Mkwabwino koposa KT mauthenga a MMA foniwo aponyedwe pa social media coz kupitisa Kwa awo akafukufuku, kupangitsaso Kuti chilungamo chibisidwe coz we never know Kuti akafukufuku wo mwawadyetsa kale but we need the truth
kunkuyu ndiwe galu ndipo nyani otheratu uyang'ane kumwamba komanso uzifunse ukagona usiku wekha kuti kodi zikachitika zimenezi kwa my brother are you going to be silent? stuoif of all stupidity bciz of money unapghanso witika coz of chibwenzi mbuzi galu pusi nyani iweee
You know that we know for what you did,where are the brave soldiers of 1992 of operation bwenzani, to take over this country. Burkina Faso is doing well with soldiers
iwe kunkuyu palibe cha nzeru kwa inr moti idont notice that theres someone existing in malawi so called kunkuyu next it will br someone wjo is still alive like you sorry to say this
Tell kunkuyu why not even one member of Mcp involved Where is a black box Why taking many hours to tell public Where are the gadgets of deceased Why is the rader missing Who was searching the bodies Why the president suspended the seach We need best answers
Guys what should be done? they can't asnwer questions because they know what they have done as long as they still on powerful seat, asking them brings no solution, only People needs to you unite and discuss the permanent solution. That's it otherwise all these are giving rhem away to come out and hide all information. Let's stand and fight the rights of Malawian
Athuwa akuziwa chomwe chinachitika even ma parachutes munalibe mu ndegemo kodi after emergency thing like this angwirisile tchito more over ndege ya asilikali a boma
Sizoona zimenezo zoti anthu alowetsapo ndale ,Koma anthu akumva kuwawa kwambiri
Akulu inu musaoneke ngati dolo poyakhula just weit iwenso ulipa list yoti ulangidwe sharia low oyipa iwe hope nga khumba chonch
Koma iyeyo akudziwa kuti adzafaaa ndanzakewo
Chakufwa Chihana once said and quote " Kambuku ndi kambuku basi, sangachoke sidyalina nkusanduka fisi ayiii" MCP showing it's true colors
Akhukuyu nanuso zinazi muzikana anthu sangakulipilire inuyo chifukwa cha mfuti yanu inapha Alan witika ija mu chipasa ulemu chipani chanu mcp singawine kamba ka inu anthu inu atidwe nawo
Apwanga mulimva dziko likutembenukirani
Mwaphera tsogolo ana aeni Ake ndipo mtendere uzakusowani Moyo wanu onse
Good Explanation from Hon.Moses Kunkuyu.Mwayankhula bwino kwambri
Mkwabwino koposa KT mauthenga a MMA foniwo aponyedwe pa social media coz kupitisa Kwa awo akafukufuku, kupangitsaso Kuti chilungamo chibisidwe coz we never know Kuti akafukufuku wo mwawadyetsa kale but we need the truth
Apeleke koyenera kutiko ndiye inu simufuna kuzivesera zimenezo akalakhura mndegemo mkufuna tivere zanu osati eni ovakupwetekedwawo chifukwa ndamene amawona zmene zikuwachitikira, yudas chenjera uzikhweza ndichingwe ngat wadyesedwa chibanz
Aaaah kuyankhula Mwantudzutu uku please
mulungu anarenga kumwamba ndi dzikorapasi kodi chifukwa nyumba yanu imakhara ndi pira ndichiyani muthu ariyese amabitsa chisisi koma ngati ariyenga wosati awiri satana ndiwabodza mulungu achita yekha chirungomo chilima wachita ku pangibwa chipogwe
Akufotokoza zomwe zimachitika mundege koma zinthu zopanga record za mundege zinasowa.
kunkuyu ndiwe galu ndipo nyani otheratu uyang'ane kumwamba komanso uzifunse ukagona usiku wekha kuti kodi zikachitika zimenezi kwa my brother are you going to be silent? stuoif of all stupidity bciz of money unapghanso witika coz of chibwenzi mbuzi galu pusi nyani iweee
mwawagila achibalewo abale a chilime a mcp musatitanamizre
Ndikungova chinyengo chokha chokha, chilungamo chiwoneke basi, enawa adyesedwa chibanzi,
Iwe ndiye uti akumkuyu ndinu omveza chisoni kwambili kunyasa khopeko zikukukhalani ndizomwe mukuyakhulazo.
Anthu oyipa inu mulungu akulangeni, chilungamo mukuchidziwa
Mayakhidwe ake exactly akuwoneselatu kuti akuziwapo kathu akuthawa chulungamo
Kunkuyu ndi gulu lako, dont think you can fool malawians, not this generation, people are smarter than u think.
I agree with you,your right
Mwakanika kuyankha mafuso nzeru mulibe....
Anthuwa aphedwa basi, chilungamo chikubisidwa. Koma mu dzina la Mulungu chilichonse chionekera poyera.
