I'm very proud with this man and I love him so much ,samadzipanga proud ku ma social media moyo wake za family yake ayi ,komanso ngati muthu woti wagwira ntchito m'boma simudzamva any speach ina iriyonseyo ayi , amachita kukhala ngatinso ku Malawiko anachoka koma ayi ,amawonetsa kuti ziii ameneyo amakhala busy kumasamalira zopanga tsogolo la ana ake ,ndi momwe mwamvera apapa za mamphunziro awana ake ,uhule ngati anthu woyimbawa momwe timamvera iyeyu ayi ndithu ,ndimamumva kukoma mkati mwangamu koopsya ada awawa
Ati ku ndale sikoti kuli ndalama zoti ukhoza kuphunzisila ana aaaah ndie kuti zimveke bwanji? Iweyo billy anthu ambili amakuziwila mu music and umaimba bwino and kuimba uku kunapeleka chidwi kwa anthu ovutika kukuika mu m'boma ndi maganizo oti ukhoza kusintha ziko, koma anakaziwa kuti umapanga za moyo wake ndi family koma pa chilungamo ndiwe munthu oipisisa kwambili pa ndale ziko lako sumalikonda wadyela sangatukule ziko.
Ndietu ukayankhula amati ndiwe wa nsanje aaah zichani umakhala umakhala kuti pena ukunena chilungamo. Uyu anthu samamuziwa bwino bwino coz sanakhale nae , amamuziwila mu nyimbo and kwa ine ku nyimbo amaimba bwino mumakhala nfundo , koma kumuonesesa amapanga za family not ziko ndi munthu oipa kwambili
I'm very proud with this man and I love him so much ,samadzipanga proud ku ma social media moyo wake za family yake ayi ,komanso ngati muthu woti wagwira ntchito m'boma simudzamva any speach ina iriyonseyo ayi , amachita kukhala ngatinso ku Malawiko anachoka koma ayi ,amawonetsa kuti ziii ameneyo amakhala busy kumasamalira zopanga tsogolo la ana ake ,ndi momwe mwamvera apapa za mamphunziro awana ake ,uhule ngati anthu woyimbawa momwe timamvera iyeyu ayi ndithu ,ndimamumva kukoma mkati mwangamu koopsya ada awawa
Nyimbo Za billy Kaunda yemwe samazikonda Ali ndi nsanje
Munthu wamkulu kwambiri , A bwana ozichepesa kwambiri . Inuyo big ,God bless you .
kuphudzitsa Ana mopereka chidwi kwa anthu omvera ndikutha kuona kuti palibe mphwepwa mwa Ana onse
I thank God I was part of your generation as well as your music, we are blessed by your art
BK my legend... We love you honourable here in Zambia. Your music is so classic.
Ulemu wanu Mr billy ndimakunyadirani kwambir ❤❤❤
Ndine emweuja,my favorite song
Opanda mbiri yoipa Billy kaunda pitilizani kukhala munthu wa bwino achimwene ❤❤❤❤❤ from Capetown
❤❤ precious
My favorite artist n the role model himself
I like Billy Kaunda mainly the number NALIYERA
Ndiye emwe uja… watching in the States.
onabo bile mkaunda voice very nice ❤❤ Mr. nkhumani
Eeee iwe phe ameneyu timadziwa kuti ndinu biggy Inu🔥
Ndangosilila maphudzisidwe a ana ooo God bless you big and humble man
two
My favourite musician Bill Kaunda
Billy u stil young boy lv ur music
❤❤❤watching from south Africa sand
The old legend still lives on.
Munthu wodzichepetsa kwambli ndiyamba kumvela nyimbo za billy kaunda mucha 1999
Big respect to Billy kaunda 💚🇲🇼💪
Oyimba opanda matukutuku God bless you
Few seconds into the interview and yep. Great voice from the host
A classmate timakunyalani
May God bless you all the time
Zikomo kwambiri oyimba yemwe sanavekepo ndi nkhani zanyasi ndi Billy kaunda ndipo ndioyimba okhazikira pa luso lake timakunyadirani malume k
Mwacheza ndi Munthu wa bwino uyu kwambiri
Ndi big man pophunzitsa Ana ake sukulu
I like that guy so much
Munthu odekha ndi dzeru zache ,I really like him, with his songs too
I remeimber when I was a kid pa chiwembe
Cool man yoh ilove the personality
I like your songs MR
Well done Mr BK, we love you more
How can i access the book "Hills and Valleys"'?
THIS MAN IS CALM.
The best
Bless you Bro
Ati ku ndale sikoti kuli ndalama zoti ukhoza kuphunzisila ana aaaah ndie kuti zimveke bwanji? Iweyo billy anthu ambili amakuziwila mu music and umaimba bwino and kuimba uku kunapeleka chidwi kwa anthu ovutika kukuika mu m'boma ndi maganizo oti ukhoza kusintha ziko, koma anakaziwa kuti umapanga za moyo wake ndi family koma pa chilungamo ndiwe munthu oipisisa kwambili pa ndale ziko lako sumalikonda wadyela sangatukule ziko.
Ulemu wanu Mr presidente 🙏🙏🙏🙏
Very inspired ❤
Very humble man ❤
Mawu a billy kaunda takumbuka amalawitonse
Ahhhh mwakafupikisatu abale
Legend
Amandidalisa kwambili wakwanthu kupoto ndine symon phetera munthu imozi amandisangalatsa
Aaaa nde kachepatu ka inteviewko
Nice 🔥
Humble mn ❤❤❤❤❤
A humble Man
Our new MP
Cool man
Abily timakunyadirani mwasinthisa zambiri mziko muno
Ndi oimba yemwe sayangana pansi pa nyimbo zake ,.. amatha
Uli boh bily
Humble man
Master
It is his music career not carrier.
Awawa kungowataya basi palibe angamasule zingwe Nsapato zawo
Timati Mzimba osati Nzimba😮
50+ koma looking fresh...
My man.
Zazelu basi
Wa akulu tsopano timakunyadirani mumatha.
In politics ku Blantyre palibe chomwe tingaloze chomwe amapanga chothandiza
Ndietu ukayankhula amati ndiwe wa nsanje aaah zichani umakhala umakhala kuti pena ukunena chilungamo. Uyu anthu samamuziwa bwino bwino coz sanakhale nae , amamuziwila mu nyimbo and kwa ine ku nyimbo amaimba bwino mumakhala nfundo , koma kumuonesesa amapanga za family not ziko ndi munthu oipa kwambili
mwimbanga makola akulu tingateta yayi
Oh koma wabeleka
Ana sachuluka man🔥
Komatud makolo anu anabeleka mpaka ana 11,,ayi ntchito anaigwira
Nthawi inachepa koma.
Munthu ozichepesa kwambiri komaso wanzelu
Billy uli ndi Ana 7 ine ndiri ndi 8 ndichitsomo cha namalenga
Sikefa chimoto
Koma nde unasosolatu man, ana 7 alone?, kkkkkkk
Amavuta kuphunzira ndi kulela osati kubeleka kkk
Kwabac
I love this man,and i wish him to contact me (please got your message).