ZOMWE ZIKUCHITIKA KU BALAKA PADAKALI PANO PAMENE PRESIDENT CHAKWERA NDI VICE MICHAEL USI AFIKAKO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 6 сен 2024

Комментарии • 262

  • @user-gd2kl1fx1q
    @user-gd2kl1fx1q Месяц назад +19

    Balaka ppo mwachìta bwino osapitako keep it up

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya Месяц назад +11

    Ayi a Manganya mukuoneka okondwa, chasala nchiweruzo basi pa imfa ya nzanu, continue rest in peace SKC, tizakulira mpaka kale kale Biyeni

  • @petroszgambo9949
    @petroszgambo9949 Месяц назад +22

    Manganya is a happy man nowadays, he is exactly where he wanted to be all along. RIP CHILIMA.

    • @user-lj7lm6ly7z
      @user-lj7lm6ly7z Месяц назад +1

      Ndiposoo

    • @stephancommercial580
      @stephancommercial580 Месяц назад +1

      He is more than happy

    • @user-cs3lq5mr9t
      @user-cs3lq5mr9t Месяц назад +3

      He is just a puppet wa apule uyu😅😅 kd anthu simukuona what's going on...
      😅😅 8:35

    • @user-ep7gu2td6y
      @user-ep7gu2td6y Месяц назад +1

      He got opportunity he was looking for 😢😢

    • @vukanifracksonchinkonde7324
      @vukanifracksonchinkonde7324 Месяц назад

      You guys are unrealistic,you expect him to always morn....remember you can not keep crying for a workmate as if it's your mam and Dad.
      Why shouldn't he be VP ?

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb Месяц назад +5

    Mr chikangawa ndemwawondatu nde mkuwonda pano lbani kaye zomaliza nthwi lripo agogowo alibe chochita china muboma lakupha lanuro mzit zikomo chilima mwawulawa udindo ndikumuphaso ziko lapasi koma 😢😢 pitilizani kupuma bwana chilima

  • @user-lu5db5qk2o
    @user-lu5db5qk2o Месяц назад +6

    Koma anthu aku Balaka congratulations mumatha anthu amenewa tisawaoase mpata please.

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama Месяц назад

    Good job Mr president and vis wanu limbikitsa ndinthu ulimi umenewuu

  • @user-rz8qp8tj8e
    @user-rz8qp8tj8e Месяц назад +3

    Koma guys sindikufuna kuseka ati monica imeneyi wig yanji 😂😂😂😂😂😂😂😂😂ndakomoka ❤Dr chikangawa woyeee and mr short chakwera ndi manganya mukuvala mochititse manyazi bwanji Kwachema ndi ku Balaka no people 🙌🙌🙌

  • @user-mv1ho9pp7o
    @user-mv1ho9pp7o Месяц назад +8

    Mamie ndiye mumangolondora kuli konse mulibe zochita zanu ndiyekut eti achakwerawo ndiye ayamba kuondatu chonsecho akudya misokho ya malawi or mutero chaka cha mawa muchoka mudyeretu misokho ya malawiyo paja dzina lina ndi chikangawa 😂😂😂😂😂😂

    • @chrisschikozera7271
      @chrisschikozera7271 Месяц назад +2

      😂😂😂😂😂😂😂 koma akuliziwa dzinali LA chikagawali

    • @user-cs3lq5mr9t
      @user-cs3lq5mr9t Месяц назад +2

      Ndipo pansana pawo ndithu😅😅😅

    • @prettytambala5687
      @prettytambala5687 Месяц назад +1

      Kumaka, dad asayende okha angayambe kukodwa ndi ana anjoka😅

    • @chitanibenito1109
      @chitanibenito1109 Месяц назад +2

      Ka msanje bwa???? Mix ti atsikana tosezenzedwa ma unduna tili ku mcp kkkk kuopa kulandidwa

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Месяц назад +3

    Ulibe manyazi manganya kuchenjera konsekuja kumupha nzanu ngat galu ndi chikangawa nzakoyo,anthu akakuona akumakumvera chison chifukwa mawa ndiwe.utm yake itiyo yomwe uli iweyo,popeza chilima ali Moyo sunasapotepo utm.anthu amagazi mmanja

    • @anthonynkhoma4265
      @anthonynkhoma4265 Месяц назад

      With or without anthu program yachitika basi. Zomwe amakapanga president ndizothandiza anthu omwewo. Kupanda nzeru eti. Ndale zanji zimenezi. Nsanje paMalawi

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb Месяц назад +5

    Amanganya mwamasuka pano mukumva kukoma mutamuphesa chilima ndi abraz anuwo lnuso muzafa mutu kuwumawo ngt nguli

