The problem with Malawi is nkhondo timawasiira anthu ochepa kumenyera ufulu,no wonder akalowa mu boma amakasakaza chuma.We all need to fight for our freedom
Or abadwe mwatsopano Koma mizimu ya anthu anapha ija imufafanthabe Mulungu wake uti okumba mapemphero a munthu opondeleza oipa wakupha okondela ngati ameneyo
kkkk mwakumana usazindikila nokha nokha vuto mli busy pa ma phone mwayiwala kuti azanu ali pa ground . zoti peter analamula bwino mkunama matha ma albino ambiri
Komanso boma ili manyaka eni eni koma ndlama zikuwonongedwazi ndi zabwino bwino? Mzipatala mulibe mankhwala koma ndlama zogula anthu muli nazo shame Malawi government shame Mulungu kumwambako muzimutetezera Bon kalindo kwina kuli konse angapite
Nanuso bwanji Joyce Banda mbuzi yamunthu chakwera mutu ngati phwala lambuzi
Kuyankhula zomveka bwino ndipo zaphindu zokhazokha congratulation boss
Born you always talk the truth ❤❤😂
azibale athu amene anaphedwa ndi chakwera kuchikangawa ndi zomvesa chison kudziko lino chakwera ndi chigawenga
Ulemu wanu
The DC akamuna okakha NDI mawaya
The problem with Malawi is nkhondo timawasiira anthu ochepa kumenyera ufulu,no wonder akalowa mu boma amakasakaza chuma.We all need to fight for our freedom
Long live Boooon Kalindo !!!!! The D C ccc !!!! The Wise Guy !!! Iweyo palibenso !!
The DC bon kalindo the great 💪💪💪💪
zoona Bon kalindo ngakhale kuno ku south Africa zimatikwana kwa basi zimene akupanga president
Ati bon Kalindo amangidwebe😂
Or abadwe mwatsopano Koma mizimu ya anthu anapha ija imufafanthabe Mulungu wake uti okumba mapemphero a munthu opondeleza oipa wakupha okondela ngati ameneyo
Mumakwana boss,osawanyengerera makape achina kumkuyu,zikhale ndi chakwera yemwe😙😙
😅😅😅😅😅 Kakakakakakakakaka DC 😂 our president kkkkmwana owopsa heav😂😂😂
Akhwakhwananda amenewa 🐊🐊🐊🐊 atitola kwambiri
kkkk mwakumana usazindikila nokha nokha vuto mli busy pa ma phone mwayiwala kuti azanu ali pa ground . zoti peter analamula bwino mkunama matha ma albino ambiri
😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥kuti buuuuuuuuuuuuuu
Mbambande Mr
Machine bon kalindo ❤❤❤❤
Zoonadi Mr Kalindo simukunama Chakwera ndi gulu lake they are mbunzi za anthu they are fools
Bon kalindo our president
Iweyo umandiwaza chifukwa umayankhula chilungamo. Palisouyu Limpopo FM NDI bakili muluzi TV anthuinu ndinu madolo❤
Zakeyu powonetsa kubadwa mwatsopano anabweza theka lachuma cheke kwawomwe anawabera ndiye Chakwera pamodzi ndi amithenga Ake onse abweze zomwe atiberazo powonetsa kubadwa mwatsopano
60 years subtract 4 years yamazumzo ya chakwela
Mumakwana Avon karindo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Abon kuyilawilira😂😂😂
Sowuna auseni agalu amenewa achakwera
My Hero..The Dc
Izoooh Hankonnani pwiya aleleni iiwesese😂
Bon k amatha ❤
Chakwela mhuzi ya muthu
Bon muuzeni chakwera kuno ku mangochi asazafike tizapha tokha ndi galu
Iwo andale si bola akhutitsa mimba zawo
Kkkkkk winiko samatopa mumamuseweletsa😂
Koma thawi ikubwera ndithu mlungu atiyakha ndithu mlungu wathu salephera❤
I agree with Kalindo..the #thinkalike
THE D C BOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOON KALINDO 💪💪💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
President omvetsa chisoni chakwera ulamuliro wake ngati dzaka 100 chifukwa cha dyera
Iweyo ndi one
Machende awo awa
You saying the truth
Inetu ndi mchewa koma nyasi izii sitikukondwa Nazo ,from nathenje
Mwana oopsa kwambiri
Koma opposition ikalowa mu boma imasinthanso kuiwala zomwe ife amalawi tinkalira .
Vuto a Malawi ife mantha
awa akungolankhula Loma palibe zomwe zikuchitika.mmalo mot tipange zinthu ngat kukenya.
