GWEDE-GWEDE PA 27 June 2024🙌🙌🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 29 сен 2024

Комментарии • 60

  • @JacobMsukwa-q6v
    @JacobMsukwa-q6v 3 месяца назад

    We're living in the world where the book of smouldering charcoal is still working.Chilima,,, John Phombe magufuri gone some few months/yeas ago
    NB:there legacies remained unshakable

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 месяца назад +5

    boma ili lolamulila zigawenga zokha zokha zitsiru mbava chakwera ndi chitsiru chotheratu chigananga

  • @MarvGerald
    @MarvGerald 3 месяца назад +2

    Kumibawa inu nokha ndiamene ndimakufilan mumanena chilungamo boma ili ndilofoira

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 3 месяца назад +1

    Zimene mwanena stive banda ndizoona a police akupanga zopupuluma chikwa cha ndale ena.vuto boma ili ambiri zeru alibe chifukwa chopana cheru ndichifukwa amapupulumisa a police. And munthu walakwa ku mzuzu makhoti alikoko police ili koko basi bwerani naye kuno ku lilongwe kuli chani ku lilongwe.

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 месяца назад +3

    kungoti kuyambira chakwera 'apolice' army ndi nduna zonse ndi zitsiru zokha zokha mbava zigawenga

  • @nasibukombo4302
    @nasibukombo4302 3 месяца назад

    Cyber act will not yield anything, freedom of speech is enacted in our mother law( Constitution).

  • @KayangeNicholas-vl6nu
    @KayangeNicholas-vl6nu 3 месяца назад

    Ine koma chomwe ndikuona chimalakwika mdziko muno ndichokuti:Civil servant akalakwila munthu/anthu,nkhuluza mulandu,chipepetso chimachoka ku boma.Monga a waterboard kumwetsa anthu madzi onyasa(uku ndikunyalanyaza chabe,just lack of seriousness) Anthu onyalanyazawa pa ntchito bwenzi akuwadula salary nkhupanga compensate ma victims.

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад

    Su Chakwera ma constitution ndi abakili muluzi....koma we pray munthu wamulungu azabwera malamulo onsewo azawathese

  • @NedsonKanjira-qj2ig
    @NedsonKanjira-qj2ig 3 месяца назад +2

    Onsewa mubomamo ndi zisiru za anthu panali azanu akamanga anthu , kupha anthu uzifuse kuti ali kuti

  • @ChawasoMlotha-ys6bf
    @ChawasoMlotha-ys6bf 3 месяца назад

    Under mcp government, chilungamo ku mzuzu mnthu kumtenga kupita ku lilongwe kuononga mafuta ma orders za ziiii.

  • @MirriamKambale
    @MirriamKambale 3 месяца назад

    Chakwera nzeru alibe muzamuona chipumi bilubilu kaluka panga nawo participate pa function ya CCAP after all this ndikuti ndi galu ndithu

  • @MirriamKambale
    @MirriamKambale 3 месяца назад

    Ngati kuli mbatama za anthu mmalawi ndie a police ndipo ngati kuli anthu ophwanya komanso osaziwa malamulo ndie a police ndipo galu ameneyu mukuti president wamalawwiyu Kaya mukuti chakwera wapepelesa kwambiri a police amenewa

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад

    Ma demo amenewo akufunika ku Malawi, zimagalimoto zodula zonse zigulitsudwe...

  • @MarcFelson
    @MarcFelson 3 месяца назад

    Umakhala uchitsilu wa boma pamodzi ndi umbuli wa apolisi Koma ka pay kang'onong'ono

  • @WillyMajiya
    @WillyMajiya 3 месяца назад

    A police athu amalephera kugwira ntchito yawo mwa professional chifukwa cha ma politicians ena ake a nkhope ngati manyi

  • @RashdShalos
    @RashdShalos 3 месяца назад +2

    AMwene program ya gwede gwede musamayi phonye pilizi bulasa 🎉wanu

    • @lonjezompaso9512
      @lonjezompaso9512 3 месяца назад +1

      mukhoza kumaiona pa official page ya mibawa nthawi zonse

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад

    You two God bless you speaking honest ❤❤❤❤

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 3 месяца назад

    Chakwera afuna axiophyeza athu ngat anayamba kulamulila ndiiye

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 месяца назад +1

    Steve ndayamika pa nkhani yomaliza, President ndi nduna azidzipangila okha zonse osati zaulele m'mene zilili pano. Anthu akuvutika ku midzi. Ndicho chifukwa kudzikhala ma Demonstrations osonyeza kukwiya.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 месяца назад +1

    Apolice akumalawi ndi mbamva chifukwa chake alowesa ndale pa ntchito yawo shame on you

  • @innocentkapachika6591
    @innocentkapachika6591 3 месяца назад

    Nanga training ya ntchito umapanga 6 months and think you can get quality staff

  • @VictorAmos-my8ne
    @VictorAmos-my8ne 3 месяца назад

    Mayi Aja mukuti wankula wapolice ndiwankhunyu

  • @emmanuelchirwa3420
    @emmanuelchirwa3420 3 месяца назад +2

    More 🔥🔥🔥🔥 kodwa Banda umuwalero big man

  • @LemosBanda
    @LemosBanda 3 месяца назад

    Vuto Malawi Police inatha panopa ndi MCP Police.

