NJIRA ZINA ZOPEZERA UMBONI WA CHOMWE CHINAPANGITSA NGOZI YA NDEGE YOMWE INAPHA DR SAULOS CHILIMA
HTML-код
- Опубликовано: 13 июн 2024
- NJIRA ZINA ZOPEZERA UMBONI WA CHOMWE CHINAPANGITSA NGOZI YA NDEGE YOMWE INAPHA DR. SAULOS CHILIMA NDI ANTHU ENA 8.
Развлечения
Kuyankhura koma kumeneku ithink ndinu munthu wowopa Mulungu. God bless you
It's not all aircrafts that carry data and voice recorders because the equipment is very expensive in most developed countries only planes that carry above 16 passengers and they are commercial,all planes are mandated to have a transponder which sends a ping that to show position for the air craft.And this aircraft being military less hope it was carrying data and voice recorders and that they were recovered safely for engineers to analyse.On top of that service records, communication between pilots and traffic control also plays a big role in investigation.
This is the type of wisdom we need, ndamva audio yanzeru since i started following this issue. Stay blessed
My deepest condolences to our beloved sister country of Malawi. As a Zambian citizen I mourn with you. The Lord is your strength!😢
This is so clear
Zikundiwawa kuchiona chichakwera pamwambo umenewu aaa amalawi please 🙏 munthu wationjeza uyu
Ose anali kuja amaziwa siku lakwana inuyo mumaona ngati chilima azamfa imfa yodwala yokha kapena ndi wamuyaya mulungu uja mmamulila uja kuti zithu zikudula akumva mapemphelo aja
Usapiteko tisie tiike maliro a president wathu mwaulemu
He wasn't suppose to be there
It's accident you never pridict or know if the pilot loss the control so what ? He was not God chilima
@@glorynkhata1185the pilot never lost control. The villagers that live near that place said that the plane landed perfectly do not blame the pilot 😑😑
Munthu amene anapanga kuti chilima ayende pa ndege akhale munthu oyamba kupereka umboni chifukwa iyeyo ndiamene ali ndi nkhani yonse ya imfa ya chilima ndipo akuziwa chilichose chomwe chinachitika ndipo ndiyemwe anapanga plan yonse ya mmene chilima amayenera kuyendera
Bwana ndinu munthu wanzeru koopsya. Nkanakonda nkanakudziwani.
Your are a matured person, civilized.
Mafana oganiza bho ena ndi amanewa kupeleka upangili ukwanila bwino
Ndipo kwambiri!
May the Lord bless you brother for your wise and humane speech may the Lord give you abundant wisdom...
God bless Malawi with wise and intelligent people like you bro.
But such good ideas can't be welcomed now in Malawi we are amongst the weakest people.
But you are talking well bro
My heartfelt condolences from Zambia
Thanks brother mwayankhula bwino
This massage is open a Malawian eyes let work together to find what cost deaths of our peoples RIP
Umbuli these record information no one can stop it... This man is talking something very sensible ❤❤
Inu abwana mnapitadi ku school mnthu wa school amalankhula motelomo zikomo God bless you.
We need people like u God bless you ❤❤❤❤❤
Not need people like him.... We have to be like him
We have lost our dearest father my your Saul Rest in Everlasting peace my the good lord provide love Mary
Very true.
Takumvan abwana
Well said sir. It's my hope that the two devices were collected from wreckage site, are secure and will be made available during enquiry.
May their souls rest in peace.
This massage makes a lot of sense
Thanks for this massage 🙏
Kulakhula kwa wisdom brother
Well said bravo may the souls of those who were in the plane rest well
Well spoken, keep on giving better and good advice to the nation of Malawi, only God knows what really happened the day our beloved deputy president passed on, let only the investigation reveal the truth
May the souls of the deceased rest in eternal peace 😭😭😭😭😭😭
May the lord show his grace through our brothers and sisters who lost their lives due to this accident
God bless upangili wabwino
Thanks polangiza ndikuphuzisa komwe koma ino ndithawi yoti athu alakhule zakukhos kwao iyi ndi imfa yowawa so do pray with it
Good message
Malawi 🇲🇼 my country,mourning together here in Zambia 🇿🇲
Ambuye akudalitseni. Thus strong word
Kufotokozela bwino,nzika ya nzeru.Ambiri ndi okhudzidwa koma kulira ndikosiyana-siyana.Tiyeni tilireni,tiyike maliro,then kafukufuku achitidwe mosasiya kanthu mpaka zidziwike zeni-zeni zomwe zinachitika,inali ngozidi kapena umbanda.
Well said but kwathu kuno chilungamo chimabisala when people in power, rich and highly trained and educated are involved coz they influence the outcome of the investigations
Koma this time they will fail miserably
God have mercy...
