This what we are looking for our leaders to do. Go to the ground yourself sometimes and a look on your own. May you strength the leadership spirit to be like this. Bravo Dr Usi
Zomvetsa chisoni kwambiri, dziko silingatukuke chonchi, Koma Michael Usi Ambuye akusungeni ndi moyo. Izizi anthuwa amapanga dala, they make them to be loops for cash gate leakages. Wish long life Dr Usi
People can you see that this guy has an ability to deliver something to this Malawi guys lets stop kuyang'ana zinthu mwa ndale and lets spot chilungamo he has something special that Malawian politicians are lucking
Usi this is a way to go.I like you that you dont pay attention to politics,but real development.You will never be loved by selfish politicians who cherish in rallies
Ididn't know that Dr michal usi is that serious oooh my God. This kind of head is out of Malawi education system indeed. And he don't tolarate nonsense which means it also pains him as aleader. Just imagine if we have such leaders.
Mudzaendeleso mseu wamkati mwa town ya balaka from ngwangwa filling station to balaka escom house ka mseu kosakwana 3kms chaka chino chachiwili sakumaliza
Poor thinking capacity, in Japan or China they can build that in less than a week. But they infrastructures are way much too strong than ours omangidwa 10 years iyo
Usi. Yes you can make this country change and we need you to check our mbelwa university why are we not on the ground work regards swank Ibrahim mzimba pelekezi constuency
Time out nothing happens failing to organize his source as UTM leader not well organized original UTM leader was starting doing as such but cruel mcp leaders stop him now they realize and regret too late stop it it's no sense
If we had leaders like Mr Usi before! Aaaaa Malawi would have been a beautiful country. Let's support him to transform our country.
Koma vuto Ali under mimbulu
Mr vise president is jeniours
Uyutu ndimuvotela
Michael usi loves his country... AND jealous people are feeling painful to see him doing this 😅😅
This what we are looking for our leaders to do. Go to the ground yourself sometimes and a look on your own. May you strength the leadership spirit to be like this. Bravo Dr Usi
Zomvetsa chisoni kwambiri, dziko silingatukuke chonchi, Koma Michael Usi Ambuye akusungeni ndi moyo. Izizi anthuwa amapanga dala, they make them to be loops for cash gate leakages. Wish long life Dr Usi
You have started well Dr Usi may God be with you , we need courageous leaders to transform our nation. This is a servant leader not a boss one
Uyu ndiamene akufunika kukhala mtsogoleli wadziko osati zinazi kumangokhala mu offers ,my vote for usi
Ndipo zooon apitenso ku migration
Zinazo zili apo
Koma chilungamo apapa malawi akhoza kusitha zitapitilira zoterezi
Vuto ndiwe mwana ku ndale .. mcp imafuna munthu oti sangawapase mpeshupeshu kundale .. why sanamupase chilima this chance
100%
they are not talking about the pope kkkk😂😂😂😂
Mukamaliza.... Muwaitanitse ma contractor Omwe anapasidwa ntchito yomanga bridge ya Mulanje mkando
Exactly
Zowonadi, anthu akutha pa bridge imene ija
People can you see that this guy has an ability to deliver something to this Malawi guys lets stop kuyang'ana zinthu mwa ndale and lets spot chilungamo he has something special that Malawian politicians are lucking
Dr Chilima ankapanga zimenezo ndipo Anthu anakamuuza president kuti akushaina mpakana kumupezera zifukwa zambiri mbiri till kumuchepetsera mphamvu kenako milandu later kumupha
Mr Usi , Continue monitoring development we need your leadership. I salute you Mr vp
Yes that is magufuli spirit,
Michael usi zachbwana sakupanga nawo that's what we all need in Malawian leadership
Bwana Usi ndakukondani alesi sakufunika zikomo
ndipo zikamakhala choncho bwenzi Malawi alipena pake
good job vp
Where were you Utsi?