Dziko lamkaka ndi uchi lija pano ndi sabora ekhaekha😢😢😢😢
Our Hero
Aaaa kuba mistake kuyika MCP papando iiiiiii tinalakwitsa
Kodi cakwera akufuna anthu amuvotere 2025 afuna adzidzatani poti iye sadziwa kanthu akufuna adzapitilidze kuba conde. Cakwera usavutike amalawi sitikukufuna ngakhale pangono watilidzatu iwe watidzudza dzaka 5 ngati dzaka hundred
Ulemu wanu comrade
The DC Bon kalindo ❤
Koma why sakuyamkhulapo za manganya vice president ku mcp
Morning
Wamsala iwe amalawi umanenawo ndi ati? enafetu sutifuna zolandila zimene umafuna iwezo ife amene timalima tikusangalala kabwebweta ndi misala yakoyo
The DC
madala madala born k
💪💪💪💪
We respect fools so no need to reply... 😂😂😂😂
❤❤❤❤❤
I just watch so that kalindo can make some money
The D.C.
Vuto amalawi mumawombele mmanje fiti kodi simudziwa kut mtambo ni akalindo vinanyeza kwambili pita muthali mpaka apita analuza masankho anazikambe amenewa
Nkhani ya ma ID muikokomeze kt apart from mcp zipani Zina taonetsetsani zomwe zikuchika mmaderamu,tabwerani kunathenje midzi ngati monga mphete village,mtsotsa, sanjiko,nyama ,kaphala ,matapira,Chatha ana osafikamo Zaka,
6 July ndiye chani
Koma akamati abadwa mwasopani akuyesa kuti ndiopusa Never ever changes my mindset
Komanso boma ili manyaka eni eni koma ndlama zikuwonongedwazi ndi zabwino bwino? Mzipatala mulibe mankhwala koma ndlama zogula anthu muli nazo shame Malawi government shame
Mulungu kumwambako muzimutetezera Bon kalindo kwina kuli konse angapite
The DC 💥💥💥💥💥
Truth must be told plainly without fear
Chamba kkkkkkkkkk
Wapenga chakwerayu
Abon kuyilawilira😂
Mutayeni uko Joyce Banda ndihule wachabe chabe
The dc
ine Mchewa Koma Chakwera Guy osamuvoteraso
Ufulu unali mbuyomu koma pano ufulu uja anatilanda,kumangomangidwa ...Boma ili lankhaza zedi.
Empty tins
60years of independence but nothing to show
Kkk
Tell them where to get off your ass The DC. Chakwera amadya maliro
Terelini
Chakwera wationjedza
Wow
Chakwera ndi pa msete seriously
😂😂100%
Kuyankhula mwachulumgamo
😂😂 telelini
Let's not be negative for everything. Peter was also useless
Kodi aborn kalindo mapemphero ndikuti ndichinthu choyipa kodi nayesa unali mwambo wamapemphero koma inuso zina mumangolankhura zopepela zokhazokha ndipo amene amakupasani ma coment okutamandani nkupanda nzeru pa inuyo tikuwona ndipanja zowona dairy kubwera pa air basi nkhani za ziii zopanda phindu
Kungosiya kuvera bas coz mutopa🥺
Koma muli nkuchikanwa kosatopa now it's boring
Kodi zinachitikira kuti? Sindizisate nane 😂😂😂
😂😂😂😂😂
Kkkkkkkk Born K the DC
Bon kalindo the great💪💪💪💪💪
Wapengatu chakwelayu😂😂😂😂is Dog.
Pangoline the DC ❤❤
Kalinda mtambo niamene anayika chakwela paudindo vitsilu vimenevi vikutenga ngati amalawi opusa amene omatsatila zokamba zanu nose awili ndinu munayika amcp pampando mwemwe vitsilu amalawi osavela viwanthu vimenevi😅😂😊😊
Mumuuze Kalindoyo kuti ndiodwala komaso ndichitsiru kwabasi zinthu zinaipa kuyambila pa Bakili mpaka pano
Iwe osamuudza wekha bwanji
Iwe ndi mbudzi kwabasi, zitaipa nthawi imeneyo unapangapo chani😂😂
Iwe ndi chisiru nthawi ya maprezdent enawo fanta timagula 200 kwaca nthawi yachakwera 750 wakumudzi angamugulire mwana fanta manyi amako wava cakwera waononga dziko kukwera kwa zinthu ndiye anthu tikamalira iwe wati tikunama mbusa wasatanic akucoka 2025 mdipo adzamumanha ndende yace tikumba dzenje mpaka adzafera momwemo munthu oipa mtima ngati konyera
@@user-hm9nc7lz6e galu kwabas
Mwapenga inu eti
Chakwera ndi bakha weniweni.
Wandiwazaso ndi busa ujayo wamzeru kwambiri kulalikila mwaphavu
Abon kuyilawilira😂