You guys are unrealistic,you expect him to always morn....remember you can not keep crying for a workmate as if it's your mam and Dad. Why shouldn't he be VP ?
Koma guys sindikufuna kuseka ati monica imeneyi wig yanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂ndakomoka ❤Dr chikangawa woyeee and mr short chakwera ndi manganya mukuvala mochititse manyazi bwanji Kwachema ndi ku Balaka no people 🙌🙌🙌
Mamie ndiye mumangolondora kuli konse mulibe zochita zanu ndiyekut eti achakwerawo ndiye ayamba kuondatu chonsecho akudya misokho ya malawi or mutero chaka cha mawa muchoka mudyeretu misokho ya malawiyo paja dzina lina ndi chikangawa 😂😂😂😂😂😂
With or without anthu program yachitika basi. Zomwe amakapanga president ndizothandiza anthu omwewo. Kupanda nzeru eti. Ndale zanji zimenezi. Nsanje paMalawi
African countries need different type of Democracy designed by Africans them self. The one we follow now has a lot of European influence, control, and interest. It contains ideas whose goals are to control and pin down developing. countries. China has its own type, and Russia has its own. Many European countries have what fit them better. While in Africa, we are controlled by the West. People who shared our continent among themselves in 1884 without involving any African representative. So, let's not blame our leaders so much. But let's fix come up with our own type of Democracy.
Sikulina anthu azapanga transfer ena Azapita ku Zambia ena ku Tanzania 🇹🇿 chifukwa cha mavuto boma silibwino ndalama zimabedwa kwambiri chithandizo palibe
Balaka ppo mwachìta bwino osapitako keep it up
MBAMBANDE
Ayi a Manganya mukuoneka okondwa, chasala nchiweruzo basi pa imfa ya nzanu, continue rest in peace SKC, tizakulira mpaka kale kale Biyeni
Mmmmmmm,,,koma Malawi,,,,z
Manganya is a happy man nowadays, he is exactly where he wanted to be all along. RIP CHILIMA.
Ndiposoo
He is more than happy
He is just a puppet wa apule uyu😅😅 kd anthu simukuona what's going on...
😅😅 8:35
He got opportunity he was looking for 😢😢
You guys are unrealistic,you expect him to always morn....remember you can not keep crying for a workmate as if it's your mam and Dad.
Why shouldn't he be VP ?
Mr chikangawa ndemwawondatu nde mkuwonda pano lbani kaye zomaliza nthwi lripo agogowo alibe chochita china muboma lakupha lanuro mzit zikomo chilima mwawulawa udindo ndikumuphaso ziko lapasi koma 😢😢 pitilizani kupuma bwana chilima
Koma anthu aku Balaka congratulations mumatha anthu amenewa tisawaoase mpata please.
Good job Mr president and vis wanu limbikitsa ndinthu ulimi umenewuu
Koma guys sindikufuna kuseka ati monica imeneyi wig yanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂ndakomoka ❤Dr chikangawa woyeee and mr short chakwera ndi manganya mukuvala mochititse manyazi bwanji Kwachema ndi ku Balaka no people 🙌🙌🙌
Mamie ndiye mumangolondora kuli konse mulibe zochita zanu ndiyekut eti achakwerawo ndiye ayamba kuondatu chonsecho akudya misokho ya malawi or mutero chaka cha mawa muchoka mudyeretu misokho ya malawiyo paja dzina lina ndi chikangawa 😂😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂 koma akuliziwa dzinali LA chikagawali
Ndipo pansana pawo ndithu😅😅😅
Kumaka, dad asayende okha angayambe kukodwa ndi ana anjoka😅
Ka msanje bwa???? Mix ti atsikana tosezenzedwa ma unduna tili ku mcp kkkk kuopa kulandidwa
Ulibe manyazi manganya kuchenjera konsekuja kumupha nzanu ngat galu ndi chikangawa nzakoyo,anthu akakuona akumakumvera chison chifukwa mawa ndiwe.utm yake itiyo yomwe uli iweyo,popeza chilima ali Moyo sunasapotepo utm.anthu amagazi mmanja
With or without anthu program yachitika basi. Zomwe amakapanga president ndizothandiza anthu omwewo. Kupanda nzeru eti. Ndale zanji zimenezi. Nsanje paMalawi
Amanganya mwamasuka pano mukumva kukoma mutamuphesa chilima ndi abraz anuwo lnuso muzafa mutu kuwumawo ngt nguli
Kunganakhala ku maliro tikanati angokhala po ananfedwa okha
Kuononga ndala kukayendera nyemba basi ndi matumba angat achimanga mukanagura kupasa anthu akusowa chakudya 😢😢😢😢😢
Watching from Johannesburg
❤ Maiko usi a chakwela pano a kuyendela nzeru za Maiko usi
Akugofuna kumugwilitsa ntchito then asamuphe mcp plan
Bolanso kukanapita anduna okha mwinako kukanakhala anthu not as it is manyazi bwanji koma!!