Well impact information Leader
Following with interest
Thank you sir ❤❤
A big respect to you sir
God bless you Mr
Loud and clear milandu sorted km funso tizinthu timeneto tilipo
God bless you man
Thank you sir
This is a good talk
Ambuye wakumwamba bwelesani nthenda yamisala pa mbeu yose ya chakwera ndi azake ose achiwembu😢😢😢
Mavuto abwerakale pano Kaya atimanga. Atimange basi chakwera wapha chilima 😭😭😭😭
Mwayakhula Mr
God bless you sir
Leader par excellence.MHSRIP 🙏
Sad story to loosing anthu omwe amatipatsa chiyembekezo Pa malawi mizimu yawo iwuse mu myendele
aboma azifufuza chani aboma ndi amene apha anthuwa anachoseranji zimenezo nfusen kunkuyu 'chakwera 'zikhale ng'oma ' ndi asilikali ndi apolice achita kuphedwa ndi mcp umboni ndiwuti
Umboni ngati muli nawo tionetseni ugwire ntchito
Zikuwawa abale 😢😢😢😢😢 taluza anthu dziko Muno
Kom Chilungamo chimaziwika nthawi ikakwana ndipo muzachita manyaz kut Amalawi aziwa chilungamo sopano akuteng step ina yot kuyikilaba kumbuyo sizagwira😢
Respect Sir
Awa ndimaganixo womwe ndimaganiza cox ndidavaposo zama devices amenewa kuchoka kwa bwana wanga wa chi China 🇨🇳
Well said 👏👏
Nice one 👍 bro message yamphamva imeneyi, maka potiziwitsa bwino lomwe dza tizida Tosunga information tamundegeti kuti timakhala malo olimba or Ndege itayaka moto komano tizida timeneti sitikhuzi ndi moto, I hope tizida timeneti tilipo, ambuye alemekezeke
God bless you
Respect🙏
Komanso ma phone a ma passengers can also be used because amongest passengers one might think of recording or eri
That's only way to find out the foult of the crach of our plan
Respect,🙏
Iwe Mbuz umafuma azibisa Kut anthu asazione azione kumene oro akanakhala malophyata akanatulutsa coz ngoz siingavule tayi,shat,jekete zose
Bambo uyu ali mbali yachakwera angoyenda mbali apa
Perfect said 😢
Too sad rip our brothers and sisters we believe almighty is with your souls Amen
Eish ndiri kudandaura ini why why mara, forever in our hearts
Well Spoken
Zimenezo zili Ngati macamera anthu amatha kuzimitsa magesi Chocho camera singajambure Chocho musawanamize anthu , zimenezo kutheka Kuti anazipanga off ndizipanga anthu
Zidakakhala izizi zachitika ku America bwezi zitapezeka ndithu
Mukamati legend mukutanthauza chani
This doesn’t need a forensic expert to unearth the truth of the demise of Chilima.
There are only few questions to be asked.
1. Not a question as per se BUT just follow the sequence of things that have happened around Chilima the past two months.
2. Who can stand to benefit from Chilima’s demise?
3. Those that can benefit from Chilima’s passing, what strange things did they say or do in the past two months or so????
These are just some of the few questions that if correctly answered, we can have a pointer to what really has happened to Chilima and who is or are behind the so called accident.
Live from rustenburge
Lord have mercy on us
Kulankhula kwa mkhalapakati❤
Amen
Good Messnge koma Chakwela you mast go
Its hard
Wich radio station onse ndi anomaly palibe, umboni uziwike maliro asanaikidwe
Never give up
Kuyankhula uku ndi kwa umunthu koma pakakhala kuti kafukufuku watha anthu izi amaziona, monga momwe anali public figure? Za enawo tiribe nawo ntchito koma chilima. Pali mau ngati mukuona kuti chilungamo chidzavuta gwiritsani u salvage. Usaone ngati pali umbuli
Mulungu lowreranipo, tiziwe zoona za ngozi yimeneyi.
Nkhani ndiyoti zimenezo aboma azibwelese kuti azipange cleare okha
Okay following 😢😢😢😢😢😢😢😢
🙏
May their souls rest in peace what a tragic
God please give big disease family for chakwera 😢😢😢 mukantheni chonde mulungu wanga napota nanu
Not only Malawi but all maneba mu africa
Zomvesa chison rest in peace Mr chilima
Kachiduloko nkutheka chakwera anatuma wanthu kuti akachoseko
😢😢😢 Amen 👏👏👏👏
Good message But impeachment process go ahead
Rest well ❣️❣️❣️
kupepesa ndikomweko koma ndizomvesa chison kwambiri chifukwa mpungwepungwe ulipowu ndi chifukwa cha zithunzi zake zomwezo
They must not remove these devices from
Kutheka titapezeka timeneto umboni ungapezeke pakugwa kwa ndenge mmm ambuye ayendelepo ndithu
Straight
Am so Hurt 😭 with this death Eeeh 😢
Bro lnuyo msg yanu munayamba bwino kenako kulakwisa ndinu achitsiru abise zinthuz chifukwa chani zikukusangalasa lwe ndege lri ndimanja kutu lkavure zovara munthu nanga ma4n a Dr chilima ndi anthu ose alikt lweso kape information lkunenayo palibe chazeru atapangepo chakwera apa umboni owona uli muanthu
koma phone ikakhale moyo pangozi yoopsayi!!! Malawi tidzuka liti ku umbuli
Akutuma kt utikhazike chete ifeyo
Tikumva kuwawa my brother koma zikomo mwayankhula bwino pitilizani kutilimbikisa
chomwe chasarapo ndi holiday basi mumuona chakwela azayika holiday yoti ndege inagwa kumalawi chosecho wapha anthu ndi iyeyo
Zokayikitsa ngati zida zimenezo zingapedzeke mu ndege imeneyi ndakqyikila kwambili
muziti amene amapezeka kumeneko ndi zigawenga zokha zokha zimene zimatumizidwa ndi chakweta ' kunkuyu 'zikhale 'ndi army mosaopa
Mr.. Mulungu akudalitseni poyankhula bwino chonchi no mistake 😢😢
Technology
I see the same happenings of 1986 when Samora Machel died in the same act
Onse omwe atisiya mizimu yawo iuse mumtendere zoyakhula ziziyakhulidwa koma answer yeniyeni ndiyokut Malawi waluza anthu ofunikila Basi.