Tiyankhulireni bwana❤ azimai amasiye sakutipatsa ndrama za.malemu ku Capital hill pano zaka zitatu tikungovutika ndi ana bambo awo anamwalira kalekale koma ndrama zikukanika kutuluka ma demo asalepheleke
Ku Malawi kulibe chifunga choti chingagwetse NDEGE, maiko ena ndege zimayenda muchifunga osati ngati wathu kuno komaso ndege zimatha kuyenda ndi chifunga koma usiku ndiye Boma lingopeleka chifukwa chenicheni basi osati kumatinamiza ngati akunamiza ana Zikomo Bon Kalindo chifukwa cha message yamphavu
Ndipo akanakhala President wa mzeru pofuna kupewa Kuti anthu asamamunene Mr Chikangawa anayenera kuchosa Cabinet yonse imene ikumupasa maganizo opepera . Koma ngati akuyisungabe Cabinet yake yokubayo ndiye kuti Mr Lazarus Macathy Chikangawa ndi Mtsogoleri wa nyansi zonse zikuchitika Mmalawi. You are evil Mr Chakwera and your Cabinet.
Tikufuna Mademo asalephereke please,, Chakwera akulephera kuwauza a Malawi report la Ngozi ya Ndege, ndipo zikuonetsa kuti akudziwapo kanthu za imfa ya anthu 9 aja.
Power full speach chakwera sakuganizira anthu amalawi tikuvutika ndiye ndiye aziti munthu WA reti azipereka misokho ndarama zomwe mukungo mwaza mumisika ndi mumisokhano zachepa ase
Munthu ngati sunalakwe, if you are innocent sungadandaule but when you're guilty nde umapupulumadi ndi kumakwiya.anthu akamayankhula kuti wagwetsa ndenge. God will surely punish him
Powerful message Mr bon kalindo,mukugwila ncthito pomwe ma advicer a president angodya ndalama zamphawi osathandiza president
More 🔥🔥🔥🔥🔥 my president❤❤❤❤❤❤
Powerful speech freedom fighter born kalindo
Power full speach Mr bon kalindo. More fire
Mr dcccccc. Muka wona fumu ikusiya kukapepe maliro kunyumba ya maliro ndikukapepesa malo olakwika muziwe mafumu kumeneko akupezako chuma. Akuziwa kuti kwa marry chilima sakabwerako ndi makobiri.ndichifukwa amapota kumene ndalama sizivuta kuzipeza. Anthu asiya mawu a Mulungu woti munthu adzadya thukuta lake pano aliyese akufuna kudya thukuta lazake. Anthu ena akulemerera ngati wina wagweredwa mavuto ndipamene amapeza mupata wodyerapo. N
President wathu ife osauka ❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Ndipo true aziona sanati😂
And what l believe its that soon apita komwe watsogoza azake kuja trust and Mark my words 💔
✊💪✊ our president ❤❤ we waiting for demonstration bwan
Kalindo the great
Our KING
Mr boooon kalindo mumatiyimilila kwambili ife tili pambuyo panu❤️❤️💪💪💪💪💪
Tilinanu pamoz bwana 💪💪
The DC, imfa ndiyowawa straight up and sakuyenera kupanga zibwana pa issue imeneyo 😢
That's our president speaking on our behalf ❤❤❤
Bon is the best before❤
Koma amalawi tiyeni tidzuke chifukwa chiyani maliro akwina kukapepesa maliro kwina zinayamba zitachitikapo zoterozo,komaso iyeyo akubisa report chifukwa chiyani amalawi akuyenela kudziwa za report
Komatu tikufuna report, lakuchikangawa
❤❤❤❤❤❤ give it 🔥 🔥 🔥
This is time of ng'alulaizeshoni
Inu ndi bwana bon kalindo
Kalindo is a lady? Very talkative
Our Hero Mr born kalindo mumatiimila ife timakukondani
❤ I love you too ❤️
More 🔥🔥🔥 the DC
Bwana bon kalindo
We love you mr Bon kalindo❤❤❤
First person to view
Tiyankhulireni bwana❤ azimai amasiye sakutipatsa ndrama za.malemu ku Capital hill pano zaka zitatu tikungovutika ndi ana bambo awo anamwalira kalekale koma ndrama zikukanika kutuluka ma demo asalepheleke
Sorry ukapitaso Pena amatha kukuuza Kuti utigailako zingati Kuti zituluke changu ndalama zimenezo
Kuswakuswa chilungamo
Kalindo chindere chakufikapo
We love you kalindoooooooooooooo!!!!!!!!!
