Комментарии •

  • @bi8942
    @bi8942 Год назад +22

    A Brian tamubooleni mimbayo zikhale ng'oma mwina mimbayo iphwe kenako aziyankha . Ndichinduna cha mwano komanso Makati kwambiri.
    Changoseza mimba uko phwiiii kumapanga makani apa ngati ndi munthu ozindikira power ndi mbuzi ya munthu. Musazachiitanenso pa hot current kawiri , chizikhala ndi chakwera wakeyo kudikira kuchoka 2025.
    AIP ikuyenda bwino pakhomo pakwawo osati kwa amalawi anthu okuba Mulungu awalanga pompano anthu amenewa

    • @eliffagondewe8214
      @eliffagondewe8214 Год назад

      Kkkkkkk

    • @gavinpillay1253
      @gavinpillay1253 7 месяцев назад +1

      Galu wammpha dzikodi silingalongosoke ili nduna yaza chitetezo ikuyikiraso kumbuyo mbwererazi

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus 20 дней назад +2

      Chilbe nzeru chunkhumba chimenechi
      He uses his udindo wrongly

  • @KinziwindassoniKinzi
    @KinziwindassoniKinzi 9 дней назад +3

    Nzeru ilibe ndunayo ubwino wake 2025 mbava zikuchoka

  • @zechariah265
    @zechariah265 Год назад +9

    This shows how hot current bases on issues with no tract evidence. Please Brian learn to be prepared for the program

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 Год назад +11

    The nduna himself doesn't know how to argue,,too much emotions ķkkkkkkkkkk hahaha MCP is dangerous party indeed

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Год назад +8

    Kodi mlendo anali ndani pa Hot current imeneyi.... nduna yoonjedxera nkwiyo kwa A malawi

  • @user-eh1gn1nj9d
    @user-eh1gn1nj9d 3 месяца назад +4

    2025 ndi Chaka chamawa Why panic with this thing Let's go and work for our better

  • @BenissoneErnesto-kn9bd
    @BenissoneErnesto-kn9bd Год назад +6

    Nduna imeneyi ndichisiru chamuthu ndposo ndisatana ndikufunisisa kt mulungu amulange panse pompa aziwe chimo lake akuphesa A2 osalakwa Aku ruwanda ndimuthu oipa kwambir ameneyi osamusekerera chisiru chamuthu ndiwadyera kwambir

  • @MotivatedI
    @MotivatedI Год назад +10

    This is exactly how government lives in denial. Very interesting. All this time there is nothing you can point that the minister was able to answer. Like nothing

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 Год назад

      He forgot we're in a democracy with his dictatorship mentality.

  • @Mbesa09
    @Mbesa09 Год назад +15

    I love The Hot Current and I always look forward to it. However, for so long, I have had issues with the show to where the hosts don't usually "think" of how important this show is to the students in colleges and universities world over. It is very difficult for a student to use what is said on this program as real evidence because the hosts take it as a discussion would have with someone at a bar. The hosts are barely ready for it and do not cite their outside sources, something that, maybe, morden universities do not accept. Much as I was not in agreement with The Minister, he seemed to challenge the hosts to produce evidence of what they wanted to ask him. I know the hosts, more specifically, Brian Banda, is educated enough, he should take this as a learning process and always cite his sources when asking the people 'he' invites to the show. This program has been a wonderful addition to Malawian programs but if it was done the right way, it could do much better than it has already done. Let members of parliament use it as a source of evidence in parliament. Let people sue one another using this program to change the face of Malawi. That cannot happen if the discussion is only done as a casual discussion. I was impressed seeing the minister showing his notes on things because he is an educated fellow who knows not to say something on a national television without evidence. Fox News in America paid big money for spreading false news without proper evidence. Please, Times Television, let your producers cite their stories or use the word "hypothetical" so some of us can really know if it's worth it or not.

    • @user-ux8bc6wy1i
      @user-ux8bc6wy1i Год назад

      😂

    • @tadalarhostinchiphwanya7891
      @tadalarhostinchiphwanya7891 Год назад +1

      Hundred percent I agree with u. I think it's high time Times find some guys well-informed on today's current affairs and issues to do so socials economics and governance.

