Limpopo Ntanyiwa watulukila lero ndipo boma ligwa ndi BP ndithu chifukwa eeeh sakupeleka mpata

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 28 авг 2024

Комментарии • 103

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp Месяц назад +14

    Tufuna group Yanu amtanyiwa tikulira mpaka pano

  • @SymonYohane-i5q
    @SymonYohane-i5q Месяц назад +7

    Mbambande iweyo ukundimvesa kukoma kwambiri timafuna anthu ngati antanyiwa ky dziko lanthu likhale lamphavu 🎉🎉🎉🎉🎉

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Месяц назад +8

    More 🔥 comrade mtanyiwa ❤❤😂

    • @yusufbakali
      @yusufbakali Месяц назад +4

      We will waiting for nkhanga zawona

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Месяц назад +4

    Big up mtanyiwa❤ km ine ndikuifuna nyimboyi mwaika kumapetoyi guys

  • @FrankHaruni
    @FrankHaruni Месяц назад +3

    Ofunika kuwayakhula amalawi mr usi atiwayamba kunamidza athu khati wa utm aliwa mcp amalawi akuiwala kutindi thawi yakapeni akutengeka audzeni bwino amalawi mr tanyiwa

  • @GraceZumazuma
    @GraceZumazuma Месяц назад +2

    Tidya ife ndalama zo Koma vote yathu ndiye ng'ooo aiwale tiyeni tidye

  • @NizigiyimanaChantal-c2p
    @NizigiyimanaChantal-c2p Месяц назад +1

    May God bless you ❤❤❤❤❤ god loves you more

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Месяц назад +4

    Akagawa kwandan pot kumangochi nd kwa ayao ndy akut akufun achewa km kul zinthu 🤞🤞🙌🙌🙌🙌🙌😎😎😎😎😎

  • @DavieKidison
    @DavieKidison Месяц назад +4

    Limpompo FM 🔥🔥🔥 bro umakwana akhale poyela agalu amenewa

  • @bensonnamizinga9750
    @bensonnamizinga9750 Месяц назад +2

    Keep it up brother ntanyiwa

  • @ChristinaLigomeka
    @ChristinaLigomeka Месяц назад +3

    Ife mai dzimbiri amatithandiza tili mudzi umodzi anali be sankho zimai ozichepetsa 2014 anali MP wadera lathu tisalile

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 Месяц назад +3

    We love ❤you too ntanyiwa ❤❤❤🎉

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Месяц назад +3

    Pambuyo pa Limpompo yomweyo

  • @user-oj2jr6kf9c
    @user-oj2jr6kf9c Месяц назад +6

    Yooooo!!!!!!! Iweyo mmmm umakwana njala simafika ndikamamvera limpopo

  • @user-ny3it3jp9l
    @user-ny3it3jp9l Месяц назад +4

    Lipopo fire 🔥

  • @ChrisEnos-to5uv
    @ChrisEnos-to5uv Месяц назад +5

    Yomweyo Galu iweeeee😂

  • @RoseChiphiri-ts8jx
    @RoseChiphiri-ts8jx Месяц назад +3

    Ntanyiwa zulo ndinakusowa 😊

  • @user-cd4df3vg4y
    @user-cd4df3vg4y Месяц назад +4

    Ulemu wanu ali Limpopo fm❤

  • @RhodaBandah-sh1ir
    @RhodaBandah-sh1ir Месяц назад +4

    Koma Bt isakhe mbali ku ndix nde anthu anakwiya kalekale

  • @FatimaBakali-v7q
    @FatimaBakali-v7q Месяц назад +1

    Timakukondani Kobasi a Mtanyiwa

  • @HaliJana
    @HaliJana Месяц назад +2

    KOMA CHAKWERA UMAGANIZA CHANI PAKUMUPHA CHILIMA,ULI NDI UMUNTHU IWEYO KOMA?

