AKUTI OLO KAMBA ATADIKULA DPP SINGALOWE M'BOMA ~ WATERO JESSE KABWELA PA MSONKHANO WA MCP PA 15 SEPT
HTML-код
- Опубликовано: 17 сен 2024
- AKUTI OLO KAMBA ATADIKULA DPP SINGALOWE M'BOMA ~ WATERO JESSE KABWELA PA MSONKHANO WA MCP PA 15 SEPT
Welcome to our channel, where we dive deep into the intricate and evolving world of Malawi’s politics. From the rise of powerful political parties like the Democratic Progressive Party (DPP) and Malawi Congress Party (MCP) to the powerful impact of the UTM Party, we bring you insightful analysis on the key players shaping the nation. Explore the journeys of leaders like Lazarus Chakwera, Saulos Chilima, and the influential activist Bon Kalindo as they navigate the challenges of governance, power struggles, and the quest for a better future.
Our channel is dedicated to unraveling the complexities of Malawi’s political landscape, offering you detailed breakdowns of alliances, rivalries, and the significant events that continue to define the country’s destiny. Whether you're interested in historical perspectives or current political dynamics, we provide in-depth coverage and engaging content that keeps you informed and inspired.
Subscribe to stay updated on the latest developments, and join us as we explore the fascinating stories that shape Malawi’s political narrative.
#MalawiPolitics #PoliticalAnalysis #DPP #MCP #UTM #LazarusChakwera #SaulosChilima #BonKalindo #AfricaPolitics #PoliticalActivism #petermutharika
Ku Mangochi kuno kulibe vote ya mcp
Yiwalani
Ife ndizingokudyerani ndalama koma vote ndiya APM
Pa mtumbo pako wazobwirabwira iwe
Miseu,kaya chani?Ndi ndalama za Misonkho yathu.
Jessy galu amwa mafutao anthuo DPP boma
Malawi ndizomwe adzasankhe sipakamwapo ayi DPP boma
Ndanena ndanena mufune musafune koma dpp ili pa pando kare or ma vote asanaponyedwe koma dpp yili boma
Achimwendo ndinuopusa komanso ndiwembuli msewutu sithandizo pezani zochita
Chakwera akusiwa mavuto amalawi😢😢 koma ndalama
It's treu m c p is going to Winn again,
Mcp imandinyasa bwanj😢😢
Boma lake liti
.
Boma la mbava komanso zigawenga
May iwe panyopako ndichakwela ndiwe opanda zeru patumbo machakwela ndi iwe womwe
So sad, dzimayi olimba ntima kuyakhula kwa ndinthe ndithe ,tidzavelaso vidio iyi chaka chamawa🙏🙏
Ndipo azalira
ndipo video iyi tisunga bas
Chikangawa
Mcp kupha , kuba , kunama .
Mcp out , no more chance
Only savages can say kwachaaaaa 😂😂😂
Abig,😊 YES
Opusainu mcp yokupha komaso yodalila usatanic
Uyu sinakubala uyu
chitsilu cha chiwanda ichi
Sasamba ngati simkazi
Nonsense the government that fails to make passport and license...
Uyu asandipalamulise agalu okupha wa shupiti
Amayi awa ndiachitsiru kwambiri akachita thupi kusawa ngati amamwa matokoso kuli kusamva mafuta ngati amadzola mchere.
Zaziiii mukuwona muwina never
koma bwanji mawi amenewa kodi mwaredzela zipaseni ulemu mai
Kabwirayu Mutuwake sugwira,
Vomekezani kuti chakwera walephela,kabwila ma pilisi amukwana
Paja amatamika mmalankhulidwe awa
MCP singawine
Mmmm iwe
Useless government
Ukamba nonsense Kabwira, just tell them you want money ku MCP end story
Jeassy Kabwila Ovotaotu ndi Amalawi
Zimenezo ndizale tizaziwona po kolola musiyeni tiligu nasongole akulile limodzi
MCP ingozilimbitsa mtima achimwendo banda muli ndi thumazit ndipo MCP ikupita olosera talosera kale MCP is going for good DPP iri mudzit osati town olo mutamanga nsewu wakumudzi sakukumvani Iwo angoti chakwera sitivotera , makhwala zipatala anenamo mulibet makhwala. Ndipo MCP yationesa Malawi muno 2025 pitani kapumeni for ever .
