BON KALINDO 7 JULY 2024 KUKHDZULASO PA CHI SUNDAY

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 5 июл 2024

Комментарии • 115

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 10 дней назад +11

    Nanuso bwanji Joyce Banda mbuzi yamunthu chakwera mutu ngati phwala lambuzi

  • @KelvinMangwengwe
    @KelvinMangwengwe 10 дней назад

    Kuyankhula zomveka bwino ndipo zaphindu zokhazokha congratulation boss

  • @limbanimtitima9170
    @limbanimtitima9170 10 дней назад +5

    Born you always talk the truth ❤❤😂

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 10 дней назад +2

    azibale athu amene anaphedwa ndi chakwera kuchikangawa ndi zomvesa chison kudziko lino chakwera ndi chigawenga

  • @chiefjusticie
    @chiefjusticie 10 дней назад +2

    Ulemu wanu

  • @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un
    @WITTNESSMBOBADINHONJOLOM-bv4un 10 дней назад +1

    The DC akamuna okakha NDI mawaya

  • @owenmanda1741
    @owenmanda1741 10 дней назад +2

    The problem with Malawi is nkhondo timawasiira anthu ochepa kumenyera ufulu,no wonder akalowa mu boma amakasakaza chuma.We all need to fight for our freedom

  • @MacreaChilingulo-ob9gb
    @MacreaChilingulo-ob9gb 10 дней назад +1

    Long live Boooon Kalindo !!!!! The D C ccc !!!! The Wise Guy !!! Iweyo palibenso !!

  • @BinwelLukali
    @BinwelLukali 10 дней назад +3

    The DC bon kalindo the great 💪💪💪💪

  • @DanielChima-zl2uo
    @DanielChima-zl2uo 10 дней назад +1

    zoona Bon kalindo ngakhale kuno ku south Africa zimatikwana kwa basi zimene akupanga president

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 10 дней назад +1

    Ati bon Kalindo amangidwebe😂

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 10 дней назад

    Or abadwe mwatsopano Koma mizimu ya anthu anapha ija imufafanthabe Mulungu wake uti okumba mapemphero a munthu opondeleza oipa wakupha okondela ngati ameneyo

  • @TecksonKaima-dr6er
    @TecksonKaima-dr6er 10 дней назад +2

    Mumakwana boss,osawanyengerera makape achina kumkuyu,zikhale ndi chakwera yemwe😙😙

  • @RichardMedi
    @RichardMedi 10 дней назад +2

    😅😅😅😅😅 Kakakakakakakakaka DC 😂 our president kkkkmwana owopsa heav😂😂😂

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 дней назад +3

    Akhwakhwananda amenewa 🐊🐊🐊🐊 atitola kwambiri

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 10 дней назад +1

    kkkk mwakumana usazindikila nokha nokha vuto mli busy pa ma phone mwayiwala kuti azanu ali pa ground . zoti peter analamula bwino mkunama matha ma albino ambiri

  • @EstherNangomba
    @EstherNangomba 10 дней назад +1

    😂🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥kuti buuuuuuuuuuuuuu

  • @AustinMangani
    @AustinMangani 10 дней назад +1

    Mbambande Mr

  • @DYSONKUMPEREMBE
    @DYSONKUMPEREMBE 10 дней назад

    Machine bon kalindo ❤❤❤❤

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja 10 дней назад +2

    Zoonadi Mr Kalindo simukunama Chakwera ndi gulu lake they are mbunzi za anthu they are fools

  • @JosephMichael-x7v
    @JosephMichael-x7v 10 дней назад +1

    Bon kalindo our president

  • @trifoniachilunda6263
    @trifoniachilunda6263 10 дней назад

    Iweyo umandiwaza chifukwa umayankhula chilungamo. Palisouyu Limpopo FM NDI bakili muluzi TV anthuinu ndinu madolo❤

