Nkhondo Yolimbana Ndi MCP Si Ya APM Ndi Atupele Muluzi Koma Ife A Malawi - D Phiri
HTML-код
- Опубликовано: 13 сен 2024
- On Nyasa VoiceBox, D Phiri says that the battle to get rid of the MCP is not dependent on one particular politician but is a group effort that must be undertaken by all Malawians.
Ku Nyasa VoiceBox, D Phiri wati nkhondo yochotsa chipani cha MCP sikudalira wandale m'modzi koma ndi gulu lomwe Amalawi onse amayenera kuchita.
#malawi
Anthu opanda nzerunu mumkati muone Zina, lero bwa? Osamunamizira APM ndi Atupele Muluzi, anatiuza koma kusamva. Tiyeni nazoni.
Vuto sii Atupele kapena APM ayi..vuto ndife ovota ..2020 anatiudza ndipo anazungulira dziko lonse kuti Ana anga musavotere idzi koma sitinamve .nde mukufuna kuti APM ndi Atupele atani
Amalawi vuto ndiwunkhutukumve APM ndi Atupele ananene lelo wina azibwela pano kunenazopusa boma munapereka ku Chikanga Congress party.
Ndipo di kupusa zedi to blame these people..
Ndizoona don't point them fingers because its malawians who voted for chakwera even themselves they did not vote him its malawians
Zoonadi amene watulisa vedio imeyi yoti APM ndi Atupele ndi odzikonda ndi wopusa kwamniri akuyesa amalawi ndi omweaja a 2019 Amalawi a lero 2024 ndi odxindikira. APM Atupele staya away from Malawi politics until 2025. Osamvera afiti a ku Malawi
Mwalankhula bwino.God bless you
Zowona osalimbana ndi atupele kapena APM zofunazathu ndizimene tikukolola ulemuwanu achimwene apa nde mwandifikapo god bless you always ❤
Pamenepo ndiye wayankhula bro point taken amalawi tokha tinawakana anthu awa 😂😂😂
Paja ananenatu 2020
Good points mumatha broz Zofuna iziiii.. Tidikile 2025 achotse basi olakwa ndamene Ana votera chikangawa 💔💔💔
My brother kulankhula uku kokha may God bless you 🙏 ndiyeno uthenga wanga mmawa uno upite kwa Mbuzi yomwe imalankhula kuti a APM ndi At.M ndi ozikonda mumuuze kuti mapwala ake
Very true, it's our fault APM 2025
Kuganiza mwakuya uku...
For sure brother yr true, ndipo Malawi ndi otengeka ndizithu zopanda pake .chakwela ngat anakwanisa kupha nzake kwa asembules mukuganiza ngat angakhale ndichison ndi munthu.
Ulemu wanu mr d phiri munthu wazeru mulungu akupatseni moyo wautali🇲🇼
Totally agree 100% Malawians we are crazy tnasakha achakwera tiyeni tilimbe nazo bas
Kkkkkkkk anangendedwa Kale awa apume basi
Akunena zoona nkuluyu.
APM ndi atupele ndi ana achepa kwambiri sangalimbane ndi MCP
How did mcp win tel me?
APM ndi Atupele Muluzi wonsewo pamtumbo pawo, nyini zamawo, mkongo wa mawo, sangapange china chili chonse. Atupele Muluzi mbolo yake ya jando sangalhale president wa Malawi. Zapamtumbo basi
I totally disagree with the one accusing APM and Atupele Malawians who voted for MCP are are blind. APM and Atupele are humble leaders .
Kuyankhula kwanzeru ndithu kp it up boss
Zoona bwanawe ameen
Ndie APM wakakamira bwanji pa president nkhondoyi ndi yake basi komanso Atupele ukunenayo paja adalephera ndi u mp omwe kwawo
100% True bro wayankhula facts ndipo anthu mumaganiza 👏👏
Bro mwayankhula za nzeru.
Very true
Zoonazake malu
Very true boss
Correct
Mau achilungamo. Auseni. Oponya voting ndi amene amasankha ntsogoleri
Zoona broz walankhula bwino anthu akafuna kuona kusintha lero ndi zimenezi mabvuto amalawi munachita kufuna. Mwayi mulinawo osinthaso zinthu mu 2025 mukazafuna kupitiriza zizakhala ndi inu
Yes ndipo ana kosamva Andi a tupele ndi a Peter amayankhula koma kosamva ndiye mukubulema anthuwa and ine ndikutukwana amene akuti anthu akuzikonda no don't blaming them you must blame your self
Ddp kapena UDF akareso limosi 2025 inshall allah
Iweyonso nyasi zako zileke
It's true brother
Indeed bro
❤❤❤❤❤❤❤
Sidzingatheke voti yamuthu mozi kuwinisa muthu dzikufunika Ife amalawi tigwilane manja amalawi mcp itipha those tinsamale komaso tichenjele may akulu akoma akagonela kumalawi tasala ndiathu awili apm ndi atupele Basi tikangoaludza away Tanya kumaganiza
Ndipo mwayakhula zoonad bro zofuna za Malawi bas
Ameneyo khansara wa MCPigs amenyedwe kotheratu.
