Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
Koma Mai kaliyati ndi kagulu kanu choonde nvelani kulira kwa anthu ngati ku UTM kuli anthu olimba nde ndinuyo mumakhala chifupi ndi Chilima musakomedwe ndi ndalama mukwiitsa anthu ochuluka nthawi yatha kale iyi musanvere MCP kukunyengeleleni ndi ndalama misozi ili manso ndithu mutenga tsoka
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
Bon kalindo amalankhula zoona zokhazokha koma anthufe timangoti ndi wama comedy let's support him as malawians
Wamisala anaona nkhondo,,lero Bon kalindo mukumuyamikila koma mmene munkamunyozela siizi😂😂😂😂
Thanks sir for ur update
Kalindo amatha kwambili❤
Your the best the DC bon kalindo❤
Ati amakutengan ngat manyi😂😂😂😂 chi booooniiiiii kalindoooo
Kuyankhula mopanda mantha ngati wakhalira mfuti Bon kalindo 😮😮
Ndpo inu
Uyu ndiye activits yemwe timamudziwa, Bon kalindooooooo!! Mwana owopsa kwambiri.
Uyu ndiye ❤
Yomweyo fadaa🎉
God bless you Kalindo
Umakwana
Good advice sir.
Zikomo bwana DC UTM yitulukedi kumeneko iyime pa yokha basi
Born kalindo🔥🔥🔥🎷🎷
Always your the best all the time mr president Bonie Kalindo
Good advise Mr born kalindo thank you 😅
Mumaitha bwana d c ndi more pachilungamo😊
Like this guy or not , but he is very sharp
The DC🔥🔥🔥
Good advice
Komatu bon kalindo amayakhula ngati wamisa koma ndizoonadi zimene amayakhula anhtu inu muzichenjera
🎉🎉🎉 following
I love you so much
U always stand in true mr Bon l love u more than
Mr Kalindo mukutitsegula mmaso kwabasi keep it up
Tikumupemphani a Born kalindo bwelelani ku UTM please
Ndipo president akakhale iyeyu ndimunthu wamaso mphenya❤❤we love him❤
Utm siingatuluke mugwilizano ngakhaleso atatuluka palibe chazelu chomwe angapeze
Salute
The DC mwana ohopya kwambili
Kalindo amalankhula zoona uyu ndi mpulutsi.
Kulankhula mwachilungamo. UTM tsegulani maso. Tulukani mu tonse alliance monga akunenela Bon Kalindo please.
A MCP asakupusitseni ife tili mbali yanu ndi SKC osaopa, osatopa, osafooka 💪
Kalindo is trying his best,chikufunika osusa agwirane manja!,ku UTM apereke mpata kapena position imene Mary chilima angatenge icho chiperekeranso mphanvu ina yapadera muchipani.
Bwana DC mumatiimilira
Chilungamo chimamasula go ahead the DC
Kmat uyu tiyen Tzimuvela zimene amayankhulaz
Big up to you 🎉🎉🎉🎉🎉 umatha kung'alura
President wathu wathu,Mr Kalindo lero ndilomwe tidziwedi kuti UTM ipitilira ndipo SKC waphera chilungamo.
Mbambande Bon Kalindo
Mumatiimilira a bon
Umaitha bon
Khan nd yoona
In short Utm ibwerere ku DDP....tigwetse vinyau tikinze dziko
Mr DC 2025 woyyeee.
Bon kalindo akunena zowona lelo muchoke ku mcp mukapitiliza ndiye kuti mukusangalala ndi ife ya chilima chipani chimene chingawine ndi UTM kampeni wake zikolose lapasi lipanga saport
😹😹😹 iwe umakwana aaa nilinje mau
True
Tiyeni tiyeni tiyeni Mr DC
What if mrs Chilima is not a politician? Komanso akuti anthu azilowa kuchipinda ndi candle nkumakatchula dzina la Chilima kodi Chilimayo wasandukano mulungu?
kalindo umakwana ase
President wathu Mr DC
Bon kalindo umakamba zoona
Mayi chilima to be president, braund banda,mwana wachilima awa kaliyati, awa musankhemo mumozi ankhale president mwana wa chilima anyamata ose ankhala ndi chidwi
❤❤❤❤❤❤❤
Powerful spetch
My vote kalindo umatha umatiimirila
Chilungamo ndimwano❤ The DC pick up man
Sanena boza uyu
Umakwana winiko
A UTM uthenga ndiumeneo zili ndiinu kunyalanyaza kapena kutengapo kanthu km mawa pangatalike muzawakumbukira mau a Bon sadutsa pachabe
DC Huma kwana
The DC
DPP+UTM+UDF+AFORD....
