ZOMWE VICE PRESIDENT MICHAEL USI WAYAKHULA KWA MA VENDOR A PAZIBOLIBOLI LERO MU NZINDA WA BLANTYRE

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 7 сен 2024

Комментарии • 114

  • @KayMohamed-g7d
    @KayMohamed-g7d Месяц назад +10

    Kodi maesa pafupi ndi immigration bwanji wosapita kumeneko akulimbana ndi malo woti kulibe mvuto ambiri

  • @SophieMbengo
    @SophieMbengo Месяц назад +6

    Tidyatuu Koma MCP ikuchoka basiii,kudya ndiulere

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Месяц назад +5

    Amalawi ndalama zo akunena manganya mugulisa moyo ziko ana anu pamutengo osika. Komaso muwuzeni kuti timaowoza zisiro zaboza kuti ziziwike uchisiro wake. Palibe andale amene amatuma anthu kuti aziwowoza. Palipose pamene mungapite nkhani ndingongole ndikuti amalawi akusangala ndingongole. Amalawi please ganizani mozama atsogoleri ndi fundu less ya ngongole. Munthu wazeru sayika ndalama pasogolo koma amapereka zofunikira kwa anthu osati ndalama. Ndalama simulandila nose kuma school ithandiza nose chipatala chithandiza nose misewu chakudya osati ngongole ndikupupuluma kumeneko

    • @victorkachepa3515
      @victorkachepa3515 Месяц назад

      U Vice winawu. Hopeless. Becoming NEEF officer zoona?

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d Месяц назад

      Ndipo ndizoonadi ambuye atithandize

    • @Nga-y1k
      @Nga-y1k Месяц назад

      Gwilani ntchito basi

  • @HarryKandani
    @HarryKandani Месяц назад +7

    Tapitani ku immigration bambo a sikono

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Месяц назад +1

    Kodi osamuthibula bwanji kape ameneyu

  • @Anti_social_938
    @Anti_social_938 Месяц назад +1

    Very well said Mr Vice President Sir.. Mumakwanira

  • @andreabanda7838
    @andreabanda7838 Месяц назад +4

    Malawians let’s be careful.

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад +3

    Apanga bwanj tsogolo mmayesa munkat mupereka ntchito 1 million nde mumati adzitani

  • @LidyaGoodson-fb4tt
    @LidyaGoodson-fb4tt Месяц назад

    Amen

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu Месяц назад +1

    Muziyenderanso kumuzi muone umphawi not ntown mokhamo.

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 Месяц назад +4

    Zachibwana

  • @user-kt2yc6dp7q
    @user-kt2yc6dp7q Месяц назад +2

    Please bwana kudya ndi ulimi tindalamato pitisani Ku fertilizer tigule fetereza mochipa osati k 100,000 thumba limozi

  • @gkay-striker
    @gkay-striker Месяц назад +1

    Nde zikwana anthu angat ndalamazo amalawi osapusa

  • @enockkanyerere784
    @enockkanyerere784 Месяц назад +1

    Be careful Malawi

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Месяц назад +1

    Chinjerani akufuna kukupusitsani Ambuye!

  • @gearardphiri6904
    @gearardphiri6904 Месяц назад

    Nice said Mr v president

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Месяц назад

    Azingoyendera osati kuwauza kuti avotere mcp. Mcp ichoke basi

  • @memoryziyaya2593
    @memoryziyaya2593 Месяц назад

    Bambo athu aShaker,Mr Odilo &Gift kazembe ndskuonani😄

  • @BusumanNzengeza
    @BusumanNzengeza Месяц назад

    Ntchito 1 million zija zili kuti chisankho chisanafike other wise dpp my vote

  • @user-bi6pb5gc8t
    @user-bi6pb5gc8t Месяц назад +1

    Tapitani kuchipatala mukawawone anthu odwala amene akusowa mankhwala osati kukawona ogwila nthito ayi

  • @mayachikadewa7551
    @mayachikadewa7551 Месяц назад +2

    Mmmmmmm ndale

  • @BrightonKennedy-jd6fl
    @BrightonKennedy-jd6fl Месяц назад

    Iwe usi ndi chipani chako cha MCP ndiweso ukumatuma achinyama kumawowoza mumizinda ndi miseu,powapasa ndalama. Ndiye ukuti chiyani

