Eeeh wachita kutembelera boma lonse andale onse Prophet Mbewe kuti awalange Mulungu

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 июл 2024

Комментарии • 99

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e 13 дней назад +8

    Ndimo mudzina la yesu mau Anu agwile ntchito pa andale okubawa mu dzina la yesu

  • @mthawisakaunda
    @mthawisakaunda 21 час назад

    Amen man of God. We are tired wth that thng we call chakwera

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z 8 дней назад +1

    Only Young president can do better... Coz they can do it in new model...NOT 60'S MODEL

  • @MussahIman-cw1cu
    @MussahIman-cw1cu 13 дней назад +1

    U man of God continue to pray for those bad people to gate pushed from god

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo День назад

    God bless you man of God

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 13 дней назад +1

    Mau owoona mulungu atimenyele nkhondo ameeen

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 13 дней назад

    Amen mau ishiii ziko lathuli ai zikomo akuluakulu kuntunda mavuto okhaokha bsi.

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 13 дней назад +1

    Perfect said 👏 🙌

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 13 дней назад +2

    Ndipo athu atizuzuza yawa sitizaiwala m, pakana kale kale mmm ndipo asatana

  • @PaulKambuzi
    @PaulKambuzi 3 дня назад

    amen aprophert power full

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 13 дней назад +1

    Mulungu wamatembelelo kkkkk mwayamba zibwana ndimulungu ky pot ndi business yanu ndimulungu wanu

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne 12 дней назад

    Tiye prophet awawa mulungu awachose 2025 zikutiwawà .

  • @AlickBaton
    @AlickBaton 13 дней назад +1

    This is 2023,, but only God knows

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 13 дней назад

    Kodi chakwerayu tu bvuto ndi school komanso mtundu komwe akuchokera mmmmmmmm so shame walephera basi 2025 azipita !!

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 13 дней назад

    Very bold.....the only Man of God that have told govt the truth

    • @TheresaKuluwemba
      @TheresaKuluwemba 12 дней назад

      Koma ndipo! Koma nthawi ya APM azibusa ma prophet ansembe palipose kunali kuyakhula zoipa zaboma lija koma pano kuli ziii, palibe akukamba zoipa kapena zabwino za bomali uyuyu ekha basi, ayi zikomo

  • @kennedybanda
    @kennedybanda 13 дней назад +1

    Matenda ake ena mwa iwo ndi misala.

  • @ellenMakoloma
    @ellenMakoloma 9 дней назад

    Amen prophet

  • @PiscaDicksoni
    @PiscaDicksoni 13 дней назад +1

    Amen man of God

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 13 дней назад

    Oooh yes tatopa ndi boma ili please azibusa lowereranipo ndithu timenyereni nkhondo Kuti kumwamba kuseguke tatopa ndikulira amalawi

  • @DanielJuwawo
    @DanielJuwawo День назад

    Amen

  • @julietmussa5103
    @julietmussa5103 12 дней назад

    Alavule ndalama zikenezo in Jesus Name

  • @user-gj8td8pc4d
    @user-gj8td8pc4d 12 дней назад

    Names nkukhala mommo mundalemo.😂😂

  • @MafunaseKamoto
    @MafunaseKamoto 12 дней назад

    Basi man of God ndalamazo andipatsira ine tikabweze komwe zinabedwa...kkkk

  • @user-xe5lb4uf3n
    @user-xe5lb4uf3n 10 дней назад

    Walankhula munthu wa Mulungu

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie 13 дней назад

    Iwe usankhepo chimodzi pakati PA ubusa ndi Der wamva osamphatikinza za mulungu ndi Zadary 😂😂😂

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 13 дней назад +1

    Gen Z is watching

  • @user-pn6ic9yr1t
    @user-pn6ic9yr1t 12 дней назад

    Amen amen

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 13 дней назад

    May God restore our country

  • @Dorah-zl9uf
    @Dorah-zl9uf 13 дней назад

    Amen may God bunish them

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie 13 дней назад

    Koma pamenepo ine kukhosi mweee😂😂😂

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j 13 дней назад

    Mulungu akuwonesa ukulu wake sopano mzimu wa Chilima Uli pakati pa Malawi

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 13 дней назад

    Nkhale Lili LA 2023 akuphempha ndi chimozi mozi tikuyembekezera amipingo ina tinve kunyasidwa kwanu Asilam tiye maduwa

  • @masterchitabwino898
    @masterchitabwino898 11 дней назад

    Kkkkk 2023 izi Aaaa

  • @user-lu8px7td6p
    @user-lu8px7td6p 13 дней назад

    Amen mudzina la yesu

  • @BrianZenengeya
    @BrianZenengeya 13 дней назад

    Yes 100% truth

  • @michaelsakala8884
    @michaelsakala8884 13 дней назад +1

    100% true

  • @user-fb6kh2dk1y
    @user-fb6kh2dk1y 13 дней назад

    we are after message not chaka chakacho sungani inu

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 13 дней назад

    Ameeeeeeeeeeeeeeen

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 13 дней назад

    Ifenso tikupemphera mwachinsinsi ndipo mapemphero athu akutheka. MCP mthawi yanu yatha kale. Ndipo MCP yatheratu. Mark my words.

  • @WisdomMaseko-fi5sv
    @WisdomMaseko-fi5sv 13 дней назад

    May God also punish fake prophets

  • @user-po7zs9zd7u
    @user-po7zs9zd7u 13 дней назад

    Amen amen amen amen 🙏🙏🙏❤️❤️❤️

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 13 дней назад +1

    Tell dem men💯

  • @user-hg2cw1om1p
    @user-hg2cw1om1p 13 дней назад

    ❤❤

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v 13 дней назад

    Osaopa mbewe chilungamo Nena boma lotopesa ili ipondeni mbewe yomweyo

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i 13 дней назад +1

    Izizi ndizakalekale,Kodi chifukwa chani mumabweretsa zinthu zoti ndi zakale?

