Mudziko Muno Mulibe Chitetezo Phalombe Big Boy
HTML-код
- Опубликовано: 18 окт 2024
- On Nyasa VoiceBox, Phalombe Big Boy asserts that Malawi is not secure. He made this statement after a soldier was allegedly attacked by thieves within the boundaries of Cobbe Barracks in Zomba.
Pa Nyasa VoiceBox, Phalombe Big Boy wanenetsa kuti dziko la Malawi silili bwino. Iye wanena izi msilikali wina yemwe ati anamenyedwa ndi mbava m’malire a Cobbe Barracks ku Zomba.
#malawi
Ife a Malawi timaombeladi mmanja zinthu zopusa ❤❤
U continue playing with history God bless you
Wangalula big boy
Mukamachula kuti alhomwe mulibe nzeru usamsleee wamva wanyau iwe upole moto wamva ukapitiriza muona pole,, big boy goes on,, asirikali zofuna zawo Mesa amaderera mukamawauza,, iwo ndiodziwa akuti akusata malamulo
We are really not safe in this country ❤❤❤
Walakhula bwino big boy
Dziko LATHU silinaopsepo ngat panopa dziko LATHU njala kuphedwa anthu ziwembu katangale,God help Malawi muphuleni Malawi pamoto.
Mmmmuwuzeni kuti sitikudya mafuta a petrol ife koma so misewu sitinga dumphe pasewu ndinjara zopusa mabweya amake mafiah yoooooo mr chikangawa yooo 😂😂😂😂
Please MDF, chitanipo kanthu pazomwe zachitika ku Cobbe barracks.
Usamati munthu wina wagura mifuti tchula straight kuti chakwera wagura mifuti wagawa kwanyamata ake
Amene amatsutsawo nde kuti amadya nawo ndlama za mcp
Achiya bwino aakuba amenewo, bde mawa kunsewu
Zoona zake ife amalawi tilimumavuto kwambiri ameneyo achoke tisalolere amalawi kumuvotelaso achoke basi
Ndipo chakwela sitizamuiwala mu mbili ya Malawi koma chimwe ndimava nacho chisoni athu akuvutika kwambili kuno ku Malawi ambuye atithandize ndithu
Zoona big
MDF operation ija bwa ,munaichita 199..Pagani changu.
Ndipo he is no more
Ndipo live munthu uyu satana kwambiri mr chikangawa
Mkulu ameneyu ndi ogona eti munsewu amadutsa olemera okha Chilomwe chikumuyabwa eti?
☹️☹️☹️☹️ koma ndilibe mau dziko lamalawi 🤔
They don't have a love for each other
Malawi watani aliyese akasowa ndiwo kuthamangila pa media kubwebweta zopanda mutu
IZI SI ZODUKA MUTU NAWENSO UKUFUNA KUNENACHANI IWEYO CHIBADWIRENI UNAYAMBA WAMVAPP KUTI MSILIKALI WAPHEDWA NDI ACHIWEMBU KOKHALA KU BARACKS? LERO CHACHITIKA NDICHIYANI CHITETEZO KULIBE KUNENE MUSATSUTSE CHIFUKWA CHOTI MWADYA ZA MCP
Inu ngat ndinu a MCP please shut up your mouth tisanaku lakwile wava
@@ChristopherKawilam iweyi wakuuzakiti ndine wa MCP NDINDANI sindipanga zandale ine ndiyekuti iweyo ndamene sunamve message yanga uyambitenso KUWERENGA komaso iwe sungalakwireine uzilakwirawekha ase ndipo ine sindinyunwitsidwa NDIMUNTHU uone ma sms angaomkachikena then uyambitenso kuyankha zikuonesakuti wathamanga kuyankha usanamve
@@HalisonSolomon Koma Sina pange reply comment yako tuu
Zoonadi Big
Ukunena zoona palibe choyimbila manja kubwera kwa mafute pa stima koma mafutawo osasika anthu awa ndi afiti
A Malawi ndi anthu opusa kwambiri zitsiru zeni zeni za anthu
Anthu auleso kukonda kulongolola ndikutukwana basi. Musauka ndipo mukhaula
LERO NDIYE AZIONATU ASILIKALI CHIFUKWA CHOTI NAONSO SAKUMVA ASANKHA KUGWIRA NTCHITO NDI CHIPANI LERO ZAYAMBA KUWAVUTA OKHA
Komanso Asilikani amalawi anagona kwambiri panopa sizikuyenda ndithu
Ai ndithu takumvani
Anthu ndiopusa akumapitabe kunsokhano wa mfitiyu
Palibe chobisika,tonse tinadziwa kut siwakuba ,Koma ndiotumidwa,zigawenga Za boma.God knows
Sure sure correct
Tidasankha molakwikathu pano tikulira
Misewu komweko kulilongwe kokha nde asati sokosere
Alomwe ndinu mbuzi zawanthu mcp 2025 boma musobva
Yaa
Mhuzi ndiweyo galu a kobe barack aphana okha okha ndiponso 20 million singakwanitse anthu 20 million kod School yake iti ? Imene munaphunzira zimenezi
NKHANI IYI SIYOPITA NAYO KUTALI ANTHUO ANACHITA KUTUMIDWA NDI BOMA ZOSATHEKA MUNTHU WAMBA KUKAFIKA KU BARRACKS NDI ASILIKALI OMWEO ANATUMIDWA MWINANSO AKUFUNA KUBISA UMBONI WA KU CHIKANGAWA
Ndipo straight