Это видео недоступно.
Сожалеем об этом.

Zomwe wayankhula Bon Kalindo Lero pa 13 July 2024 pa nkhani ya kutuluka kwa UTM mu Tonse Alliance

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 11 июл 2024

Комментарии • 116

  • @shumbapatience6063
    @shumbapatience6063 Месяц назад +12

    UTM back to DPP never we r on our own🔥🔥🔥🔥🔥

  • @GiftJacob-z4c
    @GiftJacob-z4c Месяц назад +5

    Koma fact ndiyakut apapa a UTM mwaphunziladi angakhale achedwa koma this is brave idea , tili ku mbuyo kwanu .

  • @DRIPPAPIE_2lyrics
    @DRIPPAPIE_2lyrics Месяц назад +2

    ❤❤❤This guy he's genius Ndipo amati fightiler kwambiri 🔥

  • @ruthsambaleni-hw5gu
    @ruthsambaleni-hw5gu Месяц назад +2

    UTM should first stand on its own. Build the party

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg Месяц назад +2

    Asiyeni a UTM apange zomwe agwirizana

  • @ThokoMpelembe-ji7fj
    @ThokoMpelembe-ji7fj Месяц назад

    Mumakwana Mr DC

  • @cosmasnkanda8193
    @cosmasnkanda8193 Месяц назад

    Iwe ndi machine🔥🔥🔥

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam Месяц назад +1

    From town centre Mitchell's capetown bon ndimakudyadilan kwambili God ahead u bro

  • @user-cq8fz5ud2e
    @user-cq8fz5ud2e Месяц назад +1

    Mupwetekana

  • @PeturosiNyirenda
    @PeturosiNyirenda Месяц назад +1

    Kalindo salimoyesa 🎉🎉🎉🎉🎉🎉👍👍👍👍💯

  • @MphaKampala
    @MphaKampala Месяц назад +3

    Uyuyu a Malawi ambr mmamupeputsa ,.koma nthw idzakwana ubwino wake muzaudziwa
    Chitsime chimaoneka chokuya madzi akaphwa

  • @Eli-u2d
    @Eli-u2d Месяц назад +2

    Ndale zokha zokha,mwasiya masewero abwino, ndalama iwonongesa mbiri

  • @smartchitimbe2450
    @smartchitimbe2450 Месяц назад

    The DC is right

  • @EmmanuelNkosi-ts8bn
    @EmmanuelNkosi-ts8bn 29 дней назад

    Nkhani ikhale UTM , AFORD ndi UDF apange alliance, president achoke ku UTM ndekuti azapeza ma vote Ku north , central pang'ono koma ochuluka ku southern nde kuti azaiphula bho bho

  • @SebenzileMsebe
    @SebenzileMsebe Месяц назад +1

    Utm bwelenani ku dpp kuti udzamange amene anapha chilima

  • @user-yq1mc3nm1f
    @user-yq1mc3nm1f Месяц назад +2

    Kkkkkk Manganya adali Yudasi zoona, bwato satsilana pakati pa nyanja kkkkkk

  • @GogoKasiketi
    @GogoKasiketi Месяц назад

    God first

  • @RhodaNombo
    @RhodaNombo Месяц назад

    Fakafaka mumatiimilila braz

  • @PemphoSmart
    @PemphoSmart 29 дней назад +1

    Propaganda at its peak. Ife anthu osauka takana kuti ndiwe president wathu

  • @daudinussah2232
    @daudinussah2232 Месяц назад +1

    Ubwino wake ovota ndife, and kalikonse kochitika pansi pathambo Mulungu amachionetsa poyera