We love you brother born kalindo
The DC ndi no 1
Umakwana DC
Go ahead the DC.
The DC God bless you
Atukwanidwa zenizeni a dr Chikangawa aziona.
booooooooooooonnnnnnnnnnnn kalindo
Ku Malawi kulibe chifunga choti chingagwetse NDEGE, maiko ena ndege zimayenda muchifunga osati ngati wathu kuno komaso ndege zimatha kuyenda ndi chifunga koma usiku ndiye Boma lingopeleka chifukwa chenicheni basi osati kumatinamiza ngati akunamiza ana
Zikomo Bon Kalindo chifukwa cha message yamphavu
Zoonadi
Chakwela must park and go
sangatuluse lipoti chigawenga chinapha a chilima ndichomwecho chakwera
More fire 🔥 Booooon kalindoooo
Koma pa pension po ndiye mwalasa a DC komaso Pali za P9 ku MRA sakupeleka chiloweleni achakwera mu 2020 mpaka pano.
Ndipo akanakhala President wa mzeru pofuna kupewa Kuti anthu asamamunene Mr Chikangawa anayenera kuchosa Cabinet yonse imene ikumupasa maganizo opepera . Koma ngati akuyisungabe Cabinet yake yokubayo ndiye kuti Mr Lazarus Macathy Chikangawa ndi Mtsogoleri wa nyansi zonse zikuchitika Mmalawi.
You are evil Mr Chakwera and your Cabinet.
Ife alend athu azasamusidwa muzaapasa nyumba ku bomako
💪💪🔥🔥
Zikomo the DC mene zililimu mafuso atha taziwa kuti anachita kukoza simukuona panopa akuvala ma black titedi kkkk eti amachita manyazi
Vumbwe wa munthu chakwera, munthu ungabise report something is wrong apule 😮
Tikufuna Mademo asalephereke please,, Chakwera akulephera kuwauza a Malawi report la Ngozi ya Ndege, ndipo zikuonetsa kuti akudziwapo kanthu za imfa ya anthu 9 aja.
Power full speach chakwera sakuganizira anthu amalawi tikuvutika ndiye ndiye aziti munthu WA reti azipereka misokho ndarama zomwe mukungo mwaza mumisika ndi mumisokhano zachepa ase
😢😢
Munthu ngati sunalakwe, if you are innocent sungadandaule but when you're guilty nde umapupulumadi ndi kumakwiya.anthu akamayankhula kuti wagwetsa ndenge. God will surely punish him
Olo atuluse report anapha vice wake munthu denge kusowa 10 o'clock kukayamba akufuna munthu 5 o'clock zoona
Koma nde afiti afiti eeeeee chonena ndilibe
Anyozedwaditu sanati ndipo aziona
The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC bon kalindo 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Moto kuti ❤❤❤❤
Mbiri yamuipila amene uja
Hahaha umatha the Dc
Mafumu wo akumapita kukapepesa maliro kapena kukalandira ndalama???
Ndarama
Kuchema
😂😂😂😂😂😂second person to view
Ng,alulalaizetion
Ambuyanu
Kodi tifunika ukapepesa kuti , pakati pa chikangawa chakwera olo ku banja ya chilima .
Ndiye muziti anthu ali utukwana .report ituluke
Koma ma VN anthu akumuzi akumamvela
Ai
Iwe ndiwa town????
Kkkk
Komatu mutukwane palibe chomwe mungapindule
Nde ngt palibe chomwe tingapindule nanga akuyakhuliranji mr chikangawayo
Nanga akudandauliranji. Naweso uli wa chikangawa kapena
Tipindula ife ndo bon karindo anaba ndalama za bamboo anga awa za chibalo
Chakwera anaba mumene tikuvutikila kuno inu amangoti muzipereka ndalama kukama mkaka ng'ombe yo wonderful kare
Bon kalindo my president
Kkkkkk the DCccccccc
Bon the DC ndipo uthenga wa ma demo ukhale wakuti atule udindo basi.