Nyimbo yasenderayo tailekani achakwera sikuwakhala imakhala BINGU IYOOOO OSATI MANYAKAWO
Akudalile kubela mavote namachende amenewa
Tikufuna tikuveni kwakonda kwanu amalawi anakusisani kuti ndege yazaza ndindani pano kwasala masiku4
Amasuta chamba kabwila mudzimuona mayanthulidwe akewo
Walandira 2000 ameneyo ..DPP my vote
Ndinu. Opusa. Mayi. Muzinamiza. Amalawi. Ngokwiya. Tsegulani. Maso... Akudikira. Kukutuludani. Boma.. 2025.DPP. Boma... Muziyamika. Chilima.... Simungawine. Nokha. Opanda. Alliance mukapuma. Mpaka. Muyayaaaaa!!! '
Boma ndilomweli abrayan mungochitika ngat mburi bwanji
Zaziii mayi opusa kwmbri iwe
Tiona 2025 JESSY ndindaniso uyuyu kape kwambiri
Inu mwapha chilima
Mumayakhula mutamwa Makhwala ozunguza ubongo eti kapena mutamwa mowa azimayi ophika mowa
DPP boma
Uyu ndiwankhunyu
It's treu mama
KOMA AMZIMAI OSASAMBA AMCP NDIOMVESA CHISONI KWAMBILI ,KUMUONA MZIMAYIYO ARI MBUUU KHOPEYO , KHUNGU , NGAT PANSANA PA NG,AZI AWA ALIRA 2025 DPP IKUTENGASO M,BOMA NDIPO KAMBAYO AZADIKULA KUONESA MCP KULUZA TILI PANO IFEE
KODI INU MSEU WAKE UTI AKUMANGA CHAKWERA CHIMWENDO UYU ANALI KUNJA INU DPP MOMWE YAMANGILA BLANTER LILONGWE INU UYU AKUONA NGATI IFE WANA ETI
Kodi inalikuti mcp inu minali ku opposition for 26 years kapanda chilima ukadakhala muli ndani inu
INU IFE AMALAWI SITIKUFUNA NKHAZA ZOPHANA ZOGWESA NDEGE AAA INU CHAKWERA SITIKUMUFUNA
agaluu awanthu a mcp aziona 2025
Mkwiyo paja ndi ufiti. Tisayiware
Kabwira mbuziyako wamva ndi chikangawa team yakupha nonse agalu n okha
Akuopa mgwirizano wa dpp ndizipa zina akuziwa zangawine 50+1 chipani chilichoze chikuopa kukapanga ndi gwirizano chifuka ochewa ndale zawo kumapheto ndikupanda akamutenge nakhumba ka nakhumwa akuganiza angawine mcp chitukuko chomwe akunena chakulilongwe only ife kuno kuzimba kulibe mcp komweko kulilongwe ife ikabwela mcp ndikudyelani ndalama koma voti zimungathole kd misewu yomwe ukunenayo ilipalipotse kuti mukanika msewu wabalaka to ntchewu
AMALAWI AKUKUGENDANI AMALAWI MUKUNENAWO NDI ATI SOPANO
Zawugalu zenizeni
Chinsiru cha mzimayi ichi
Koma na khani ya misewu adpp imawabaya kwabasi.
Kulibe njanji kumalawi
Kkkkk...koma yah!Mai uyu ali ndi NZERU dzopusa.Koma mukanadziwa Mai,ayi musandilakwitse.
Misewu yo yenda mnyawu
Adamuona kamba kuti sadikula, chitsilu
boma ndilomwali ❤❤❤
Eya zoonadi boma ndilomweli ife tingosintha president basi
Eya tingosota chipani cholamula mcp must go
Maziko ndikupha munthu ngakhale chikhulupiriro changa ndi chofowoka koma ndimaziwa Kuti kumwamba kuli mulungu achimwendo banda muziwe
Koma amabwereka ameneyu chisiru cha zimayi
Komatu mukayakhula zindikilani kuti mawa limafika mulungu si Lazaro
Aaaaa Mcp izawine ndithu kuzakhala nkhondotu njala yake tikudya chitedze
Kabwira wamisala chimwemdo wamisala palibe chazeru chimene akulakhulapo pamusokhano kungokamba za ena basi ndani angabotere tambala wa black wakumudima tizaona yakhulani chilichose chabwera mumutu wanu koma amalawi akuona ndi maso awo 2025 ikubwera
Malankhulidwe awawa mwandilakwitsa dala panyopako mayi osasamba komanso galu iwe Chimunthu Banda chitukuko chake chiti chokuba ndikupha ndikunama
Boma lake liti lingodziwa mfundo zokha pa ground 0 pa 10 mbava zokha
Chitukuko chake cha m'makomo mwanutu masatansm fake government
Ndihule ameneyo alive fundo chifukwa amawafuna apeter kudikula uhule bwasi walowa liti MCP huleyu
Hule ameneyo bwanji kodi akuganiza ngati kuti azawinaso mcp. Osangonena kuti kwinako munaba ndalama iwe ndi hule kwa basi
Azibeans wukuikila kutiko beans yovundayo iwe wamva
Tionana chaka chamawa uzayankhileso after zisankho
Tiwavotera kuti tizadye chitedze, fertilizer 200,000.
