GURU LINA LONYASIDWA LAWOPSYEZA A PRESIDENT CHAKWERA LERO KUTI ACHOTSE PA MPANDO A ZIKHALE NG’OMA

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 24 окт 2024

Комментарии • 51

  • @jacomw5797
    @jacomw5797 2 месяца назад +7

    Kunkuyu amazitenga dolo poyankhula while ku immigration zinthu sizikuyenda

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 2 месяца назад +6

    Kumkuyu iwe galu kwabas iweso ukuyenela kuchoka sutha ntchito ai mbalame yenyen gwape

  • @Yoxym
    @Yoxym 2 месяца назад +3

    Achoke 💪💪💪💪💪💪💪💪

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 2 месяца назад +2

    akunkuyu ndi a chakwera chonde muwuzane kuti pantumbo pa chamanu zitsiru za anthu lino ndi dziko kapena mudzi wakwanu boma la zitsiru zokha zokha

  • @BenjaminKamanga-p8w
    @BenjaminKamanga-p8w 2 месяца назад

    Anthu sakuziwa zimene akufuna it's straight forward isue chajwera achoke basi

  • @AaronMsewezi
    @AaronMsewezi 2 месяца назад +1

    I think the problem we have with our president is , ali soft kwambiri , and ali ndi chifundo kwa even ma ministers ,so chimene ayenera kuziwa church ndi dziko ndi zosiyana ,Iwo asamanyengerere munthu Kaya akuoneka bwanji,

  • @amosmuluwane4182
    @amosmuluwane4182 2 месяца назад +1

    Azimaywa amazipangitsa okha akasankhidwa palibe chomwe amachita mwachitsazo phungu wa ncheu bwanje North akhala paunduna zaka zonsezi koma dela lake ndilovesa chisoni pamudzi omwe amachokela mayi amenewa school idasasuka denga Chaka chatha koma mpaka panopa school iyi sinakhomedwe amene mumadutsa pamudzi wa akaiya kupita ku balaka kapena kugolomoti mundivomeleza phunguyi ndi nase chaola ndoko

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 2 месяца назад

    Apm akubwera kudzakonza dzikoli tazunzika mokwana 4yrs ngati 400 yrs?

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 2 месяца назад +1

    Achosedwe watikwana galu ameneyo even chakwera achokeso sitifuna .. futso koma zikhale ng'oma azalola kuti achoke si nankha mcp yakwawo nankha kkk

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON 2 месяца назад

    😂😂😂😂 ndalama kulibe nanga zomwe akuba m'boma akuba kkuti ndalama zoooooo tatiwuzani

  • @ChristopherMakamo-ky4pq
    @ChristopherMakamo-ky4pq 2 месяца назад +3

    Apule achoke basi

  • @PanganoChilambe
    @PanganoChilambe 2 месяца назад

    Ok, kondi munthu angapite kusuku ya ukachenjede asanate ku pulaimale? izo ndindale zaku Malawi mukafu kupitiriza kumba mumatenga omphunzira amenewa why thandinzo yanuyo siyambe muchipatara olo kundende,ku pulaimale? Osatimvetsa mutu ife Malawi timudziwa musateye ndalama zoti ana amasiye asamalike ndeye nkhumbo langa ngati Malawi. Koma ndati mudziwe kuti mawa silero.

  • @SolomonAmiduh
    @SolomonAmiduh 2 месяца назад

    Keep it up comrades atule pansi udindo

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi 2 месяца назад +1

    Chikangawah party ichoke basi

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf 2 месяца назад

    Vuto si zikhale ng'oma koma galu uyu otchedwa Chakwera tiziti iyeyu sakuona kuti immigration zinthu sizikuyenda contract angapereke kwa mwana wake Chenjela Nick ndi makutu akowo okhala ngati bowa masiku akuthera mbuzi iwe

  • @MirriamKambale
    @MirriamKambale 2 месяца назад

    Boma mpaka kumapanga passport ya feki?Nigerian mmodzi kumaposa boma la malawi?coz feki passport yopangidwa ndi Nigerian individual ilibwino kuposa yopangidwa ndi boma la Malawi.