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j Месяц назад +2

    Kunganakhala ku maliro tikanati angokhala po ananfedwa okha

  • @ThokoGomeza
    @ThokoGomeza Месяц назад +2

    Kuononga ndala kukayendera nyemba basi ndi matumba angat achimanga mukanagura kupasa anthu akusowa chakudya 😢😢😢😢😢

  • @user-gd6zb2bv8f
    @user-gd6zb2bv8f Месяц назад

    Watching from Johannesburg

  • @yusufbakali
    @yusufbakali Месяц назад +2

    ❤ Maiko usi a chakwela pano a kuyendela nzeru za Maiko usi

    • @yusufbakali
      @yusufbakali Месяц назад

      Akugofuna kumugwilitsa ntchito then asamuphe mcp plan

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Месяц назад +3

    Bolanso kukanapita anduna okha mwinako kukanakhala anthu not as it is manyazi bwanji koma!!

  • @CleverJosafat
    @CleverJosafat Месяц назад +4

    Ai zikomo anthu aku Baraka ❤❤❤❤❤

  • @MalitaKapesi
    @MalitaKapesi Месяц назад +5

    Km ndie kuli chinamtindi cha anthu!!! Kkkkkkk

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Месяц назад +2

    Keep it up balaka people mupitilize wosapitako achikangawa akamabwera kumeneko

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f Месяц назад +15

    Manganya or utavala zofafana ndi chilima sungamake 😂😂😂kod apule mwachedwa nazotu nthawi yonseyi munalikut

    • @joyahmedjoma4615
      @joyahmedjoma4615 Месяц назад +1

      Ndipo live ife tikufuna chilima basi

    • @JeanKambala-gm1zr
      @JeanKambala-gm1zr Месяц назад +1

      Ndipo inu galu manganya Kwa basi ufiti basi kulakwa Koma chomumohela munthu ndichani mmmmmmmmm takaoneni kufupika

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 Месяц назад +3

    African countries need different type of Democracy designed by Africans them self. The one we follow now has a lot of European influence, control, and interest. It contains ideas whose goals are to control and pin down developing. countries. China has its own type, and Russia has its own. Many European countries have what fit them better. While in Africa, we are controlled by the West. People who shared our continent among themselves in 1884 without involving any African representative. So, let's not blame our leaders so much. But let's fix come up with our own type of Democracy.

  • @LindaKeston
    @LindaKeston Месяц назад +2

    Sapato ya madam yo eeh😅

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn Месяц назад +2

    Ku Balakatu anthu anafika kukenani mkona mwapeza kulibeko😂😂😂

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no Месяц назад +1

    Athu kod alikuti zukhala bwanji kumeneko😂😂😂😂

  • @RhodrickBanda
    @RhodrickBanda Месяц назад +6

    🤣🤣🤣🤣🤣 koma Malawi penapake zimaoneka ngat ena tidakali muzaka zamma 1980 nanga tikamunene munthu chifukwa choti wavala mofanana ndiwina wake kkkkkkk 🛌🛌🛌🛌🛌🛌🛌

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r Месяц назад

      😂😂😂😂😂😂😂

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo Месяц назад +1

    Kkkkkkkkkk koma kuli anthu kapena kuli achina yudasi okhaokha?😂😂😂😂😂😂😂mbali yakuno chikangawa yomweyo msonkhano wa Mr chikangawa.Balaka number one pitilizani mtima umenewu❤❤❤❤❤❤ ndakukondani ndife abanja limodzi zigawengazo mutalikile Nazi zingakupheni zili ndi poison

    • @MonyaNtchona
      @MonyaNtchona Месяц назад

      A Malawi chenjerani chakwerayo ali ndi asilikali akulwan

    • @MonyaNtchona
      @MonyaNtchona Месяц назад

      A Malawi chenjerani chakwerayo ali ndi asilikali akulwan

    • @RachelNkhoma-vn2jo
      @RachelNkhoma-vn2jo Месяц назад

      Ok

  • @BenjaminMtima
    @BenjaminMtima Месяц назад +2

    Kodi sound yanuyo mukumveka ngati muli nchigubu bwanji?

