PROPHET DAVID MBEWE WASAMBWAZA OPPOSITION- ndipo wati mukamalimbirana mipando simuzawina

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 1 фев 2025

Комментарии • 101

  • @NarthBestern
    @NarthBestern 2 месяца назад

    Amen papa😍😍😍😍😍

  • @austinharawa720
    @austinharawa720 Год назад +2

    Powerful saying man of God.....

  • @KingsleyWakusa
    @KingsleyWakusa Год назад +3

    Video iyiyi ikamupedze Nakhumwa,,, straight point

  • @MaryRasmussen-mr4zo
    @MaryRasmussen-mr4zo Год назад +1

    Amen
    May God bless you

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Год назад

    Zoona pastor Mbewe akulephera kutsutsa koma akufuna kudzalamulira.chiyembekezero cha anthu ndichotani kwa anthu ngati amenewa.Boma la MCP likutizuza.ndalama zikupezeka ndizoyendera maulendo ake.ndipo mkazi wa Chakwera ndi galu.mzimayi wathundu wanji olephera kudzudzula mamuna wake kuti bambo anthu akuvutika uku.

  • @stanleykaludzu-bm4pm
    @stanleykaludzu-bm4pm Год назад +1

    Very very true Man of God

  • @PreciosNdlovu
    @PreciosNdlovu Год назад

    Prophert Mbewe .izi ndizona zikhazokha anthu mumalawi muno akuvutika kowophya
    malawi alipamoto .kuiguptonso pangono .Mulungu ayendere malawi.Mbava sitikuzifuna .usogoleri wazuza anthu uwu

  • @kennethjere9502
    @kennethjere9502 Год назад

    I agree he is right.

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 Год назад +2

    This is true,
    Opposition Mps and leader of Opposition ali weak kwambili, akungoganiza zautsogoleri

  • @KonkaMonka-ir2ug
    @KonkaMonka-ir2ug Год назад

    You are a great person

  • @innocentliyawo3943
    @innocentliyawo3943 Год назад +1

    The dude is spilling the facts

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 Год назад

    Prophet Mbewe you're right about opposition and what I can see here is that Malawi has no opposition leader and because of weak APM that's why all these things are happening if it was Bakili or late Bingu this wouldn't happened

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 Год назад

    True mr prophet , here in malawi we don't have opposition parties , all of them ndi adyela, even pac nayonso inalowa mbwelela

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Год назад +1

    Ndagwilizana nanu prophet

  • @FlocyMollyGrant
    @FlocyMollyGrant Год назад +1

    This is so true,,,if they are wise enough let them start now,,,it's high time our leaders start seeing this nation that it is for all of us the government and the opposition

  • @IBRAHIMCHIPASULA
    @IBRAHIMCHIPASULA Год назад +1

    God is very Merciful and All_Knower. Almighty God knew that in fact there are no opposition parties in Malawi, then God has brought the hope for poor Malawians hon. Bon Kalindo, the president of the poor Malawians. This is shown by the way the called opposition parties in Malawi are silent while nothing is working in Malawi. Only hon. Bon Kalindo is condemning this bad leadership. May Almighty God bless our president Bon Kalindo and his comrades with long live and strength against the devils sent to destroy our peaceful and beautiful country, Malawi.

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 Год назад +2

    I wish Born Kalindo azatiimilire u president 2025

  • @ronaldchirwa2506
    @ronaldchirwa2506 Год назад +3

    Powerful

  • @chikumbutsotsalangu5511
    @chikumbutsotsalangu5511 Год назад

    Good advice sir

  • @GIFTNAMPINGA
    @GIFTNAMPINGA Год назад +1

    powerful message

  • @WisdomMwitha
    @WisdomMwitha Год назад +1

    This reall prophet David mbewe what he said it's true

  • @lloydmakumba6479
    @lloydmakumba6479 Год назад

    I agree

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq 11 месяцев назад

    Great

  • @AbelKaludzu
    @AbelKaludzu Год назад

    Exactly MoG

  • @AlfredNjoka-n2w
    @AlfredNjoka-n2w Год назад

    He is right

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Год назад +1

    Especially Nankhumwa is busy fighting with APM and he think like it's easy to be a President of Malawi while people are dying with hunger in the hands of Chakwera.