Ai zikomo anthu aku Baraka ❤❤❤❤❤
Km ndie kuli chinamtindi cha anthu!!! Kkkkkkk
Fanz mphwanga
Keep it up balaka people mupitilize wosapitako achikangawa akamabwera kumeneko
My district ,keep it up
Manganya or utavala zofafana ndi chilima sungamake 😂😂😂kod apule mwachedwa nazotu nthawi yonseyi munalikut
Ndipo live ife tikufuna chilima basi
Ndipo inu galu manganya Kwa basi ufiti basi kulakwa Koma chomumohela munthu ndichani mmmmmmmmm takaoneni kufupika
African countries need different type of Democracy designed by Africans them self. The one we follow now has a lot of European influence, control, and interest. It contains ideas whose goals are to control and pin down developing. countries. China has its own type, and Russia has its own. Many European countries have what fit them better. While in Africa, we are controlled by the West. People who shared our continent among themselves in 1884 without involving any African representative. So, let's not blame our leaders so much. But let's fix come up with our own type of Democracy.
Sapato ya madam yo eeh😅
Ku Balakatu anthu anafika kukenani mkona mwapeza kulibeko😂😂😂
😂😂😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Athu kod alikuti zukhala bwanji kumeneko😂😂😂😂
Kaya alikutiko kkkkkk
Inu simukuwona noka akuwopa kuti akawagesa
🤣🤣🤣🤣🤣 koma Malawi penapake zimaoneka ngat ena tidakali muzaka zamma 1980 nanga tikamunene munthu chifukwa choti wavala mofanana ndiwina wake kkkkkkk 🛌🛌🛌🛌🛌🛌🛌
😂😂😂😂😂😂😂
Kkkkkkkkkk koma kuli anthu kapena kuli achina yudasi okhaokha?😂😂😂😂😂😂😂mbali yakuno chikangawa yomweyo msonkhano wa Mr chikangawa.Balaka number one pitilizani mtima umenewu❤❤❤❤❤❤ ndakukondani ndife abanja limodzi zigawengazo mutalikile Nazi zingakupheni zili ndi poison
A Malawi chenjerani chakwerayo ali ndi asilikali akulwan
A Malawi chenjerani chakwerayo ali ndi asilikali akulwan
Ok
Kodi sound yanuyo mukumveka ngati muli nchigubu bwanji?