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 10 дней назад +1

    Zakeyu powonetsa kubadwa mwatsopano anabweza theka lachuma cheke kwawomwe anawabera ndiye Chakwera pamodzi ndi amithenga Ake onse abweze zomwe atiberazo powonetsa kubadwa mwatsopano

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 10 дней назад +3

    60 years subtract 4 years yamazumzo ya chakwela

  • @BeatrizUlanda-ht2th
    @BeatrizUlanda-ht2th 10 дней назад +1

    Mumakwana Avon karindo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @AbondBolbo
    @AbondBolbo 10 дней назад +3

    Abon kuyilawilira😂😂😂

  • @user-ty5zh2xi9b
    @user-ty5zh2xi9b 10 дней назад

    Sowuna auseni agalu amenewa achakwera

  • @ShaibMusa
    @ShaibMusa 10 дней назад +2

    My Hero..The Dc

  • @blessingsmwale6007
    @blessingsmwale6007 9 дней назад

    Izoooh Hankonnani pwiya aleleni iiwesese😂

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 10 дней назад

    Bon k amatha ❤

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r 10 дней назад

    Chakwela mhuzi ya muthu

  • @SilverMkwatula
    @SilverMkwatula 10 дней назад +1

    Bon muuzeni chakwera kuno ku mangochi asazafike tizapha tokha ndi galu

  • @ChikumbutsoTsalangu
    @ChikumbutsoTsalangu 10 дней назад +2

    Iwo andale si bola akhutitsa mimba zawo

  • @AliceMpaso
    @AliceMpaso 10 дней назад

    Kkkkkk winiko samatopa mumamuseweletsa😂

  • @GanizaniKamvazaana
    @GanizaniKamvazaana 10 дней назад

    Koma thawi ikubwera ndithu mlungu atiyakha ndithu mlungu wathu salephera❤

  • @user-ve7rx7vj1g
    @user-ve7rx7vj1g 10 дней назад +1

    I agree with Kalindo..the #thinkalike

  • @eliaschinoko2086
    @eliaschinoko2086 10 дней назад +1

    THE D C BOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOOON KALINDO 💪💪💪💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma 10 дней назад

    President omvetsa chisoni chakwera ulamuliro wake ngati dzaka 100 chifukwa cha dyera

  • @TorshKadango
    @TorshKadango 10 дней назад +2

    Iweyo ndi one

  • @charlesmataka1700
    @charlesmataka1700 10 дней назад

    Machende awo awa

  • @IanChidothe
    @IanChidothe 10 дней назад

    You saying the truth

  • @KennethChazama
    @KennethChazama 10 дней назад

    Inetu ndi mchewa koma nyasi izii sitikukondwa Nazo ,from nathenje

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 10 дней назад +1

    Mwana oopsa kwambiri

  • @EliaMhone
    @EliaMhone 9 дней назад

    Koma opposition ikalowa mu boma imasinthanso kuiwala zomwe ife amalawi tinkalira .

  • @CollinsHala
    @CollinsHala 9 дней назад

    Vuto a Malawi ife mantha

  • @chestermajora
    @chestermajora 10 дней назад

    awa akungolankhula Loma palibe zomwe zikuchitika.mmalo mot tipange zinthu ngat kukenya.

  • @JeremiahChilenje
    @JeremiahChilenje 10 дней назад

    Dziko lamkaka ndi uchi lija pano ndi sabora ekhaekha😢😢😢😢

  • @marychavula698
    @marychavula698 10 дней назад +1

    Our Hero

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 10 дней назад

    Aaaa kuba mistake kuyika MCP papando iiiiiii tinalakwitsa

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 10 дней назад

    Kodi cakwera akufuna anthu amuvotere 2025 afuna adzidzatani poti iye sadziwa kanthu akufuna adzapitilidze kuba conde. Cakwera usavutike amalawi sitikukufuna ngakhale pangono watilidzatu iwe watidzudza dzaka 5 ngati dzaka hundred