  • @AffectionateDachshund-tz6dk
    @AffectionateDachshund-tz6dk Год назад

    Ndale zapamalawi anthu akutaya nazo mulungu kusatila mdale nconco mulungu akakwiya mudziyankhula zambiri inu anthu odziwa mau amulumgu nanga mukuphatikizilanji ndizachikumja inu ndiye musintha zinthu analipo anzanutu alipo lerowa amayenda bawo kudya usipa pamsika komaso kudya midzimbe ndi anthu komapo amazitcha ku mdiopemphela kom pano zikut tangopitilizani kuuza anthu zanjira yakumwamba bs musapanga ziwiri zandalezi mudana.ndikholo lanu amene ali mulungu

  • @PreciosNdlovu
    @PreciosNdlovu Год назад

    Prophert mbewe abwera poyera mosaopa kuzuzula boma .kusiyana ndi achakwera anabisarila kuti Ndi abusa koma boza lokhalokha .oyitanidwa ndiambili koma osankhidwa ndiochepa .

  • @AlexKaunda-x3p
    @AlexKaunda-x3p Год назад +2

    Nankhumwa ndi wa mcp simuziwa

  • @SquareKandulu-kg3ui
    @SquareKandulu-kg3ui 9 месяцев назад

    Continue 😂

  • @FrancisMazamba
    @FrancisMazamba 6 месяцев назад

    Zoona zake

  • @francomwachandejnr6745
    @francomwachandejnr6745 Год назад

    Very true

  • @tenexchikumba
    @tenexchikumba Год назад

    Sananeso MP wa DPP kut there opposition is doing nothing

  • @sulaimanamiduh5633
    @sulaimanamiduh5633 Год назад

    Mawu amphamvu mr mbewe

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 Год назад

    It will be a very big mistake for people to vote for Nankumwa as a presidential candidate and he's not supposed even to be called Vice President of DPP. That's why DPP will have no future and it's shameful for the party that was strong to finish like that because of selfish people like this

  • @MartinNkhoma-y1b
    @MartinNkhoma-y1b Год назад +1

    Zoona kulibe oppositon kumalalawi kuma aphungu odzikonda ndi adyera osaganizira anthu osauka

  • @proactiveisaacbandah4072
    @proactiveisaacbandah4072 Год назад

    Exactly

  • @AlickChima
    @AlickChima Год назад

    Thus my prophet talking ., Tell them.greedy zombies busy waiting for their turn to loot....sizitheka.

  • @CharlesTambala-zn2bd
    @CharlesTambala-zn2bd Год назад +1

    Things are not okay.... our country looks so pathetic

  • @asiyatujuma5507
    @asiyatujuma5507 Год назад

    ❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 Год назад +1

    Uĺaliki kuchokera palemba lanji m'baibulomo aneneri achinyengo ukatero naweso ukuzipangira kampeni

  • @FrancispChipatula
    @FrancispChipatula 11 месяцев назад

    Kumeneko ndiye kuyankhura

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w Год назад

    Mulungu atisakhile president oopa mulungu

  • @SharomKapenga
    @SharomKapenga Год назад

    This is true

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Год назад

    Za ziii.

  • @victorkaunda8551
    @victorkaunda8551 Год назад

    Wat do u expect wen you put MSCE graduates to deal with crucial matters concerning the economy and country

  • @Ertyvhk
    @Ertyvhk 7 месяцев назад

    Mfondo yabwino kwambiri a prophet

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Год назад

    It's true though.

  • @aminrajab5482
    @aminrajab5482 Год назад +1

    Zooona mbewe

  • @chimwemwechiundira6002
    @chimwemwechiundira6002 Год назад

    Truth

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr Год назад

    Koma zokuti mudziko lamalawi zinthu zikusokonera chifukwa opposition leader ikufooka idzo ndiye zoona opposition iri mbali ya m c p osati anthu ndiye.kusogoloku adzitisokosa muvotere nankhumwa tidziti ndizolondola ?pomwe asakuyimira osauka .😂😂😂😂

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Год назад +1

    Auzeni zoona Ali tondovi kupusa angoti ndwiiii kungoyanganira .

