theeee DC iweyo ndi one zomwe umanena zimachitika🇲🇼✊

  • @MaryMary-dz2th
    @MaryMary-dz2th 16 дней назад

    Akuti mademo tsopano tizipanga bwino....The DC ✊

  • @UmarMasame
    @UmarMasame 17 дней назад +1

    Booooooon kalindo the comred💥💥💥🇲🇼🇲🇼🇲🇼

  • @BichahpostKasambala
    @BichahpostKasambala 15 дней назад

    Booooooniiiiiiiiiii kaliiiiiindooooooo! Katundu osamangia unyolo koma chulungamo 😅😅😅

  • @OWENROBERTS-hf7xd
    @OWENROBERTS-hf7xd 17 дней назад +1

    Salute my homie 🔥

  • @user-qy9xf4rw4e
    @user-qy9xf4rw4e 17 дней назад +3

    Kkkkkkkkkkkkk koma amalume😅😅😅😅😅😅

  • @blessingschiwaya-zn8is
    @blessingschiwaya-zn8is 16 дней назад

    Koma Kalindooo

  • @rodricklanjesi2430
    @rodricklanjesi2430 16 дней назад

    Ma background music wo akuononga zinthu fix that guys ... almost ma videos Anu got the same prob

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 16 дней назад

    Live from south Africa cape town

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r 16 дней назад

    Bon Kalindo The DC ofunika azikhala ku State House ndipo tikamuthamangitse Satana Ali kumenekoyo

  • @ChipiliroLungu
    @ChipiliroLungu 16 дней назад

    Vuto umaphatikiza za zelu ndi zofoila zomwe nde makhala kaye ndi zofoila zakozo

  • @amonprincegenamu7203
    @amonprincegenamu7203 17 дней назад

    Booooonnn Kalindoooooo 🔥

  • @christopherpetro-pen3678
    @christopherpetro-pen3678 17 дней назад +1

    Apolice onse aja? Amabwelela ineyoooo🤪🤪🤪 akut pozamutenga Bon kalindo pazikhala kasinja

  • @TitusShumba
    @TitusShumba 16 дней назад

    Kalindoooo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @pemphoashani4619
    @pemphoashani4619 17 дней назад +2

    Komano Kodi anthu osawukawo mukumawauza kuti azipangako chani kuti mu umphawimo adzachokemo. Chifukwatu kulimbana ndi BOMA sizingasinthe status ya osawukawo koma zitha kusintha status yanu. Mukalimbana nalo BOMA chonde tilimbikitseniso kuchita ma business chifukwa chete chete sautsa nyama

    • @Boystarpluss
      @Boystarpluss 16 дней назад

      Men ma business wo mupangira kutiko?dZiko silikuyenda bhoo amayenera kumadzuzula kut amalawi wo azikhala pabwino...ngongole Zama business mutenga kut?Amati mukonze chapansi kut chapamwamba chikhale bhoo...

  • @GilbertKuchipinda
    @GilbertKuchipinda 16 дней назад

    Pa ma china pokhapo nde wabayatu driver, operator gad zose zikugwilidwa ndi ma china lebala wawo ndi bwana wa anthu aku malawi.

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 16 дней назад

    Inuyo ndi 1. More 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @johnussenu2848
    @johnussenu2848 17 дней назад

    You are welcome in mangochi bon kalindo

  • @samuelazumah1050
    @samuelazumah1050 16 дней назад

    Munyengo ya ku ng'alula

  • @TrizerDoller
    @TrizerDoller 16 дней назад

    Number one kalindo

  • @innocentsathasteven4093
    @innocentsathasteven4093 16 дней назад

    Iwe ndi nyooo ndikukudziwa bwino bwino

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m 15 дней назад

    Oipayo alephera yekha

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 17 дней назад

    Ngati Satan simumuziwa melowere ku state house Satan amakhala kumeneko pamodzi ndi Angelo ake azikhale ng'oma ,,kunkuyu ,,,mkaka ,,Monica,,chityola ,,nick amenewa nde Angelo asatana

  • @UTHMAN-WAYA
    @UTHMAN-WAYA 17 дней назад

    T/A MABUKA 😂🔥 AND THE LAST MAN STANDING ✊🌹

  • @StanleyChirwa-d6b
    @StanleyChirwa-d6b 17 дней назад +2

    Chi booooniiiiii kalindo 🤣🤣

  • @KENETHMAJASA-ud5ee
    @KENETHMAJASA-ud5ee 17 дней назад

    Kutchaya kugwetsa, shatapuuu!

