Guys Kamlepo ndi One of True democrat ku Malawi kuno tsopano kodi kuzunza mukumuzuza munthu wobweretsa democracy koma kokoliko ndalama zamisonkho yamphawi zakomadi
Collect your phone via the attorneys and high court on releasing it without prejudice and bias. We are praying for you. Ndine kuno ku Great Britain. Yes the late dad Green Ng'oma used to w for Southern Bottles even when they lived in Mzimba before moving to Zingwangwa Blantyre and after ZINGWANGWA THEY MOVED TO ALIMAUNDE AREA 25 LILONGWE. We must all pray for each other and the countries experiencing the political tarmoils.
Ine president wanga ndi Dad Bingu wa mutharika kwa ine sanafe i can see kuti anapanga chani. Kma mbuz zinaz zimangozuza amalawi osalakwa anyway sindili ku malawi kma home is best mbuziyi izaziwa kazachopa pamwambapo
Boma iliri azitsogoleri mitu sikuyenda bwino why still keeping cellphones of Born kalindo and kamlepo why why Malawi President and the Police why can you please change your decisions why.
Uku mkuchikweza amputa olakwika, voice imeneyo ikumveka mwa simple koma ili fire😊
Even neba ku Zambia they know that we don't have president in Malawi
Inu a mcp nenani kuti tonse amalawi tichokemo tifune kolowela muone kuti mudzilanulira ndani?
Mr Kaluwa i appreciate you,,,you a true gentleman a hero,, if it takes you to go back to your past to resolve this chakwera issue so it be,,
Wise man from the North side
You have to take this Government to court for this damage.
Well said, loud and clear
Wise man mr kamulepo ❤❤❤❤❤
Guys Kamlepo ndi One of True democrat ku Malawi kuno tsopano kodi kuzunza mukumuzuza munthu wobweretsa democracy koma kokoliko ndalama zamisonkho yamphawi zakomadi
Am agreed with you
Pipo shud open their eyes
Wise man
Bora ilili tikachotsa chakwera a police ambili akuyenera kuchotsedwa tchito
Politics is dirty game
Chomwe wachiona wankulu atakhala pansi, mwana olo atakwera mumtengo sangachione. Welcome Big
Yooo zilichonchoso 😢
Ndikatundu ameneyu aboma musamutengele masewelo zomwewakambazo ndizoona ndithu
Ask Bakii Muluzi anamtangwanitsa kooopya 😂😂😂😂😂
Collect your phone via the attorneys and high court on releasing it without prejudice and bias. We are praying for you. Ndine kuno ku Great Britain. Yes the late dad Green Ng'oma used to w for Southern Bottles even when they lived in Mzimba before moving to Zingwangwa Blantyre and after ZINGWANGWA THEY MOVED TO ALIMAUNDE AREA 25 LILONGWE. We must all pray for each other and the countries experiencing the political tarmoils.
Kulibedi wamuyaya
Aputa olakwika tu....
Sizitheka mulungu alipo kumwamba osamara
Amen Amen...
Apolice yakhani kuti umuyaya uja udakalipobe kapena ai?
Ine president wanga ndi Dad Bingu wa mutharika kwa ine sanafe i can see kuti anapanga chani. Kma mbuz zinaz zimangozuza amalawi osalakwa anyway sindili ku malawi kma home is best mbuziyi izaziwa kazachopa pamwambapo
Wise man❤❤❤
Deal with them bwana kalua
Amenewo ndie mawu amphamvu mbuzi za police zogwilisidwa ntchito ndi chikangawazo makape amenewo akuti agulidwa ndi mcp gvrt Makamaka mai yolamu nayeso chipawa chosamukhala mutu chija mbuzi ya munthu aziwona makape amenewo mu 2025 wonsewo akathela ku mawulapalibeso kuwakhululukila inshaAllah
Zinazo muzipanga koma za artist fredokiss mukangoesera 😮 malawi tiyatsa mukangopha fredo achinyamata tifafaniza state house
Pambuyo panu bwana..iponden
You fought ngwazi , who are these dogs to fear .
Oh no osat Fredo ayi.Komano kukhetsa Mwazi chifukwa Cha mpamdo Kaya Mulungu amaona amakantha
Zosaesanda
😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Wise man
Boma iliri azitsogoleri mitu sikuyenda bwino why still keeping cellphones of Born kalindo and kamlepo why why Malawi President and the Police why can you please change your decisions why.
I feel ur pain father 💔
Good 👍
Iponden fadah,,,,,
🆓✊
Pena pache MCP tu , mukuonjeza eti!!?? Is this what we wanted? Why why why??
Mcp ikuyenera kuchoka basi ikuzuza athu osarakwa chakwera wakupha ayende basi
Athu akupha abusa wokopha kodi eeeeee athu akumpoto mwasiye mutha ndinu achakwera ndi azanu wood
Awuzeni makapewa adziwe kuti inu madala madala
Chana?? Ayesele
chonde bwelerani muzakale bwana tithane nawo anthu oipawa
Akupa mcp
Ask late kamazu about u
Mwaonjeza English enafe sitimva nde izizo muzilankhulako chichewa chifukwa nzatonse amalawi kuti timve