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 Год назад +1

    Chilungamo chimawawa, uyu chilungamo anabadwa nacho

  • @user-frasernamaona14
    @user-frasernamaona14 Год назад +1

    Mawu bwana prophet

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 Год назад +1

    Zowona

  • @stephanchatatahshezi7036
    @stephanchatatahshezi7036 Год назад +1

    Zowona zake,

  • @AnessNezala-jt5fe
    @AnessNezala-jt5fe Год назад +1

    Ndipo mulungu azikuonjezilani masiku ena amen

  • @Kamwachale
    @Kamwachale Год назад

    How can DPP oppose the government that the citizens chose to the best of their knowledge. The citizens said DPP was worse than mcp how then DPP can oppose what the citizens chose as best. Don't accuse DPP because of your wrong casting of your vote, don't push DPP to clean the mess you created on your own, be the solution to your political mess

  • @vusoacquaron9084
    @vusoacquaron9084 Год назад +1

    Vuto atsogoleri anthu saganiza zokodza dziko lathu koma kutupisa mimba zawo

  • @TayeleKumwenda
    @TayeleKumwenda 11 месяцев назад

    Ur prophet or multiparty member

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Год назад +1

    Kaya ndi nneneri onyeli koma akunena chilungamo

  • @EmmanuelThom2-xf6ij
    @EmmanuelThom2-xf6ij Год назад

    Nankhumwa ndi mbuz

  • @MastonStanley
    @MastonStanley 6 месяцев назад

    Kulidandaulila dziko

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Год назад

    Zoonadi man of God

  • @ChristinaSimwaka
    @ChristinaSimwaka 6 месяцев назад

    Sure farther tell opposite

  • @TayeleKumwenda
    @TayeleKumwenda 11 месяцев назад

    Ndiwe cisilu ukunamizira mulungu eti

  • @jeanbotomani9081
    @jeanbotomani9081 Год назад +1

    Mau zosaenda olo

  • @ChifundoBeston
    @ChifundoBeston Год назад +1

    Mneneli wonyenga uyu, mwa uyli mulibe umulungu

    • @lewisbonongwe8518
      @lewisbonongwe8518 Год назад +1

      Kodi zome akunenazi ndi uneneri kapena zochitika

    • @ronaldchirwa2506
      @ronaldchirwa2506 Год назад +1

      Zomwe akulankhulazi ndizonyenga? You must be very stupid citizen

    • @MalizinZinazizi-in4wk
      @MalizinZinazizi-in4wk Год назад +2

      Kkkk Anthu wenanu sidziwa kusiyanitsa zinthu.. apapa sakupanga uneneli apa akunena ZOMWE zikuchitika..kodi M kulakwa kudzudzula pomwe sipalibwino?? Huuuu umbulitu umenewu

    • @chrispartsogolani0928
      @chrispartsogolani0928 Год назад

      Ndipo live this is true man of God

    • @BenjaminKamanga-p8w
      @BenjaminKamanga-p8w Год назад +1

      Munthu wamulungu sayenera kuopa apa ndiye waonesa kuti ndi mtumiki weniweni

  • @isaackaphuka
    @isaackaphuka Год назад

    Zoona

  • @lukainnocent5380
    @lukainnocent5380 Год назад

    mawu koma awa Iwo Ali busy kunyoza chakwera chifukwa akufuna mpando zausatana basi

  • @AleksaWilliams
    @AleksaWilliams Год назад +1

    True

  • @ZioneMkangadzula
    @ZioneMkangadzula Месяц назад

    zoona

  • @raymondchilimba7010
    @raymondchilimba7010 Год назад

    Well said fake prophet....
    This time you nailed it.

  • @khadijailiyasa5315
    @khadijailiyasa5315 Год назад +1

    Awuzeni busy kumangokangana uko

  • @calvinjamal7117
    @calvinjamal7117 Год назад

    Nankhumwa empty head

  • @husseinmoffatt
    @husseinmoffatt Год назад

    Zoonadi dzikoli sililibwinoyi

  • @greychizaka4088
    @greychizaka4088 Год назад

    dzidzudzuleni dzitsirudzi

  • @edwinlerwill6978
    @edwinlerwill6978 Год назад

    Evil people what kind of man of God ?

  • @thondoyaenterprise3795
    @thondoyaenterprise3795 11 месяцев назад

    Dude stay in your lane.
    U clearly shows u know nothing about economy and procurement. Otherwise u should have talk of solutions.

  • @edwinlerwill6978
    @edwinlerwill6978 Год назад +2

    Shut up neneli onyenga uyu

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 6 месяцев назад

    Powerful

  • @evaromeo1897
    @evaromeo1897 Год назад

    True