I can say bravo to the directors of security for both parties of MCP and DPP of what happened in Mzuzu, that was true exercise of a good Democracy. Let peace reigns this is nice. Zikhale choncho Ku madistrict onse especially South and Central regions Ma campaign akhale aufulu. Political tolerance a way to go.👏👏
Ku Mzuzu kuli anthu ozindikira zimenezi ku Lilongwe sizingatheke and always pamakhala special team ya ziwawa so amadutsanawa zaziwawa sizimawakhudzudza.Alipo ma baunsa amene amayenda ndi zikwanje aja
Ma top positions should not be appointed by the president but should be appointed through parliament like mec chairs, inspector genal , nrb chairs not by the president because president belongs to a certain political party.
It always pains me when we Chewa tribe are taken like fools or all mcp funs. Some Chewaz are exceptional. TTV big up!! Osagawa ma sweet no!! We need leaders who love our Malawi through right decisions and good governance.
Tipex yili ndi zolinga ziwili. Kwa oipa kubera. Kwa olungama kukhozera pomwe paonongeka. Koma cholinga chenicheni ndi kukhodzera pomwe pa wonongeka. Pa nthawi yija anali kukodza momwe m'naonongeka
Kmanso mmene mwayamikila ma supporters a MCP ndi DPP apangira liwudzeninso bola la MCP kuti kalembedwa ka ma ID zikhalenso chimodzmodzi ma boma onse mMalawi muno
Kosdi zoti ndege idafika ku mzuzu amamvana ndichani kuti ndege izathele? Nanaga mawu amenewo ku control alipo ngati Mundege mudalibe box ,,,yaku control ilikuti sound
Kodi imu mesa a ndevu zamwayi milati simutenga information ya social media mde za kumangidwa kwa mtambo munazitenga kuti? Inuyo mukudziwa kuti imali plan ya mvp yomwe imafuna kuipitsa mbiri ya dpp bwanji simukunena?
If the government wanted a fair and transparent election they could have reappointed Mr Chifundo Kachali because he did the last election religiously. But because the current government is aware that they can not win without kubela that's a Ntalimanja was appointed.
Tisayiwale koma kuti Chakwera was attacked in Mzuzu pa Katoto pompo when MCP was an opposition party. Ku Karonga was almost a no go zone area mpaka was nicknamed Bengazi for its terror nthawi ya DPP. Ndiye Northern Region is not as a holy region as is being speculated.
Achewa ake ati Ali ndi dziko mwana wahule iwe, uku sindiko kubweresa chisokonezo kumenek mmalawi muli mitundu yambirimbiri mchewao wapambana chani kt dziko likakhale la achewa kupusa basi kuzolowera kumangogwiritsidwa ntchito ndi andale kt muzikhapa azanu in the name of mitundu
Well speaking men, chikangawa mwamuyankhula koma samamva za wanthu
I can say bravo to the directors of security for both parties of MCP and DPP of what happened in Mzuzu, that was true exercise of a good Democracy. Let peace reigns this is nice. Zikhale choncho Ku madistrict onse especially South and Central regions Ma campaign akhale aufulu. Political tolerance a way to go.👏👏
Ku Mzuzu kuli anthu ozindikira zimenezi ku Lilongwe sizingatheke and always pamakhala special team ya ziwawa so amadutsanawa zaziwawa sizimawakhudzudza.Alipo ma baunsa amene amayenda ndi zikwanje aja
Good idea times yendani mudziwe zoona ndazikonda❤
Ku mzuzu ose ndi a DPP awo mukuona ndi amodzi ena angopita ku mcp kufuna ndalama koma vote yawo ndiya Dpp
Hmmmm ili nde bodza ili
𝐞𝐲𝐚 𝐱𝐨𝐨𝐧𝐚 𝐚𝐥𝐨𝐧𝐝𝐚𝐤𝐨 𝐧𝐝𝐚𝐥𝐚𝐦𝐚
Bola MCP DPP ayi tu kumpoto kuno
Well done guys mumalankhula chilungamo keep it up
Kungong'alura zilungamo pwiiiiiiiiiii!
Kuyankhula kofunira zabwino dziko lanu, zikomo.
I could be much impressed if all sensitive positions in the country were approved by a parliamentary commission where all parties are involved .