    • @ezekielchihana2927
      @ezekielchihana2927 11 месяцев назад

      @@tadalarhostinchiphwanya7891true

  • @fedson2050
    @fedson2050 Год назад +15

    This
    Hot Current palibe chimene tatola ngat ife ma Listeners ndim'mene akuyakhira wakubayo

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 Год назад +4

    Big up minister for taking these kids to school.

  • @rasulrayman4517
    @rasulrayman4517 Год назад +6

    Increasing the AIP beneficiaries will mean increase in poverty on household. This initiative is pathetic n we can't do better. Smallholder farmers are failing to extend their farm sizes due to high level of dependence on AIP same way as we depend much on foreign Aid. Teach more farmers on how they can manufacture mbeya fertilizer and do some extensions to their farms..

  • @BenissoneErnesto-kn9bd
    @BenissoneErnesto-kn9bd Год назад +1

    Watching from mozambique

  • @user-nz1tf2ie6n
    @user-nz1tf2ie6n 6 месяцев назад

    Wotching from South Africa

  • @dellingsmunthali2669
    @dellingsmunthali2669 11 месяцев назад +1

    Nyama zikulu-zimulu dada zikhare munthu murara chomeneeee ntchindii zikumwenererani chomene pa yankho rakut president azakhara chakwera motoooo💥💥💥💥💥💥

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 Год назад +2

    Now tell the minister about Quantitative and qualitative data, qualitative part of AIP is negative osamatinamiza apa

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 3 месяца назад +2

    Mr Zikhale Ng'oma udindo wakulilila sakudziwa chimene akunena

  • @user-qs2tx7wt6g
    @user-qs2tx7wt6g 10 дней назад +1

    Mwakumana ndi nyama zikuluzikulu ndichochenjelaaa ichiii

  • @user-uz6tr2db6g
    @user-uz6tr2db6g 14 дней назад +3

    Nzeru ilibe ndunayi

  • @g_deonm5793
    @g_deonm5793 Год назад +8

    I like this . The minister is a very interesting political figure., He was able to spin out of questions and provide alternative view and he slipped out of Brian's popular "monkey wrench" questions.

  • @leonardjika2100
    @leonardjika2100 Год назад +2

    A NEW VERSION WISE GOOD THINKER WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD

  • @kamuchirwa8940
    @kamuchirwa8940 Год назад +5

    The worst hot current, zikhale is too much into politics.

  • @DakahNakhuku
    @DakahNakhuku 4 дня назад

    Zambiri sitiyankhula koma zambiri koma tnm isamale👌👌👌

  • @ephraimkadamika
    @ephraimkadamika Год назад +2

    Minster uyu ngozikonda

  • @languitoneelias9972
    @languitoneelias9972 Год назад +1

    Wakumana nawo anzako akhambi iwe Brian umaziona ngati ozindikila ukamafunsa mafunso amzako apa taziyankha osati zibwibwi its true pamafunika kumakamba zinthu uli ndi umboni osati kumangopeka nkhani or ena akangoyim a foni basi mwakhulupilira One day adzakutenga sukudziwa Kuti akukuuza zimenezoyo ndiwamalamulo becareful Brian de

  • @geee7672
    @geee7672 Год назад +5

    ...I really wonder why the anchor seems to be touting this guy a if he has some extra-ordinary skills and talent. What does nyama zikulu-zikulu mean? Lets not get excited and worship the same people who are promoting poverty amongst us. And I think we are micro-managed by Rwanda and collecting kickbacks by hunting refugees that he still seeks to kill. Well, I look at it as the most stupid thing for us to be proud of having more AIP beneficiaries. Instead of graduating these subsistent costly farmers into viable and productive citizens….on the US ambassador, I have never seen an ambassador who enjoys strange diplomatic protocol. He even finds himself in locations eating mandasi with locals, now, if he enjoys that freedom, then it is not a problem if he decides to walk into a media house as a news source. After all, the Malawi economy is surviving on debts, loans and credits that he approves every week, perhaps every day…The problem in Malawi is lack of ambitious leadership. We, currently do not have anyone fit for the position he holds in this government apart from the female ministers.