Uyu ndiye mfiti amazitenga dolo
Mwapsa mtima ndi ma picture wo chifukwa mwa ululika anthu akudziwani kuti mwapha chilima inu akumkuyu
Mavuzi pwiii agalu inu machende anu muuzane a MCP zigawenga izii
Mizimu ya anthu amenewa ikubvutitsani nonse amene watenga nawo mbali pa imfa za anthu amenewa😭😭😭
Ifeso tinaina ndege drive wa mkazi uja akuyankhuso tinamuona inuso ndaleyu ndiyopusa tionana chaka chamawa
Mwamulakwira chilima😭😭
Which hills did the aeroplane hit
Gayezi tiyeni tidziponya mapic wo adziwe kumene kuti nkhanga zaona.
Mzeru ulibe kunkuyu machende Ako ndi Chakwera wakoyo
Amuses kumkyu Abwana, musadandaule, zonse, tisiye manja mwa Chauta, amene anatirenga tonse. Athu akhoza kukamba zambiri, I u musadandaule, chikwa, Mulungu yekha ndiamene akudziwa zoona. 4:44
Mulungu yemwe anarenga xiko lapasi ndilakumwamba akukathen, mesa akubaja akukanisani mukuona ngat sitikuxiwa?
Aziponye zonsezo anthu adziwe chilungamo palibe kubisa apa akumkuyu
Akuyesa ngat a UTM apita ku MCP mukhaula ng'oooo!
Kalonga shawa mwazizilitsa mtima wanga zikomo! Tisasokoneze mwambo wa mfumu yathu ya angoni! Kauseni mumtendere wawa
Ukati zisaponyedwe pa social media ukutanthauza chani mesa iwe tikukuwona pa social media pomwepo, galu
😢nyapanu a mcp mitumbo yanu nonse
Uziti machende awo
Awa musawamvere ndiafiti okupha
Kaye
Kathupi kokanika soap machende ako
Kuyankhula kotani uku mpaka chovuta ngati ichi chizachitikanso kwanu kapena tisazitengere?
Uyu kumkuyu akadya chamba amapanga zamisala
Achinsiru Inu mwapha adzanu inuyo 😊
Koma MA videoyo asakoneza chani kwenikweni
Mbuzi iwe sikuyankhula kwabwino kumeneko, umaona ngati anthu angokhala chete ngati, akasambala? Chilima anali pulezidenti, tikuenela kuyankhula
Bas takusiyilan malizani nokha mcp ndi utm bas mukutitenga kamwa kakusalilan kameneko nokha
Wabodza satana iwe
Mcp ichoke eeeee anthu oipa
Ndipo adxipitaa ndithu
Kwadusa moto kwatha koma kumene kwasara tchire😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Kumkuyu ndi chitsilu koma aaaa mcp out chaka cha mawa
Musapusise anthu Dziko ladziwa choonadi anthu oyipa inu . Ubwino wake mwaonjezera umboni kt Mcp ndi yakupha. Mwazi waonsewa uzafunsidwa pa Mutu panu.Komanso inu muziwerengera masiku amoyo wanu.
Koma kuyankhula kotani uku?
Anthu akulira kuposa eni asiwa?? mxie
Ndingozi yopanga iyi chakwera chifukwa dyera ndi undindo
Aaah
Kd kudzikokuno sikunachitikeko ngonzi yadzidzi nakha inuyo mukufuna kudziwa zangonzinu kd imfa yanu idzakhala yotani Mulungu anampasa aliyense manyamukidwe ake ndekutinso Achilima imeneyo ndiimfa yawo
Cho
ka wa mcp iwe ukut chani apa
Thanks for update will be together till end of burial services thx hon Mr kunkuyu
You honour him
Not 99% of Malawians
Your mad
Ma videos asokonodza bwanji, mmesa ma videos ndiyeno ofunikilawo
You know that we know for what you did,where are the brave soldiers of 1992 of operation bwenzani, to take over this country.
Burkina Faso is doing well with soldiers
amene ndimunthu amwalira guys imfa sisankha munthu koteleko tonse tiliimfa
Zigawenga izi zichoke zatiphela Malawi
Akumkuyu kulankhula uku ndikopanda nzeru kodi andale amene akutuma Anthu ndindani mukuwona ngati Anthu akumalawi ndi mbuli? Mutiwuza. Koma osanamizira zipani mukufuna Anthu asalankhule kuti mudziti akutumidwa ndi andale ? Asatana Anthu oyipa musawopweze dzikolono ndirathu palibe kuwopwezana ngati tife tidzafela mbendela imeneyi. Sitikuwopa.
Tikuyankha bwino tikayika malilo ukufuna kuti ife tisayankhulepo chifukwa simbale wathu mmm tiyakhulane lachitatu bwanji
Mr man CHIFUKWA chani achipatala samatumizidwa pa Malo angozipo?
