We're living in the world where the book of smouldering charcoal is still working.Chilima,,, John Phombe magufuri gone some few months/yeas ago NB:there legacies remained unshakable
Zimene mwanena stive banda ndizoona a police akupanga zopupuluma chikwa cha ndale ena.vuto boma ili ambiri zeru alibe chifukwa chopana cheru ndichifukwa amapupulumisa a police. And munthu walakwa ku mzuzu makhoti alikoko police ili koko basi bwerani naye kuno ku lilongwe kuli chani ku lilongwe.
Ngati kuli mbatama za anthu mmalawi ndie a police ndipo ngati kuli anthu ophwanya komanso osaziwa malamulo ndie a police ndipo galu ameneyu mukuti president wamalawwiyu Kaya mukuti chakwera wapepelesa kwambiri a police amenewa
Steve ndayamika pa nkhani yomaliza, President ndi nduna azidzipangila okha zonse osati zaulele m'mene zilili pano. Anthu akuvutika ku midzi. Ndicho chifukwa kudzikhala ma Demonstrations osonyeza kukwiya.
Point take big man .komaso aziganiza kuti kunyumba kapena kulokecheni kulibe police officer,tisatenge malamuro pamanja azanja lathu. Ndi ye tiyeni tigwilentchi to kulingana ndimalamo , komaso Pali mwambe wakuti ukakhala pabwino lero usayiwale zamawa,chawonamuzakochapita mawa hilipayiwe..ndangoyimapamenepo, amoyo salekana,
Ngati wa Mpingoyo anapalamula nde asamangidwe,iyeyo ndi munthu, aaaaaaa ,munakangodzudzula zolakwikwazo,osati mpingo ,mpingo nde chiyani, Mesa mpingo ndi anthu,nde munthuyo ngati walakwitsa nde lamulo lisangwire Ntchito
We're living in the world where the book of smouldering charcoal is still working.Chilima,,, John Phombe magufuri gone some few months/yeas ago
NB:there legacies remained unshakable
boma ili lolamulila zigawenga zokha zokha zitsiru mbava chakwera ndi chitsiru chotheratu chigananga
Kumibawa inu nokha ndiamene ndimakufilan mumanena chilungamo boma ili ndilofoira
Zimene mwanena stive banda ndizoona a police akupanga zopupuluma chikwa cha ndale ena.vuto boma ili ambiri zeru alibe chifukwa chopana cheru ndichifukwa amapupulumisa a police. And munthu walakwa ku mzuzu makhoti alikoko police ili koko basi bwerani naye kuno ku lilongwe kuli chani ku lilongwe.
kungoti kuyambira chakwera 'apolice' army ndi nduna zonse ndi zitsiru zokha zokha mbava zigawenga
Cyber act will not yield anything, freedom of speech is enacted in our mother law( Constitution).
Ine koma chomwe ndikuona chimalakwika mdziko muno ndichokuti:Civil servant akalakwila munthu/anthu,nkhuluza mulandu,chipepetso chimachoka ku boma.Monga a waterboard kumwetsa anthu madzi onyasa(uku ndikunyalanyaza chabe,just lack of seriousness) Anthu onyalanyazawa pa ntchito bwenzi akuwadula salary nkhupanga compensate ma victims.
Su Chakwera ma constitution ndi abakili muluzi....koma we pray munthu wamulungu azabwera malamulo onsewo azawathese
Onsewa mubomamo ndi zisiru za anthu panali azanu akamanga anthu , kupha anthu uzifuse kuti ali kuti
Under mcp government, chilungamo ku mzuzu mnthu kumtenga kupita ku lilongwe kuononga mafuta ma orders za ziiii.
Chakwera nzeru alibe muzamuona chipumi bilubilu kaluka panga nawo participate pa function ya CCAP after all this ndikuti ndi galu ndithu
Ngati kuli mbatama za anthu mmalawi ndie a police ndipo ngati kuli anthu ophwanya komanso osaziwa malamulo ndie a police ndipo galu ameneyu mukuti president wamalawwiyu Kaya mukuti chakwera wapepelesa kwambiri a police amenewa
Ma demo amenewo akufunika ku Malawi, zimagalimoto zodula zonse zigulitsudwe...