  • @HarryYottam-ft1bo
    @HarryYottam-ft1bo 10 дней назад

    Ulemu wanu comrade

  • @AffickChaona
    @AffickChaona 10 дней назад

    The DC Bon kalindo ❤

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 10 дней назад

    Koma why sakuyamkhulapo za manganya vice president ku mcp

  • @AustinMangani
    @AustinMangani 10 дней назад

    Morning

  • @ClementChisemphele
    @ClementChisemphele 10 дней назад

    Wamsala iwe amalawi umanenawo ndi ati? enafetu sutifuna zolandila zimene umafuna iwezo ife amene timalima tikusangalala kabwebweta ndi misala yakoyo

  • @MarkinaJohn
    @MarkinaJohn 8 дней назад

    The DC

  • @user-ss9bj5eh6b
    @user-ss9bj5eh6b 10 дней назад

    madala madala born k

  • @IbrahimRaphael-z3l
    @IbrahimRaphael-z3l 10 дней назад

    💪💪💪💪

  • @AndrewChitsamba
    @AndrewChitsamba 10 дней назад

    We respect fools so no need to reply... 😂😂😂😂

  • @ShafieIdrissah
    @ShafieIdrissah 10 дней назад

    ❤❤❤❤❤

  • @rhinovaheke6614
    @rhinovaheke6614 10 дней назад

    I just watch so that kalindo can make some money

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete 10 дней назад

    The D.C.

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 10 дней назад

    Vuto amalawi mumawombele mmanje fiti kodi simudziwa kut mtambo ni akalindo vinanyeza kwambili pita muthali mpaka apita analuza masankho anazikambe amenewa

  • @KennethChazama
    @KennethChazama 10 дней назад

    Nkhani ya ma ID muikokomeze kt apart from mcp zipani Zina taonetsetsani zomwe zikuchika mmaderamu,tabwerani kunathenje midzi ngati monga mphete village,mtsotsa, sanjiko,nyama ,kaphala ,matapira,Chatha ana osafikamo Zaka,

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z 10 дней назад

    6 July ndiye chani

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d 10 дней назад

    Koma akamati abadwa mwasopani akuyesa kuti ndiopusa Never ever changes my mindset

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 10 дней назад

    Komanso boma ili manyaka eni eni koma ndlama zikuwonongedwazi ndi zabwino bwino? Mzipatala mulibe mankhwala koma ndlama zogula anthu muli nazo shame Malawi government shame
    Mulungu kumwambako muzimutetezera Bon kalindo kwina kuli konse angapite

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 10 дней назад

    The DC 💥💥💥💥💥

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 10 дней назад

    Truth must be told plainly without fear

  • @yobesaikonde6166
    @yobesaikonde6166 10 дней назад

    Chamba kkkkkkkkkk

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn 10 дней назад

    Wapenga chakwerayu

  • @AbondBolbo
    @AbondBolbo 10 дней назад

    Abon kuyilawilira😂

  • @FaruckMuhammad
    @FaruckMuhammad 10 дней назад

    Mutayeni uko Joyce Banda ndihule wachabe chabe

  • @PatronChanza
    @PatronChanza 10 дней назад +1

    The dc

  • @ChikuMatemba
    @ChikuMatemba 10 дней назад

    ine Mchewa Koma Chakwera Guy osamuvoteraso

  • @user-dd1qq5xq1k
    @user-dd1qq5xq1k 10 дней назад

    Ufulu unali mbuyomu koma pano ufulu uja anatilanda,kumangomangidwa ...Boma ili lankhaza zedi.

