FELIX NJAWALA WASAMBWANZA CHIPANI CHA MCP NDIPO WASIMIKIZADI KUTI ANATULUKA MU TONSE ALLIANCE

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 17 окт 2024

Комментарии • 120

  • @violetpotani
    @violetpotani 2 месяца назад +14

    Munasowatu Mr Njawala.. Welcome back

  • @RafickOsama-k2r
    @RafickOsama-k2r 15 дней назад

    Your welcome to Malawi 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 🇲🇼

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 2 месяца назад +11

    Exactly mr njawala u ar true man osati uyu akumuti manganya

  • @deniskondani1305
    @deniskondani1305 2 месяца назад

    Felix ndi more fire

  • @afritouch4660
    @afritouch4660 2 месяца назад +3

    APA NDAWONADI KUTI UTM INAKALU YAMPHAMVU.. Ndubwera konko bola osamphwekensaso..!! More fire 🔥 UTM

  • @MuyaoComedies
    @MuyaoComedies 2 месяца назад +3

    I'm following, Salam alaikum

  • @BeatriceProfessor
    @BeatriceProfessor 2 месяца назад +1

    Tell them ❤❤❤

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 2 месяца назад

    More fire Njawala

  • @sesfikileshop7344
    @sesfikileshop7344 2 месяца назад

    Felix Njawala my man

  • @CarolynMtegha
    @CarolynMtegha 2 месяца назад

    Good speech Felix Njawala.

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 2 месяца назад +1

    Madam kaliyati for President ❤❤❤

  • @BrianNowa
    @BrianNowa 2 месяца назад +1

    Please akulu akulu a UTM takhaliranani pansi pasakhale kugawanika mmachitidwe together we can, pasamapezeke Ena odzipatula, pakhale mtsogoleri yemwe adzibwsletsa umodzi ngati mmene SKC amachitila, SKC adali munthu odziwa zomwe akuchita komaso zokomera aliyese, kulibwino kukhalirana pansi kukambilana kusiyana mkumanenana ku ground
    Munthu olalata kwambiri samakhala ndi mphavu, kupita pa ground mkumakalankhula za awo ndi awo sizithandiza chipani koma kuwauza wanthu pomwe muli ndi komwe mukupita ndi zomwe mukufuna kukachita, pewani a Utiko okhala pazenera ooneka ngati Ali nanu koma mkati mwawo Ali kwina, samalani ndi anthu omwe akulowa posatengera mbiri yawo,

  • @RodneySupply-tx3ul
    @RodneySupply-tx3ul 2 месяца назад +7

    Elder my brother ndi zoona zedi mwayankhula and keep it up osaopa

  • @modestamhango7737
    @modestamhango7737 2 месяца назад

    Powerful speech. 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 2 месяца назад +3

    Njawala motooooooooo!!❤

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 2 месяца назад +3

    Anthu ndiomwe amuphetsa Chilima chifukwa iyeyu saamafuna MCP

  • @FrancisMazamba
    @FrancisMazamba 2 месяца назад

    Njawala keep it up mulungu ankhale nawe

  • @AgnessKavalo
    @AgnessKavalo 2 месяца назад

    Kuchotsa mboraaaahhh imene ili MCP 😂😂😂😂😂😂

  • @doreendzimuuzani7180
    @doreendzimuuzani7180 2 месяца назад

    Chilima is still living through his people ❤

  • @isabelmartin7567
    @isabelmartin7567 2 месяца назад

    UTM on🔥🔥🔥🔥❤❤❤

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 месяца назад

    Bomaw ilooo my vote

  • @CathyYobe
    @CathyYobe 2 месяца назад +1

    Utm more fire

  • @NazaniNoah
    @NazaniNoah 2 месяца назад

    Mudalitu limodzi lero muyikana poyera ok,oh!zikomo yenkhova poti inu nokha simukhumudwitsa

  • @EleniJames-rc3ot
    @EleniJames-rc3ot 2 месяца назад

    Mjawala ndimakunyadilani pamodzi mayi kaliyati ndi onse a utm mulandile ulemu wanu 2025 mavoto aku utm