MCP out 2025..
Musapusisidwe a utm mcp sichipani .muzifunse kuti kodi chilima chamupha ndichani kodi mukugona a utm, tsegulani mumaso
It's true bwana president woyamba wa anthu osauka muno Malawi
Kalindo more 🔥 ❤
Na pa Bone Kalindo palibeso same same Mtanyiwa anthu awa amanena chilungamo chokhachokha
Big up de DC our pool p
Koma Mai kaliyati ndi kagulu kanu choonde nvelani kulira kwa anthu ngati ku UTM kuli anthu olimba nde ndinuyo mumakhala chifupi ndi Chilima musakomedwe ndi ndalama mukwiitsa anthu ochuluka nthawi yatha kale iyi musanvere MCP kukunyengeleleni ndi ndalama misozi ili manso ndithu mutenga tsoka
Zoona mb'ale
Wise man
Ndipo a mcp ndi athu ochenjela ndi kuipa komwe ndipo chilima amusasa lelo akuyanja otsalao mukapusa akumezani
Kalindo good advice
A UTM mukapanda unvera za bon kalindo muzalira moyo wanu onse
Amakwana koma ❤
Our freedom fighter ndiwe kawawa ndithu
The DC ,lankhula chilungamo bas
The Dc bon kalindo 🎉🎉🎉
Makwana mr keep it up
🎉More fire!!!!!!!!!!!
The Dc bon kalindo ❤
The DC kkkk konda u ife
Nice
Usazafe kalindo uzangotsowa ngati eliya
Koma manganya asamuwelengele ndiwa MCP kuyambila kale
The DC agogo anga akufuna azakuoneni
Gwilizano a mcp adayedzeka amamukana chilima dzuwa likuswa mtengo achakwera kumayankhula zonyazitsa chilima Ali pompo chilima sanapuse sanayambane ndi munthu ndie lero zatani RIP chilima.
Ndipo ndizoonadi amamukanadi chilungamo ndiye lelo ayanja otsalao
Very true
Brayani Banda ndimunthu wa chikondi ndi ziko Lake mayi cilima tiwona ngati chilimayo alipo anthu tivota ambiri mwana wachilima anakonda achinyamata ndiye achinyamata ose ali ndi ife
The problem is anthu akumudz unthengawu suwapeza cz of social media
Kd zimenez zitithandiza osapita pa galaundi kukapanga ma demo ngati tikuona kuti zithu sizilibwino,, Timakunyadilan mr DC,Km please dziko ndilathu tiyeni tipange zaku Kenya 🇰🇪 basi
Mmm
Bhooooooooo nikalindo😂❤
The DC mulomwe wathuwathu odziwa zinsinsi
Tidziwe basi.
Ma traitor tiwadziwa lero
Ndiwamisala daily ma audio Iya ndimbuzi President osauka kwanu konko
Uzifuse wekha kut ndi angat omwe akumuyamikila,? Nanga omwe akumunyoza n angat?
@@MathewsChitambe zako zimenezo cadet ine ayi ok. Your opinion is not my opinion. Ine yanga ndi MCP basi
Mzimu wa bwana Chilima uwavuta.mukaone maruwa ngati akukanika kufa .musamale kwambilitu.
Good Good news
My vote umakwana
Gibo Pearson wachita misala, is zikumveka kuti zadza kamba kangozi ija
Iwe ulongosoke
The DC mwana oopsa kwambiri satekeseka ndi Uniform ya a police,ingankhale Unyolo. Tell them 😅😅😅😅
THE DC PANGOLINI 💪💪💪💪💪
Mumatha