Innocent Mutholo On The State of Good Governance In Malawi
HTML-код
- Опубликовано: 28 сен 2024
- On Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo comments on the Court ruling regarding Kalumo's position as Director General of Immigration and Citizenship Services, as well the state of Good Governance in Malawi.
Ku Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo anenapo ndemanga pa chigamulo cha bwalo la milandu pa udindo wa a Kalumo ngati Director General of Immigration and Citizenship Services, komanso za ulamuliro wabwino m’Malawi.
I salute you Mr I mutholo
😢😢😢😢😢
More fire big auzeni kuti apm ikulowaso
Pro Arther Peter Mutharika ndi munthu wanzeru not zi abulutu zili panozi
Ine boma limeneli likundivesa kuning'ina kwambir Mr... Timenyereni nkhondo inuyo pamodzi ndi DC Kalindo kuti anthu ena asakomedwe ndi zomwe angawachitire panoz nda apapa ndi ndale ya nyooo kuti ena aiwale padzana mkukumbuka lero ndipo sangazindikire konse tsogolo lawo... More 🔥🔥🔥 APM bas
Awuzen akanganya amenewa malume!
😢😢😢😢😢
Mmmmmm
ngati kuli kotheka Born kalindo ndi ena nonse mukutiimilila chonde ku mec marthah chizuma uja abwelekoso ku mec
Maulemu
😂😂😂😂😂 voice 😂😂😂😂
Makamaka ma passport kulipila ndrama ndikudzidya ndrama tikuzileza movutika zochita kukongola athu olemela kutidyela ife athu ovutika ndithu adzalilipila ndithu
Peter mutharika boma
More fire more fire Mr muthoro ulemu wanu❤
Apm wooooyeeee!!!!
Tili Pano kuchosa Chakwera pa U President mwayankhula mfundo Mr Game Changer
listern from RSA zipiteso ku mec kukonzedwe akhumbo katchali achokeko pampando
Chakacha mawa kukala ngondo chakwera avuneasa vune akuchoka 2025 agaluwa achokwe sitikwavunaso olokupedwakumen boma likasinda ndikandakona atapedwa sindinga dandauleso eetu💪💪💪chatap agalu
Ndipo mulanduwo si umodzi okhatu oti azayankhewo, ilipo migolomigolo , mitolomitolo ya milandu
President akuononga dziko ,aiwala anasakidwa ndi anthu
Ndi zoona Pali kusiyana kwakukulu si nkhwali zili m'boma lelozi
More fire azasa ndalama zathu
Nde mwati asanza misonkho iiiiii koma sono
Two blind persons will mislead each other vonsequently they will follow into a ditch.
God bless you game change
Thanks God 🙏🙏🙏
Alomwe inu mulilaso 2025 mukhaula simunati chakwela sakuchoka
Mudzafa msanga man
Zaziii
Eya zazii, iwe bweretsa zotethazotu.
😢😢😢😢😢
iyayi innocent mussati DPP ndi APM anali bwino ayiiiiiiii.akuluwaotu anatikwanansotu.onsewa awonnga basi.ukakwatira mkazi osabeleka banja likatha nkukwatira wina nayenso osabeleka baba sumabweleranso ku mkazi wakala uja noooo.APM was sleeping on duty.kambani anthu ena man.again APM has no new blood in his team to run the country.iiiiiiiii nooooo its the same people that massed up last time aaaa man izozo ayiiiiiiii
You don't know what you're talking about, it's better to be quiet than to demonstrate your ignorance.
Amen brother mutholo