Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
Penapake gayz mulungu timamulakwila izi vuto nditokha Malawi achina kalindo akhazula kuchikamwa paka kutopa so don't blame god please 😢😢😢😢😢😢😢
Mulungu izizi zoziyanba dalazi Koma akulu akulu tiyeni Pena tizikhala serious Anthu ambiri alankhyladi ndikutopa kunikira ndikutopa nsiyeni Mulungu
Lack of philanthropy and genuine patriotism in Malawi has brainwashed divers leaders into thinking in very negative and limited terms.
Mulungu atithandize
Gwetsaso kwacha
We are cursed as a nation
AAA mavito ku Malawi ochita kwakozawo
Mbaleme iwe wabodza nanga mchifukwa chiyani anthu mukungomanga?
Kunkuyu ndiye palibe zomwe amayankhula bas oyankhulana zake zomunyengelela chakwela kut aziwoneka kut ali mbali yake kubisa chilungamo kut ziko lamalawi bwana sili kuyenda bwino bas kumangokwakopa ndimaboza alibe zelu kunkuyu
Kkkkkk pamenepo ndipamene mungadziwe kuti mcp onse ndi anthu oononga ndipo kulibe Utsogoleri.
IMF must go
Tsogolo logwetsaso kwacha layamba kunukhila a Malawi tili pamavuto akulu
After mutamwanza ndalama zankhaninkhani....
We are not crc as country 😭
Guys tiyeni tidzuke mwa mphamvu coz izizi zitiwonongera Malawi wanthu
Dzuka wekha iweyo zitilipirira fee Ana zimenezo
Corrupt minister
Mulungu atithandiza
Penapake gayz mulungu timamulakwila izi vuto nditokha Malawi achina kalindo akhazula kuchikamwa paka kutopa so don't blame god please 😢😢😢😢😢😢😢
Mulungu izizi zoziyanba dalazi Koma akulu akulu tiyeni Pena tizikhala serious
Anthu ambiri alankhyladi ndikutopa kunikira ndikutopa nsiyeni Mulungu
Lack of philanthropy and genuine patriotism in Malawi has brainwashed divers leaders into thinking in very negative and limited terms.
Mulungu atithandize
Gwetsaso kwacha
We are cursed as a nation
AAA mavito ku Malawi ochita kwakozawo
Mbaleme iwe wabodza nanga mchifukwa chiyani anthu mukungomanga?
Kunkuyu ndiye palibe zomwe amayankhula bas oyankhulana zake zomunyengelela chakwela kut aziwoneka kut ali mbali yake kubisa chilungamo kut ziko lamalawi bwana sili kuyenda bwino bas kumangokwakopa ndimaboza alibe zelu kunkuyu
Kkkkkk pamenepo ndipamene mungadziwe kuti mcp onse ndi anthu oononga ndipo kulibe Utsogoleri.
IMF must go
Tsogolo logwetsaso kwacha layamba kunukhila a Malawi tili pamavuto akulu
After mutamwanza ndalama zankhaninkhani....
We are not crc as country 😭
Guys tiyeni tidzuke mwa mphamvu coz izizi zitiwonongera Malawi wanthu
Dzuka wekha iweyo zitilipirira fee Ana zimenezo
Corrupt minister
Mulungu atithandiza