Ku Malawi olo ku talowa President wanzeru ......sizizasintha pokha pokha system ya Democracy itasintha. ....Mumumve Yeremia Chihana ...Exclusive anapanga ndi Brain Banda. .......Please next time a Bakili Channel pangani mobilise anthu za Federal Government System ....otherwise mzakhalabe munena zomwezi mwinaso mati bola manyazi awawo
Problem of chakwera is , he does not have advisor! What you must know Malawians is every rich family there is a strong wife behind so the wife of chakwera she doesn't think. Bingu wamutharika did a lot of development because the wife was strong and loving woman. Good advice always Start from the bedroom.
Za bodzazo, za zii ndiye uganiza idzawine ndi UDF? Mangochi ndi Machinga singawinitse munthu, forget your hypocrisy, your wishes will never come true. Wishful thinking.
My fellow Malawians quote me right-Malawi will not and never transform if our political leaders are power hungry.Besides, if our religious leaders are cupidity minded and politically oriented.
Akulu mwakwiya ndi chakwera tu mpakana akangomanga nyumba ku bwalo la ndege komweko😂😂😂😂😂 you never disappointed us bro
😂😂😂
@@davenchimadzi6529 😀😀😂
😂
Akamangedi sakunama akutipasa busy kapeyi
🤣🤣
None knows this. The future is determined by the Creator. Leave everything in his hands
The creator has people to inform his people about the future
Ku Malawi olo ku talowa President wanzeru ......sizizasintha pokha pokha system ya Democracy itasintha. ....Mumumve Yeremia Chihana ...Exclusive anapanga ndi Brain Banda. .......Please next time a Bakili Channel pangani mobilise anthu za Federal Government System ....otherwise mzakhalabe munena zomwezi mwinaso mati bola manyazi awawo
🤣🤣🤣🤣🤣 Angomanga ka gowelo kodi, kkkkkkkkkkk
Athu onama kwambiri achakwera Ndi achinana chiima
IA just dreaming
Problem of chakwera is , he does not have advisor! What you must know Malawians is every rich family there is a strong wife behind so the wife of chakwera she doesn't think. Bingu wamutharika did a lot of development because the wife was strong and loving woman. Good advice always Start from the bedroom.
Inu nde mabodzatu awa
Good observation,congrats
No! vito sima adivicer, koma kuuma mutu kwake.iyeyo president yo
Tonse alliance ikazangoyelekeza kuwina mobela , ndithudi mundimvesebwino Malawi adzayaka moto , pokhapo mundimvese bwinobwino , Lelo date ndi 30 June 2023 , aliyense akhale ready chakacha 2025
Zoonadi tidzakhapanamo muno
Akuwona ngati Malawi wake wakale, ayembekezele kuzumidwa akayamba kuyenda misonkhano. Ineso ndnakwiya naye kale😒😒😒
Za bodzazo, za zii ndiye uganiza idzawine ndi UDF? Mangochi ndi Machinga singawinitse munthu, forget your hypocrisy, your wishes will never come true. Wishful thinking.
Well done
Ubwino wake azungu savota nawo, ife timuvormtela
Ndipo ndiye chakwera watikwana abale, ngati 2025 likhale mawa, mavuto anyanya abale,nanga kumangodya mbatata,nanga mbatata zikatha abale
Never give up ❤
Akadzavota okhatu a intelligence ndi iweyo chitsiru we
Chakwera ndigalu heavy palibe kuzakhalanso president ndizake chilima agalu opusa
Edgar Nkanda the one who has big lips?