  • @RachelNkhoma-vn2jo
    @RachelNkhoma-vn2jo Месяц назад +1

    Mwamuona pharaoh ndi Yudasi anthu oipa kwambiri bola winayo asasanduke Chulu Cha mchere

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Месяц назад +3

    Kodi ku Balaka anthu anapita kuti kukumangowoneka asilikali okha ndi Chakwela zikukhala bwanji

    • @AleksaWilliams-qc6cn
      @AleksaWilliams-qc6cn Месяц назад

      Anafika kukenani mesa

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d Месяц назад

      Anthu ali busy kupanga zaphindu osati kukaona Chikangawa ngati ndi anawafera 😂

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw Месяц назад +2

    Balaka ndikumene inayambila referendum thawi ya kamuzu balaka siyogonatu ayi

  • @ManuelMalunga-mb4hr
    @ManuelMalunga-mb4hr Месяц назад +1

    Watching from Capetown

  • @user-ol1hf7ru1v
    @user-ol1hf7ru1v Месяц назад +1

    Anthu aku balaka Mulungu akudalitseni kwambiri ndinu okonda dziko lanu anthu tikuvutika palibe chifukwa chokhalira busy ndi anthu amagazi mmanja

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Месяц назад +3

    Bala wooooye mwachita bwino Mr chikangawa ndi Mr chifunga osapitako

  • @iangondwe6857
    @iangondwe6857 Месяц назад

    leave chakwera and usi God bless them

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Месяц назад +2

    Koma guyz kkkkk anthu alikutiko kwangoti ziiii😊😊😊

  • @EviChio
    @EviChio Месяц назад +1

    Ndipo ameneyu olo mavoti osadzamupatsa galu ameneyu. Tikuvutika

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz Месяц назад +2

    Kkkkk Koma ndiye kwadza zatu anthu 😂😂😂😂😂😂 chikangawa yomweyo

  • @user-co6sc8om5n
    @user-co6sc8om5n Месяц назад +2

    Aaa uchisilu basi 4 years munali kuti afiti inu Dr chikangawa ndi mr chikangawa

    • @thomasbotha9790
      @thomasbotha9790 Месяц назад +2

      Mfiti za zikuru zikuru zikufuna kunamiza anthu zakupha anthu opanda chifukwa, akatura pasi udondo sadzawonaso ma vote ameneyu chikangawa

    • @thomasbotha9790
      @thomasbotha9790 Месяц назад +1

      Sizoba khahlera landuku laba banthu bazonya, tinabangoni hakisabe bayabeda, kumafunika kuzayamba yamaja

  • @Lucy-p5s
    @Lucy-p5s Месяц назад +2

    Great

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e Месяц назад +1

    Manganya kutalika kwakeko😂😂😂😅😅😅

  • @zimmekapachika6784
    @zimmekapachika6784 Месяц назад +4

    😅😅😅😅😂😂😂😂😂😅😅😅Balaka woyee 😅😅😅😅😅😂😂😂

  • @user-wx1jt5fd2j
    @user-wx1jt5fd2j 2 дня назад

    Amalawi tiyeni tipitilize kuchita ngati zachita anthu akubalaka osamasekerera NG, onazi zikumatha anthu mkumaziseketera aziona sizinati munthu osaweluzika ndalama kumangoononga osamva chisoni amalawi akufa ndi njala otembereredwa inuu

  • @RobertChimenya
    @RobertChimenya Месяц назад +4

    Chisiru Cha president ichi nchewa paja sayendatu ndye apa mwai wapezeka ayenderetu 😂😂😂😂😂😂

  • @ajasikalonga3210
    @ajasikalonga3210 Месяц назад +4

    Nosence where were you all these days

  • @user-ww4ei5fb7d
    @user-ww4ei5fb7d Месяц назад

    Kkkkkk anthu muli kuti guys 😂😂😂😂.
    Yomweyo Chikangawa 😅😅😅

  • @JesseKanjanga
    @JesseKanjanga Месяц назад +1

    Koma SKC udindo wauVP umkamukhala osati zinazi

  • @jeremiahmalikebu2393
    @jeremiahmalikebu2393 Месяц назад

    Kodi ndiye mwati ku farm ya Demeter ku amakataniko. This farm has been there b4 iyeyu kulowa m'boma.

  • @user-mw8dq4is6k
    @user-mw8dq4is6k Месяц назад +1

    Mr chikangawa ndi VP nde akuyendatu ngat campaign yayambika kale😮

  • @thomasbotha9790
    @thomasbotha9790 Месяц назад +1

    Sikulina anthu azapanga transfer ena Azapita ku Zambia ena ku Tanzania 🇹🇿 chifukwa cha mavuto boma silibwino ndalama zimabedwa kwambiri chithandizo palibe

  • @prettytambala5687
    @prettytambala5687 Месяц назад +2

    Koma mpaka kukayendera nyemba like seriously apule?

