I think the problem we have with our president is , ali soft kwambiri , and ali ndi chifundo kwa even ma ministers ,so chimene ayenera kuziwa church ndi dziko ndi zosiyana ,Iwo asamanyengerere munthu Kaya akuoneka bwanji,
Azimaywa amazipangitsa okha akasankhidwa palibe chomwe amachita mwachitsazo phungu wa ncheu bwanje North akhala paunduna zaka zonsezi koma dela lake ndilovesa chisoni pamudzi omwe amachokela mayi amenewa school idasasuka denga Chaka chatha koma mpaka panopa school iyi sinakhomedwe amene mumadutsa pamudzi wa akaiya kupita ku balaka kapena kugolomoti mundivomeleza phunguyi ndi nase chaola ndoko
Vuto si zikhale ng'oma koma galu uyu otchedwa Chakwera tiziti iyeyu sakuona kuti immigration zinthu sizikuyenda contract angapereke kwa mwana wake Chenjela Nick ndi makutu akowo okhala ngati bowa masiku akuthera mbuzi iwe
Boma mpaka kumapanga passport ya feki?Nigerian mmodzi kumaposa boma la malawi?coz feki passport yopangidwa ndi Nigerian individual ilibwino kuposa yopangidwa ndi boma la Malawi.
Koma pamenepa pothandiza school President Chakwera timuyamikire osamangosusa zili zonse chifukwa cha ndale pena zabwino kumayamika so zonse munthu sangakhale 100%
Palibe chomwe akuchita zikhale ng'oma pakuti iye ndi chakwela ndi zigawenga nde akuba okhaokha safusana kuti chithu ichi wachitenga kuti pomwe ose ndi akuba,,, koma chomwe amafusana ndikuti kodi ichi unakaba kuti bas,, ndee chakwela sangamuchotse zikhale ng'oma pakuti zonse zimene akupanga iye amapanga limodzi ndi chakwela Kuba kupha katangale akupangila limodzi
Kunkuyu amazitenga dolo poyankhula while ku immigration zinthu sizikuyenda
Kumkuyu iwe galu kwabas iweso ukuyenela kuchoka sutha ntchito ai mbalame yenyen gwape
Achoke 💪💪💪💪💪💪💪💪
akunkuyu ndi a chakwera chonde muwuzane kuti pantumbo pa chamanu zitsiru za anthu lino ndi dziko kapena mudzi wakwanu boma la zitsiru zokha zokha
Anthu sakuziwa zimene akufuna it's straight forward isue chajwera achoke basi
I think the problem we have with our president is , ali soft kwambiri , and ali ndi chifundo kwa even ma ministers ,so chimene ayenera kuziwa church ndi dziko ndi zosiyana ,Iwo asamanyengerere munthu Kaya akuoneka bwanji,
Azimaywa amazipangitsa okha akasankhidwa palibe chomwe amachita mwachitsazo phungu wa ncheu bwanje North akhala paunduna zaka zonsezi koma dela lake ndilovesa chisoni pamudzi omwe amachokela mayi amenewa school idasasuka denga Chaka chatha koma mpaka panopa school iyi sinakhomedwe amene mumadutsa pamudzi wa akaiya kupita ku balaka kapena kugolomoti mundivomeleza phunguyi ndi nase chaola ndoko
Apm akubwera kudzakonza dzikoli tazunzika mokwana 4yrs ngati 400 yrs?
Achosedwe watikwana galu ameneyo even chakwera achokeso sitifuna .. futso koma zikhale ng'oma azalola kuti achoke si nankha mcp yakwawo nankha kkk
😂😂😂😂 ndalama kulibe nanga zomwe akuba m'boma akuba kkuti ndalama zoooooo tatiwuzani
Apule achoke basi
Ok, kondi munthu angapite kusuku ya ukachenjede asanate ku pulaimale? izo ndindale zaku Malawi mukafu kupitiriza kumba mumatenga omphunzira amenewa why thandinzo yanuyo siyambe muchipatara olo kundende,ku pulaimale? Osatimvetsa mutu ife Malawi timudziwa musateye ndalama zoti ana amasiye asamalike ndeye nkhumbo langa ngati Malawi. Koma ndati mudziwe kuti mawa silero.
Keep it up comrades atule pansi udindo
😂😂😂😂, Achoke Achoke!
Chikangawah party ichoke basi
Vuto si zikhale ng'oma koma galu uyu otchedwa Chakwera tiziti iyeyu sakuona kuti immigration zinthu sizikuyenda contract angapereke kwa mwana wake Chenjela Nick ndi makutu akowo okhala ngati bowa masiku akuthera mbuzi iwe
Boma mpaka kumapanga passport ya feki?Nigerian mmodzi kumaposa boma la malawi?coz feki passport yopangidwa ndi Nigerian individual ilibwino kuposa yopangidwa ndi boma la Malawi.
Kunkuyu nayenso achoke, onse achoke akuononga dziko la Malawi. Tatopa ndi boma labodza ili
Koma pamenepa pothandiza school President Chakwera timuyamikire osamangosusa zili zonse chifukwa cha ndale pena zabwino kumayamika so zonse munthu sangakhale 100%
boma la zitsiru zokha zokha ili zigawenga
Chikangaws😂😂😂
Ma passport a fake a Nic Chakwera
Enanu mkumat boma nd lomweli kma likulephera kukonza zinthu shame😢
Ayende basi aaaa atikwan
Kodi chifukwa chani maudindo kumangopasana anthu oti saziwa ntchito
Ufune oti uwapusitse Chakwela wamva
Chakwerayonso achoke palibe chichita iye panopa chilichonse ndichosokonokera
A CDED please now take things seriously
Please we are suffering like God created people from to suffer
Awatu palibe chomwe akupanga boma lawoli onse ndizitsiru zokhazokha zikhaleyo sangasokoneze zinthu payekha alipamodzi
Kamajekete apite 😮
Ndipo zoona
Boma la Chakwera zavuta ndithu 😂😂😂😂😂
Bora pamenepo achokedi saziwa ntchito amalawi tikuvutika
Palibe chomwe akuchita zikhale ng'oma pakuti iye ndi chakwela ndi zigawenga nde akuba okhaokha safusana kuti chithu ichi wachitenga kuti pomwe ose ndi akuba,,, koma chomwe amafusana ndikuti kodi ichi unakaba kuti bas,, ndee chakwela sangamuchotse zikhale ng'oma pakuti zonse zimene akupanga iye amapanga limodzi ndi chakwela Kuba kupha katangale akupangila limodzi
Achoke kamajeketi zikhale Ng,oma foseki Thabo chakaka nayeso alibali ya MCP sakutithandiza ayi nayeso foseki
Iweso kumkuyu uchoke
Boma, limapanga chidodo kwambiri, pop anga ziganizo.
Musanapange upload muzimvera kaye zinthu zanuzi, this is very unprofessional.
Anthu amatopatu amafika poti topi 😂😂😂😂
😂😂😂😂😂
Achoke kumene
Boma lalephera so mkuyu asamati president razarus mphamvuzo tinangomubwereka osati adzitumbwanazo apa
Mmmh nawesotu uzilankhula bwino wava, alindi mphanvu basi Chakwela.
Anyamuke
Athutu amanena kuti mcp sizithu
Achakwela awombeledwe
😂 ndpo live
makosana😋😋😋😋
Bolan pamenepo