Amai awa ndiwopusa zedi.mmene akuvutikila amalawi osamva chisoni
Mai amenewa alezera
Hule kwabasi APM
Kamba yo asanadikule udzayamba ndiwe Jessy Kabwira kudikula mpamene udzadziwe Kuti unatha mawu.
God created heaven and Earth and everything living in it. Dzikoli si la MCP . Udzingodya ndalama za magazi akupasazo.
History is the best teacher.
Mbiri yanu a MCP ngakhale mwana akuyidziwa.
You are Evil 😈👹👹😈🐊🐊
Moti maso mulibe kuti muone zoti takutsikani.
Ajese kabwila anthu akudya nyika inumubweretsa mafuta palinzulu auze bulaani
Lehu iwe
Akulu akulu ngati mwamuonetsetsa azimayi a mcp akumayamba ndi kumwa mowa kokeni ndi chamba Jesse kabwira ndi ena akumapanga ngati osungulira mutu
Kulakhula zakachaso azimayi akachaso amwaso pamenepo
Panyinipako mai iwe ......😂 uzavota ndiiweyo we ll vote 🗳 u ll wait and see
Za ziii
Mayi inu mutu wanu sukugwira ma Rv akudzungudzani
Mulungu akupase moyo wautali galu iwe
Iweo kabwilabwila kaya ndi hule wako umenewo iwe ndichisilu kwambiri hule iwe kwachela amanu agalu inu muonanso 2025 DPP ikubweranso APM our vote ana a satanic inu iwe ndi chakwera wakoyo ndinu dzisilu
𝙸𝚌𝚑𝚒 𝚌𝚑𝚊𝚗𝚍𝚒𝚔𝚞𝚖𝚞𝚍𝚠𝚒𝚝𝚜𝚊 𝚔𝚠𝚊𝚖𝚋𝚒𝚕𝚒, 𝚘𝚕𝚊𝚗𝚔𝚑𝚞𝚕𝚒𝚝𝚜𝚊 𝚝𝚒𝚘𝚗𝚊 𝚗𝚎𝚡𝚝 𝚢𝚎𝚊𝚛, 𝚠𝚎 𝚊𝚛𝚎 𝚑𝚎𝚛𝚎 𝚝𝚘 𝚔𝚞𝚘𝚗𝚎𝚕𝚊
Anyani aku dpp kubwebweta anga ali mtulo
Izi utha kulakwa Mai ochomwitsa okulakwisa
Kod chakwera wapanga chan akukhalira kuba ndalama kupha ndpo wagulisa Malawi palibe wapanga ndpo anthu akufa ndi njara Mai iwe galu iwe
Iwe mayi opusa kwambili pa nyapanu inu mayi
Komaso ukunena kuti mwapanga zitukuko misewu zosezo ndi misonkho ya amalawi zitukuko siza president ayi iwe ndimisonkho ya amalawi palibepo chitukuko cha president mu malawi
Hule wachabe chabe iwe galu et
Azizinyenga choncho ...nde ngt akukufunani bwanji mwabwerako ndi miyala
Oky
Mukuyakhula ngati kuti mulibe ubongo bwanji tikumana 2025 usathe mau kabwira
Yokagwa nayo kumanda ndi ya mcp mboni ndi anthu 9 aja.aliyense anaona yekha.
Chimwendo ndi ( tilembe mchichewa) kompyuta mwava kodi
Mayi uyu amagwa chifufu sabereka ndichisiru cha zimayi. Panyapako wava
ndipo pa ntumbo Pako chabwera
Chimwendo kod zipatala zomwe akumanga achakwera zopanda mankhwala akhala ma gest house zupusa