  • @SamuelJoseGaviteni
    @SamuelJoseGaviteni 2 месяца назад +6

    Dr chilima wasiya chipatso ana afundo

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 2 месяца назад +2

    I love u mr njawala

  • @jahmanmakwinja-ef7zn
    @jahmanmakwinja-ef7zn 2 месяца назад

    Words❤

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 месяца назад

    Zikomo Felex njawara kumeneko ndiye kuyankhula tikuziwa zimakuwawani nafeso zimatiwawa

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 2 месяца назад +2

    Zoona zoona Mr njawala auzeniiiii

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 месяца назад

    Zoona zoona

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 месяца назад +5

    Felix kumeneko ndiye kubwela

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 2 месяца назад +1

    Njawala ,,Fredo ndi Kaliati tikulimba mtima

  • @DynessMsiska
    @DynessMsiska 2 месяца назад

    Moto kuti 🔥🔥

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu 2 месяца назад +1

    Tinkakuuzani ife kuti sapita kawiri, inu munkachita makani lero ndi izi

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 2 месяца назад

    Chimene ndinapeza ine ndichakut Chilima uja was bigger than UTM itself.

  • @DENSONZULU
    @DENSONZULU 2 месяца назад

    ❤❤❤ UTM 🔥

  • @nelsonkajawo5176
    @nelsonkajawo5176 2 месяца назад

    😂😂😂😂 awa palibe cha nzeru anganene ndakayikanso ngati ali ndi ma followers

  • @ewn-mc6jv
    @ewn-mc6jv 2 месяца назад +1

    UTM more fire.

  • @AlexSamalan
    @AlexSamalan 2 месяца назад

    ❤❤ one love

  • @MakawaBenjamin
    @MakawaBenjamin 2 месяца назад

    Akumanga chakwera

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 месяца назад

    Mkango ukafa,ana ake sangaleledwe ndi fisi tanthauzo monga ife ana autm kholo lathu mmene lidafera (SKC)mcp singatisunge ndiye tosefe itimenza.

  • @FatimaLuwembe
    @FatimaLuwembe 2 месяца назад

    Welco😊me❤❤

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 2 месяца назад

    Koma mwanena miyambi yamphamvu Felex chilima adakuphuzisadi eti kkkk

  • @Biath-m4b
    @Biath-m4b 2 месяца назад

    Gwilanani manja a UTM ine vote yanga ndzakupatsan, manganya ndi oipa ndpo waonekelatu kuipa kwake sakudzwika mbali

  • @AustinMhone-r3s
    @AustinMhone-r3s 2 месяца назад

    MCP Chipani chankhaza kwambiri don't make alliance with them again.

  • @StalloneButao
    @StalloneButao 2 месяца назад

    Awa ndi adolo

  • @TrizaGeorge-q8w
    @TrizaGeorge-q8w 2 месяца назад +3

    Ndipo ndizoonadi abale mulungu ativa kulila kwathu ndithu

  • @PETERSINKADZIWA
    @PETERSINKADZIWA 2 месяца назад +1

    Kuswa kuswa basi. Emusipi No chance

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 2 месяца назад

    Mwini wake wa miyambi anapita inuyo simungaikwanitse pangani fundo zenizeni

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 2 месяца назад

    Uku ndiye kuyankhula osaopa.chiuzeni chilungamo chipani chakupha ndi chakupha basi fisi sasintha ndi fisi basi

  • @GraceLobart
    @GraceLobart 2 месяца назад

    🎉🎉🎉🎉🎉 yomweyoooo❤

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga1781 2 месяца назад

    Ndiye mwabweretsa Kabambe kuti akupititseni ku DPP😢

  • @brownodalla
    @brownodalla 2 месяца назад

    kuthana ndi ululu wa njuchi ndikuchotsa mbola

  • @aggiemlotha1208
    @aggiemlotha1208 2 месяца назад +2

    Chipani chapa FB😂

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire 2 месяца назад

    Inde inde ichotseni mbolayo

  • @JamesChiphwanya-m4v
    @JamesChiphwanya-m4v 2 месяца назад

    Inu a UTM musafooke chifukwa a MCP nawoso anayamba pang,ono pang,ono sanafikile kutenga boma inutso pachedwe pasachedwe muzalowa boma