  • @PeterJanga-wv9nz
    @PeterJanga-wv9nz Месяц назад

    Born kalindo akamuna bambo

  • @chrisneySwanepoel-yu5vd
    @chrisneySwanepoel-yu5vd Месяц назад +1

    Born kalindo ndakamuna

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe Месяц назад +2

    UTM ISAPHATIKIZANE NDI DPP CHIFUKWA MKAZI WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POTHAWA MOTO KU SODOMU..PAMENE NGELO WA AMBUYE ANAWAUZA KUTI ALIYENSE ASAYANG'ANE MBUYO. KOMA MKAZI WAKE WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POGANIZIRA MOWA WAKE WOMWE ANKAPHIKA KUSOMUKO NKUMAGULITSA. IYEO ANASANDUKA CHULU CHA MCHERE. SO UTM NSO MUKAPHATIKANA NDI DPP MUSANDUKA CHULU CHA MCHERE.MUKHALA STUCK AND DORMANT DEAD WOOD .!!!

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e Месяц назад

    Mawu a Bon sapita pachabe nd Yosef mwana wa maloto😅

  • @user-iz3qr1gu9d
    @user-iz3qr1gu9d Месяц назад +1

    UTM welcome back to DPP family

  • @Yuze_Matukula
    @Yuze_Matukula Месяц назад +1

    Boooooooooon Kalindo!🔥

  • @InnocentSayenda
    @InnocentSayenda Месяц назад

    Mmakwanila big

  • @Africanbwoy185
    @Africanbwoy185 Месяц назад

    Uthenga ukupita kwa Michael Usi aka Manganya

  • @KhalideNerve-mu1eq
    @KhalideNerve-mu1eq Месяц назад +1

    Mission possible

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Месяц назад

    Pakhala mabvuto olimbilana utsogoleli APA ifee phee Ku MCP basi

  • @AlbertNambwale-sm9qe
    @AlbertNambwale-sm9qe Месяц назад

    Well did
    L

  • @user-dj5hd4ys3n
    @user-dj5hd4ys3n Месяц назад

    Kalindo the man of the momenti %100

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 Месяц назад

    Pangolin iweyo the DC

  • @MarkTembo-ut9sv
    @MarkTembo-ut9sv Месяц назад +2

    Ku dpp tikataniko? Chilima anatulukako ndipo sanabwelere mpaka kufa kwake ndiye ife tufuna mufuna mzimu wake utikanthe?

    • @MosesNjanje
      @MosesNjanje Месяц назад +2

      Ndeee kupusako do you think kut utm payokha ingagwetse mcp yotiiii ili m'boma inuyo dziko lanu simulikondayiiii amkolo chilima ananena yekha kut ku dpp anachokako analibe vuto lililonseee ndee inu ndare simuzidziwa Bola mungokharah chete ngt muganiza kut mungazawine panokha kuchotsa chipan cholamulachi

    • @franciskameko2586
      @franciskameko2586 Месяц назад +1

      A UTM panokhs simungalamule dziko ndpo position yanu izingokhala 3 or 4... Koma chifukwa chot ndinu okulamtima mumadzimva ngat muli nkuthekera... Kachipani ka ma MP 4 koma matama thooo🤣🤣🤣

    • @mikesandali8425
      @mikesandali8425 Месяц назад

      Kkkkkk

  • @McDonaldMakina
    @McDonaldMakina Месяц назад +1

    Pangolini tsopano

  • @AnthonyPhiri-qp8fn
    @AnthonyPhiri-qp8fn Месяц назад

    Mr bon kalindo thanks live on zambia Lusaka

  • @YusufujohnSeruweke
    @YusufujohnSeruweke Месяц назад

    Chilungamo kalindo

  • @user-wh6zp4vx1n
    @user-wh6zp4vx1n Месяц назад +1

    Chikati hahahaaa Ndipo chimaseka modelela Chi Born Kalindooooo

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe Месяц назад

    And madam Patrucia Kaluati being the leader of utm presidential.candidate.cos she is has got experience of leadership.by profession she is a teacher and again she has experience of political leadership.she was in dpp .wurh Bingu wamutharika and peter mutharika

