A Brian tamubooleni mimbayo zikhale ng'oma mwina mimbayo iphwe kenako aziyankha . Ndichinduna cha mwano komanso Makati kwambiri. Changoseza mimba uko phwiiii kumapanga makani apa ngati ndi munthu ozindikira power ndi mbuzi ya munthu. Musazachiitanenso pa hot current kawiri , chizikhala ndi chakwera wakeyo kudikira kuchoka 2025. AIP ikuyenda bwino pakhomo pakwawo osati kwa amalawi anthu okuba Mulungu awalanga pompano anthu amenewa
This is exactly how government lives in denial. Very interesting. All this time there is nothing you can point that the minister was able to answer. Like nothing
I love The Hot Current and I always look forward to it. However, for so long, I have had issues with the show to where the hosts don't usually "think" of how important this show is to the students in colleges and universities world over. It is very difficult for a student to use what is said on this program as real evidence because the hosts take it as a discussion would have with someone at a bar. The hosts are barely ready for it and do not cite their outside sources, something that, maybe, morden universities do not accept. Much as I was not in agreement with The Minister, he seemed to challenge the hosts to produce evidence of what they wanted to ask him. I know the hosts, more specifically, Brian Banda, is educated enough, he should take this as a learning process and always cite his sources when asking the people 'he' invites to the show. This program has been a wonderful addition to Malawian programs but if it was done the right way, it could do much better than it has already done. Let members of parliament use it as a source of evidence in parliament. Let people sue one another using this program to change the face of Malawi. That cannot happen if the discussion is only done as a casual discussion. I was impressed seeing the minister showing his notes on things because he is an educated fellow who knows not to say something on a national television without evidence. Fox News in America paid big money for spreading false news without proper evidence. Please, Times Television, let your producers cite their stories or use the word "hypothetical" so some of us can really know if it's worth it or not.
Hundred percent I agree with u. I think it's high time Times find some guys well-informed on today's current affairs and issues to do so socials economics and governance.
Increasing the AIP beneficiaries will mean increase in poverty on household. This initiative is pathetic n we can't do better. Smallholder farmers are failing to extend their farm sizes due to high level of dependence on AIP same way as we depend much on foreign Aid. Teach more farmers on how they can manufacture mbeya fertilizer and do some extensions to their farms..
I like this . The minister is a very interesting political figure., He was able to spin out of questions and provide alternative view and he slipped out of Brian's popular "monkey wrench" questions.
Wakumana nawo anzako akhambi iwe Brian umaziona ngati ozindikila ukamafunsa mafunso amzako apa taziyankha osati zibwibwi its true pamafunika kumakamba zinthu uli ndi umboni osati kumangopeka nkhani or ena akangoyim a foni basi mwakhulupilira One day adzakutenga sukudziwa Kuti akukuuza zimenezoyo ndiwamalamulo becareful Brian de
...I really wonder why the anchor seems to be touting this guy a if he has some extra-ordinary skills and talent. What does nyama zikulu-zikulu mean? Lets not get excited and worship the same people who are promoting poverty amongst us. And I think we are micro-managed by Rwanda and collecting kickbacks by hunting refugees that he still seeks to kill. Well, I look at it as the most stupid thing for us to be proud of having more AIP beneficiaries. Instead of graduating these subsistent costly farmers into viable and productive citizens….on the US ambassador, I have never seen an ambassador who enjoys strange diplomatic protocol. He even finds himself in locations eating mandasi with locals, now, if he enjoys that freedom, then it is not a problem if he decides to walk into a media house as a news source. After all, the Malawi economy is surviving on debts, loans and credits that he approves every week, perhaps every day…The problem in Malawi is lack of ambitious leadership. We, currently do not have anyone fit for the position he holds in this government apart from the female ministers.
I do understand a minister wants everything wth a prove coz amalawi timangoyankhula zongomva,,,is really nyama zikuluzikulu wth more intelligent I enjoy this kkk
This zikhale ng' oma has shown he is an intellectual....he can cite his sources...Brian Banda didn't come prepared...this time.i hope u do better next time around.this minister has killed the interview.
The minister is intelligent,has really handled the hosts,he is really based on facts from my observation.A china Brian and pamkuku accept a defeat,the guy has really outweighed you.