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON Месяц назад

    Mukufuna kumangoba zitukuko chamuthu chabe osati ndi boma linalima zimenezo mabodza basi 😅😅😅😅😅😅😅😅 koma azitsogoleri Enawa eeeti

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON Месяц назад

    Sazidziwa zawulimi mukungo tha mawu palibe chomwe chikulowa mmakutumo. Koma zomwe akuganiza akachoka kumeneko ndi kukaba mitsonkho ya thu avutika ba mutamuwuza zamitsokho nde nde eeeeeee sngajowejowetu Tsinzina mntole mr Raza 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @muhammadisaid3968
    @muhammadisaid3968 Месяц назад

    Zachita bwino osapita anthu, chipani chokupha chimenecho, chondee ma boma ena mutengelepo phudzilo osawasekelera akanganya amenewa , I'm White Willison from machinga T/A chamba , Lulindi villege

  • @DavisonKambia
    @DavisonKambia Месяц назад +5

    Bomaloooooo!¡!!

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e Месяц назад

    Utsi watengekatu nawenso ukwela ndege pompano nd zigawenga zimenez😅

  • @PatriciaMbewe-xn7ke
    @PatriciaMbewe-xn7ke Месяц назад

    Kubalaka kuno tinali busy kusaka ya thumba lachimanga mpata opita Kwa apulesidenti sitinaupese😂

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6no Месяц назад

    Abale azanga musiyen manganya ,usamunyoze zakutsogolo sizidziwika , adzatero Ali ana anu Ali pa mpando wa up resident

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 Месяц назад +1

    Ife tidya masambao za ziii munali kuti nthawi yoseyi aaaaa ife si zisilu

  • @user-nv3rf7bl7r
    @user-nv3rf7bl7r Месяц назад +2

    Ulimu wanu ma pulezdent athu ❤❤❤❤❤❤

  • @bristonmwenga5286
    @bristonmwenga5286 Месяц назад

    Wow!what a good initiative

  • @NellieMaulidiChimanda-p5t
    @NellieMaulidiChimanda-p5t Месяц назад

    Tiyeni titenge ngongole za Neef kuti titukule Business zathu ndi magulu a business Ndalama zimene akhazikitsa a President

  • @user-im8bv2el9b
    @user-im8bv2el9b Месяц назад +3

    Kodi Michael usi wavala kut afanane ndi big akunamatu uyu komanso iye kuzavula chipewa.
    Manganya iwe ndiwa map to see tikuziwa

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Месяц назад +1

    Mr chikagawa akuondatu mzimu wachilima ukuzuguza

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani Месяц назад +1

    Idzidzi sidzingapangitse kutsitsa katundu ndi kukweza mphavu Kwacha

    • @anthonynkhoma4265
      @anthonynkhoma4265 Месяц назад

      Ngati ndinu mbuli ingokhalani musaonetse umbuli wani

    • @FrankKambwani
      @FrankKambwani Месяц назад

      Inuyo kuzindikira kwanuko kulipati?

  • @giftblack7690
    @giftblack7690 Месяц назад

    Chakwela akumukonda manganya Chifukwa choti akudziwa kuti sangamusokoneze olo zinthu zikulakwika akudziwa kuti yemwe akanandisokoneza ndi chilima anamupha uja munthu wachabe uyu zoti ndale ndi mfundo wowinayo awine koma osati kuphana nde paliso ndale ngati mukuphana atsogoleli kusokoneza ndale kumeneko

  • @user-qb4pj5yy5b
    @user-qb4pj5yy5b Месяц назад

    Balaka! Balaka! Balaka! How many times have I called you?😂

  • @UsumanLuwayo
    @UsumanLuwayo Месяц назад +1

    Muwaudze akadulitse magalasi ofanana ndi nkhope yawo a vice president, ma galasi akuwpatsa busy

  • @hesidomi
    @hesidomi Месяц назад

    Komaso kodi mwati nkwawa zunguwa akatero azizakamba ngat Iwo apa

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Месяц назад +1

    Chikangawa ndi chifunga akuti akukayendela chiani

  • @MeriaMasinga
    @MeriaMasinga Месяц назад

    Mayi chakwera ndakaika ngati akuvanawo

  • @BlessingsSeleman
    @BlessingsSeleman Месяц назад

    Kod zolimadzo zoti zalimidwa kuchokera kundalama yatu yamisoko kapena dzida ngati zimenezi zoti sizadzungu koma tagula toka nditimisoko tathu tiziona Lori poti mukulimbika kuonesa mukuti mamega famu kod ndi anthu kapena angelezi

  • @user-ss9sr7bi6f
    @user-ss9sr7bi6f Месяц назад

    Ulimi ndiwabwino kwabasi kananji othilira umapindula mwachangu

  • @bristonmwenga5286
    @bristonmwenga5286 Месяц назад

    Ngati sanapite so what?good show a PULE

  • @AmosMilanzi
    @AmosMilanzi Месяц назад

    Boma la MCP kukamba mowona mtima labwera kudzakhala komanso kuthandidza a Malawi.