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Месяц назад

    This is the truth utm plz bwererani ku dpp

  • @SmithChisoni-x4r
    @SmithChisoni-x4r Месяц назад

    Dolo kwambiri bonte kalindo😂

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Месяц назад

    So good 👍

  • @langsonbanda9265
    @langsonbanda9265 Месяц назад

    Inu kusokoneza basi

  • @desmondshugar4585
    @desmondshugar4585 Месяц назад +1

    Good

  • @OmecxKondwan-dx7do
    @OmecxKondwan-dx7do Месяц назад

    Mr DC hohoho🔥🔥🔥

  • @SteveNkhambule
    @SteveNkhambule Месяц назад

    We don't have opposition in Malawi

  • @LevieMwanayaya
    @LevieMwanayaya Месяц назад

    Mwana wakwathu DC tie nao kung'alurako

  • @KelvinLawrence-q1o
    @KelvinLawrence-q1o Месяц назад

    The fact is Kodi Njoka kudulidwa Mutu ingayende?

  • @OliviaFour-rk9ir
    @OliviaFour-rk9ir Месяц назад

    Booon kalindo ❤❤❤❤

  • @mishasjambo4793
    @mishasjambo4793 Месяц назад

    Eeeh ndine bon ...... 😂😂😂 Kuipatsatu fireee

  • @MECChiona
    @MECChiona Месяц назад

    UTM 🕊️🕊️🕊️

  • @SteveGemini
    @SteveGemini Месяц назад

    This is boooooooorn Kalindo🤣🤣🤣💯🔥

  • @JonathanChimwaza
    @JonathanChimwaza Месяц назад

    Tiuze zoona ife tiri nga nga pa mbuyo pa DC

  • @AlidiMdala
    @AlidiMdala Месяц назад

    Munyengo yong'alula🔥

  • @FrancismkopokahIshmael
    @FrancismkopokahIshmael Месяц назад

    The DC 💥💥💥💥💭

  • @DenessTchabe-og6cs
    @DenessTchabe-og6cs Месяц назад

    The DC Born Kalindo

  • @raymondlupiya
    @raymondlupiya Месяц назад

    Ichichi chinabwera🔥🔥🔥.

  • @EdisonNgolomibanda
    @EdisonNgolomibanda Месяц назад

    Carry on pangolin

  • @rodrickkulimakaunde7928
    @rodrickkulimakaunde7928 Месяц назад

    Musiyeni Manganya asangalale ndi mdalitso wake, ndi Mulungu adalola kuti akhale pa mpando umenewo. Sizoti iyayi wa UTM weniweni apange resign, kuti chani? Kulephera kwanu musade nako anzanu amwayi.

  • @LDeeNdilimunjila-zs1qh
    @LDeeNdilimunjila-zs1qh Месяц назад

    Born!!!!!!!!!!!! Kalindo!!!!!!

  • @user-xn5jl3sp6d
    @user-xn5jl3sp6d Месяц назад +1

    Born💥💥💥

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c Месяц назад

    Zikomo kwambiri azaona chomwe Chinameta nkhanga mpala mcp palibeso

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe Месяц назад +2

    Correction utm has vast followers so let utm.stand alone..and its gonna win with the majority.nos

  • @FatsaniMchenga
    @FatsaniMchenga Месяц назад

    Zimene ukufuna iweyo abwelere ku Dpp ....

  • @wairutchukambiri8011
    @wairutchukambiri8011 Месяц назад

    🔥

  • @innocentmusuli7380
    @innocentmusuli7380 Месяц назад

    Akakhala okha olo atapanga bwanji olo atatani sangawine ndipo akazabera dziko lizakhala mmanja mwa chinyamata

  • @IssahFrank-vt9hu
    @IssahFrank-vt9hu Месяц назад

    Apa mwapala, za alliance so ayi

  • @heavenpromotions
    @heavenpromotions Месяц назад

    Akuti anzanu wo anavota kale😂😂

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge Месяц назад +1

    Manganya 🚮🚮🚮

  • @FatimaUmali-pc8sy
    @FatimaUmali-pc8sy Месяц назад

    😢😢😢😢

  • @mwaisulaimana
    @mwaisulaimana Месяц назад

    Tisasogoze kukangana tieni tione patsogolo...