2025 kwatalika. Chakwera and chilima must go... they're wasting our time
Kkkkkkkkkkkkkk
Azipita uyo
Chakwara ndi galu uyu ndipo akundinyasa kwambiri 🤦🏻♂️🤦🏻♂️
😅😅😅😅 Komad azigona ku airport komweko
🤣🤣🤣
😅😅😅😅
Koma ya Chanel yanga lero 😂😂
😂😂😂😂koma ndaseka azigona kuti?😂
Komweko mama zachabetu
My brother from another mother umakwana respect
I like the way you analyze your story, iweyo ndi m’banga
😂😂👍👍
@@aggogokina8992 nkulu uyuyu ndikatswiri mmmm amafukulira ngini
@@jacksonmaster2288 eee kwambiri awa big man👍
Koma ndiye angomanga gowelodi kkkkk
😂😂😂😂 komatu lwe kagowero kodi 😅😅😅
Zoona ndpo sixaboza
Well done ❤❤❤
Ndpo inu
We like you brohh help us to more
Guys kamwendo mnjira kunena president😂😂😂😂😂😂
Kkkkkkk koma iyiyi ndiye munamenya amangeni ka gowelo ku airport kokodi
Thanks a lot for your polite, true and honest words concerning the M. C. P. WITH THE PASTOR LAZARUS MACARTHY CHAKWERA... SHAME ON YOU 😂😂😂😂
Umakwana bwanawe
Ndipo galu ameneyu akadzachoka m'boma tidzakwizinge zingwe mwamphamvu
Izipita ndipo yatikwanadi
Big up bakili muluzi tv
Lifulendamu achakwera must go
Chakwelayi ndi bwantasa
Mcp uyelekeze kuwina 2025, secret revolution Army yathu tidzayambisa nkhondo dikira tidzakuonesa
Kkkkkk kokapempha bas achakwela
Vuto ndilakuti amalawife ndinafasa mopusa kwambili .....pamene zafikapa kunali kugwilizana ma demostrations dziko lonse ......chakwera ndi mbuzi ya munthu
My brother loves you so much ❤
Eeeish Galu palibe chichita iye
Koma Anthunu mukuganiza bwanji zitukuko zosezo 4 years malawians
pama president onse uyu nde zero pa handede kkkkk
My fellow Malawians quote me right-Malawi will not and never transform if our political leaders are power hungry.Besides, if our religious leaders are cupidity minded and politically oriented.
We shall vote him in power again
28june yake yiti poti panopa ndi pa1june2024 osamanama pasocial media.muzichita manyazi ponena bodza
Yanama imeneyo ndipo amen sadzirima akhaula ndipo mcp mpaka 2035 wooooh. Mulira ndipo mulengeza zonama za Achakwera koma ife fziko lino ndipatsogolo ndi mcp ndipo patsogolo ndi Achakwera. Ife tikufina mmene fziko lasinthira sitisowekaso kuti wina afxitinamiza
😂kamwendo njira anadya mathako agalu mbuzi iyi yamunthu. Thanks very much bg mn respect ndawi zangawine uyu srs
If Malawians cannot remove this president come 2025, know that we are doomed as a nation..
MUTHU wakupha chakwela MCP yoipa please don't try again
Or ndiotchetcha tchire omwe sanayambe😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Aliyense akudziwanso ndiye mudzayelekeze mudzabere anthu adzaphana
😂😂😂😂😂 koma abale azigonadi konko ku airport
Olo achipanda kutero ndizachidziwikile kut sangawine kumene.
Ndipo asazinyase akwakhuluoirila umve bwanji
I know the president saw what happened to Kenya is also coming to Malawi soon
Moses ngati adapha Wittika ndiye angakhale ndichisoni kwa Mmalawi osamudziwa?
Political leadership is not religious leadership.
My brother loves you so much ❤
Udzakhumudwa akadzawina. Ungoyamba ndale udzawwine ngati ungadzawine. Iwe ukuona kuti angadzawineso ndani? Pamudzi sipalephera ozungulira mutu.
