This type of leadership is nonsense,,,where were you in the previous years,,,mwatifuna pano??? I can't forget and forgive you guys,,,manganya stop blind folding malawians plz,,supervision yomwe mukupangayi is full of fault finding not rectification,,
Kodi maesa pafupi ndi immigration bwanji wosapita kumeneko akulimbana ndi malo woti kulibe mvuto ambiri
Tidyatuu Koma MCP ikuchoka basiii,kudya ndiulere
Amalawi ndalama zo akunena manganya mugulisa moyo ziko ana anu pamutengo osika. Komaso muwuzeni kuti timaowoza zisiro zaboza kuti ziziwike uchisiro wake. Palibe andale amene amatuma anthu kuti aziwowoza. Palipose pamene mungapite nkhani ndingongole ndikuti amalawi akusangala ndingongole. Amalawi please ganizani mozama atsogoleri ndi fundu less ya ngongole. Munthu wazeru sayika ndalama pasogolo koma amapereka zofunikira kwa anthu osati ndalama. Ndalama simulandila nose kuma school ithandiza nose chipatala chithandiza nose misewu chakudya osati ngongole ndikupupuluma kumeneko
U Vice winawu. Hopeless. Becoming NEEF officer zoona?
Ndipo ndizoonadi ambuye atithandize
Gwilani ntchito basi
Tapitani ku immigration bambo a sikono
🤣🤣🤣🤣🤣🤸🐐
Kodi osamuthibula bwanji kape ameneyu
Very well said Mr Vice President Sir.. Mumakwanira
Malawians let’s be careful.
Apanga bwanj tsogolo mmayesa munkat mupereka ntchito 1 million nde mumati adzitani
Amen
Muziyenderanso kumuzi muone umphawi not ntown mokhamo.
Zachibwana
Please bwana kudya ndi ulimi tindalamato pitisani Ku fertilizer tigule fetereza mochipa osati k 100,000 thumba limozi
Nde zikwana anthu angat ndalamazo amalawi osapusa
Be careful Malawi
Chinjerani akufuna kukupusitsani Ambuye!
Nice said Mr v president
Azingoyendera osati kuwauza kuti avotere mcp. Mcp ichoke basi
Bambo athu aShaker,Mr Odilo &Gift kazembe ndskuonani😄
Ntchito 1 million zija zili kuti chisankho chisanafike other wise dpp my vote
Tapitani kuchipatala mukawawone anthu odwala amene akusowa mankhwala osati kukawona ogwila nthito ayi
Mmmmmmm ndale
Iwe usi ndi chipani chako cha MCP ndiweso ukumatuma achinyama kumawowoza mumizinda ndi miseu,powapasa ndalama. Ndiye ukuti chiyani
Dr utsi he is busy collecting data good job
koma the DC uja nkatundudi sizija amanena zija izi, kampeni yavutadi pamalawi end kubomaku kuli dola zoseweretsadi eti
Tidya ndalamazo koma your fired
Atsanakhadzikike usi watsegula kare file kuva udindo kukoma akuti
Afunseni kuti nchifukwa chiyani izi zabwera nthawi yino kuti muonese kulephera kwa chilima ; voti ndi mumtima
Kachibowo malunga ndakuona braz kkkk
Vice president wopenga uyu, alibe mfundo
Pano nde akuti ndalama zopanda chikore mesa iyeyo akupanga kampeni ,si booza ana anthu azavutika kugula zinthu ,tikapanda kusamala
Abazanbili akufna atpake Ife azatnamizle pa m'mawa Kut tinadyanawo
Akuti fuso not ndemanga bwanji Kodi
Mwajijirikatu
Kumbali yanu mukukwanisa koma mukafikenso kumapasipoti kulinso mavuto
Ndalamatso ndizatu amalawi osakana landirani koma osapanga mistake kukafotera mcp please anthu awa akutipanga chikole .awononga kwacha alibe mphanvu pano
Chaka cha mawa wina alira
Mupusa kwa Nthawi yochepa yomweyi ndithu kkkkkkk tabalandilani muzawavoteleso kuti muzililabe ndi mavuto omwe akufuna akuyiwalitseniwa timiyezi tochepa tomweti kuti muzalile kwa zaka zinaso 5 😂😂😂😂😂😂 ine pheee kuno kupanga ndalama zanga
Just listen to him he said July and August 😂😂😂 which July?
Ausi akuwoneka ngati ndiotha zinthu,zaziii basi,mwaziwachilima uli pamutu pako ndichikangawa nzakoyo .truth shall prevail.our anger will not vanish unto our memories.