Amadanitsa anthu ndi ma politicians. Zinachitika ku mzuzu ndizabwino
Congratulations 🎉 Northern region this is what we call democracy
In that commission of enquiry you should also include some of Chikangawa villagers please anthu akumeneku Aliso ndimau komaso umboni wabwino
Pasakhale ndipo pasapezeke ntundu wa anthu ndi umodzi omwe odziona kuti ndiye oyenera kutsogolera dziko la Malawi .
guys yehova akusungeni pobisika mwaima pa chilungamo mokonda dziko lanu mosatengela mbali pitilizani
Bravo Times TV continue kuyima pachilungamo
North is special
Ma top positions should not be appointed by the president but should be appointed through parliament like mec chairs, inspector genal , nrb chairs not by the president because president belongs to a certain political party.
It always pains me when we Chewa tribe are taken like fools or all mcp funs. Some Chewaz are exceptional. TTV big up!! Osagawa ma sweet no!! We need leaders who love our Malawi through right decisions and good governance.
Nice speech with very good logic
Kachali is a gentleman ❤
Tipex yili ndi zolinga ziwili.
Kwa oipa kubera.
Kwa olungama kukhozera pomwe paonongeka.
Koma cholinga chenicheni ndi kukhodzera pomwe pa wonongeka.
Pa nthawi yija anali kukodza momwe m'naonongeka
😂😂😂😂😂 guys mwathira nchenga mumpunga wagulu
Apapa sungadyeke olo kumezanso ayi😂😂🎉
Waiting for them in southwest and 😊😊
Dpp yokhayokha iyi agendana bwanji awo akungopita kukatengako ndalama basi
Gentlemen,khalani serious munkhanizi.Mwina chifukwa mulibe Brain.
Mukuonjeza kutseka kwambiri.
Powerful massage
Ayitanise ndithu aaa asazembe
We can say mzuzu is the most civilized city.
It was nice indeed yoooh..😊😊
Chigawo chapakati sangapamge zimenedzi kwanyawu kumene kuja zitsilu za anthu
Ndipo sukunama,mbuli za anthu
Congratulations 🎉 wana wakukaya
Nice speech ❤❤❤
Kmanso mmene mwayamikila ma supporters a MCP ndi DPP apangira liwudzeninso bola la MCP kuti kalembedwa ka ma ID zikhalenso chimodzmodzi ma boma onse mMalawi muno
Very good
Yah Kung,alula
Amai aja ananena choncho chifukwa Mcp ndi imene imayambitsa za chiwembu ndinkona ananena kuti Mcp isadzapangitse ku phalombe
Koma nde kung'aluratu no mantra times kip it up
💓💓♥️♥️💪
Mayi Yolamu akugwilitsidwa ntchito ndi Chakwera yemweyoi nothing can change as mcp they are commanding Malawi police to favour them
👋👋 kuyakhula komatu uku
ine ndi chewa koma mawu oti dziko ndilachewa nde mmm musasalalkhule wangokhala kuti mtsogoleli uyu ndi onyasa mtima ndipo sakukhalaso pampando
Achita manyazi aDpp nthawi zonse kuyipaka mbiri zoipa MCP anthu akuonetsanitu.
Kodi zikutheka kubela masankho? Ndizowina tipex 2019 MRs jean assah Tipex
Kkkk Koma anthu Inu pulizi 😂😂😂😂😂😂
Kwathukuno kummwela sitingalole Kuti MCP tidusane ndimagazi amenewo
I think ikhale Dpp yomweyo zinazi ndizakupha, Kuba .chomwe tikudikira ife Peter akangolowa Ayesetse Anthu amenewa amangidwe basi
Km kumalawi kuli ntchito eeeesh ai zikom
Enafe tinapitila kukapeza 2 pin yandiwo koma ife tikavotela dpp
Palibe wandale amene azakufere iwe mpanda dzina wakunchira okonda chipani ngati cha mnyumba mwako. Support a party responsibly.
Umu nde asambwazadi
Kusekedwa ndi kutsekedwa ndi zinthu ziwiri zosiyana .
Kosdi zoti ndege idafika ku mzuzu amamvana ndichani kuti ndege izathele? Nanaga mawu amenewo ku control alipo ngati Mundege mudalibe box ,,,yaku control ilikuti sound
Ndikuona ngati malamulo adziko amakhwila tchito kumpoto kokha, chifukwa chake mmaboma Ena ake kumakhala chikulilano
Ine ndimawayamika anthu aku north amakondana
Ndazikonda kwambili zimenez
Week ya mawa abishop azakhaleposo
Kodi imu mesa a ndevu zamwayi milati simutenga information ya social media mde za kumangidwa kwa mtambo munazitenga kuti? Inuyo mukudziwa kuti imali plan ya mvp yomwe imafuna kuipitsa mbiri ya dpp bwanji simukunena?