Mulungu azakulangani
Chimunthu choipa ndi nkhope yomwe
Kd umadziwaso kuti udzafa ndye bwezi mukumapanga chiwembu amzanu?
Ndiwe fiti kumene km udziwe ichi 20 25 kulibe chanu agalu inu
Koma iwe uli ndi mzimu?
Zimenezi ndiye zachamba ndiye iye chikukhuza chan kuopa osanamizi amalawi zikufunika ziikidwe pa social media akuopa kuyaluka ndiye atankhale ndinkhawao ndani mantha sunati phwanga zifala unyasa zenzen
Inu makubitsa maumboni, pame ndege asilikali anaipeza mafoni anthuakufuwo anapeka kut palibepo anatenga ndani mafoniwo. Muyaluka
Opusa iwe wasala iwe zakoyoso azakupha ukuona ngati wafika
Inuyo akunkuyu ndiwe wakupha kale nafenso tikupani nonse a M C P manye anu nonse
Athu timafa munjila zosiyanasiyana RIP chilima
Inu uyu Mazila ake ndithu
Chidawakomela a Chakwela kt mzawo abatsogola kaye kt iwo akhale momasuka opanda omucheukila , R.I.P Mr Chilima
Machende ako galu iwe or manyazi ulibe chitsiru
Chakwela you mast go
For sure bro he must go
Anthu oipa inu afiti opephera
iwe kunkuyu palibe cha nzeru kwa inr moti idont notice that theres someone existing in malawi so called kunkuyu next it will br someone wjo is still alive like you
sorry to say this
Pamatso ngat anthu abwno km mmmmmm mkhope zanu zkuwurula cobiska. Kmx kulira salessana
kodi lero mukupasa ulemu atamwalira iwe moses ,ndi bwana wako mulungu akupase moyo mudzaone chidzachitike
Tell kunkuyu why not even one member of Mcp involved
Where is a black box
Why taking many hours to tell public
Where are the gadgets of deceased
Why is the rader missing
Who was searching the bodies
Why the president suspended the seach
We need best answers
Guys what should be done? they can't asnwer questions because they know what they have done as long as they still on powerful seat, asking them brings no solution, only People needs to you unite and discuss the permanent solution. That's it otherwise all these are giving rhem away to come out and hide all information. Let's stand and fight the rights of Malawian
Iweso kunkuyu ndi chakwera ndi zikhale ng'oma ndi Ena mwa inu muli pay list mukhale pheeee
Aaa a kumkuyu palibe chimene tikumva chifukwa simukuyankha mafunso koma kufotokoza, Boma ili sitidziwa mkomwe chapha chilima mmmmm
Ulemu wanji omupatsa munthu atafa?
mwapha pofuna mpando nyimbo yachingoni new song
Ndinu zitsiru nonse kmso zomwe mukuyankhula zithu zopanda nzeru ndinu anthu osavinidwa nonse
Kunkuyu usawaseke pakamwa athu. Kodi kunku ukuziwaso kt zomwe mwachitadzi inuso muzafaso at okay
Opoila kwambiri
Kukuyu dziwa kuti simuungazembele mulungu thawi yanu yatsala pang,Ono iweso ndiye ndani satana wakupha ngati iwe mulungu adzakulangani kwambili ndipo mudzafa ngati agalu
Bweretse uthenga cholinga muwamphe ndikongoresitu imeneyo
Koma chiwanda ichi mchoopusa
Zoona anthu akupanga kampeni adpp akuti amamopa chilima
Mauthenga apa4nio aponyedwe anthu awaone. Shaaa Congress chpan cha magazi. Manyaz mulibe mpaka pamenepo????? Chakwera kunkholo kwako ndthu
Athuwa akuziwa chomwe chinachitika even ma parachutes munalibe mu ndegemo kodi after emergency thing like this angwirisile tchito more over ndege ya asilikali a boma
Kodi mu ndegemo munali black box atolankhani tafunsani chonde
Timpase ulemu chilima mabwana kuno sa ayamba kufusa ku kodi kumalawi kuli anthu osaziwa ngozi kapena malilo wina akamwalila ndiye kuti walozedwa timakanika kuyakha mmalo molila mwachulusa ndale abale kod inu simzafa pepani apa sipopangila ndale ayi
Mmmm mukayakha ndithu
Anthu amagazi mmanja akupha awaa, manyazi alibe
Ndiwe chitsiru machende ako osadulawo wakupha iwe kaye kanthupi ngati satana
Demos
Zikutiwawa ukuyankhula mwa nsulinzo
Akubanja kwa achilima,akafika kunyumbakotu muitane achipatala kuti azamupime bwino mumve chinampha chilima
Enanunso ndinu zitsiru mukuona, kuti mcp idayndetsa ndege kuyankhula kopusa
Nkhan ndiyoti mcp yapha basi eeetu