  • @PraiseMitton
    @PraiseMitton Месяц назад

    Kodi tinene kuti a chakwera akuonda ndichani makamaka 😂 mwina ndi bakili muluzi tv eti kkkkkk achoke!! achoke!! Chakwera achoke!! Achoke.

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y Месяц назад

    Kapoli wankulu adafika mu Mbalaka 😢😢😢 uyo wamfupiyo Yudas 😢. Ayi zikomo 😢😢😢

  • @magex887
    @magex887 Месяц назад

    Chikangawa crue

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Месяц назад +1

    Athu sangapiteko akulira maliro a chilima NDI Lucius Banda

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Месяц назад +1

    Madam Ake a VP ndioukilatu

  • @BMDMasulani
    @BMDMasulani Месяц назад +1

    Mufuti yonseyo ngati mukupita ...kunkhondo zikumakoma bwana usi akayenda okha ulimi ukuchita kukongola koma bwanji mifuti choncho?

  • @HaliJana
    @HaliJana Месяц назад

    😂😂😂😂 ZIKUTANTHAUZA KUTI CHAKWERA AKAMUVOTELE NDI ASILIKALI NDI APOLIC AKEO KKKK CHIKANGAWA YOMWEYO

    • @anthonynkhoma4265
      @anthonynkhoma4265 Месяц назад

      Ku mangochi aja avotera councilor wa mcp ndi asirikali?

  • @brownpetroscoplandmalemia1551
    @brownpetroscoplandmalemia1551 Месяц назад

    Wasting Tax payers money

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад +1

    Ausi zobvalazo sizikukukhalani bola Chilima zimamukhala😂

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms Месяц назад +5

    Kulibeko anthu bwanji kodi

  • @RebeccaNvenya
    @RebeccaNvenya Месяц назад

    Chikangawa ikungoononga ndalama ndinu agalu kwabasi

  • @BlessingsBanda-ol2pg
    @BlessingsBanda-ol2pg Месяц назад +1

    Azalira chikangawa😂😂😂😂😂😂😂

  • @user-rz6vf9wh5c
    @user-rz6vf9wh5c Месяц назад

    Chakwera ndiwowinawina palibe angamake

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6no Месяц назад

    Mudzafa ndi ukapolo onyaweza kadzinyoza , mwina umapwza mphoto

  • @williamsalexmbonga
    @williamsalexmbonga Месяц назад

    Zama big izi guys ndipo MCP siikugonja amtaaa

  • @AlexMlenga-kc5cz
    @AlexMlenga-kc5cz Месяц назад

    😂😂😂😂 km monica yekha ulusi amayika sangachite kufuna phunzitsi 😂😂😂😂😂😂

  • @MeriaMasinga
    @MeriaMasinga Месяц назад

    Balaka ndiyozindikira siphwekesa akupherani mayi shanil zimbii

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft Месяц назад

    Amanganya oro kuvara jombo osatalikabe

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 Месяц назад

    Kwanti ziiiii anthu akubalaka ulemu wanu ndinthu

  • @finiasmtete
    @finiasmtete Месяц назад

    Gwilani ntchito yanu yabwino a Vp.Mwayamba bwino

  • @YohaneColumbus
    @YohaneColumbus Месяц назад

    Dr. Chikangawa Chifunga mwapeza nyekhwe, balaka siimasekelera zopusa. Rest in peace Dr. Saulos klaus chilima

  • @barnettbmphanda108
    @barnettbmphanda108 Месяц назад

    Olemba zoyipanu kalembani nsanje ikakula ndi choncho

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Месяц назад +1

    Yakuli andu ambili 😂😂😂 2024 mtionazindu 😂

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Месяц назад +1

    Koma mavalidwe amonica yooooo9😂😂😂😂

  • @TinoCharamba-hr9el
    @TinoCharamba-hr9el Месяц назад +1

    Kkkkk km zilikotu mangabya kuuluka ulusi monga malemu chilima

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em Месяц назад

    Anthu aku Balaka mumakwana, mumaopadi mulungu

  • @MarvellousTech-kz6no
    @MarvellousTech-kz6no Месяц назад

    Unyozawe ukamaliza kunyoza mphoto imene ulandire utionetse