Mwamuona pharaoh ndi Yudasi anthu oipa kwambiri bola winayo asasanduke Chulu Cha mchere
Kodi ku Balaka anthu anapita kuti kukumangowoneka asilikali okha ndi Chakwela zikukhala bwanji
Anafika kukenani mesa
Anthu ali busy kupanga zaphindu osati kukaona Chikangawa ngati ndi anawafera 😂
Balaka ndikumene inayambila referendum thawi ya kamuzu balaka siyogonatu ayi
Watching from Capetown
Anthu aku balaka Mulungu akudalitseni kwambiri ndinu okonda dziko lanu anthu tikuvutika palibe chifukwa chokhalira busy ndi anthu amagazi mmanja
Bala wooooye mwachita bwino Mr chikangawa ndi Mr chifunga osapitako
Kkkkkkkk
leave chakwera and usi God bless them
Koma guyz kkkkk anthu alikutiko kwangoti ziiii😊😊😊
Ndipo ameneyu olo mavoti osadzamupatsa galu ameneyu. Tikuvutika
Kkkkk Koma ndiye kwadza zatu anthu 😂😂😂😂😂😂 chikangawa yomweyo
Munthu paliponse
Aaa uchisilu basi 4 years munali kuti afiti inu Dr chikangawa ndi mr chikangawa
Mfiti za zikuru zikuru zikufuna kunamiza anthu zakupha anthu opanda chifukwa, akatura pasi udondo sadzawonaso ma vote ameneyu chikangawa
Sizoba khahlera landuku laba banthu bazonya, tinabangoni hakisabe bayabeda, kumafunika kuzayamba yamaja
Great
Manganya kutalika kwakeko😂😂😂😅😅😅
😅😅😅😅😂😂😂😂😂😅😅😅Balaka woyee 😅😅😅😅😅😂😂😂
Amalawi tiyeni tipitilize kuchita ngati zachita anthu akubalaka osamasekerera NG, onazi zikumatha anthu mkumaziseketera aziona sizinati munthu osaweluzika ndalama kumangoononga osamva chisoni amalawi akufa ndi njala otembereredwa inuu
Chisiru Cha president ichi nchewa paja sayendatu ndye apa mwai wapezeka ayenderetu 😂😂😂😂😂😂
Udzaziona wakula watha
Nosence where were you all these days
Kkkkkk anthu muli kuti guys 😂😂😂😂.
Yomweyo Chikangawa 😅😅😅
Koma SKC udindo wauVP umkamukhala osati zinazi
Kodi ndiye mwati ku farm ya Demeter ku amakataniko. This farm has been there b4 iyeyu kulowa m'boma.
Mr chikangawa ndi VP nde akuyendatu ngat campaign yayambika kale😮
Sikulina anthu azapanga transfer ena Azapita ku Zambia ena ku Tanzania 🇹🇿 chifukwa cha mavuto boma silibwino ndalama zimabedwa kwambiri chithandizo palibe
Koma mpaka kukayendera nyemba like seriously apule?
Kusowa chochita
Mukufuna kumangoba zitukuko chamuthu chabe osati ndi boma linalima zimenezo mabodza basi 😅😅😅😅😅😅😅😅 koma azitsogoleri Enawa eeeti
Sazidziwa zawulimi mukungo tha mawu palibe chomwe chikulowa mmakutumo. Koma zomwe akuganiza akachoka kumeneko ndi kukaba mitsonkho ya thu avutika ba mutamuwuza zamitsokho nde nde eeeeeee sngajowejowetu Tsinzina mntole mr Raza 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Zachita bwino osapita anthu, chipani chokupha chimenecho, chondee ma boma ena mutengelepo phudzilo osawasekelera akanganya amenewa , I'm White Willison from machinga T/A chamba , Lulindi villege
Bomaloooooo!¡!!
Utsi watengekatu nawenso ukwela ndege pompano nd zigawenga zimenez😅
Kubalaka kuno tinali busy kusaka ya thumba lachimanga mpata opita Kwa apulesidenti sitinaupese😂
Abale azanga musiyen manganya ,usamunyoze zakutsogolo sizidziwika , adzatero Ali ana anu Ali pa mpando wa up resident
Ife tidya masambao za ziii munali kuti nthawi yoseyi aaaaa ife si zisilu
Ulimu wanu ma pulezdent athu ❤❤❤❤❤❤
Wow!what a good initiative
Tiyeni titenge ngongole za Neef kuti titukule Business zathu ndi magulu a business Ndalama zimene akhazikitsa a President
Kodi Michael usi wavala kut afanane ndi big akunamatu uyu komanso iye kuzavula chipewa.