This is why you can't choose your family partner kukhala okuthandizila cz pakakhala vuto saangayankhule olo kusamala zaena apadela kuposa m'bale wake olo m'bale akulakwisa Malawi ali pa moto i hope wi know what to do next year to save our lovely country mayi Malawi 🇲🇼🙏🏾
A Brian tamubooleni mimbayo zikhale ng'oma mwina mimbayo iphwe kenako aziyankha . Ndichinduna cha mwano komanso Makati kwambiri.
Changoseza mimba uko phwiiii kumapanga makani apa ngati ndi munthu ozindikira power ndi mbuzi ya munthu. Musazachiitanenso pa hot current kawiri , chizikhala ndi chakwera wakeyo kudikira kuchoka 2025.
AIP ikuyenda bwino pakhomo pakwawo osati kwa amalawi anthu okuba Mulungu awalanga pompano anthu amenewa
Kkkkkkk
Galu wammpha dzikodi silingalongosoke ili nduna yaza chitetezo ikuyikiraso kumbuyo mbwererazi
Chilbe nzeru chunkhumba chimenechi
He uses his udindo wrongly
Nzeru ilibe ndunayo ubwino wake 2025 mbava zikuchoka
This shows how hot current bases on issues with no tract evidence. Please Brian learn to be prepared for the program
The nduna himself doesn't know how to argue,,too much emotions ķkkkkkkkkkk hahaha MCP is dangerous party indeed
Kodi mlendo anali ndani pa Hot current imeneyi.... nduna yoonjedxera nkwiyo kwa A malawi
2025 ndi Chaka chamawa Why panic with this thing Let's go and work for our better
Nduna imeneyi ndichisiru chamuthu ndposo ndisatana ndikufunisisa kt mulungu amulange panse pompa aziwe chimo lake akuphesa A2 osalakwa Aku ruwanda ndimuthu oipa kwambir ameneyi osamusekerera chisiru chamuthu ndiwadyera kwambir
Nduna imeneyi ndimanyi
This is exactly how government lives in denial. Very interesting. All this time there is nothing you can point that the minister was able to answer. Like nothing
He forgot we're in a democracy with his dictatorship mentality.
I love The Hot Current and I always look forward to it. However, for so long, I have had issues with the show to where the hosts don't usually "think" of how important this show is to the students in colleges and universities world over. It is very difficult for a student to use what is said on this program as real evidence because the hosts take it as a discussion would have with someone at a bar. The hosts are barely ready for it and do not cite their outside sources, something that, maybe, morden universities do not accept. Much as I was not in agreement with The Minister, he seemed to challenge the hosts to produce evidence of what they wanted to ask him. I know the hosts, more specifically, Brian Banda, is educated enough, he should take this as a learning process and always cite his sources when asking the people 'he' invites to the show. This program has been a wonderful addition to Malawian programs but if it was done the right way, it could do much better than it has already done. Let members of parliament use it as a source of evidence in parliament. Let people sue one another using this program to change the face of Malawi. That cannot happen if the discussion is only done as a casual discussion. I was impressed seeing the minister showing his notes on things because he is an educated fellow who knows not to say something on a national television without evidence. Fox News in America paid big money for spreading false news without proper evidence. Please, Times Television, let your producers cite their stories or use the word "hypothetical" so some of us can really know if it's worth it or not.
😂
Hundred percent I agree with u. I think it's high time Times find some guys well-informed on today's current affairs and issues to do so socials economics and governance.
@@tadalarhostinchiphwanya7891true
This
Hot Current palibe chimene tatola ngat ife ma Listeners ndim'mene akuyakhira wakubayo
Big up minister for taking these kids to school.
Increasing the AIP beneficiaries will mean increase in poverty on household. This initiative is pathetic n we can't do better. Smallholder farmers are failing to extend their farm sizes due to high level of dependence on AIP same way as we depend much on foreign Aid. Teach more farmers on how they can manufacture mbeya fertilizer and do some extensions to their farms..