Umakhala uchitsilu wa boma pamodzi ndi umbuli wa apolisi Koma ka pay kang'onong'ono
A police athu amalephera kugwira ntchito yawo mwa professional chifukwa cha ma politicians ena ake a nkhope ngati manyi
AMwene program ya gwede gwede musamayi phonye pilizi bulasa 🎉wanu
mukhoza kumaiona pa official page ya mibawa nthawi zonse
You two God bless you speaking honest ❤❤❤❤
Chakwera afuna axiophyeza athu ngat anayamba kulamulila ndiiye
Steve ndayamika pa nkhani yomaliza, President ndi nduna azidzipangila okha zonse osati zaulele m'mene zilili pano. Anthu akuvutika ku midzi. Ndicho chifukwa kudzikhala ma Demonstrations osonyeza kukwiya.
Apolice akumalawi ndi mbamva chifukwa chake alowesa ndale pa ntchito yawo shame on you
Nanga training ya ntchito umapanga 6 months and think you can get quality staff
Mayi Aja mukuti wankula wapolice ndiwankhunyu
More 🔥🔥🔥🔥 kodwa Banda umuwalero big man
God bless you boss mwayakhula
Vuto Malawi Police inatha panopa ndi MCP Police.
Big up family,,Nothing but chilungamo
Kuyambila chakwela ndi kabineti yonse apolice army zonse ndi zitsilu za kuba boma la mcp ndi la manyi
BOMA lopanda nzelu iri
Anakangosiya kulamulira awunikire bwino ndithu chakwera chitsiru aribe nzeru kwao kwatha garu ameneyo
Mr S banda mukunena zoona bwana
Chilungamo
God bless you guys 🙏🙏🙏🙏🙏🙏
And ziko la Malawi litha kutukuka chachikulu kuchosa mbava zikuononga misokho yamalawi. Nduna president asayendere zinthu zaulele ndichifukwa akupanga matama kutenga ngati ife amalawi ndizisiro
Walephera chakwela akambe church
Chimwendo wadya1 pa nkhaza ku mcp
Komaso akumanga bwanji anthu Ma umboni aupeza bwanji mene zinakhalila kuchikangawa
Point take big man .komaso aziganiza kuti kunyumba kapena kulokecheni kulibe police officer,tisatenge malamuro pamanja azanja lathu. Ndi ye tiyeni tigwilentchi to kulingana ndimalamo , komaso Pali mwambe wakuti ukakhala pabwino lero usayiwale zamawa,chawonamuzakochapita mawa hilipayiwe..ndangoyimapamenepo, amoyo salekana,
Tikupempha program iiii achisili Achawezi asazalowelere
Chilungamo plus❤ twapukene amagwetu
Mulingo omwe wamuyezera mzako nawenso adzakuyezera omwewo
A police chitani manyazi mukulephera ntchito yanu
Chadwell chinsiru kwambiri
Ndipo ife ana athu timalipira tokha fizi bwanji
Uchigawenga wachuluka kwambiri mmalawi.
Kom iweyo umaganiza bwino bwino kobasi
Useless police of malawi
Kondwani umayankhula. Bwino
😊
JB uja sakumalakwisa akamatukwana msogoleri ndinduna zake
Nanga akamatukwana amalawi nose amalondolaso
@@NancyNyirenda-v9oof course. Ndifedi anthu ogona ambirife
JB amangotukwana chamba kwambir alibe fundo
Chigamulo changa chiyende moteremu chilimat waphedwera agree ment yake ndi chakwera komaso mlandu wasatar , choncho ngat achakwera amupha chilima kuti asale ndiudindo sizitheka , ngat agreement yalephereka pomupha chilima ndibwinoso achakwera aduse aliyese asakhaleposo muthu chilima amalakwa chani ? Nsupa zatulukat taombeza achakwera mwaphat chilima dala inuso mudusa udindowo aliyese asatenge chilima mwapha ife amalawi tiphaso inu bas 50-50 chilungamo titero
Ngati wa Mpingoyo anapalamula nde asamangidwe,iyeyo ndi munthu, aaaaaaa ,munakangodzudzula zolakwikwazo,osati mpingo ,mpingo nde chiyani, Mesa mpingo ndi anthu,nde munthuyo ngati walakwitsa nde lamulo lisangwire Ntchito
Azibusa asiyenso kulowelela ndale
Alowelera bwanji iwo akunena chilungamo inu multi mbali iti? Anzathu?
Ndipo zowona mumalo mokalalikila uko timadabwakuti ku zolozolo bwanji kwabuka ndeu mu church chawoneka kuti niwachinyengo mubusa uyu
Inunso ngt muli opemphera nde musiye zomalimbana ndi anthu
@@NancyNyirenda-v9o mukamva kupenga nde uku kd zigandanga zilipo gulutu kd za Infa imeneyi sidzinamukhuze ndindani km anthu akanike kulira fukwa nda zibusa nonsense