Inu mukulimbana ndichakwela iye akumumenyela nkhondo ni ambuye
Zoonadi mavutowa ndi chisankho chathu vuto si APM kapena Atupele
D phiri mulungu akudalitseni pa mawu anu anthu ena wa kuganiza kumawavuta ndipo mene anatikondela ife apita muthalika mmmm amalawi tinataya udzu omwetamweta
chisilu iwe galu ndi madala ako okalamba wo Malawi siyikufuna zinthu zokutha kale
Kulakhula koma ndi kumeneko me phiri zikomo
That's true
Point bro
Ayi atupele anationetselatu pa chiyambi, kuzikonda kwake atani awuzeni mfumu a malawife kusamva , chilipo apa tigwilizane tichotse manyiwa basi, tisatonse zala awawa, koma ngati udf , dpp, utm, boma
Zoona blz wel speach. and kuvutika tukuvutika ndife .
Thank you my boss audio yanu ndiyovek
Zoonadi tinakana tonkha ndiye lero tisayakhule moipa ndani amene saziwa kuti mcp sichipani chochi votela mavuto tinabwelesa tonkha timavota ndi ife lero zinthu zafika ponunkha ndiye sisatenge peter ndi atupele kukhala anthu ozikonda ai mavuto osewa akubwera chifukwa Cha kusava kwatu ndiye tisayakhule morakwika
Chachitikacho ndichiweruzocha amalawi eniake amavota masana sizokokelanazo ayi anthu akuonaokha Chilungamo musapangilezoipa ngati umadana ndichipani zikuvutani ife sitikuyang'ana chipani koma chitukuko mukaluza muzivomera osamangomenyana nokhanokha palibe amafunakuluza koma mukaluza vomelani
Zoona zokha zokha boss mavuto awa tinazilowetsa tokha
Iwe ndi.munthu wanzeru Apm ndi a tupele ndiosalakwa vuto ndife timafuna kuona zina nanga taona kale zinazo?, ngati apm oyipayo angamalimbane ndi kutsutsa zomwe timkafuna? Poti timkafuna izi. Tiphunzire kulemekeza zomwe tili nazo apm akabweranso tizaziwano ku wapatsa ulemu ndipo sitizanamizidwa ndianthu adyera
Vuto si azisogoreli awa ayi koma thokha ndimen tinasakhir
Ndizoona amalawi sitimachedwa kuiwala timakopeka ndi zinthu zosakhalisa poononga nazo zinthu zomwe zikanatithandiza mavuto tawaonawa takhaulatu tisinyuke tisachitenso masewera anthu omenyera ufulu sakugona siku ndi siku kukulangizani anthu oti muzawabvotere tibvomereze boma lina Lili lonse linali ndi mavuto ake koma izizi zanyanya amalawi timakuuzani kuti ngati simukwanisa kukana zopasidwazo chifukwa cha mabvuto landilani koma muzawabvotere
Izi ndiye ziti?nkhani ya chisankho kumangochi uyu akukamba zina,,,,,kupanda manyazi.Chakwela my vote
Zoonadi brother
Ukunena zoona broo
Congratulations 🎉🎉
Zoona zache siboza ai tooonse ambiri ndiamene tiwachose pampando
Ndichoncho big man
Otiuza analipo Koma kusamva kwanthu mayoooooo
Mzoona mbuyanga mtokha tinaika mcp
Man penapake mukunama ife sitizawavoteranso
Ndipo wachinyitsa chigoli mkumati couche walephera kkkkk koma adha
zowona zake okanika ndife anthu
Kikkkk kodi wakuuzani ndani kuti APM/Atupele atsogolele nkhondo??? Kubwera ena tiyeni tipemphere otherwise pair imeneyi sangayithe MCP zinakanika kaletu paja....
Zoonad ife anthu awa tinawada nde lero tikwafunaso
Palibe chanzeru walankhulapo apa
Wanena za nzelu ase
Ukunama iweyo, mboro yako. Who is Atupele Muluzi
Ma scandal a Chakwera
1) Atangolowa kumene anapita ku nsonkhano wa virtual koma iyeyo anapitakobe ndi anthu 10. Chi hall chonse analimo yekha ndi mwana wake; ankolo ake; mpongozi wake
2) Anakagula fetereza ku butchery
3) Analemba ntchito munthu oti apapanga kale retire mthawi ya Kamuzu ku immigration
4) Anapha Chilima, Shanir, Sidik Mia, Raph Kasambala
5) Anamanga Chizuma. Kenako anakhazikitsa commission of enquiry yomwe inapeza kuti Chizuma ndi olakwa
6) Anagwetsa kwacha ndi 100%
:
:
Mbambande
Mukunenadi zoonadi
Awaso ndi achisilu kusephana ndi nkhani
Koma ndizoona atupele komanso DPP akugona iya
APM odzikonda kwambr kaka pa udindo
Chakwera ali pa 3rd Term ku MCP pomwe APM ali pa second term. Mitu yanu simaganiza musanaphwise ndi pakamwa panu.
Chakwera mthawi yake ku MCPigs inatha kalekale koma akufuna kukhala president wa muyaya.
Mcp kuwina ku mangochi?ndafabwatu ine
Ndadabwatu
Palibepo chamzeru apa!!
Za zii!!!!!!!
Chamnzeru koma kugwetsa kwacha ndi kugawa ndalama mmisokhano. Pamtumbo panu a MCP afiti nonse
Zoonad ndithu