  • @lukepangani1373
    @lukepangani1373 Месяц назад

    Dr utsi he is busy collecting data good job

  • @LottiAffati
    @LottiAffati Месяц назад

    koma the DC uja nkatundudi sizija amanena zija izi, kampeni yavutadi pamalawi end kubomaku kuli dola zoseweretsadi eti

  • @PreciousHenderson-qc1hq
    @PreciousHenderson-qc1hq Месяц назад

    Tidya ndalamazo koma your fired

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Месяц назад +1

    Atsanakhadzikike usi watsegula kare file kuva udindo kukoma akuti

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Месяц назад

    Afunseni kuti nchifukwa chiyani izi zabwera nthawi yino kuti muonese kulephera kwa chilima ; voti ndi mumtima

  • @RobertNyaude
    @RobertNyaude Месяц назад +1

    Kachibowo malunga ndakuona braz kkkk

  • @musasiyama9423
    @musasiyama9423 Месяц назад

    Vice president wopenga uyu, alibe mfundo

  • @user-jb5hr4rz2s
    @user-jb5hr4rz2s Месяц назад

    Pano nde akuti ndalama zopanda chikore mesa iyeyo akupanga kampeni ,si booza ana anthu azavutika kugula zinthu ,tikapanda kusamala

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m Месяц назад

    Abazanbili akufna atpake Ife azatnamizle pa m'mawa Kut tinadyanawo

  • @Brihippo
    @Brihippo Месяц назад

    Akuti fuso not ndemanga bwanji Kodi

  • @YamikanKhofia
    @YamikanKhofia Месяц назад

    Mwajijirikatu

  • @emilynthite6545
    @emilynthite6545 Месяц назад

    Kumbali yanu mukukwanisa koma mukafikenso kumapasipoti kulinso mavuto

  • @IsmaelBilal-lh1pi
    @IsmaelBilal-lh1pi Месяц назад

    Ndalamatso ndizatu amalawi osakana landirani koma osapanga mistake kukafotera mcp please anthu awa akutipanga chikole .awononga kwacha alibe mphanvu pano

  • @praisechikuni8200
    @praisechikuni8200 Месяц назад

    Chaka cha mawa wina alira

  • @giftblack7690
    @giftblack7690 Месяц назад

    Mupusa kwa Nthawi yochepa yomweyi ndithu kkkkkkk tabalandilani muzawavoteleso kuti muzililabe ndi mavuto omwe akufuna akuyiwalitseniwa timiyezi tochepa tomweti kuti muzalile kwa zaka zinaso 5 😂😂😂😂😂😂 ine pheee kuno kupanga ndalama zanga

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Месяц назад

    Just listen to him he said July and August 😂😂😂 which July?

  • @OliverChimsewu
    @OliverChimsewu Месяц назад +4

    Ausi akuwoneka ngati ndiotha zinthu,zaziii basi,mwaziwachilima uli pamutu pako ndichikangawa nzakoyo .truth shall prevail.our anger will not vanish unto our memories.

    • @sarahmphande6108
      @sarahmphande6108 Месяц назад

      Never vanish suspect akupezekabe

    • @Nga-y1k
      @Nga-y1k Месяц назад

      Malawi ndi ndale zake, ine Phee kukumverani kkkkkkk

  • @YamikaniMwale-bo7cv
    @YamikaniMwale-bo7cv Месяц назад

    This type of leadership is nonsense,,,where were you in the previous years,,,mwatifuna pano??? I can't forget and forgive you guys,,,manganya stop blind folding malawians plz,,supervision yomwe mukupangayi is full of fault finding not rectification,,

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb Месяц назад

    Manganya mukumva kukoma mutamupha chilima kufana udindo chosecho anakuyikani kale pabwino kumuphasa km zikoli muliphe ndi dr chikangawa

  • @MirriamKambale
    @MirriamKambale Месяц назад

    Bambo a sikono ndi Tikuferanji tsopano

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Месяц назад

    Atsanakhadzikike usi watsegula kare file kuva udindo kukoma akuti nde antinte ndevu akuti aoneke ngati Chilima🙄🤔

  • @RabanChiumia
    @RabanChiumia Месяц назад

    Awa assavutike mwiniwake amakwanitsa chilima awa alibe molaro

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Месяц назад

    Waaaaa nza boma kwene kkkkkkk ndikanakhala ku Malawi ndikanazitenga kuzidyaidya ine cheteeee

  • @YohaneColumbus
    @YohaneColumbus Месяц назад

    Microphone ndiodula kwambiri Kodi?

