Chibadwileni Sindinamvepo Dziko Likujudula Ma Passport - Comrade Ntanyiwa

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 4 июн 2024
  • There are rumours that some members of the First Entourage to Switzerland had their visa denied by the Swiss Embassy in South Africa due to the quality of the Malawian Passport. So, On Nyasa VoiceBox, we have Comrade Ntanyiwa commenting on the same.
    Pali mphekesera zoti mamembala a gulu la First Lady kupita ku Switzerland anakanizidwa visa yawo ndi ofesi ya kazembe wa dziko la Switzerland mdziko la South Africa chifukwa cha kachitidwe ka Malawian Passport. Ndiye, Pa Nyasa VoiceBox, tili ndi Comrade Ntanyiwa akufotokoza zomwezi.

Комментарии • 28

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g 21 день назад +2

    Indeed we have the president but we have no leader we need someone to lead our country

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609 21 день назад +1

    M'Malawi Boma tilibe

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy 21 день назад +1

    Kkkk Monika wazionera ekha ..omuperekeza kubwezedwa amalawi akamadandaula kumaona ngati akunama Malawi wanunkha

  • @MilacleSankhani
    @MilacleSankhani 21 день назад

    More fire

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 22 дня назад +1

    Amenewadi ndi akanyimbi man eish!,

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 22 дня назад +1

    Ndipo mulungu atimenyera nkhondo sanati antanyiwa amenewo ayaluke zeni zeni kuti awake pambala mbanda

  • @user-iu6mr5xu6r
    @user-iu6mr5xu6r 2 дня назад

    Pa nkhani imenei ndiganizo langa kuti ndalama za passport ya fec zizilowa mthumba la acipani.

  • @SibwenzaLevisoni-gm6rv
    @SibwenzaLevisoni-gm6rv 21 день назад

    Chilima ndi chakwera ndi mabi enieni MBAVA

  • @BertharrySecurity
    @BertharrySecurity 22 дня назад +3

    Boma ili ndila fake,chinthu ukachita kulanda ndichoncho.boma ili anachita kulanda m,'manja a DPP

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x 21 день назад +1

      Ndipo koopsa zedi, upresident siu group admin, ndimakape.

  • @ShwiiWinesi
    @ShwiiWinesi 21 день назад +1

    Ulamuliro wa MCP ndi wa fake ndichifukwa akupanga zinthu za fake apangiletu c u 2025

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 21 день назад

    Komatu anthu wa simadolo ayi,, ndi anthu opanda nzeru chabe coz anakakhala ma dolo sibwezi ma deal awo akumenyawo akungogwidwa,, zopoila

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 21 день назад

    Ambuye atithandize 😢😢

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 21 день назад

    Boma la mtundu wanji lopang ma passport afeg boma lopanda nzeru

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 21 день назад

    Kumalawi kuli so makhoti

  • @JamesMalango
    @JamesMalango 21 день назад

    Boma lomvesa chisoni zedi mcp

  • @user-oq5rg5mz7q
    @user-oq5rg5mz7q 18 дней назад

    We need to have reader

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 22 дня назад +2

    Anthu onse amene amayankhula pa nkhani za ulamuliro wabwino ali chete pamene Dziko lathu likuyendetsedwa mwa ukatchali chonsecho tili ndi President mdziko,, Chakwera tulani Pansi udindo mwationongera dziko.

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc 21 день назад

    Kumalawi kulibe boma

  • @GrecianWyson
    @GrecianWyson 22 дня назад

    Mr mtanyiwa mumatiyimilila

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v 22 дня назад +1

    Kunkuyu apeza choyankha, crook sasowa choyankhula

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 22 дня назад

    Sheeeeee!!!!!

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 22 дня назад +1

    Achakwela mizimu ya kwiya 😂😂😂😂😂😂😂

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn 21 день назад

    Akulu akulu zoona mpaka zinthu zizitere m'dziko lathu koma tili ndi police and army ?

    • @SanudiJaymofred
      @SanudiJaymofred 21 день назад

      Police ndi army zakumalawi amazionetsa udolo kwa ife tomwe . . Koma kudya ndikunyela basi

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 21 день назад

    Dziko lopusa lomvesa chisoni worst government in Malawian history shame on u chakwela

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 21 день назад

    This Government is fake, mwinanso tingonena kut tili ndi Chifanifani cha Boma,,,,, Chilima unandilakwisa pondiuza kut ndikavotere Boma ili.