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 13 дней назад

    Amen zikomo🙏❤️💖

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 13 дней назад

    Paja adanena zoti akantheni

  • @user-rg4du4vu9r
    @user-rg4du4vu9r 13 дней назад

    Anzanuso asanarowe mboma anaringat auzimu ngat inu km anasintha mawanga amarawi osangot amen zirizonse ngat simuziwa mawu bwanji munthu wowopa chauta sankhara busy ndizandare chifukwa kundare kuribe kuopa murungu baibo rimat muthange mwafuna ufumu wake ndipo zonse zizakusatani auzeni zaufumu wakumwamba osat zazikozo ayi panopa amarawi asavoteraso azibusawa ayi asibusa nomwenu ndinu amene mwawononga zikori mawonekedwe achipembezo km mphwnvu yake munaikana kare pezani njira zina zosakira ndarama akuru

  • @DorrahBanda
    @DorrahBanda 13 дней назад

    Amen❤❤

  • @yowasschitsosa5348
    @yowasschitsosa5348 13 дней назад

    Kkkkkk zamanyazi a prophet m'malo molalika zamulungu mwayamba ndale

    • @TiyanjaneMkwate-we8gu
      @TiyanjaneMkwate-we8gu 13 дней назад

      Udzimu umaenda bwino anthu akamakhala umoyo wabwino, kuvutika ndi kupemphera siziyenderan, away akuzuzula nchitidwe omwe andale athu oipawa amapanga pozunza aMalawi kuti zao ziyende, ndikupempheranso kwa Mulungu kuti ndalama akubazo zithere kugula ma kidneys, zaoneneni nkhalamba momwe zikuzunzikira kumiziku yet they were promised alot for them to win.

  • @AminAbbass-xc4qk
    @AminAbbass-xc4qk 13 дней назад

    🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 13 дней назад

    Iweso ndiwa bodza mulungu wake UTI

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 13 дней назад

    Iweee ukubwera anthuwo ndizako

  • @curtisewilliams8784
    @curtisewilliams8784 13 дней назад

    Cant you see that, the video was recorded in 2023? bloggers be serious

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 13 дней назад

    Tell them

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 13 дней назад

    Ameen

  • @MarkManyowa
    @MarkManyowa 13 дней назад

    Amen 😂😂😂

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf 13 дней назад

    Fire abusa

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 13 дней назад

    Yes boma ili ndi lolephera koma zoti uyu ndi fake prophet sizisintha.

  • @kingsleyhopematchaya5184
    @kingsleyhopematchaya5184 13 дней назад

    Simulungu mbewe ndipo tsogolo la muthu sangalidziwe ndindani amewneyu tikusauka chifukwa cha kuba kwa dpp

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 13 дней назад

    Ameen 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 13 дней назад

    Amen😂

  • @ruthkundwe7448
    @ruthkundwe7448 13 дней назад

    😮😮😮😮😂😂😂😂😂

  • @user-nr8oq4tr1i
    @user-nr8oq4tr1i 13 дней назад

    Fake prophet, yang'ana za Mulungu, waisted time

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e 13 дней назад

    Zakale izi akulu

  • @ShentrycChinoko
    @ShentrycChinoko 13 дней назад

    Wabodzi

  • @isaacchiwaula731
    @isaacchiwaula731 13 дней назад

    Aaaa m'busa wanji olowerera zadziko?? Ufumu wamulungu siuli wadziko lapansi baba, onvera awawa palibe chomwe akutsata

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 13 дней назад

      Chitsiru iwe mchifukwa chake mwapha chilima

    • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
      @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 12 дней назад

      NDE ZOTI DZIKO LAPANSI NDI LA ANTHU OIPA ANANENA NDANI,,MULUNGU SANGAOPE KUYANKHULA ZANDALE CHIFUKWA IYEYO NDE MWINI MPHAVU

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 12 дней назад

      Ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 12 дней назад

      @@CHIFUNDOCHINA-lp9lg ndikanakonda Ndikanakhala ndi number yako kut ndikufotokozere zomwe baible limanena pankhani imeneyi chifundo

    • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
      @CHIFUNDOCHINA-lp9lg 9 дней назад

      ASE UTSOGOLERI WACHIPEMBEZO NDI WOYAMBA KUPOSA U PRESIDENT,,DZIKO LAPANSI LIMADUNIKA LIZIYENDERA MALAMULO AMULUNGU,,TIKAWASIRA ASATANA KUT ALAMULIRE ANTHU AMULUNGU SIYIGWIRA

  • @TimothyNkhutembaChirwa
    @TimothyNkhutembaChirwa 13 дней назад

    Amen pastor

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 13 дней назад

    Amen ❤

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 2 дня назад

    God bless you man of God

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef 13 дней назад

    Amen

  • @user-xe5il4cg5d
    @user-xe5il4cg5d 13 дней назад

    Amen prophet

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb 13 дней назад

    Amen amen

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah 13 дней назад

    Ameen

  • @malitajere1609
    @malitajere1609 13 дней назад

    Amen

  • @user-nv7qt1yp7g
    @user-nv7qt1yp7g 13 дней назад

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 13 дней назад

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 13 дней назад

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 13 дней назад

    Amen

  • @user-no2sn1fo1h
    @user-no2sn1fo1h 13 дней назад

    Amen

  • @MaryJefry
    @MaryJefry 13 дней назад

    Amen prophet

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 13 дней назад

    Amen

  • @Twayibu15Chimbama
    @Twayibu15Chimbama 13 дней назад

    Amen