  • @MADALITSOJoseph
    @MADALITSOJoseph Месяц назад

    Sakunama anyamata kungozuka basi ku mow

  • @user-ln5hw7dn9g
    @user-ln5hw7dn9g Месяц назад

    Asanduka adad

  • @lawrencemakina2882
    @lawrencemakina2882 Месяц назад

    Good advise VP

  • @user-rv8gi4ro6r
    @user-rv8gi4ro6r Месяц назад

    Nkhani ndi yakuti kodi ndalamazi siotse omwe angalandile ..sizingatheke kuti musitse zinthu kuti wina aliyetse aziyetse kumbali yake not ngongole ..ngongole salandila yonse

  • @realsu7816
    @realsu7816 Месяц назад

    Ine mundipatse number ya vp'wo ndili nawo zowalankhula

  • @StevenMughogho-m1f
    @StevenMughogho-m1f Месяц назад

    Mantha akewo😂

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga 29 дней назад

    😂😂😂😂😂koma bambo a.SIKONO

  • @ClydeNyasulu-tk6fj
    @ClydeNyasulu-tk6fj Месяц назад

    😂😂😂koma

  • @aaronmagombo9805
    @aaronmagombo9805 Месяц назад

    Ndalama zabooka kuboma kobasi

  • @ChikumbutsoTsalangu
    @ChikumbutsoTsalangu Месяц назад

    1 million ndi drama nanuso akulu

  • @AndrewUnbreakable
    @AndrewUnbreakable Месяц назад

    Ngati akupanga comedy

  • @cyrusmichael6906
    @cyrusmichael6906 Месяц назад

    Wayamba bwino

  • @Brihippo
    @Brihippo Месяц назад

    Koma ndalama izo mutipasadi

  • @user-ox4dh3ey6b
    @user-ox4dh3ey6b Месяц назад +1

    Michael Usi Ali ndi matama

  • @emmanuelpiffano259
    @emmanuelpiffano259 Месяц назад

    Campaign yayandikira 😂😂😂😂

  • @ELLENZAPS
    @ELLENZAPS Месяц назад

    Amalaw tachangamukani achilima amkatani Kodi pano anatisiya mmanja mkhosi mabodxa okhaokha anthu Andale ndi agalu tsekurani maso amalaw musangopusitsidwa