koma inu ndi one
Aluze kumene zindisangalasa kopya boma loyipa kwambir ili
Moses kunkuyu ndi chakwera chimwendo Banga zakhare ng'ono chakwera azalamulira anthu ake amenewo km ifeyo a Malawi zosatheka sazawona voti ya amalawi
This is chakwela and his poor government
Sazawinaso sitikuwafunaso palibe cha nzeru chomwe apanga
😂😂😂😂😂😂😂😂 kulakhula kwa bwanj uku angomanga nyumba ku airport 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
The guy is legend😂😂😂😂
Iweyo osabazako bwanji zikuvuta bwanji mbuzi imadya pomwe ayimanga
MUWAUZE A BRITAIN KUTI AZATITHANDIZE CHIFUKWA AGALU AWA AKONZEKERA KUBERA MASANKHO NDIYE UBWINO WAKE AKUZIONA ZOMWE ZIKUCHITIKA ASATISIYE CHONCHO
Or adzaluze koma ngati inu simulimbikira tchito mudzafera mu uphawi chazelu pezani zochita muziona chogulitsa kuzolowera kupepha
Abambo amenewo kuyenda ñdi kwawo mene anali ku president wa church amayendaso choncho ngati ofuntha ambuye awakhululukire awonongelatu malawi yathu kaya idzabwerelaso monga kale pano ili worse tiyeni tidikilire 2025 sakuti awinaso nawonso akunkuyo atisale mwina adzavotera anthu mudzi mwawo wokha
❤❤❤ More love to you big boss for ur information
Zoona zake man
Zoonandi big chitsilu cha president buzi yamuthu watichititsa manyazi koma uyu galu
Azatifuna chakwela ife amalawi 2025 komanso azagwada ameneyi matako ake
🛌 ndiuse ine
Achakwera angopeselapo mwayi oti aziwe mayiko bas ndikuba komaso kudzudza anthu osalakwa ngat ma bulundi
achake basi abusa anazolowera kudya zosakhetsela thukuta.ntchito kudya ndi kuba ndalama za amphawi.
I will deal with Chakwela my self on 2025
Chakwela wationjeza mmm zambili wangotiyenda pansi
Chakwera sadzatheka paka kufikira atasamusidwa pa udindowu. Uyu chomwe adziwa ndi bodza komaso kusaphweketsa nkhani ya mayendedwe.
Bola idzavote chifukwa ovota ndi ena iwo ndi ma prophet chabe
Kumkuyu alibe nzeru akuona national amalawi ndi ogona ku.kuyu ndikuudze amalawi tinDzindira ndiwe opusa
Kkkkkkk km adawa eeeea akut tangomangani kagwel komwek
Koma agalu awa atikwana ka nthawi kochepa ndipo kungowinanso abale tikhala pamavuti azaoneni
Chitsiru ichi chakwera ndi mbuzi yamunthu uyu ndi satana wenwen
Vuto kumalawi kulibe asitikali bwezi ataba galu ameneyo axikhara kunjakoko
Mumatiimirira Ife osatha kuyakhurafe zikomo
President dzina lake latsopano ndi kamchacha
Chakwera koma ndiwe onyasa ngati maliro 😂😂
Mwangowada bwanawa britain si malawi makosana tiyeni tivomereze abale malawi tiyeni tisamupange kukhala godi wa anthu andale ayi koma malawi tiye tidzidalire pa nzose kodi tidzasintha ma president mpaka liti chenjera malawi dziko lanthu la malawi muli anthu ochepa ophunzira bwino koma vuto lawo amanamidza kwambiri anthu omwe sanaphunzire koma nyengo ndizosintha nthawi nzotse zamoyo kodi chani chomwe tikuyembekezera olo achakwera atachoka pampando abale anga chonde malawi azungu asatirekanitse ndipo amankhala kosiyana ndi malawi pa chilichose koma amapindula kudzera ku zinthu zili ndife anthu akuda
Km ngati panopa zinthu zikutenda ndichifka chakuyenda kwacha kwela zitukuko zomwe akumaliza chakwela ndizomwe azipani zomwe zinatuluka boma zamwe ndalama zake anabamo nthawi yomwe ankalonjeza anthu km chakwela wakwanitsa zosezi nde zona ma zakozo peza ana akoo uziwanamiza boma lilose limakhala ndi anthu osangalala ndi onkhumundwa maboma osewa ifeyo tinalipo tikudziwa u bwino komaso kuipa kwake
Eee munthu uyu chopanda nzelu bwanji osamasilila maiko ena mmene akutukukila kungowina ka mwendo njilayi ndi nkhondo yayambika pamenepopo tasukusula nafe
Angomanga kagowero adzigonera ku airport komko kt asamawavutitse anthu
Chakwera ndi galu sitikumufuna ife chonde
Amange nyumba ku airport kamwendo njira