Watching from mozambique
Wotching from South Africa
Nyama zikulu-zimulu dada zikhare munthu murara chomeneeee ntchindii zikumwenererani chomene pa yankho rakut president azakhara chakwera motoooo💥💥💥💥💥💥
Now tell the minister about Quantitative and qualitative data, qualitative part of AIP is negative osamatinamiza apa
Mr Zikhale Ng'oma udindo wakulilila sakudziwa chimene akunena
Mwakumana ndi nyama zikuluzikulu ndichochenjelaaa ichiii
Nzeru ilibe ndunayi
I like this . The minister is a very interesting political figure., He was able to spin out of questions and provide alternative view and he slipped out of Brian's popular "monkey wrench" questions.
A NEW VERSION WISE GOOD THINKER WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD
The worst hot current, zikhale is too much into politics.
Zambiri sitiyankhula koma zambiri koma tnm isamale👌👌👌
Minster uyu ngozikonda
Wakumana nawo anzako akhambi iwe Brian umaziona ngati ozindikila ukamafunsa mafunso amzako apa taziyankha osati zibwibwi its true pamafunika kumakamba zinthu uli ndi umboni osati kumangopeka nkhani or ena akangoyim a foni basi mwakhulupilira One day adzakutenga sukudziwa Kuti akukuuza zimenezoyo ndiwamalamulo becareful Brian de
Inuyo kuzitenga kuzindikila ??
...I really wonder why the anchor seems to be touting this guy a if he has some extra-ordinary skills and talent. What does nyama zikulu-zikulu mean? Lets not get excited and worship the same people who are promoting poverty amongst us. And I think we are micro-managed by Rwanda and collecting kickbacks by hunting refugees that he still seeks to kill. Well, I look at it as the most stupid thing for us to be proud of having more AIP beneficiaries. Instead of graduating these subsistent costly farmers into viable and productive citizens….on the US ambassador, I have never seen an ambassador who enjoys strange diplomatic protocol. He even finds himself in locations eating mandasi with locals, now, if he enjoys that freedom, then it is not a problem if he decides to walk into a media house as a news source. After all, the Malawi economy is surviving on debts, loans and credits that he approves every week, perhaps every day…The problem in Malawi is lack of ambitious leadership. We, currently do not have anyone fit for the position he holds in this government apart from the female ministers.
Mr Based on facts😊...
Useless cabinet minister who could not explain 🚮
Akuluwa angonenepa ndi achisilu kobasi😊
Thanks zikhale
We are sad Nation
You, not we😅, I am not
Mximm zautsiru anduna anuwo akuyankhula zichani😊
Akuti zinthu zitsika😢! Koma Chimunthu chi ndi cha Pokoso bwanji!!
I do understand a minister wants everything wth a prove coz amalawi timangoyankhula zongomva,,,is really nyama zikuluzikulu wth more intelligent I enjoy this kkk
Andunawo nzeru alibe sakutha kuyankha funso
Azikhale muziopa kumwamba uliposo moyo wina oposa umene mukubela anthuwu kudziko kuno,
Musamale
Give each other Chance 😢
Tell him mr Nanyon is a human being also
Mpaka ali ndi nyolo ndani aaaaa ife tiwope unyolo za ziiiiiiiiii
Azikhale akukwana pa udfend
Ndaonera mbalame
This zikhale ng' oma has shown he is an intellectual....he can cite his sources...Brian Banda didn't come prepared...this time.i hope u do better next time around.this minister has killed the interview.
No ndiwopoira
Aaaaaa awanso
Poyamba ndimaona ngat Times imadana ndi DPP koma now ,,,,,ndazindikira kut it's only times yomwe tingaipange trust❤❤❤❤❤
Nduna yoononga dziko kwambiri, katangale ali thoooo
Uyu panyapa xikhale Ng,oma kaye kutopa mawonekedwe
Za trend zo munthu wakumudzi azidziwa bwanji abale?
Brain wawoneka m'sana after kubisala m'mbatata
Wadya 2.5 biliyoni ameneyo
Phone yooooo ikutani koma all in all tikudziwaaa
The minister is intelligent,has really handled the hosts,he is really based on facts from my observation.A china Brian and pamkuku accept a defeat,the guy has really outweighed you.
Exactly
Exactly the host defeated
Ndunoyo ivomeleze skuye nda
Zinkhali Ng"oma is skilful at his work.Hon.Minister please,keep watch on illegal influx of immigrants here Malawi.