  • @francistonysanena5349
    @francistonysanena5349 8 месяцев назад

    Mr Based on facts😊...

  • @stanleymatolabanda5460
    @stanleymatolabanda5460 Год назад +4

    Useless cabinet minister who could not explain 🚮

  • @mbumbajilowele6511
    @mbumbajilowele6511 Месяц назад +1

    Akuluwa angonenepa ndi achisilu kobasi😊

  • @user-th4dg9bn9i
    @user-th4dg9bn9i Год назад

    Thanks zikhale

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 Год назад +7

    We are sad Nation

  • @user-jr9oh3ye9u
    @user-jr9oh3ye9u Год назад +1

    Mximm zautsiru anduna anuwo akuyankhula zichani😊

  • @jacquesnsabiyaremye3166
    @jacquesnsabiyaremye3166 Год назад +2

    Akuti zinthu zitsika😢! Koma Chimunthu chi ndi cha Pokoso bwanji!!

  • @user-hy4ty2ig1t
    @user-hy4ty2ig1t Год назад +2

    I do understand a minister wants everything wth a prove coz amalawi timangoyankhula zongomva,,,is really nyama zikuluzikulu wth more intelligent I enjoy this kkk

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 Год назад +2

    Azikhale muziopa kumwamba uliposo moyo wina oposa umene mukubela anthuwu kudziko kuno,
    Musamale

  • @SusanPhiri-el3dx
    @SusanPhiri-el3dx День назад

    Give each other Chance 😢

  • @chikoko-uj2tt
    @chikoko-uj2tt Год назад +1

    Tell him mr Nanyon is a human being also

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 8 дней назад

    Mpaka ali ndi nyolo ndani aaaaa ife tiwope unyolo za ziiiiiiiiii

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Год назад +1

    Azikhale akukwana pa udfend

  • @damianodonda2494
    @damianodonda2494 4 дня назад

    Ndaonera mbalame

  • @PeterThawi-jc7zl
    @PeterThawi-jc7zl Год назад +2

    This zikhale ng' oma has shown he is an intellectual....he can cite his sources...Brian Banda didn't come prepared...this time.i hope u do better next time around.this minister has killed the interview.

  • @mercythom5868
    @mercythom5868 7 месяцев назад

    Poyamba ndimaona ngat Times imadana ndi DPP koma now ,,,,,ndazindikira kut it's only times yomwe tingaipange trust❤❤❤❤❤

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Год назад +2

    Nduna yoononga dziko kwambiri, katangale ali thoooo

  • @GiftMakowa-k9f
    @GiftMakowa-k9f 6 дней назад

    Uyu panyapa xikhale Ng,oma kaye kutopa mawonekedwe

  • @dalisoulphiri3094
    @dalisoulphiri3094 Год назад +2

    Za trend zo munthu wakumudzi azidziwa bwanji abale?

  • @phillipstamaley7901
    @phillipstamaley7901 11 месяцев назад

    Brain wawoneka m'sana after kubisala m'mbatata

  • @joaquegerman2250
    @joaquegerman2250 Год назад +3

    Wadya 2.5 biliyoni ameneyo

  • @DakahNakhuku
    @DakahNakhuku 4 дня назад

    Phone yooooo ikutani koma all in all tikudziwaaa

  • @vukanifracksonchinkonde7324
    @vukanifracksonchinkonde7324 Год назад +2

    The minister is intelligent,has really handled the hosts,he is really based on facts from my observation.A china Brian and pamkuku accept a defeat,the guy has really outweighed you.

  • @FatsanTobiyas
    @FatsanTobiyas 7 месяцев назад

    Ndunoyo ivomeleze skuye nda

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 13 дней назад

    Zinkhali Ng"oma is skilful at his work.Hon.Minister please,keep watch on illegal influx of immigrants here Malawi.