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 2 месяца назад +2

    😂😂😂😂😂 koma miyambi yabwino bwanjiii?❤❤

  • @violetkamvanthupi2443
    @violetkamvanthupi2443 2 месяца назад

    Izi ndi zoona

  • @TanazioUziyele
    @TanazioUziyele 2 месяца назад +2

    Aaaa chilima kulibe pangani fundo zanu ajawala

  • @MacfelsonMunthali
    @MacfelsonMunthali 2 месяца назад

    Last kicks of the dying horse,umaliro wachipani

  • @elsontmsukwa4356
    @elsontmsukwa4356 2 месяца назад +1

    Uthenga ogwira mtima 🙏🙏

  • @Chikumbuso-l5m
    @Chikumbuso-l5m 2 месяца назад

    Wayakhula bwino tichose chakwela

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo 2 месяца назад

    Ndiye munalephera bwanji kumusitha chakwalawo poti mwati inu mumasitha

  • @FelistasNkasalaMakumbo
    @FelistasNkasalaMakumbo 2 месяца назад +1

    UTM in my blood

  • @MaryChipeta-y4l
    @MaryChipeta-y4l 2 месяца назад

    Mfundoles Udali kuti wabodza iwe

  • @ShurahbilMakiyi
    @ShurahbilMakiyi 2 месяца назад

    Sindimaganiza kut UTM yatha koma mmmmm❤❤

  • @SamzyTimechisaleh
    @SamzyTimechisaleh 2 месяца назад

    ❤❤

  • @AnaLourencokan
    @AnaLourencokan Месяц назад

    Mwapilila

  • @MpapiParadise
    @MpapiParadise 2 месяца назад

    Kkkk awa angomataya nthawi kachipani aka plus ka aford sazalamulilapo boma ai

  • @peterchiutsi
    @peterchiutsi 2 месяца назад

    Guys chipanichi timachikonda koma stop zomangoti chilima chilimazi Mukumatiwawisa mtima

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 2 месяца назад +4

    Kuyankhula chilingamo kulifela dziko mulungu akutetezele

  • @IsaacAmiyele
    @IsaacAmiyele 2 месяца назад

    Kd guys manganya ndiutiyo paja😢😢😮😮

  • @elvisnjoka8428
    @elvisnjoka8428 2 месяца назад +1

    Mudyelatu dzina la malemu hahaha😅

  • @MatthewsJohn-kv8fj
    @MatthewsJohn-kv8fj 2 месяца назад +1

    Boza munali nose atose alliance mumanga nose musathawe inu a utm palibe chanzeru apo ife tikufuna Dpp ndiyimene inakwarisa zodya katatu inu alliance mwalowesa njala mziko nd umphawi oopya bon kalindo president wa Dpp

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 месяца назад

      Mmm musova inu simumaona ndeu zimachitika zija hiyaaa fundo zanu ndi ziphwasula lembani zina ndani yemwe samaona kuti anthu sakugwirizana??

  • @MartinMajola
    @MartinMajola 10 дней назад

    Jawala moto ku buuu

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 2 месяца назад

    Kutuluka m'boma kupanga campaign kufuna kulowaso m'boma mukuzitendetsa bwanji kodi ana amasiye inu kufuna undunu kokhakokhako kkkkk nkhope zake zimenezo anjawala mukhale nduna yamalawi aaas pitani ku dpp komko mwaiwalaso muja dpp onazizira chilimamu kathetseni kachipani kothaithako

  • @AlexanderYovatiKhumalo
    @AlexanderYovatiKhumalo 2 месяца назад +2

    Tiyesetse kuzolowera kulankhula zodzetsa mtendere .