❤
😮koma olo itakhala vote zikhaleyu walephereratu akumuikira kumbuyo or asanu osakwana
Guys u r losing control of your interview
Economy ikhala bwino bwanji utanena kuti zinthu zilibwino?
Ali busy kuba ndalama zobwerekazo
Duna imeneyi kodi imakhalira kuti zoti anthu adalandidwa ma 30 pn iyeyo sakuzidziwa koma ameneyi
Here ngumbe chileka
This guy need an evidenve from you guys but was he producing the the documentantion ya constitution yo?
Ndunayi ikamayankhula idzidziwa kuti Ili pa tv komanso palibe wa dzelu kuposa nzake pa dziko pano ngati kunvana kukuvuta thesani program
mukungovutikatu a brian ndigaluyi dzikoli akuona ngati ndilamayi awo tikakumana komweko
Kuyakhula kwa anduna kosapatsa chiyembekezo aaaa
Ndunayo ilibe nzeru chocho dziko ikayende bwino
Uyu si nduna koma chigawenga😢😢😢 wofunsa mesa ndi mtola nkhani?
Nduna iyi ikhadzangolowatsa mboma it means dera lakero ladzaza zitsiru zokha zokha
Ndipo nzeru alibe zedi zawonekelatu kuti mfundo alibe kusemphana ndi mafuso
I like how nduna imeneyi pays attention when someone is on the flow
He pays attention to details Eish
Chisilu chimenecho chikundisekesa heavy
brian tawasiyan awa ndiopepela saziwa kut munthu amayankha with explanation.
Akuruwa ndi oderela yeee
Ameneyo mumamuitaniranji wamakani ngat ameyo
Koma akunena zoonaaa
This is why you can't choose your family partner kukhala okuthandizila cz pakakhala vuto saangayankhule olo kusamala zaena apadela kuposa m'bale wake olo m'bale akulakwisa Malawi ali pa moto i hope wi know what to do next year to save our lovely country mayi Malawi 🇲🇼🙏🏾
There is no sense why the visitor is now presentating a program
Very wise minister
Zikhale ndi mbuzi kma adzinga azake bas akukanika kuyakha mafutso ake amakani bas born kalindo must release 😮
Za ziiii
Guys let's gather here for comments😂🤣🤣🤣
Lero suti sanavale mwina nkona sakuyankha chilungamo
The Big 5 imeneyo ikhare Njobvu kkk
Iyi ndi ng'oma basi sidziwiwakathu
Abrian mumenyeni mbama ameneyo
Iyi ndi mbuzi yamunthu ,, brian muzititengera anthu azeru iwowo anadya ma 30pin afeteredxa mpaka pano sitikupindula nd boma limenero
Koma yah😊😊
😮
Brain 4 today u hvnt show ur brain Banda but next I hope Soo .timakunyadira .
Nduna uyo anabwerera ndale .sikut amawauu,a amalawi zolondola.
Let the minister answer questions not asking questions
Ndipo mitting yanu sikumveka or akuluwo akuzimva udindo kumeneko akukhala ngati si Malawi kapena sakudziwa zomwe anthu akuziwona
Brian Banda wagwa nayo.
Anthu andale ndiagalu sure
Kkkkk kids are taken into a class, the kids have their sponsor, bravo to the minister Zikhale for the response trying to educate a bulutiwa
Nduna ya manya mavote mwana kale ndi a make koma sizitheka ife tikuziwa mulimonse
Inu tangoonani khopeyo,anganene chilungamo ameneyo....munthu mukumufusa zabwino bwino chomwe akoopsezera ndichani ife tichite mantha tiope....?
Wapha chilima nachimimbayu
The program is nice but talking too much not giving each other Chance 😮
Koma ndunazi zikamana manyazi zilibe eish
Ati timuona kusogolo kwake
Kkkkkkkkk Nduna he doesn't know what's talking about
Akugwitsa ntchito ndale
My Malawi 😭😭😭😭 y having useless minister like this one, useless government too😭😭😭😭😭
Iwowo akanalongosora wokha zomwe akudziwazo
Sikuyenda bwino kumene ndiangati akugula feteleza