on my way going to the shop kukagula mowa kut ndiufile y annabera amandipwetekesa mutu heve any question from joab chakhaza kumangot malamulo athu sakulora relo alikut 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Milandu yaku Malawi ikukhala bwanji this my first kumva kuti muthu wamangidwa kamba koti amafuna kuphwanya lamulo 😊 ma judge mulipo koma where did you get this power mudziwaletsako a mcp kuti malamulo anu samatelo👣🔊
Good and l hope everything it will be fine
Jfk all the way from cape Town pa boma ❤❤
Is good nice now Zikom mulungu asikudalisapo chakwera achoke 2025
Free Malawi, free Malawians. Freedom thou art a foot....
💃💃💃wanyera chikangawa kkkkkkk umati ungatani machende ako
Ili ndi dziko la Mulungu zikomo Ambuye ndinu Mokha mumakhala ndi mayankho anthu anu a Malawi ❤❤❤
Democracy woyeee Mizimu ya anthu 9 aja uwuse mumtendere not forgetting Ralph Kasambala ,chonde timenyereni nkondo ,
Amen nthawi ija yakwana yochoka pa pando Mr chikangawa wagwa nayo keasala nkumapita ku Court every week ya 2025 nyiiii
Chakwela ndi mbuzi yopanda zelu
Very good every body must register inorder to exercise his or her to vote.
Hallelujah 🖐️🖐️🖐️🖐️🖐️🖐️🙏🙏🙏
Ambuye musatisiyire pomwepo
NRB isamakanamizireso net work kumalemba aliyense kuchoka apo kulembesa ku mec
Mulungu sichakwela kapene chimwendo ayi dzikoli ndilamuthu Wina aliye sidzimene amafuna makape enawa
Ndipo chikangawa mmm ndigalu kwabasi
Mulungu mutiyankhe tilimuwulamulilo asatana mcp yikutizuza amalawi
Wagwa nayo Anabel izoooo usova 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Kma yesu ameneyu aaaaa watimenyera nkhondo ife tili chete
Kungopanga zoti ena azidziwe basi ❤❤❤
Osaopa amalawi dzikoli ndilathu
Khoti layamba kuopa lawyer uja kuti awaulula
😂😂😂😂
Amen kumwamba kuli mulungu
MCP yomwe ikulamula panoyi ndi yomwe ijayi ya ku Ghana ya kamuzu banda.Chakwerayu wangokhalapo ngati chukwangwani chabe.🐊🐊🐊🐊🤦🤦
Passports and driving licences belong to the government please.
Mayi Joyce banda amamupotsa chalakwe poganiza.
Chakwela wamisala akufuna kuyesa kapena Kuti kuphuzila kubela Ngati chilima komat sizitheka
Nkhani, yabwino kwa amalawi okonda ziko lawo salute
Amen mwatimenyele nkhondo ife tli chete chi satanacho chichite manyazi
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
UTM vote yangaaaaaa
Chilima musagone mwachangu paka tizavote chifukwa tizasowa zimu wanu pathawi yovota chakwela mazi basi
Smartmatic isagwiritsidwe ntchito
Ndipo watsalanso nzimai uja mtali manja atule pasi usindo hule ameneyo
Ambuye musasiile pomwepa chonde tioneni ife ana anu
The smoldering charcal👐👐👐
Kodi ndingalipeze kuti Buku la smoldering Charcoal 😂😂😂, nchere, Bota aaaaa you just reminding me in those good old days
@@JustinLipipa Tafufuzani mma book-shop Blantyre ko
Aleluya
An assessment need to be done on condition known as dyslexia
Amen
MULUNGU SI JEMUSI!!!!!! KUMENYA KUGWETSA BASI
Murungu aremekezeke ndizo timafuna zimenez
😂😂😂😂mbuzi za amalawi.....
How do you recognise the citizen without ID.....
MCP inawina musavutike....
The entire mec is MCP family
Tikavota bas🤣
Zochitika kuno ku malawi ndingoti Dzuka MALAWI
Amen ambuye zikomo mwatiyakha pepho lanthu
❤❤❤❤yaah
Mcp ija pa ulendo basi ma plan anu aduka,
Ameen
Kumwamba kulandire ulemu
Nkhani kma imeneyo
Apa mudzi onse wakwathu tikavota basni kkkkk Moto kuti buuuui
Wagwa nayo.ndani
Chiletso sichintheke
This woman has lost her senses Joyce
Atsogoleli athu simuchita manyadzi ponamiza anthu awo.
Zoona masten
Sono Za smartmatic zija zilipat guys 🤔
Ambuye tipatseni munthu ozatiimila 2025 popeza munthu tilibe
I can forsee the Rise and Fall of Eid Amin part 2, ahead 😅
Tipatseni ife chakudya chathu chalelo
Wina alila kkkk😂😂😂😂😂
Wina alira chaka chake nchino
Vuto ndi kaphunzisidwe sikali bwino.
on my way going to the shop kukagula mowa kut ndiufile y annabera amandipwetekesa mutu heve any question from joab chakhaza kumangot malamulo athu sakulora relo alikut 🤣🤣🤣🤣🤣🤣
Ali mmadzi ameneyo 😂😂😂😂😂😂
❤❤
Tili komweko bas 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
God and God alone😅😅😅
Ndubwera lne ndzarembetse lme
Kuyambila inuyo.
Hahahah izi ndazikonda, odi nkalembese ine
Ndazkonda zimenez
Pamenepa zili bwino kwambiri
Zopusa basi makape inu
Ndipo live
Apa ndye zilibwino tsopano
MEC chair finally defeated
CHITSIRU CHIJA CHI TONKHWE-TONKHWE
@@Kabwilachikangawakkkkkkkkkk 😂😂😂😂😂😂🎉
Nkhani yabwino kwambili
Indendizona
Moto kuti buuuu
Koma kumeneko 😅😅😅😅
Agwa nao akanganya amenewa
Kumwamba kudyele nyama
Zilibwino
Milandu yaku Malawi ikukhala bwanji this my first kumva kuti muthu wamangidwa kamba koti amafuna kuphwanya lamulo 😊 ma judge mulipo koma where did you get this power mudziwaletsako a mcp kuti malamulo anu samatelo👣🔊
Nthawani tidusa inu
Dusani bwana 😂
Hluuuuuuu ulemu wanu dutsani😂😂😂😂😂😂😂
Anabel 😂😂😂😂😂😂😂 dweku
Tikavota 😂😂
Deal
Ndetika votela ndani umuvotela akusowa osewa zaozimozi
Iwe sukuona, sukumwa , kapena political blindness
Political blindness