iwe ndichisiru osaganiza ndi chikangawa wakoy akupas zingat kut uzilakhula zoduka mutu galu ukuvutikaso chitsiru iwe ubwin wake tonse tikugula zodula limoz
Si Dowa ya genuine iyi. DPP siingaphule kanthu ku Dowa. Ochita kugulidwa awa kuti abebetse DPP. Phuma chipani cha DPP, kuwina sikulongolola-owina 2025 ali phee. You can tell kuti anthu awa nga phuma through their leader's speech. A Mutharika kuyankhula mbwelera yokhayokha ngati kuti ma voters onse ali mmanja mwawo."Dikira madzi apite ndipo uziti ndadala".
@@tasmania527 udolo wake pakupha chilima ndi ena aja ndi uchigawenga mzomwe akukwanisa plus kugwesa kwacha daily, mkuthwa mkamwa kma pa ground ndi 0/10
Chilungamotu chimenechi osaopatu osafooka osatopa kkkk
achewatu amenewo chilungamo kuyenda ngati manzi
Anthu awa ngati saphedwa ndi mwayi chifukwa ndi kwawo kwa chimwendo banda ....muthu amene amakonza ziwembu zonse ku mcp
Mcp ndimbola achuluka ndi anthu ufuna kusilemereza okha osanganizira mavuto awena
Ife tikufuna tidzidya msima kuyambila mamawa,masana,madzulo, usiku imeneo nde D.P.P
chakwera achewa anuwo akukukanani mukti bwanji next year 😂🙌
Ochewatu omeo😊
Zoona,zoona A.P.M wawina kale olo mr chikangawa olo adzabele sizizanukha kanthu adzipita gwape amenei D.P.P oyee!
Woyeeeeee❤❤
Angotula pas bassss
Ochewa anzanga 🙏🙏
Ogogo....shame lazalo
Sakunama amenewa nd akudowa amenewa
Palibe chikukoma analowera kuononga Malawi okondwa ochepa
Professor afa peter muthalika😂
😂😂😂😂
😂😂😅😢
Ife timuvoteraso Chakwera! Dowa yake iti inu munamepo apa! Anthu atatu oti angogulidwa ndiye kumati Dowa ingavotele nkhalamba yosankha mitunduyo
Achewa inu ndi agalu chifukwa mavuto alipanopa sakuwona kuti uyu anavotela mcp tonse tikulila limozi
Tsankho silingapose zomwe aluchita Chakwera ni nyau zinzake. Tsano anthu ali ni ufulu osankhula uyo alufuna. Dziko sila Chakwera ili ayi.
iwe ndichisiru osaganiza ndi chikangawa wakoy akupas zingat kut uzilakhula zoduka mutu galu ukuvutikaso chitsiru iwe ubwin wake tonse tikugula zodula limoz
Inuso inu nde opanda nzerudi
Kutengela kuti ndi ochewa onzanu
Muluvutika or panado muzipatala
Tsankho lipose asùweni akowo opatsa udindo okhaokha
khalabe usasunthe uwone 2025
Poti mudzabela mpake mukukula matako
Iweso uli wekha don't be stupid
Adha awa ndi anzeru akuyankhula zogwira mtima
Si Dowa ya genuine iyi. DPP siingaphule kanthu ku Dowa. Ochita kugulidwa awa kuti abebetse DPP. Phuma chipani cha DPP, kuwina sikulongolola-owina 2025 ali phee. You can tell kuti anthu awa nga phuma through their leader's speech. A Mutharika kuyankhula mbwelera yokhayokha ngati kuti ma voters onse ali mmanja mwawo."Dikira madzi apite ndipo uziti ndadala".
Mot lwe sukuwona mavutowo lne kwanthu ndikasungu Koma sininganene Za chikangawa Kut wapanga chitukuko
@@FrancisMazamba Waboza iwe ukungopanga disguise. Chakwera ndi dolo osati zinazi.
@@tasmania527 udolo wake pakupha chilima ndi ena aja ndi uchigawenga mzomwe akukwanisa plus kugwesa kwacha daily, mkuthwa mkamwa kma pa ground ndi 0/10
Ndi brother wanga uyu from dowa Ndithu Sanagulidwensoi unama zed mmmmm
@MzadziWanga Don't forget kuti munatiphela anthu 20 ku mzuzu, munapha ma Albino, munapha Njaunju, munapha Chasowa. Imfa ya Chilima yinali ngozi chifukwa ndege yinali yakutha ndipo mulibe umboni woti anaphedwa, nde shut up.Nkhanza zanu ndi kuyipa kwanu mumachita kunyada nako ndipo zinali pa mbalambanda.
DPP Moto Kuti buuuu
My vote
Bodza ili, mavuto adalipo kuchokera nthawi ya kamuzu,
Komaso inuwo a Dpp. Nthawi imene mudali boma bwanji wosathetsa mavutowo.
zoonadi akunena bamboyu
Anzawo akugaula nursery pano... Anthu awulesi awa
koma zomwe akuyakhulaz ukuzimveses bwino lomwe chikangawa iwe
Ulesi ndiwe osati
Zagwilizana pati
Mudamuphelanji chilima asatana inu
Amalawi ozindikila kwambiri
kugulidwa kotai koditu zamavuto alipano sikuti munthu ungsmunsmize