  • @RazackMofart
    @RazackMofart 3 месяца назад +3

    Big up family,,Nothing but chilungamo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 3 месяца назад +1

    Kuyambila chakwela ndi kabineti yonse apolice army zonse ndi zitsilu za kuba boma la mcp ndi la manyi

  • @EstherShaba-fh8ib
    @EstherShaba-fh8ib 3 месяца назад

    BOMA lopanda nzelu iri

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 3 месяца назад +1

    Anakangosiya kulamulira awunikire bwino ndithu chakwera chitsiru aribe nzeru kwao kwatha garu ameneyo

  • @HazwelMangazao
    @HazwelMangazao 3 месяца назад

    Mr S banda mukunena zoona bwana

  • @greymasha838
    @greymasha838 3 месяца назад

    Chilungamo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 3 месяца назад +1

    God bless you guys 🙏🙏🙏🙏🙏🙏

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 3 месяца назад

    And ziko la Malawi litha kutukuka chachikulu kuchosa mbava zikuononga misokho yamalawi. Nduna president asayendere zinthu zaulele ndichifukwa akupanga matama kutenga ngati ife amalawi ndizisiro

  • @GladMarawaMsowoya
    @GladMarawaMsowoya 3 месяца назад +1

    Walephera chakwela akambe church

  • @YellowmanMalawi-qe8zh
    @YellowmanMalawi-qe8zh 3 месяца назад +1

    Chimwendo wadya1 pa nkhaza ku mcp

  • @gibbohtrust6118
    @gibbohtrust6118 3 месяца назад

    Komaso akumanga bwanji anthu Ma umboni aupeza bwanji mene zinakhalila kuchikangawa

  • @emmanuelchirwa3420
    @emmanuelchirwa3420 3 месяца назад +2

    Point take big man .komaso aziganiza kuti kunyumba kapena kulokecheni kulibe police officer,tisatenge malamuro pamanja azanja lathu. Ndi ye tiyeni tigwilentchi to kulingana ndimalamo , komaso Pali mwambe wakuti ukakhala pabwino lero usayiwale zamawa,chawonamuzakochapita mawa hilipayiwe..ndangoyimapamenepo, amoyo salekana,

  • @MarvGerald
    @MarvGerald 3 месяца назад

    Tikupempha program iiii achisili Achawezi asazalowelere

  • @faroukakwah291
    @faroukakwah291 3 месяца назад

    Chilungamo plus❤ twapukene amagwetu

  • @emberbotoman1613
    @emberbotoman1613 3 месяца назад

    Mulingo omwe wamuyezera mzako nawenso adzakuyezera omwewo

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад

    A police chitani manyazi mukulephera ntchito yanu

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj 3 месяца назад

    Chadwell chinsiru kwambiri

  • @CliffNankumba
    @CliffNankumba 3 месяца назад

    Ndipo ife ana athu timalipira tokha fizi bwanji

  • @BenjaminKamanga-p8w
    @BenjaminKamanga-p8w 3 месяца назад

    Uchigawenga wachuluka kwambiri mmalawi.

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 3 месяца назад

    Kom iweyo umaganiza bwino bwino kobasi

  • @ThomasiSalijeni
    @ThomasiSalijeni 3 месяца назад

    Useless police of malawi

  • @WysonBilly
    @WysonBilly 3 месяца назад

    Kondwani umayankhula. Bwino

  • @tamarajoycemalata
    @tamarajoycemalata 3 месяца назад

    😊

  • @awardjafar2928
    @awardjafar2928 3 месяца назад +2

    JB uja sakumalakwisa akamatukwana msogoleri ndinduna zake

    • @NancyNyirenda-v9o
      @NancyNyirenda-v9o 3 месяца назад +1

      Nanga akamatukwana amalawi nose amalondolaso

    • @LeendaDeborah2005
      @LeendaDeborah2005 3 месяца назад

      @@NancyNyirenda-v9oof course. Ndifedi anthu ogona ambirife

    • @NikolasNanawe
      @NikolasNanawe 3 месяца назад

      JB amangotukwana chamba kwambir alibe fundo

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 3 месяца назад +1

    Chigamulo changa chiyende moteremu chilimat waphedwera agree ment yake ndi chakwera komaso mlandu wasatar , choncho ngat achakwera amupha chilima kuti asale ndiudindo sizitheka , ngat agreement yalephereka pomupha chilima ndibwinoso achakwera aduse aliyese asakhaleposo muthu chilima amalakwa chani ? Nsupa zatulukat taombeza achakwera mwaphat chilima dala inuso mudusa udindowo aliyese asatenge chilima mwapha ife amalawi tiphaso inu bas 50-50 chilungamo titero

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa 3 месяца назад +1

    Ngati wa Mpingoyo anapalamula nde asamangidwe,iyeyo ndi munthu, aaaaaaa ,munakangodzudzula zolakwikwazo,osati mpingo ,mpingo nde chiyani, Mesa mpingo ndi anthu,nde munthuyo ngati walakwitsa nde lamulo lisangwire Ntchito

  • @NoreenNaituri
    @NoreenNaituri 3 месяца назад

    Azibusa asiyenso kulowelela ndale

    • @BrendaJailosi
      @BrendaJailosi 3 месяца назад +1

      Alowelera bwanji iwo akunena chilungamo inu multi mbali iti? Anzathu?

    • @NancyNyirenda-v9o
      @NancyNyirenda-v9o 3 месяца назад

      Ndipo zowona mumalo mokalalikila uko timadabwakuti ku zolozolo bwanji kwabuka ndeu mu church chawoneka kuti niwachinyengo mubusa uyu

    • @LeendaDeborah2005
      @LeendaDeborah2005 3 месяца назад

      Inunso ngt muli opemphera nde musiye zomalimbana ndi anthu

    • @BrendaJailosi
      @BrendaJailosi 3 месяца назад

      @@NancyNyirenda-v9o mukamva kupenga nde uku kd zigandanga zilipo gulutu kd za Infa imeneyi sidzinamukhuze ndindani km anthu akanike kulira fukwa nda zibusa nonsense