  • @SafariBvumbwe
    @SafariBvumbwe 2 месяца назад

    Koma ichi chikulakhula mr njawala

  • @PatrickFicklem
    @PatrickFicklem 2 месяца назад +1

    Za ziiiiiiiii

  • @zutamgala
    @zutamgala 2 месяца назад +2

    Alibe fundo uyu

  • @TanazioUziyele
    @TanazioUziyele 2 месяца назад +1

    Mukukamba zachitukuko mwapanga zotani inu anjawala zaziiiii!!

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 месяца назад

      Chakwera wakoyo wapanga chani sikungopha Chilima basi

  • @samuelkachimphula7278
    @samuelkachimphula7278 2 месяца назад +1

    Awa ndachitsiru

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 месяца назад +1

      Chitsiru ndiweyo nd Chakwera okupha Chilima uja

  • @EmmanuelChirwa-z3n
    @EmmanuelChirwa-z3n 2 месяца назад

    Ana inu mwachepa MCP boma mpaka mpaka 😂😂

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 месяца назад

      Mwana Wa njoka iwe zachikale zimenezo anthu ake anapita ndi Kamuzu

  • @kingsleyChisenga-i8g
    @kingsleyChisenga-i8g 2 месяца назад +1

    Pja zimathera pa media pompa zosaopsa ana kulira ndi mkodzo

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d 2 месяца назад

      Pamtumbo panu inu achitsiru mulibe mzeru mkomweso apa

  • @WitnessPhiri-zr9uf
    @WitnessPhiri-zr9uf 2 месяца назад

    Wayankhula wakuva wava mulungu aliko ayankha ma pemphelo athu

  • @ElsonNsowoya
    @ElsonNsowoya 2 месяца назад

    Mawu

  • @patricksamson4852
    @patricksamson4852 2 месяца назад +1

    Uyu akukwanira pa utsogoleri

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc 2 месяца назад

    Oh yes 😂😂😂😂, nthawi yakwana.

  • @ShillahChisi
    @ShillahChisi 2 месяца назад

    UTM moto

  • @PatrickSomanje
    @PatrickSomanje 2 месяца назад +5

    Osati 1995 yokha komaso amalawi ambili timakonda chilima

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 2 месяца назад

    MCP chipani cha Kupha aaa, Chakwera Criminal,usi Yudasi adagulisa Chilima aa, Chakwera wazi Wanda aa, Wanthu wopanda manyazi Ndi mzeru u fake pastor

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 2 месяца назад +1

    Kodi muloza chiyani zimene mwapanga chitukuko chake chilikuti anjawala inu 😂😂😂😂😂😂

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 2 месяца назад +1

      Ndalama boma lawapatsa zopangira?

    • @SafariBvumbwe
      @SafariBvumbwe 2 месяца назад +1

      Mmmmmmm inu umbuli chani utm yinalowapo m'boma kkkkkkkk uziganiza kawiri usananene

    • @IssacMateyo
      @IssacMateyo 2 месяца назад

      MBatata iwe choka apa ana ama 2000 sauzande inu sanagwinetu akufunika apiteso kwina akapangeso alayasi Ina zazi

    • @temwekamlenje4358
      @temwekamlenje4358 2 месяца назад

      @@SafariBvumbwe umbuli otengera kwa inu mmesa

  • @HopesonButao
    @HopesonButao 2 месяца назад

    Koma muli fundo umu

  • @blessingsmangulama8442
    @blessingsmangulama8442 2 месяца назад +1

    lozani zanu ife tiwone. 🤕

  • @tracybennie7783
    @tracybennie7783 2 месяца назад

    Mulungu. Ali. Ndi. Chidwi. Koma so. Akuyona

  • @SophieLupiya
    @SophieLupiya Месяц назад

    😂

  • @SamuelJoseGaviteni
    @SamuelJoseGaviteni 2 месяца назад

    Osafoka

  • @FranksonKennethChipande
    @FranksonKennethChipande 2 месяца назад

    Kodi Mr Njawala campaign yanu izikhala ya Chilima???? Pangani ndale za smart.Musiyeni Chilima apume mumntendere

  • @aggiemlotha1208
    @aggiemlotha1208 2 месяца назад

    You cannot fulfil the idea of someone... chilima was best but not you maguy

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 месяца назад

    Bomaw ilooo my vote