Kumpoto amantha
Mmmh mukudziwa zomwe akuchita kuseriku awa asakupusitseni ndithu 😂
Zmukamanyoza mudziyamba kuon kut chatsitsa dzaye nchani kut njobvu ithyoke nyanga. Shhaaaaa abale
Dpp ndidye obera zisankho. Only dpp and their team b utm amakamba za chiavhine.
Onsewa akuzavotera chipani chimodzi,alipo akudyeredwa apapa.akudziwana. sizingatheke kungodusana kumalawi kuno.kkkkkk ku mpoto kuli atambwari😂
Kumpoto kuli anthu ozindikila kuti ndale zisawadanitse.
Chiripo akubisa anthu akuphawa anapha chilima ndi anzake
Mpaka ena ayedzedwe 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Ife si akumwera okonda ziwawa kapena a pakati
Amachita ziwawa ndi agule Aku lilonnge
Ndinu amanyi nosenu kuli pitala kunalibe nkhaza ? Ndinu zitsilu kwambili mcp singapange naw zaugogo ai
Hahaha 😅😅😅 yabayatu mwana wa njoka iwe ndye uphulika chfukwa simunat achikangawa party tikukhwekhwezani asatana inu
Chikangawa ichooo😅😅😅
Northern Region ndi anthu ozindikira sapanganawo zopepera
Koma akumanyegererabetu kuwatengera ku china kodi tiwakhulupilire bwanji anyamata wa
Boma sitikusintha mwayambakale kulira
Kod a bishop aja sadzabweraso ??ine amandsangalasa akamang'alula 😂
Anyamatawa mpaka uniform ku ntchito
Kuyankhula kopusa achewa zikoli ndamene amaliwonga
Kodi ukakwarila azimayi awili akadwala mozi kumawula ungapitise mzakeyo ?
If the government wanted a fair and transparent election they could have reappointed Mr Chifundo Kachali because he did the last election religiously. But because the current government is aware that they can not win without kubela that's a Ntalimanja was appointed.
This is northern region, it'll never happen in central and southern region
Tisayiwale koma kuti Chakwera was attacked in Mzuzu pa Katoto pompo when MCP was an opposition party. Ku Karonga was almost a no go zone area mpaka was nicknamed Bengazi for its terror nthawi ya DPP. Ndiye Northern Region is not as a holy region as is being speculated.
😂😂😂😂😂😂😂 kung'alula
Vuto samamvatu awa mmm
Ku mpoto kuli anthu abwino okha okhatu
Koma yah
Anthu a kumpoto ndiozindikira
Analipo azako akati nawo amuyaya anampita kut zaziiiiii
Alinse voti ilimuntima komachipani chamcp mmmmmm. Chopanda chisoni
Koma. Thawi. Ya. Piter. Kunalibe. Khanza
Chakwela ndi galu wa muthu sazatheka satanic wamagazi anapha zake chilima nyan amene uja
Kudanitsa amalawi basi
Pankuku
Zitsilu zili ku mmwela agalu eni eni mbuli mbalame za chabe chabe ,dziko ili ndi la achewa ndipo lidzakhala la achewa mpaka muyaya
Achewa ake ati Ali ndi dziko mwana wahule iwe, uku sindiko kubweresa chisokonezo kumenek mmalawi muli mitundu yambirimbiri mchewao wapambana chani kt dziko likakhale la achewa kupusa basi kuzolowera kumangogwiritsidwa ntchito ndi andale kt muzikhapa azanu in the name of mitundu
@MzadziWanga mukafuna kunyoza muzinyoza munthu osati mtundu wa anthu chifukwa mutation achewa mumanena aliyese ndiye zimatinyasa mchifukwa chake tikuti alomwe nonsense ndinu agalu kuphatikiza ayao ndinu zitsilu ndipo boma simudzaliwinaso agalu ,inu osamadabwa kuti chiyankhulidwe chathu chachikulu m'dziko muno ndi chichewa agalu mbalame dziko ndi la achewa ndipo tikupanani munya muona
@@JohnMalupiandiwe munthu omvetsa chisoni kwambiri.