  • @MadalitsoGreen-oc1xl
    @MadalitsoGreen-oc1xl 8 дней назад

  • @FrankYaumuGama
    @FrankYaumuGama 11 часов назад

    😮koma olo itakhala vote zikhaleyu walephereratu akumuikira kumbuyo or asanu osakwana

  • @SautsoBandah-lf4so
    @SautsoBandah-lf4so Год назад +2

    Guys u r losing control of your interview

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 Год назад +1

    Economy ikhala bwino bwanji utanena kuti zinthu zilibwino?

  • @livemonkaposka3714
    @livemonkaposka3714 Год назад +1

    Ali busy kuba ndalama zobwerekazo

  • @aronluka8086
    @aronluka8086 Год назад +1

    Duna imeneyi kodi imakhalira kuti zoti anthu adalandidwa ma 30 pn iyeyo sakuzidziwa koma ameneyi

  • @user-ro6hs4qw8z
    @user-ro6hs4qw8z Год назад

    Here ngumbe chileka

  • @awesomechannel7752
    @awesomechannel7752 16 дней назад

    This guy need an evidenve from you guys but was he producing the the documentantion ya constitution yo?

  • @Princemagaso77Moffat
    @Princemagaso77Moffat 20 часов назад

    Ndunayi ikamayankhula idzidziwa kuti Ili pa tv komanso palibe wa dzelu kuposa nzake pa dziko pano ngati kunvana kukuvuta thesani program

  • @user-xd9fp2bw8j
    @user-xd9fp2bw8j Год назад

    mukungovutikatu a brian ndigaluyi dzikoli akuona ngati ndilamayi awo tikakumana komweko

  • @massaucosabao40
    @massaucosabao40 9 дней назад

    Ndunayo ilibe nzeru chocho dziko ikayende bwino

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 9 дней назад

    Uyu si nduna koma chigawenga😢😢😢 wofunsa mesa ndi mtola nkhani?

  • @user-kr8bn1bb8c
    @user-kr8bn1bb8c 12 дней назад +1

    Nduna iyi ikhadzangolowatsa mboma it means dera lakero ladzaza zitsiru zokha zokha

  • @user-cg5ml7ym4v
    @user-cg5ml7ym4v 9 дней назад

    Ndipo nzeru alibe zedi zawonekelatu kuti mfundo alibe kusemphana ndi mafuso

  • @charlespaulbanda8136
    @charlespaulbanda8136 11 месяцев назад +3

    I like how nduna imeneyi pays attention when someone is on the flow

  • @farmupmalawi
    @farmupmalawi Год назад +2

    Chisilu chimenecho chikundisekesa heavy

  • @FranciscoMandawala
    @FranciscoMandawala 6 дней назад

    brian tawasiyan awa ndiopepela saziwa kut munthu amayankha with explanation.

  • @afrozwayson7482
    @afrozwayson7482 6 месяцев назад

    Akuruwa ndi oderela yeee

  • @fedson2050
    @fedson2050 Год назад +3

    Ameneyo mumamuitaniranji wamakani ngat ameyo

  • @jeuzywandasigner4908
    @jeuzywandasigner4908 13 дней назад

    This is why you can't choose your family partner kukhala okuthandizila cz pakakhala vuto saangayankhule olo kusamala zaena apadela kuposa m'bale wake olo m'bale akulakwisa Malawi ali pa moto i hope wi know what to do next year to save our lovely country mayi Malawi 🇲🇼🙏🏾

  • @SusanPhiri-el3dx
    @SusanPhiri-el3dx День назад

    There is no sense why the visitor is now presentating a program

  • @MphatsoSimiliwadi
    @MphatsoSimiliwadi 7 дней назад

    Very wise minister

  • @user-hb1ff2wd8c
    @user-hb1ff2wd8c 11 дней назад

    Zikhale ndi mbuzi kma adzinga azake bas akukanika kuyakha mafutso ake amakani bas born kalindo must release 😮

