Vuto ife ngati amalawi eni eni timaopa kulowa ku ma demo koma kulankhula pakamwa thoooo boma la manyi ili likadali kupanga zinthu mwa manyi enieni kodi vuto ndi chani kwenikweni mantha
❤❤❤ all malawian don't give up be strong enough Allah will help us malawian for fight inshaa Allah Support come from here south Africa love you all malawian ❤❤❤❤❤ game is over mr president
Asakheleso mademo Ake ophempha, boma ili siloliphempha mademo chomwe tikufuna chakwala atule Pasi udindo
Go konkoooooooooooooooo,,,, wapolisi samala. Moyo wako ngofunikira kwambiri ndiye udzipatse ulemu wekha
Mademo aketu tikufuna enien omwe tikapange not zongpchedxa zomwe zakhala zuchitika mbuyomu, tikufuna Mademo ngati omwe akuchitika ku Kenya 🇲🇼💪💪💪
Achoke achoke anati ronjeza kt ndika rephera kukwanisa zomwe ndaronjeza ziko ndizatura pansi udindo ndiye apa paribepo vuto kupanga mademo chifukwa anaronjeza ziko ndiye zomwe anati ronjeza paribe or chimozi chot tingaroze just go to kasiya man
Chakwera atule pansi mokakamizidwa don't ask him to resign but we want him to quit by fire by force 😳
Tatopa ndi Chakwera Malawi wathu wawola ndithu achike basi galuyu kayafa
Tili pambuyo
Bola osamangokamba apa then muzizalepheresaso kupangitsa 😡
💪💪💪💪
Tili nanu limodzi guyz
Komanso palibe ku perhaps fziko ndi Kathy si la chakwela
Goh komkoooooooooh
Edward kambanje power of speech Achoke galu amaneyo we don't won't chakwera mbudzi yachabechabe
Vuto ife ngati amalawi eni eni timaopa kulowa ku ma demo koma kulankhula pakamwa thoooo boma la manyi ili likadali kupanga zinthu mwa manyi enieni kodi vuto ndi chani kwenikweni mantha
Ndipo imeneyo ndimadandaula poona aMalawi amangokhala osafuna kupitako ku ma demo ndimadandaula kwambiri timaiwala kuti zinthu tisinthe zimafunika kutengqpo Action thru ma Demo
Zoonadiitu osafookayi chakwelandi mbudzi kobasi
Mademo akumalawi amakhala amasewera, maiko anzathu sachita kupempha chilolezo kwa dc amangochita basi,mukundiuza kuti mademo omwe akuchitika ku Kenya anakatenga chilolezo chochitila mademo? Amalawi turo 2much moti malawi yemwe wavutilamu tidikile mpaka 2025? Tiyeni amalawi tipite pa msewu mwaunyinji Chakwera ndi nduna zake zonse zitule pansi udindo basi enough is enough
Go konko Malawi siife amantha osaopa osafooka osapepesa ❤❤
Chakwera azachoka pampando mowawa kwambiri. Zizakhala zoipila kuposa mmene Peter Mutharika adachokela
Chakwera atule pansi udindo alephera kuyendetsa dziko ndipo ndikuchita kuona kuchedwa pa 10
Dandaulo langa kwa aMalawi please tiyeni ku ma Demo mwaunyini kuti Chakwera achokepo
Osawapempha absolutely ndiachamba aboma
Ifenso kuno ku cape Town city tilipo group pano tilowe pa sewu
Mall fire 🔥🔥
By fire by force chakwe must gooooooooo!!!!!!!!!!!!
🫡🫡🫡🫡🫡🤝🤝💪💪💪
💪💪💪💪💪
👊👊👊👊👊👊👊💪💪💪
Tiyeni komko
💪💪💪💪💪💪💪
Tiyeni Tiyeni Tiyeni
Zazii masatanic inu mkuwona mmene anthu afela kukenya poti masananic ngati pafa anthu inu mmasangasalala pephelo langa ndilakuti mkafe ndinuyo osati anthu wapa ambuye alowrlelepo kuti mkafe ndinuyo mmangoyambisa zipolowe inu mmathawa msakathawe ndipo tisave kuti anthu wamba amwalila kumeneko mmene mnayambila sitikuwonapo phindu tikungowona majelasi
Iwetu wadya zambiri koma ukunama anthu sangakumvele namapwala iwe m'mene ulili moyo pano ukusiyana chan ndikufa
Ukuganiza kut anthu angamvele kapolo ngat iwe ndikukusaka step by step ma comments ako ukupanga zosemphana ndi generation
Usaza ndalama zimenezo
Chisiru iwe, mbuzi
❤❤❤ all malawian don't give up be strong enough Allah will help us malawian for fight inshaa Allah
Support come from here south Africa love you all malawian ❤❤❤❤❤ game is over mr president
Powerful!!!!! Forward ever and backward never
Pa 10 kwatalika kwambiri
Inde
🎉
Kunena zoona ku mademo sikukhala malonda ,chimenecho chibwana cha mchombo lende
Komatu mdala uja anakuuzani kuti ngati mufuna kubwerera m'mbuyo musankhe a lerowa. Munasankha. Ajawo anapanga zionetsero potapa mphamvu zaku mdima, chifukwa amaononga zinthu pamene nkhani yao inali kubwlo la milandu. Inuyo simuononga?