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 29 дней назад

    Mau bg kkkkk😂😂

  • @isaacpiyo6792
    @isaacpiyo6792 Месяц назад

    We are not going for coalition again

  • @replacefruittreenursery
    @replacefruittreenursery Месяц назад

    Uyu ndi neneri ndithu

  • @ImmedGerrard
    @ImmedGerrard Месяц назад

    The DC

  • @SmartVictor-kz7dh
    @SmartVictor-kz7dh Месяц назад

    Kkkkkkķ tiligu mwati

  • @douglaslemison
    @douglaslemison Месяц назад

    Boooooooooooooooooon kalindo the DC

  • @handcuffmagalasi4130
    @handcuffmagalasi4130 Месяц назад

    Ichi chimaseka udyo..

  • @user-tw2zf7bj3e
    @user-tw2zf7bj3e Месяц назад

    Tidzavote popanda ID plz

  • @user-qc1yv3zk7i
    @user-qc1yv3zk7i Месяц назад

    Thawi yong'alura 😅😅

  • @MEDSONMZUMARA
    @MEDSONMZUMARA Месяц назад

    zoona kalindo chilungamo

  • @IssahFrank-vt9hu
    @IssahFrank-vt9hu Месяц назад

    Kkk

  • @user-xh4vn6ms5l
    @user-xh4vn6ms5l Месяц назад

    Munyengo yong'alula

  • @franciskameko2586
    @franciskameko2586 Месяц назад

    UTM chipani cha pa social media🤣

  • @AnthonyPhiri-jg6vd
    @AnthonyPhiri-jg6vd Месяц назад

    Kung'alura bas

  • @EmmanuelMtonya-j7b
    @EmmanuelMtonya-j7b Месяц назад

    Emrove

  • @christopherpetro-pen3678
    @christopherpetro-pen3678 Месяц назад

    Komatu ndiye kuli kung'alula🤦

  • @TishaSamu-kc4ks
    @TishaSamu-kc4ks Месяц назад

    Boooon kalindo

  • @richardkuwani3647
    @richardkuwani3647 Месяц назад

    Chayankhula bwinotu

  • @davidbulla5128
    @davidbulla5128 Месяц назад

    😂moyo moto Aye!

  • @PrescotMtengezo
    @PrescotMtengezo Месяц назад

    Koma chikuseka😅😂🤣🤣

  • @ericgowero142
    @ericgowero142 Месяц назад

    Nde dpp zabwino?

  • @SwazzyCassium-u9n
    @SwazzyCassium-u9n Месяц назад +1

    😂😂😂

  • @user-de9nx7ts2d
    @user-de9nx7ts2d Месяц назад

    kung'alura

  • @HarryKumwenda-jm1df
    @HarryKumwenda-jm1df Месяц назад

    Utm

  • @KascTollah
    @KascTollah Месяц назад

    Bwana kwambr😂😂

  • @chisomogareta1958
    @chisomogareta1958 Месяц назад

    Uyusotu amangolubwa

  • @gideonnyasa
    @gideonnyasa Месяц назад

    A Kalindo zindikirani ichi dziko la Malawi ndi latonse, is not about resignation of its members in government positions. Stop misleading people, eg Usi won't resign cos he is serving Malawians not MCP.

  • @itzfazmuslimah
    @itzfazmuslimah Месяц назад

    Uyuyu ndi 🔥🔥🔥

  • @chiluzbandah
    @chiluzbandah Месяц назад +1

    Ife dpp ayi ndipo madala team sitikuifuna kumene kuja tinachoka basi