Your excellency,Dr banda, your charitable initiatives are reflection of your remarkable character and dedication to the betterment of society. Keep shining mama , kudana ndi inu ndi thembelero chabe.God bless you
This one performed kungoti amalawi mpandila u can't appreciate because she is a woman,when she came in kunalube fuel kunalibe Forex anthu kuchipatala kumwalila because of magetsi after generator zinalibe fuel magetsi akuzima mwanyasi but she did it in just 100 days I feel that's something we need to acknowledge that she did good.
Performed where?? She is full of family politics. Look at her age kukakamila leadership in PP. I bet she was one of those voices calling for Chilima to join MCP! Fully knowing that she will get in through the backoffice.
@@mwale86why do you want to make women to look like they are the most hated beings for no reason?? Pali zinthu zina zake adachitadi bwino koma anapoilabe ndithu.
Mayiwa is one of the creams ku Malawi Kuno. Awawa ndi machine enieni. Kudana ndi mayi awa ndikudana ndi chitukuko. aMalawi amzanga alot of known countries are recognizing her as very important trustworthy and helpful woman , why not us . Lord should have mercy on us , so that we can how potential this woman is. aMalawi tinazolowera kutamikira munthu akamwalira.what a shame
Anamanga nyumba Kameme , Chisenga in Chitipa District.. Chilumba and Khwawa in Karonga Chintheche, Bandawe, Vizara, Chisala in Nkhata Bay Mzimba Boma, Njuyu, Thunduwike, Nkhamenya in Mzimba Lula and Ng'onga in Rumphi list endless under Mudzi Transformation
Kkkk Ndàlqma za cash gate zao sadzatenga kumanda.ayi..kumwamba sikufuna cuma..nkhale awawa a mr Sattargate wa a mcp wa ndi zinduna zaozi.kwa Yehovah kuchiweruzo sadzatenga Sattargate chuma chaocho amenYoù honoüable Robbers of our nation just be awaiting to be thrown in ĥll fire by Jesus Cĥrist.for crime of Stealing or Robbing malawi nation.all the same .be blessed as you walk towards jesus christ to be judged
Ambilimbili through her community Development initiative project people mainly youths benefitted kupeza chakudya in kasungu isn't that helping youths??
Ndipo zowona zake even she feeds over 15,000 children through her Joyce Banda foundation pajatu Amati mmela poyamba hence ana akakula bwino azakhala ma youth othandiza dziko lawo@@mkajikosya-uq5hs
Your excellency,Dr banda, your charitable initiatives are reflection of your remarkable character and dedication to the betterment of society. Keep shining mama , kudana ndi inu ndi thembelero chabe.God bless you
Our excellent ngat mfuna mbiri yanu izakhale yabwino mkamwalira ,tulukani mu Tonse Alliance,mpakidwa magazi oyipa kwabas
Alipo women & girls oti anapindula ndi izi akamba awa?? Atchuleni. She could've mentored a girl or girls for presidency if she was sincere😢😢
Anthu omwe munapanga ngwilizano, mumafunika kutuluka kalekale. Mwaona zisankho zayandikila muzioneka ngati okonda anthu..antku munawatengela kumavuto.
God continue bless you your excellency ma, your such a blessing to malawi
Malawi leaders are always talk wisely when they are out of gavervent,give them charnceand see there performance
This one performed kungoti amalawi mpandila u can't appreciate because she is a woman,when she came in kunalube fuel kunalibe Forex anthu kuchipatala kumwalila because of magetsi after generator zinalibe fuel magetsi akuzima mwanyasi but she did it in just 100 days I feel that's something we need to acknowledge that she did good.
Performed where?? She is full of family politics. Look at her age kukakamila leadership in PP. I bet she was one of those voices calling for Chilima to join MCP! Fully knowing that she will get in through the backoffice.
@@mwale86why do you want to make women to look like they are the most hated beings for no reason?? Pali zinthu zina zake adachitadi bwino koma anapoilabe ndithu.