  • @AndrewChitsamba
    @AndrewChitsamba 10 дней назад

    Empty tins

  • @HamitonFrank
    @HamitonFrank 10 дней назад +1

    60years of independence but nothing to show

  • @yusufbreak905
    @yusufbreak905 10 дней назад

    Kkk

  • @elishamael-shadai
    @elishamael-shadai 10 дней назад +1

    Tell them where to get off your ass The DC. Chakwera amadya maliro

  • @KhumboMunthali-jx5me
    @KhumboMunthali-jx5me 10 дней назад

    Terelini

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 10 дней назад

    Chakwera wationjedza

  • @allansili-rc9gc
    @allansili-rc9gc 10 дней назад

    Wow

  • @mikeasmachine4581
    @mikeasmachine4581 10 дней назад

    Chakwera ndi pa msete seriously

  • @MphatsoGowero
    @MphatsoGowero 10 дней назад

    😂😂100%

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t 10 дней назад

    Kuyankhula mwachulumgamo

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb 10 дней назад

    😂😂 telelini

  • @user-kw7wr4kq9w
    @user-kw7wr4kq9w 10 дней назад

    Let's not be negative for everything. Peter was also useless

  • @SlindiryLoveness
    @SlindiryLoveness 10 дней назад

    Kodi aborn kalindo mapemphero ndikuti ndichinthu choyipa kodi nayesa unali mwambo wamapemphero koma inuso zina mumangolankhura zopepela zokhazokha ndipo amene amakupasani ma coment okutamandani nkupanda nzeru pa inuyo tikuwona ndipanja zowona dairy kubwera pa air basi nkhani za ziii zopanda phindu

  • @nafejonga972
    @nafejonga972 10 дней назад

    Kodi zinachitikira kuti? Sindizisate nane 😂😂😂

  • @InnocentKandaya
    @InnocentKandaya 10 дней назад

    😂😂😂😂😂

  • @ChisamiMalota
    @ChisamiMalota 10 дней назад

    Kkkkkkkk Born K the DC

  • @HamitonFrank
    @HamitonFrank 10 дней назад +1

    Bon kalindo the great💪💪💪💪💪

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn 10 дней назад

    Wapengatu chakwelayu😂😂😂😂is Dog.

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 10 дней назад +1

    Pangoline the DC ❤❤

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 10 дней назад

    Kalinda mtambo niamene anayika chakwela paudindo vitsilu vimenevi vikutenga ngati amalawi opusa amene omatsatila zokamba zanu nose awili ndinu munayika amcp pampando mwemwe vitsilu amalawi osavela viwanthu vimenevi😅😂😊😊

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere 10 дней назад

    Mumuuze Kalindoyo kuti ndiodwala komaso ndichitsiru kwabasi zinthu zinaipa kuyambila pa Bakili mpaka pano

    • @felixmaluku5077
      @felixmaluku5077 10 дней назад

      Iwe osamuudza wekha bwanji

    • @JosephChatama
      @JosephChatama 10 дней назад

      Iwe ndi mbudzi kwabasi, zitaipa nthawi imeneyo unapangapo chani😂😂

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e 10 дней назад

      Iwe ndi chisiru nthawi ya maprezdent enawo fanta timagula 200 kwaca nthawi yachakwera 750 wakumudzi angamugulire mwana fanta manyi amako wava cakwera waononga dziko kukwera kwa zinthu ndiye anthu tikamalira iwe wati tikunama mbusa wasatanic akucoka 2025 mdipo adzamumanha ndende yace tikumba dzenje mpaka adzafera momwemo munthu oipa mtima ngati konyera

    • @ChrisMsonyo-yq2ko
      @ChrisMsonyo-yq2ko 10 дней назад

      @@user-hm9nc7lz6e galu kwabas

    • @ShamilahSaizi
      @ShamilahSaizi 10 дней назад

      Mwapenga inu eti

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki 10 дней назад

    Chakwera ndi bakha weniweni.

  • @jamesmsonkho4830
    @jamesmsonkho4830 10 дней назад

    Wandiwazaso ndi busa ujayo wamzeru kwambiri kulalikila mwaphavu

  • @AbondBolbo
    @AbondBolbo 10 дней назад

    Abon kuyilawilira😂