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d Месяц назад

      Munthu oipa kwambiri eishiiii

  • @BadmanshutterZinkana
    @BadmanshutterZinkana Месяц назад

    Salute mi comrade ✊🏻✊🏻

  • @franciscomalola92
    @franciscomalola92 Месяц назад +2

    more fire nthanyiwa

  • @LuskaMoses
    @LuskaMoses Месяц назад +1

    Tapangani group ra WhatsApp plz nyimbo iyi ngawireni la kayin ndabare plz mtima ukuwawa ine atiphera anyamata akwathu Ku magoni Ife anyaparawa akutipezerera kwambiri😢😢

  • @TenahJustinnalia
    @TenahJustinnalia Месяц назад

    Nyimboyo ndaikonda undiuza bwino zakuchikangawa km nthanyiwa umatimvesa kukoma

  • @ImanRashidi-so4oo
    @ImanRashidi-so4oo Месяц назад

    Powerful massage big up mtanyiwa ❤

  • @InoquebosiCanhosa
    @InoquebosiCanhosa Месяц назад +2

    Auzeni agalu a mcp mumakwana

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk Месяц назад +2

    Fm nomber 1

  • @lindamwanza4958
    @lindamwanza4958 Месяц назад +2

    More fire Limpopo

  • @user-xz3nz7dy1f
    @user-xz3nz7dy1f Месяц назад +3

    Ndipo azaza kale ku chikolobay

  • @FrankHaruni
    @FrankHaruni Месяц назад +2

    Pajatu amalawi ati samachedwa kuiwala adzidzudxika ife nde tinawasiila malawi waoyo

  • @UchiziMwakilasa
    @UchiziMwakilasa Месяц назад

    Munthu wamkulu Ntanyiwa,,,,,,,timakukondani kunoku bwana

  • @petermasenti2084
    @petermasenti2084 5 дней назад

    Comrade mumakwana

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Месяц назад

    Tipasen gulup yan prz tikufuna tizimwaza mauthenga awa palipoose ziko muno, ifeso tatopa.

  • @davidkayangemakala7957
    @davidkayangemakala7957 Месяц назад

    ETI akufuna kukweza msokho ndicholinga atorele ndalama zomwe akutaya pa conversation ma 70mter kkkkk amalawi tinalakwa chani misokho ckugwira karechito kkkkkk

  • @AnussaAlli
    @AnussaAlli Месяц назад

    More fire ❤❤❤ ❤❤ comrade mtanyiwa❤❤❤❤

  • @NoxyChinsembe
    @NoxyChinsembe Месяц назад

    Antanyiwa muzakaponye kanyimboko nafeso tikhale nako

  • @FunnyDimSum-hk1so
    @FunnyDimSum-hk1so Месяц назад

    Kkkkkkkk kom ntanyiwa umatokan ❤one love

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga Месяц назад

    Tipasen nyimbo yomwe yaikidwa kumapetoko

  • @user-on2me8ek5w
    @user-on2me8ek5w Месяц назад +1

    Koma mtanyiwa ndi nyatwa😂😂😂😂

  • @TressLuka
    @TressLuka Месяц назад +2

    Zilikotuuu 😂😂😂

  • @GLADYSCHIDOTHI
    @GLADYSCHIDOTHI Месяц назад

    Akamuna Mr. Ntanyiwa.
    Real comrade.

  • @FatimaBakali-v7q
    @FatimaBakali-v7q Месяц назад

    Ati mkabulamo muli juu 🤣🤣🤣🤣

  • @SelemanIssahAhmad
    @SelemanIssahAhmad Месяц назад

    😂😂😂😂😂😂limpopo😊😅

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Месяц назад

    The best TV in malawi 🇲🇼

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Месяц назад

    We do love you

  • @moosaWilson
    @moosaWilson Месяц назад

    mumakwana bro

  • @MercyMithie
    @MercyMithie Месяц назад +3

    Yomweyo

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Месяц назад

    Nde akunjawo anawalipira mmakwacha anthu akunjao nde oufoipatu

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Месяц назад

    Yomweyo Mr tanyuwa ineyo ndendimakukondani mwinatso kuposa inuyo kkkkkk awoneseni kt imfetso timatha timayenda akumfa kale

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад +1

    Shame Malawi Government shame😭

  • @MillicaBanda
    @MillicaBanda Месяц назад

    Mativetsa kukoma kuno LL makwana

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp Месяц назад +2

    Ine Kumva bwino mtanyiwa

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Месяц назад

    Mumakwala madolo

  • @CharlesChagudubuka-rm6bh
    @CharlesChagudubuka-rm6bh Месяц назад +1

    😂😂😂 nkabudula mwatentha

  • @tannexmsukwa1918
    @tannexmsukwa1918 Месяц назад

    Ndipo Agalu amenewa azangifela kutulo,Anthu woipa sinaonepo pa dziko lapansi.Mulungu siopusa