This is greatful movement. Osamasekerera zoputsa ...being a leader zimafunika choncho ndithu
Ku immigration please zibwana zichepe chifukwa ndimbali yimozi yimationongela kwacha yanthu
🎉good leadership, keep it up our VP
Izizi ndi zabwino, chabe kuti next term sakutengaso, safuna anthu otere.
Usi Can be a good President. He can deliver
Zabwinobwino. Kumeneko ndiko kulikonda dziko lathu, sianakalipe. Aaaaa! Zina zimawonjeza.
Michael Usi iiiii beautiful leader
Kkk let's start what you have not done simple then we will start from there well done Mr vice president
I like the fact that Mr VP you are dedicated to serve the interest of Malawians not yours alone big up
Usi this is a way to go.I like you that you dont pay attention to politics,but real development.You will never be loved by selfish politicians who cherish in rallies
KOMA bwana VP mwachemetsatu
That's what we want Malawi politicians and leaders to be
Ididn't know that Dr michal usi is that serious oooh my God. This kind of head is out of Malawi education system indeed. And he don't tolarate nonsense which means it also pains him as aleader. Just imagine if we have such leaders.
Outstanding 😊
Ine usi ndimadana naye Koma izi zokha nde zandisangalatsa
thus zomwe amafuna chilima but amakhomeleledwa ...mpaka mmanda ..mwayi kusiyana ...rest well chilima ...
Good VP asamangoti apita kunja apita kunja kumangotha ndalama za zii no yenderani zonse bwana apa mukapitiliza mope a ma voti ochulu ka
VP don't forget immigration sector
Suimba anthu timakawakaziwili kumeneko ndikumawalimbikitsa km pano yo no way to go
Excellent usi
Very nice koma MCP payokha ayi situyifunaso
Good work the VP koma azungu muziwakalipira mwa ukathyali kuwopa kunyula mu njira zina.
President ukhale iweo bwana usi more fire
Good job,,, big Mr VP
Uyu avutika naye anthu , that's how agood leader work's
Good job Mr Usi, tangowathamangitsani abolingo awa
Muwumiseso nyanja ya rake Malawi kuti nsomba tizigwila mosavuta
Mudzaendeleso mseu wamkati mwa town ya balaka from ngwangwa filling station to balaka escom house ka mseu kosakwana 3kms chaka chino chachiwili sakumaliza
Izi zipangitsa kupanga chithu chosalimba
Poor thinking capacity, in Japan or China they can build that in less than a week. But they infrastructures are way much too strong than ours omangidwa 10 years iyo
Malawi akuoneka kuti mbuyomu munalibe anthu
Ngati usi chifukwa usi akufuna kuti
Ife amalaw tikale ndi zochita uyu ndi
Leadership wabwino kwa ife amalaw
God bless you usi God bless Malawi
Á
Nice vp watching from mgubudu 🇿🇲 Chipangali
Usi keep it up kkkkkk you're the game changer
Ma PC mumapangira dala kuti muziday ndalama you cant change the design while the contracter is building
I wish the president also to be crc like manganya you are well done keep it up
Remind him of immigration departments people are just ducking around there
Big up bwana vip ,this is powerful ,my vote of thanks
Yes my president if we were having you b4 our country could be somewhere.
Uyuyu bola akanakhala ku utm osati mcp yakeyo
That's awesome mr vice keep it up
Kuti apezeke a Usi atatu malawi akhoza kusintha
Usi ulimutu sana keep it up
my freedom fighter mr usi keep it up
Very powerful vice president 💪💪💪💪
Awa ndiye awona chomwe chidameta nkhanga mpara
You are the right leader, continue to do so
Wonderful job Mr VP,I ministers must lean something
Nsogoleli wa Chisanzo. I m here in mozambique and as well a Mozambican
Mpasa mulandu mungoti pheee mcp ilibe zimenezo
My vote to usi❤❤❤
Usi wayamba bwino kwambiri malawa atha kusintha ndithu
😊mupitekoso kuma offence yama passport akupanga zibwana kwambiri anthu azidikira passport mupaka chaka wosatenga passport
That's awesome our VP keep it up
😂😂😂koma yaaa mwayamba boza chakwera akutumani
But ine ndikuwona ngati kuti amupatseso agriculture ministry .ameneyo akuwonetsa kuti alibe dyela atha kuthandiza ku zamalimidwe njalayo mwinaso kuthelatu.chifukwa zonsezi ndi chabe koma dziko lili ndi njala anthu akufa ndi njala.kuyambila muluzi gv,bingu,joice ,peter mpakana lelo chakwela palibe boma limene lapititsa patali zaulimi kuti njala ithe.
