BON KALINDO KU MALAWI SIKULI BWINO 🙌

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 28 окт 2024

Комментарии • 34

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 2 месяца назад +3

    Lero ndatsimikizadi kuti Bon Kalindo Mulungu amamungwilitsa ntchito ndikudziwa ambiri simuvomeleza mudziti amapangira zimenezi ndale koma aiii ndithu Mulungu anamusankha Bon Kalindo Ngati momwe anachitira ndi Mose kwa iguputo kuti akatulutse ana Israel ( GOD BLESS YOU MR KALINDO🙏)

  • @phonexDaniel
    @phonexDaniel 2 месяца назад +3

    Kod athu ndinu otani Muthu akunena zabwino bwino.inu mukut chitsilu.zangozizo zimukumva.

    • @GiftJulius-gx2kb
      @GiftJulius-gx2kb 2 месяца назад

      Anthu enatu anangobadwa opusa amangoikila kumbuyo zilizonse.akuti sakuona vuto

    • @anicakandiado
      @anicakandiado 2 месяца назад

      Eti inu

  • @MercyChimaliro-fi6mv
    @MercyChimaliro-fi6mv 2 месяца назад +1

    Kuyambira lero boni Kalindo ndizikuyitana Mose wa Lero. Soka limugwera munthu odana ndi iweyo

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 2 месяца назад +1

    Simunaonepo mfiti? Wina aliyense amene akujijirika ndi MCP ndi mfiti. Achakwera anangobaya chidole chija ndi jakison ku Malawi kunachitika ngozi.

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana 2 месяца назад

    Ndipo inenso ngoxi zimenezi nduudabwa nazo ..Ambuye Mulungu alowererepo

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg 2 месяца назад +1

    dziko lamalawi eeeee panopa lafika poopsa kwambili

  • @michaelbulaula6444
    @michaelbulaula6444 2 месяца назад

    Ya 🔥 yinabwera

  • @Paworo-h5r
    @Paworo-h5r 2 месяца назад

    Satana woyamba ndi kalindo enawoakungomalidzitsa, munthu akuti akumenyela ma ufulu anthu wosawuka, anthu ake ati anapitako kukapempha kwa anthu andale ngati iyeyu? Ndili linen anayamba wakapelekako sopo Kwawosawuka akunenawo kalindo, bigiiiiii and smart develop usadyele pamutu pa amphawi moto waselufule ukukudikila

  • @SilenceChepiano
    @SilenceChepiano 2 месяца назад +1

    Mmmm pakana 3days osapeleka what's going on

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb 2 месяца назад

    Nanu a fire akumalawi amawelengela za anthu

  • @AustinChikapa-m1x
    @AustinChikapa-m1x 2 месяца назад

    Ameen

  • @FrancisStima-sc7zs
    @FrancisStima-sc7zs 2 месяца назад

    Chakwela amakatani kwa papa Francisco

  • @beatricenkhoma1109
    @beatricenkhoma1109 2 месяца назад

    Devil at work, let's pray for our country, iyi ndi mphulupulu ya dziko imene imabwera cifukwa utsogoleri woyipa wa atsogoleri adzikolo Mulungu amakhala kt wacenjeza, waunikira atsogoleri kumangovitabe zoipa as result, amalola oipayo alamulire nkwiyo wa Mulungu then mukupwetekesa anthu osalakwa

  • @LoyidKarebe
    @LoyidKarebe 2 месяца назад

    Ng'alulazation

  • @Iwiszy-ht9ic
    @Iwiszy-ht9ic 2 месяца назад

    Today is 24 don't forget

  • @Paworo-h5r
    @Paworo-h5r 2 месяца назад

    Big devil

  • @RajhMatola
    @RajhMatola 2 месяца назад

    Ili ndiy bodza malamulo afiti sanabwele ler or chakwela anawapeza kamban zina awinik

  • @ChrisyMbewe
    @ChrisyMbewe 2 месяца назад +1

    Zoona.tipephele.amalawi

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 2 месяца назад

    Chakwera ndi wa satanic aliyense amadziwa munthu woyipa

  • @ChrisyMbewe
    @ChrisyMbewe 2 месяца назад

    iiiiiiiiii.ndipo.zoophwa.kumalawi athungati.agalu.kufa.iiiii.ambuye.atithandizendithu

    • @kingsleymsampha2260
      @kingsleymsampha2260 2 месяца назад +1

      He says andale adayika malamulo woyipa not Chakwera. Listen again

  • @phillipstamaley7901
    @phillipstamaley7901 2 месяца назад

    Choka iweee mbuli ya munthu

    • @FrancisStima-sc7zs
      @FrancisStima-sc7zs 2 месяца назад +1

      Wasala ndiwe usamale

    • @anicakandiado
      @anicakandiado 2 месяца назад

      Mbuli ndi iweyo amene sukumva kuwawa kwa imfa zikuchitikazi mpaka wina wakwanu atafa

  • @MaxwellSamuelChikapa
    @MaxwellSamuelChikapa 2 месяца назад

    Chitsiru

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga 2 месяца назад +1

      Kagwere uko pedegu iwe 😢

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v 2 месяца назад

    Chakwera ndi wa satanic aliyense amadziwa munthu woyipa