  • @clementdzakumwashowlove7814
    @clementdzakumwashowlove7814 Месяц назад

    Nyimboyi yakumapetoyo ndikufuna plz

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o Месяц назад

    Yomweyo pumbwa iwee 😂😂😂😂❤

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Месяц назад +1

    Inuso masiku ano simukunena kuswakuswa muli ndi Mantha mwasiyana ndi mluzi channel

  • @SydneySingini
    @SydneySingini Месяц назад

    Umandiwaza badly awuze chilungamo

  • @PreciousMmodzi
    @PreciousMmodzi Месяц назад +1

    Mtanyiwa umatha iweyo ndi one

  • @MalawianMediafm97
    @MalawianMediafm97 Месяц назад +1

    This is comred ntanyiwa on Lipompo FM kuzangoturikira ndi more 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @user-dq9oe8sp8k
    @user-dq9oe8sp8k Месяц назад

    Mbambande comrade ❤

  • @zoeysfunandplay
    @zoeysfunandplay Месяц назад

    Nyimbo ya Kaini yo anayimba ndani ? Nduyifuna

  • @user-ul8fp1ov1k
    @user-ul8fp1ov1k Месяц назад

    tigaireni nyimboyo,ulosi

  • @user-gg9hw4oj2v
    @user-gg9hw4oj2v Месяц назад +1

    🔥💪💪💪

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI Месяц назад +1

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Месяц назад

    Nyimbo ya ayezayayo tikufuna ya full please plus ya Kaini

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Месяц назад +1

    Palibe yemwe angachithawe chilungamo

  • @IgnatiousFote
    @IgnatiousFote Месяц назад +2

    Koma zilipo chaka chino

  • @Yahiya-wm8nd
    @Yahiya-wm8nd Месяц назад +1

    nyimbo iyi guys eeeee

  • @AlesaBiyala
    @AlesaBiyala Месяц назад

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o Месяц назад

    🎉🎉🎉🎉

  • @abdulkareemsaeed
    @abdulkareemsaeed Месяц назад

    Iwe ambuye akudalitse

  • @tracybennie7783
    @tracybennie7783 Месяц назад

    Koma. Chaka. Chale. Ndichinoncho

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq Месяц назад

    ❤❤❤❤❤

  • @ReginaNyilenda-ug1lf
    @ReginaNyilenda-ug1lf Месяц назад

    Atanyiwa 😂😂ine mukundimalinza tiyeni nazo

  • @LuskaMoses
    @LuskaMoses Месяц назад

    Ntanyiwa osaopa osaopa tiye nazo Ife tilipamboyo

  • @user-tf7yi9fp2u
    @user-tf7yi9fp2u Месяц назад

    Ntanyiwa ndi machine

  • @sandebakali
    @sandebakali Месяц назад +1

    tikhala maso tionela live

  • @user-gi1gh9ry6h
    @user-gi1gh9ry6h Месяц назад

    More ❤❤❤❤❤❤ mtanyiwa😅😅😅

  • @RachealPongolani
    @RachealPongolani Месяц назад

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm Месяц назад

    Ifenso timakukondani bro

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo Месяц назад

    Mudye koma 2025 sadzawina

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo Месяц назад

    Inuyotu mumakwana antanyiwa

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 Месяц назад

    Comryde ifenso timakukondani

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Месяц назад

    Ambuye atithandize

  • @iddikassim
    @iddikassim Месяц назад

    Umakhwana ntanyiwa

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Месяц назад

    Mungoti phee muwonee

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад +3

    Zopusa basi zazii

    • @UseniMailosi
      @UseniMailosi Месяц назад +1

      🐕🐕🐕🐕

    • @bisweckchimphamba8497
      @bisweckchimphamba8497 Месяц назад +1

      Palibe amakutuma kuti uzimvera,

    • @ShamilahSaizi
      @ShamilahSaizi Месяц назад +1

      Ndipo palibe amakugwila pa khosi kut umvere

    • @user-tk6wf2eg4z
      @user-tk6wf2eg4z Месяц назад +1

      Chilungamo kuwawa ine abale

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 Месяц назад +1

      Zopusa wapanga chakwela and his useless government zokupha vice President kuchepaa?

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg Месяц назад +3

    Kkkkkkkkkk iiiiii koditu afa chiimire cause to be honest all Malawians ndife okwiya pazimene zinachitikazi
    Mizimu yakwiyaaaa mtendere saupezaaaaaa ndipo kulibeso kudzalamulira 2025 achokeeeee

  • @HajjiSufiyani
    @HajjiSufiyani Месяц назад

    Mumati imilila AtaNyiwa pitilizani kutikonda. Kapeyu achokepo