Zoona sabsidy ija anakamapanga zinenezi Kwa ma contractors zinakayenda bcz panali ma contractors adyera oipa Moyo Koma anasekeleledwa kwambiri
Komaso tiyeni tiziyang'ana mbali zonse... Iyeyu zaka ziwiri zonsezi anali kut osabwera kuzaona ntchito yomwe anayamba... fotsek!
Usi. Yes you can make this country change and we need you to check our mbelwa university why are we not on the ground work regards swank Ibrahim mzimba pelekezi constuency
mulungu amapanga njira uyuy sikape blv me
This guy is so intelligent ❤❤❤
That contractor guy why is he whispering when responding to the VP?? Is he like that or kudelera kapena manyazi kuti wagwidwa ufiti??
God bless Usi for being aggressive to shake people in offices. Too much being wasted.
mukatha kumeneko mutapitakoso mu mzinda wa Lilongwe they are playing too much🤨
❤❤❤❤ Mr VP mukuesetsa Kumbali yanu
Bwana Usi amatha kugwira bwino koma vuto ali pa kaliyala. Pajatu wokwela Ku kaliyala siimba beru
Wangokhala kathyali koma ntchito yake ndiyonthandiza Dziko
Makina vice President usi
The former Veep wasn't aggressive
Our vise president did it well 🎉🎉
zonse ndi zanu km ine ndikungofunako chisot ndi make sikono ndi maglass bs chonde avice president
ndipitilize kupanga masewelo amanganya
Ine sindine malawian km a vp ndawakanda magwilidwe ao a ntchito
Thus good Mr Micheal usi
Sangazumalize ameneyo mavuto alipaliponse taikani chimanga kwa ADMARK apa osati zaziiiizo
Izi nzomwe ankafuna Chilima koma akati atere amamkhomelera
ndipo inu nayetu anayamba chomchi koma jelasi Anthu
Micheal "manganya" USI.litle did I know you're that brilliant
Maganizo akupanga manganya ndiabwino koma vuto chinthu chitha bwanji ndalama asanapereke zokwanira ndiye zichani ungamange nyumba ulibe ndlama yokwanira wasewero uyu😂😂😂😂
Akunenepatu bambo asikono mpando wa VP ngonona
Kugwa mowilikiza kwandalama ya kwacha kwasokoneza ntchitoyo,simukumvetsa pati Bambo asikono😂😂😂😂
That changes was just part of stealing money
Osapanga zamolalotu komanga ngat mkupanga zimenezo muchoonadi Mulungu akudaliseni
Uyu ali ngat maguful
Koma posachedwap mumva amabungw akt auful kt sakuchit bwino asiy
Sangafanane ndi magufuli..never magufuli samamwaza ndalma amachita zitukuko zoopsa kufuna chabe vote ya Malawi kt azavotele Mr chikangawa
@@CharityMhone-uk9ym ndipo ngati amalawi tipuse mukamphindi kochepaka komwe akubweresa tokoma 😂😂😂😂❤ Mcp will lead again Next year....
Believe me if hes a president we can change for sure
This is great 😂🎉😂🎉Mr Vp
He is doing the needed
Zofunikira zimenezi go ahead
Time out nothing happens failing to organize his source as UTM leader not well organized original UTM leader was starting doing as such but cruel mcp leaders stop him now they realize and regret too late stop it it's no sense
Kma apapa amaitha kwambiri ndie zikufunika Ku Malawi izi