  • @user-vn6di8hc1v
    @user-vn6di8hc1v Месяц назад

    Za ziii sm old song

  • @AbudulLatfu
    @AbudulLatfu Месяц назад

    Kape wachabechabe iwe

  • @TroubleKatsala-jp2li
    @TroubleKatsala-jp2li Месяц назад

    Sizikumukhalayi

  • @MercyMbisa
    @MercyMbisa Месяц назад

    Eee kuchita kusaka anthu kuti awapase ngongole zavuta kumpanda

  • @hopembendela
    @hopembendela Месяц назад

    Uyu anamutuma uyu akusokonezani

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Месяц назад

    Chikangawa iwe pelekani Kaye kuno nanga mwayambila paja osapeleka ndalama

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Месяц назад

    Anyamata landirani ndalama zo zaphweka koma chonde tisazavoteleso MCP

    • @MarvellousTech-kz6no
      @MarvellousTech-kz6no Месяц назад

      Iweyo asakupatse udya mwano wako omweo

    • @GraceZumazuma
      @GraceZumazuma Месяц назад

      @@MarvellousTech-kz6no ndidya Koma vote yanga yokha asayembekezele

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg Месяц назад

    Hypocrisy

  • @musasiyama9423
    @musasiyama9423 Месяц назад

    Wasowa zokamba uyu

  • @EdwardSamuel-xj8qq
    @EdwardSamuel-xj8qq Месяц назад

    Wachamba manganyayo

  • @RabanChiumia
    @RabanChiumia Месяц назад

    Mfiti izi

  • @CharlesPhiri-ds1rk
    @CharlesPhiri-ds1rk Месяц назад

    😂,,😂😂😂😂😂km usi wabwera ndi ululutu

  • @crytoniegrantliffa2431
    @crytoniegrantliffa2431 Месяц назад

    Iwe ukanakhala president ndiye zikanakhala bwino heavy.........koma vice mmmmmmm

  • @victormaluwa6710
    @victormaluwa6710 Месяц назад

    2024

  • @Steven-q4u
    @Steven-q4u Месяц назад

    Mmm Koma tiona zinthu mu 2024 kutseia pakamwa anthu kkkkkk

  • @JefreyMtambo
    @JefreyMtambo Месяц назад

    Apresdent kkkk

  • @FrynessMoyo-to2du
    @FrynessMoyo-to2du Месяц назад

    Apanga bwanji sogolo alibe dzochita machende ankhuku

  • @JuvenileDebwe-bv8ow
    @JuvenileDebwe-bv8ow Месяц назад

    Ifeyo tidya zimenezo co ndi zathu basi

  • @user-ol1hf7ru1v
    @user-ol1hf7ru1v Месяц назад

    Moti chakwera atati afe Lero basi mtsogoleri akhala USI 😂😂😂😂😂😂 manyaka enieni

    • @tamalangoma2765
      @tamalangoma2765 Месяц назад

      Ma plan a mulungu aposa amuthu

    • @PraiseKadzitche
      @PraiseKadzitche Месяц назад +1

      Mulungu amakweza zowoneka zonyozekazo. Read the story of Joseph in the Bible.

  • @user-ji4xn6me8d
    @user-ji4xn6me8d Месяц назад +1

    Uyu nchitsiru sure

  • @user-gd6zb2bv8f
    @user-gd6zb2bv8f Месяц назад

    Tapitani ku immigration, passport yannga mpaka pano

  • @Steven-q4u
    @Steven-q4u Месяц назад

    Via chikangawa ayedzeka Nadi ndale ndi usiku

  • @victorkachepa3515
    @victorkachepa3515 Месяц назад

    Mavuto kwabasi, Kkkkkkkk Kkkkkkkk!

  • @user-ve2ts3yr2n
    @user-ve2ts3yr2n Месяц назад

    Bwelani ku mzuzu bwana usi

  • @GoodsonJulio-n8f
    @GoodsonJulio-n8f Месяц назад

    Ndalama zimenezi mmalo moyika kumakampani kuti katundu asike mitengo koma kumangolimbana ndizazii

  • @CorneliousKaliat
    @CorneliousKaliat Месяц назад

    Mthawi yanu yatha inu.mutifune lero

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Месяц назад

    Guys mukakamileni ameneyu mudya naye matsiku ano mpata ukapezeka chita nawonu nawoso akumba ndalama za boma mukuziwa kale zandale zilibe ntchito

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Месяц назад

    Iwe kamanganya ndiwe kachisiri bwanji upite ku imigireshoni uko uone nimumene anthu akuririra ukurimbana nianthu omwe akugurisa ziboribori uziwanamiza anthu inu segurani maso osazawapasa voti ayi

  • @JessicaManda-zm1ug
    @JessicaManda-zm1ug Месяц назад

    Tengani ma 10milion😅

  • @JessicaManda-zm1ug
    @JessicaManda-zm1ug Месяц назад

    Nde nu nkhatabay mupita liti

  • @mathewsmbaluko8522
    @mathewsmbaluko8522 Месяц назад +1

    Ife tizakuyamikani ngati nzipatala mutakhala medicine osati zimenezo

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Месяц назад

    😂😂😂😂😂komatu.

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz Месяц назад

    Chikangawa

  • @MercyMithie
    @MercyMithie Месяц назад

    Zosamukhala

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Месяц назад

    Inetso ndikapita ku Malawi ndikukasapota mcp ndikadyele ndalama zaulele mvote ili mtima chifukwa kwasala sewelo ku Malawi

  • @jamiajafali6619
    @jamiajafali6619 Месяц назад

    Abambo asikono chibwana icho

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w Месяц назад

    Kupunsa agalu inu