  • @AuspiciousKalambula-hp7gj
    @AuspiciousKalambula-hp7gj 16 дней назад

    Ati ine ndiye ndi "kusendendani" uyuyu sakuwopa eeesh 😂

  • @JonesMalingaMalinga-nr6jc
    @JonesMalingaMalinga-nr6jc 17 дней назад

    Uyuyu mmmmm koma yeah

  • @SamsonMedson-oz7rq
    @SamsonMedson-oz7rq 16 дней назад

    Cd2d❤

  • @christopherpetro-pen3678
    @christopherpetro-pen3678 17 дней назад +1

    Akut koma chino sichimakpa kumangidwa😜🤪🤪🤪 ochatsika siyani kuononga ndalama zathu pa nkuluyu mungoziyipisila mbili

  • @AustinBanda-wg5pw
    @AustinBanda-wg5pw 17 дней назад

    Bon Kalindo the DC

  • @LzkayLzkay
    @LzkayLzkay 16 дней назад

    Ife timakukonda bon Kalindo

  • @moyo77777
    @moyo77777 16 дней назад

    Boma lopusa

  • @JonathanChimwaza
    @JonathanChimwaza 16 дней назад

    Chilungamo sichimabisika

  • @AnabandaMasauli-rk3lg
    @AnabandaMasauli-rk3lg 17 дней назад

    Ndalama zolipira Lawyer ndilibe ine

  • @MadalitsoJackson-ns3vu
    @MadalitsoJackson-ns3vu 17 дней назад

    Uyuuuuuu ase ati chiboni kalindo😂😂😂😂

  • @RichardJackson-p9z
    @RichardJackson-p9z 16 дней назад

    Zaphavu zmenez

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x 16 дней назад

    Uyu ndi woopsaaa kwambiri ‼️🤣😂

  • @Ntchindinkhwazi
    @Ntchindinkhwazi 17 дней назад

    Eeeeh !!! Uyuyu anatopa

  • @ozziehenderson9977
    @ozziehenderson9977 16 дней назад

    Akut atamangidwe ndamako😂😂😂

  • @FestonJuwawo-dn4lp
    @FestonJuwawo-dn4lp 17 дней назад

    Uyuyu ndi makina😃😆😃😆😃😆

  • @VeroNica-tp5vp
    @VeroNica-tp5vp 17 дней назад

    Eeeh kom ichi

  • @user-xg5dg7jj4d
    @user-xg5dg7jj4d 17 дней назад

    UTM president

  • @kennedyfaraimulilo4074
    @kennedyfaraimulilo4074 16 дней назад

    Ine ndine nyooo,too much drama.

  • @PeterNamphwanya
    @PeterNamphwanya 17 дней назад

    Chibooooon kalindooo

  • @AlickSquare
    @AlickSquare 16 дней назад

    Koma boma muthu uyu kungomusiya basi sidzoona paka apolisi 200 kuononga misomkho ya anthu

  • @georgefungulan6648
    @georgefungulan6648 16 дней назад

    Joab tachezaniko ndi bodyguard wa kalindo bwa?

  • @ShalomShine
    @ShalomShine 17 дней назад

    Kasunja woyeeeeeee!!!!!!

  • @awaliwilliam6472
    @awaliwilliam6472 17 дней назад +1

    Makosana nanu mwati mudyele ma views pa speech ya nzanu nanu yakhulan yanu mupange post bas Khan ya straight

  • @euccotechs1744
    @euccotechs1744 16 дней назад

    Umakwana bale

  • @PempheroKachande
    @PempheroKachande 17 дней назад

    Koma yh ,,,ichi nde Kaya😂💔🤣🤣😳

  • @marychavula698
    @marychavula698 16 дней назад

    Inu ndi one😂

  • @Yamikie-yamikie
    @Yamikie-yamikie 16 дней назад

    Ka instrumental kabpansiko kaksomoneza olo mukatsitse kwambiri😅

  • @user-qc1yv3zk7i
    @user-qc1yv3zk7i 17 дней назад

    Dc nkatundu uyuuuu

  • @Humphrey265
    @Humphrey265 16 дней назад

    😂😂😂Kalindo

  • @Fahadimalopa
    @Fahadimalopa 17 дней назад

    this is born kalindo 😂😂😂🎉

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x 16 дней назад

    Inu makosana stop kuika ma instrumental si nyimbo izi mixieew tonse ndi oimba?