Manganya iwe ndiwa map to see tikuziwa
Mr chikagawa akuondatu mzimu wachilima ukuzuguza
Idzidzi sidzingapangitse kutsitsa katundu ndi kukweza mphavu Kwacha
Ngati ndinu mbuli ingokhalani musaonetse umbuli wani
Inuyo kuzindikira kwanuko kulipati?
Chakwela akumukonda manganya Chifukwa choti akudziwa kuti sangamusokoneze olo zinthu zikulakwika akudziwa kuti yemwe akanandisokoneza ndi chilima anamupha uja munthu wachabe uyu zoti ndale ndi mfundo wowinayo awine koma osati kuphana nde paliso ndale ngati mukuphana atsogoleli kusokoneza ndale kumeneko
Balaka! Balaka! Balaka! How many times have I called you?😂
Muwaudze akadulitse magalasi ofanana ndi nkhope yawo a vice president, ma galasi akuwpatsa busy
Komaso kodi mwati nkwawa zunguwa akatero azizakamba ngat Iwo apa
Chikangawa ndi chifunga akuti akukayendela chiani
Mayi chakwera ndakaika ngati akuvanawo
Kod zolimadzo zoti zalimidwa kuchokera kundalama yatu yamisoko kapena dzida ngati zimenezi zoti sizadzungu koma tagula toka nditimisoko tathu tiziona Lori poti mukulimbika kuonesa mukuti mamega famu kod ndi anthu kapena angelezi
Ulimi ndiwabwino kwabasi kananji othilira umapindula mwachangu
Ngati sanapite so what?good show a PULE
Boma la MCP kukamba mowona mtima labwera kudzakhala komanso kuthandidza a Malawi.
Kodi tinene kuti a chakwera akuonda ndichani makamaka 😂 mwina ndi bakili muluzi tv eti kkkkkk achoke!! achoke!! Chakwera achoke!! Achoke.
Kapoli wankulu adafika mu Mbalaka 😢😢😢 uyo wamfupiyo Yudas 😢. Ayi zikomo 😢😢😢
Chikangawa crue
Athu sangapiteko akulira maliro a chilima NDI Lucius Banda
Madam Ake a VP ndioukilatu
Mufuti yonseyo ngati mukupita ...kunkhondo zikumakoma bwana usi akayenda okha ulimi ukuchita kukongola koma bwanji mifuti choncho?
😂😂😂😂 ZIKUTANTHAUZA KUTI CHAKWERA AKAMUVOTELE NDI ASILIKALI NDI APOLIC AKEO KKKK CHIKANGAWA YOMWEYO
Ku mangochi aja avotera councilor wa mcp ndi asirikali?
Wasting Tax payers money
Ausi zobvalazo sizikukukhalani bola Chilima zimamukhala😂
😅😂😂😂
Kulibeko anthu bwanji kodi
Chikangawa ikungoononga ndalama ndinu agalu kwabasi
Azalira chikangawa😂😂😂😂😂😂😂
Chakwera ndiwowinawina palibe angamake
Mudzafa ndi ukapolo onyaweza kadzinyoza , mwina umapwza mphoto
Zama big izi guys ndipo MCP siikugonja amtaaa
😂😂😂😂 km monica yekha ulusi amayika sangachite kufuna phunzitsi 😂😂😂😂😂😂
Balaka ndiyozindikira siphwekesa akupherani mayi shanil zimbii
Amanganya oro kuvara jombo osatalikabe
Kwanti ziiiii anthu akubalaka ulemu wanu ndinthu
Gwilani ntchito yanu yabwino a Vp.Mwayamba bwino
Dr. Chikangawa Chifunga mwapeza nyekhwe, balaka siimasekelera zopusa. Rest in peace Dr. Saulos klaus chilima
Olemba zoyipanu kalembani nsanje ikakula ndi choncho
Yakuli andu ambili 😂😂😂 2024 mtionazindu 😂
Koma mavalidwe amonica yooooo9😂😂😂😂
Kkkkk km zilikotu mangabya kuuluka ulusi monga malemu chilima
Anthu aku Balaka mumakwana, mumaopadi mulungu
Unyozawe ukamaliza kunyoza mphoto imene ulandire utionetse