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Год назад

    Za ziiii

  • @PeterThawi-jc7zl
    @PeterThawi-jc7zl Год назад +1

    Guys let's gather here for comments😂🤣🤣🤣

  • @YusufMoyo
    @YusufMoyo 4 дня назад

    Lero suti sanavale mwina nkona sakuyankha chilungamo

  • @user-ky4ce9gb6j
    @user-ky4ce9gb6j 9 месяцев назад

    The Big 5 imeneyo ikhare Njobvu kkk

  • @YusufuJuma-ib1ru
    @YusufuJuma-ib1ru 4 дня назад

    Iyi ndi ng'oma basi sidziwiwakathu

  • @christopherbokosi514
    @christopherbokosi514 7 месяцев назад

    Abrian mumenyeni mbama ameneyo

  • @MsosakaisiAdamson-pg6uv
    @MsosakaisiAdamson-pg6uv Год назад

    Iyi ndi mbuzi yamunthu ,, brian muzititengera anthu azeru iwowo anadya ma 30pin afeteredxa mpaka pano sitikupindula nd boma limenero

  • @user-lr7ix1tm5b
    @user-lr7ix1tm5b 7 месяцев назад

    Koma yah😊😊

  • @VuyolwethuMbabani
    @VuyolwethuMbabani 4 дня назад

    😮

  • @MichaelMwambene-hu5sf
    @MichaelMwambene-hu5sf Год назад

    Brain 4 today u hvnt show ur brain Banda but next I hope Soo .timakunyadira .
    Nduna uyo anabwerera ndale .sikut amawauu,a amalawi zolondola.

  • @DavieJames
    @DavieJames Год назад +1

    Let the minister answer questions not asking questions

  • @user-op3nx5qt4q
    @user-op3nx5qt4q 2 месяца назад

    Ndipo mitting yanu sikumveka or akuluwo akuzimva udindo kumeneko akukhala ngati si Malawi kapena sakudziwa zomwe anthu akuziwona

  • @robayami-xz2wg
    @robayami-xz2wg Год назад

    Brian Banda wagwa nayo.

  • @djchizdebs5402
    @djchizdebs5402 Год назад

    Anthu andale ndiagalu sure

  • @James-uq6hv
    @James-uq6hv Год назад +3

    Kkkkk kids are taken into a class, the kids have their sponsor, bravo to the minister Zikhale for the response trying to educate a bulutiwa

  • @user-ix7pb6hk2w
    @user-ix7pb6hk2w 5 месяцев назад

    Nduna ya manya mavote mwana kale ndi a make koma sizitheka ife tikuziwa mulimonse

  • @MadalitsoWhite
    @MadalitsoWhite 3 дня назад

    Inu tangoonani khopeyo,anganene chilungamo ameneyo....munthu mukumufusa zabwino bwino chomwe akoopsezera ndichani ife tichite mantha tiope....?

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 7 часов назад

    Wapha chilima nachimimbayu

  • @SusanPhiri-el3dx
    @SusanPhiri-el3dx День назад

    The program is nice but talking too much not giving each other Chance 😮

  • @user-eb2gi5dt6o
    @user-eb2gi5dt6o 2 месяца назад +1

    Koma ndunazi zikamana manyazi zilibe eish

  • @EsnarthSulumba
    @EsnarthSulumba 7 дней назад

    Ati timuona kusogolo kwake

  • @nickmumba2131
    @nickmumba2131 Год назад +3

    Kkkkkkkkk Nduna he doesn't know what's talking about

  • @massaucosabao40
    @massaucosabao40 9 дней назад

    Akugwitsa ntchito ndale

  • @madalitsoonale5338
    @madalitsoonale5338 Год назад +1

    My Malawi 😭😭😭😭 y having useless minister like this one, useless government too😭😭😭😭😭

  • @ChikumbutsoButao-h1s
    @ChikumbutsoButao-h1s 6 дней назад

    Iwowo akanalongosora wokha zomwe akudziwazo

  • @STARLIGHTGSM-cd8uv
    @STARLIGHTGSM-cd8uv 7 часов назад

    Sikuyenda bwino kumene ndiangati akugula feteleza