  • @user-jr6fe2gi4b
    @user-jr6fe2gi4b 16 дней назад

    Musatitopese

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o 16 дней назад

    The DC mumakwana inyo

  • @AffectionateAtom-rk2kn
    @AffectionateAtom-rk2kn 17 дней назад

    Komchi

  • @ChimwemweFredrick
    @ChimwemweFredrick 17 дней назад

    Kom ichiii inu 😂😂😂

  • @Praise-u8f
    @Praise-u8f 16 дней назад

    W

  • @Patgregorymanyumba
    @Patgregorymanyumba 17 дней назад

    Kkkkkk yeah

  • @AaronMaganga-rj1pp
    @AaronMaganga-rj1pp 17 дней назад

    Koma ichi 😂😂😂😂😂

  • @yusufdaud9663
    @yusufdaud9663 16 дней назад

    Koma ichichi eeeeh 🙌😂

  • @user-ch1jf9zk6g
    @user-ch1jf9zk6g 17 дней назад

    Kma. Ichi🤣🤣

  • @BeautyYona-vc7jp
    @BeautyYona-vc7jp 16 дней назад

    The DC

  • @ZiporahThiezy
    @ZiporahThiezy 17 дней назад

    Koma ziliko 😹😹🏃

  • @lindamankhanamba7580
    @lindamankhanamba7580 17 дней назад

    Kuli zinthu ku 🇲🇼😂😂😂😂💔

  • @TamandaniGawan
    @TamandaniGawan 16 дней назад

    kuyaka

  • @ThokiezMw
    @ThokiezMw 16 дней назад

    Koma akulu awa

  • @Post44SunSet
    @Post44SunSet 16 дней назад

    🫡🫡🫡🫡🫡🫡🫡🫡

  • @captainsisitomalawi1548
    @captainsisitomalawi1548 17 дней назад

    Chatokotatu ichochi ndichooopsa🤣🤣🤣

  • @ShadreckMtepuka-sj8ue
    @ShadreckMtepuka-sj8ue 17 дней назад

    Komatu nde watokotatu

  • @user-hq5wh3pn5b
    @user-hq5wh3pn5b 17 дней назад

    Kkkkk koma the DC

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e 17 дней назад

    Zowonadi tikudikira za ifa zimene zija.

  • @TimothyJobe-jc1ti
    @TimothyJobe-jc1ti 17 дней назад

    Akuti pa mdipiti okamutenga kalindo mudziikaposo kasinja😂😂😂

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h 16 дней назад

    🤣🤣🤣🤣🤣kasinja

  • @Simayil-qx6gj
    @Simayil-qx6gj 17 дней назад

    Wayita m,bale

  • @kha6068
    @kha6068 16 дней назад

    What's with the useless background songs ?

  • @uzacarolinakaime772
    @uzacarolinakaime772 16 дней назад

    Inde Nyo!!!!... lol

  • @user-zp1jh9xn3d
    @user-zp1jh9xn3d 17 дней назад

    😂😂😂😂

  • @bmbboymstyles5894
    @bmbboymstyles5894 17 дней назад

    Chiphe😆😆😆

  • @user-eh1gn1nj9d
    @user-eh1gn1nj9d 17 дней назад +1

    A Kalindo mukuimira ndani bwenzi mutapita kwanu ku Mulanje muzikapanga campaign muzaimire DPP yomwe ija muzapeze chochita panopa sizikuthandizani izi muzafa osauka ndithu

  • @user-ji2cu9xn7j
    @user-ji2cu9xn7j 17 дней назад

    Boooooooooooooooooon kalindo

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatundulo 16 дней назад

    Kkkk

  • @MynessChirwa
    @MynessChirwa 17 дней назад

    😂😂