Never vanish suspect akupezekabe
Malawi ndi ndale zake, ine Phee kukumverani kkkkkkk
This type of leadership is nonsense,,,where were you in the previous years,,,mwatifuna pano??? I can't forget and forgive you guys,,,manganya stop blind folding malawians plz,,supervision yomwe mukupangayi is full of fault finding not rectification,,
Manganya mukumva kukoma mutamupha chilima kufana udindo chosecho anakuyikani kale pabwino kumuphasa km zikoli muliphe ndi dr chikangawa
Bambo a sikono ndi Tikuferanji tsopano
Atsanakhadzikike usi watsegula kare file kuva udindo kukoma akuti nde antinte ndevu akuti aoneke ngati Chilima🙄🤔
😂
Awa assavutike mwiniwake amakwanitsa chilima awa alibe molaro
Waaaaa nza boma kwene kkkkkkk ndikanakhala ku Malawi ndikanazitenga kuzidyaidya ine cheteeee
Microphone ndiodula kwambiri Kodi?
Sakunama anyamata kungozuka basi ku mow
Asanduka adad
Good advise VP
Nkhani ndi yakuti kodi ndalamazi siotse omwe angalandile ..sizingatheke kuti musitse zinthu kuti wina aliyetse aziyetse kumbali yake not ngongole ..ngongole salandila yonse
Ine mundipatse number ya vp'wo ndili nawo zowalankhula
Mantha akewo😂
😂😂😂😂😂koma bambo a.SIKONO
😂😂😂koma
Ndalama zabooka kuboma kobasi
1 million ndi drama nanuso akulu
Ngati akupanga comedy
Wayamba bwino
Koma ndalama izo mutipasadi
Michael Usi Ali ndi matama
Nanunso pali za matamanso pamenepa?
Campaign yayandikira 😂😂😂😂
Amalaw tachangamukani achilima amkatani Kodi pano anatisiya mmanja mkhosi mabodxa okhaokha anthu Andale ndi agalu tsekurani maso amalaw musangopusitsidwa
Za ziii sm old song
Kape wachabechabe iwe
Sizikumukhalayi
Eee kuchita kusaka anthu kuti awapase ngongole zavuta kumpanda
Uyu anamutuma uyu akusokonezani
Chikangawa iwe pelekani Kaye kuno nanga mwayambila paja osapeleka ndalama
Anyamata landirani ndalama zo zaphweka koma chonde tisazavoteleso MCP
Iweyo asakupatse udya mwano wako omweo
@@MarvellousTech-kz6no ndidya Koma vote yanga yokha asayembekezele
Hypocrisy
Wasowa zokamba uyu
Wachamba manganyayo
Mfiti izi
😂,,😂😂😂😂😂km usi wabwera ndi ululutu
Iwe ukanakhala president ndiye zikanakhala bwino heavy.........koma vice mmmmmmm
2024
Mmm Koma tiona zinthu mu 2024 kutseia pakamwa anthu kkkkkk
Apresdent kkkk
Apanga bwanji sogolo alibe dzochita machende ankhuku
Ifeyo tidya zimenezo co ndi zathu basi
Moti chakwera atati afe Lero basi mtsogoleri akhala USI 😂😂😂😂😂😂 manyaka enieni
Ma plan a mulungu aposa amuthu
Mulungu amakweza zowoneka zonyozekazo. Read the story of Joseph in the Bible.
Uyu nchitsiru sure
Ukhalira yomweyo yotukwanayo
Tapitani ku immigration, passport yannga mpaka pano
Via chikangawa ayedzeka Nadi ndale ndi usiku
Mavuto kwabasi, Kkkkkkkk Kkkkkkkk!
Bwelani ku mzuzu bwana usi
Ndalama zimenezi mmalo moyika kumakampani kuti katundu asike mitengo koma kumangolimbana ndizazii
Akuti atsitsa chaka chamawa
Mthawi yanu yatha inu.mutifune lero
Guys mukakamileni ameneyu mudya naye matsiku ano mpata ukapezeka chita nawonu nawoso akumba ndalama za boma mukuziwa kale zandale zilibe ntchito
Iwe kamanganya ndiwe kachisiri bwanji upite ku imigireshoni uko uone nimumene anthu akuririra ukurimbana nianthu omwe akugurisa ziboribori uziwanamiza anthu inu segurani maso osazawapasa voti ayi
Tengani ma 10milion😅
Nde nu nkhatabay mupita liti
Ife tizakuyamikani ngati nzipatala mutakhala medicine osati zimenezo
😂😂😂😂😂komatu.
Chikangawa
Eee kwatani
Zosamukhala
Inetso ndikapita ku Malawi ndikukasapota mcp ndikadyele ndalama zaulele mvote ili mtima chifukwa kwasala sewelo ku Malawi
Abambo asikono chibwana icho
Kupunsa agalu inu