  • @VictoriaWilly
    @VictoriaWilly 2 месяца назад

    Kunkuyu nayenso achoke, onse achoke akuononga dziko la Malawi. Tatopa ndi boma labodza ili

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 2 месяца назад

    Koma pamenepa pothandiza school President Chakwera timuyamikire osamangosusa zili zonse chifukwa cha ndale pena zabwino kumayamika so zonse munthu sangakhale 100%

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 2 месяца назад +2

    boma la zitsiru zokha zokha ili zigawenga

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 месяца назад +3

    Ma passport a fake a Nic Chakwera

  • @JohnsonMaulana
    @JohnsonMaulana 2 месяца назад

    Enanu mkumat boma nd lomweli kma likulephera kukonza zinthu shame😢

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 2 месяца назад

    Ayende basi aaaa atikwan

  • @KawawaIbrahim
    @KawawaIbrahim 2 месяца назад

    Kodi chifukwa chani maudindo kumangopasana anthu oti saziwa ntchito

  • @Dickies-mk8cd
    @Dickies-mk8cd 2 месяца назад

    Ufune oti uwapusitse Chakwela wamva

  • @WarriorKB-u3k
    @WarriorKB-u3k 2 месяца назад

    Chakwerayonso achoke palibe chichita iye panopa chilichonse ndichosokonokera

  • @DixonChimanya
    @DixonChimanya 2 месяца назад +2

    A CDED please now take things seriously
    Please we are suffering like God created people from to suffer

  • @PatrickChagaka
    @PatrickChagaka 2 месяца назад

    Awatu palibe chomwe akupanga boma lawoli onse ndizitsiru zokhazokha zikhaleyo sangasokoneze zinthu payekha alipamodzi

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 2 месяца назад +2

    Kamajekete apite 😮

  • @DalitsoAlufeyo
    @DalitsoAlufeyo 2 месяца назад +3

    Ndipo zoona

  • @watsonmhango8794
    @watsonmhango8794 2 месяца назад

    Boma la Chakwera zavuta ndithu 😂😂😂😂😂

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 2 месяца назад +1

    Bora pamenepo achokedi saziwa ntchito amalawi tikuvutika

  • @MosesMkandawi-e2v
    @MosesMkandawi-e2v 2 месяца назад

    Palibe chomwe akuchita zikhale ng'oma pakuti iye ndi chakwela ndi zigawenga nde akuba okhaokha safusana kuti chithu ichi wachitenga kuti pomwe ose ndi akuba,,, koma chomwe amafusana ndikuti kodi ichi unakaba kuti bas,, ndee chakwela sangamuchotse zikhale ng'oma pakuti zonse zimene akupanga iye amapanga limodzi ndi chakwela Kuba kupha katangale akupangila limodzi

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 2 месяца назад +2

    Achoke kamajeketi zikhale Ng,oma foseki Thabo chakaka nayeso alibali ya MCP sakutithandiza ayi nayeso foseki

  • @NosparPalamelagee
    @NosparPalamelagee 2 месяца назад

    Iweso kumkuyu uchoke

  • @JamesGondwe-l6b
    @JamesGondwe-l6b 2 месяца назад

    Boma, limapanga chidodo kwambiri, pop anga ziganizo.

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 2 месяца назад

    Musanapange upload muzimvera kaye zinthu zanuzi, this is very unprofessional.

  • @MarthaBango
    @MarthaBango 2 месяца назад

    Anthu amatopatu amafika poti topi 😂😂😂😂

  • @HamanjaManyela
    @HamanjaManyela 2 месяца назад

    Achoke kumene

  • @thomasbodo4099
    @thomasbodo4099 2 месяца назад +2

    Boma lalephera so mkuyu asamati president razarus mphamvuzo tinangomubwereka osati adzitumbwanazo apa

    • @JafalihMitawa-u2d
      @JafalihMitawa-u2d 2 месяца назад

      Mmmh nawesotu uzilankhula bwino wava, alindi mphanvu basi Chakwela.

  • @LasieMolebatsi
    @LasieMolebatsi 2 месяца назад +1

    Anyamuke

  • @PatrickMailos-j6u
    @PatrickMailos-j6u 2 месяца назад

    Athutu amanena kuti mcp sizithu

  • @AllieJonassi
    @AllieJonassi 2 месяца назад

    Achakwela awombeledwe

  • @JoshTech-h4r
    @JoshTech-h4r 2 месяца назад +1

    😂 ndpo live

  • @kingthymus4613
    @kingthymus4613 2 месяца назад +1

    makosana😋😋😋😋

  • @adamabiyen5079
    @adamabiyen5079 2 месяца назад +1

    Bolan pamenepo