Mayiwa is one of the creams ku Malawi Kuno. Awawa ndi machine enieni. Kudana ndi mayi awa ndikudana ndi chitukuko. aMalawi amzanga alot of known countries are recognizing her as very important trustworthy and helpful woman , why not us . Lord should have mercy on us , so that we can how potential this woman is. aMalawi tinazolowera kutamikira munthu akamwalira.what a shame
Mmmmm Iwe wachibwana Eti Ameney Mesa ndimunthu Modzi adapusisa malawi
Tulukakoni masten,,asakupakeni nawo manyiwa pliz.Inu ndi mbambande
The best leader
God bless her excellence Dr Joyce Banda
Repent before it is late
Mwaganiza bwino kwambirimbiri tulukakoni kumeneko mwaganiza bwino kwambiri mayi zikomo zikomo
Aaaa awa amayi adyela adzuzitsa malawi kutipatsa MCP yokupha komatsa yankhaza iiiiii tsitidzayiwala mayi banda anatipanga nkhadza dzedi chifukwa chofuna moyo wawo kukhale pabwino otsati amalawi akhala pabwini ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii mulape mulungu akhululukileni mwanatiyika pa dzuwa
Nanga malemu SKC apepesenso?
@@mkajikosya-uq5hskumakhala ndi umunthu sometimes
Zilibwino koma zomayika background music instrumental ndizopoyila pama serious massages
Ambuye adzikudalitsani masten ntchito zachifundo ndiye mukuzichita
Amayi anthu timakukondani komanso Inu Mai mumatikonda amalawi munawamangira yumba anthu osauka ambirimbiri kuno kunkhamenya, anthu atavutika ndi ngozi za madzi munawathandiza powamangiranso nyumba kumwera
This woman is our Gem. Very good and we love you
Chipanda Dr Joyce Banda sitikanadziwa kuti mu Boma mukunedwa ndalama
Ndipo zowona no president has allowed an audit while in office it's only HE Dr Joyce Banda mayi awawa ndikatundu
Anamanga nyumba Kameme , Chisenga in Chitipa District..
Chilumba and Khwawa in Karonga
Chintheche, Bandawe, Vizara, Chisala in Nkhata Bay
Mzimba Boma, Njuyu, Thunduwike, Nkhamenya in Mzimba
Lula and Ng'onga in Rumphi list endless under Mudzi Transformation
Amai mumakwanila palipose zitukuko muno mudziko lamalawi mwapanga m, boma ririrose
Tikanena zothandiza osowa nde ndikudya kwanu ndipo simuona khope kana mtundu
Amai Banda Mulungu azikudaritsan thawi zonseeee eee
Makhuluku akumalawi
Ukhuluku wakuti anasintha dzikoli with 100 days ukhuluku anapangila kuti
Unakasiya Chilima mkamwa mwa Ng'ona.
Kkkk Ndàlqma za cash gate zao sadzatenga kumanda.ayi..kumwamba sikufuna cuma..nkhale awawa a mr Sattargate wa a mcp wa ndi zinduna zaozi.kwa Yehovah kuchiweruzo sadzatenga Sattargate chuma chaocho amenYoù honoüable Robbers of our nation just be awaiting to be thrown in ĥll fire by Jesus Cĥrist.for crime of Stealing or Robbing malawi nation.all the same .be blessed as you walk towards jesus christ to be judged
Inu mayi chilima mumanena kuti ndi mwana wanu ndiye munachilandila bwanji chipongwe chimenechi
Which youths do you assist?
Ambilimbili through her community Development initiative project people mainly youths benefitted kupeza chakudya in kasungu isn't that helping youths??
Ambiri anapindula anagawa njinga zamoto pano akulipilira ana ma school fees through Joyce Banda foundation
Ndipo zowona zake even she feeds over 15,000 children through her Joyce Banda foundation pajatu Amati mmela poyamba hence ana akakula bwino azakhala ma youth othandiza dziko lawo@@mkajikosya-uq5hs
Kodi kabaza ku Malawi kuno anabwera ndindani
Tapitani ku ma secondary a Boma mdziko muno atsikana akupelekedwa ma fees..
Anthu amalandila nkhuku kumaweta mabanja kumapeza ndalama ndikumadya bwino panyumba pawo..
Mbuzi, N'gombe
Mmmmmm m'mai otapa tapa uyu uliboh mudzapita ndindalama amzathu
hule wachabe chabe
Nzeru zawo ndizopititsa patsogolo dziko maka maka anthu ovutika ammamidzi
Nthawi yawo mankhwala mzipatala samasowa..kunalibe basi kaguleni ku pharmacy
Ndipo zowona
Ambuye azikudalitsani ndikukupatsani moyo wautali
Lankhurani chabe chichewa
Awa ndi mai amzelu sangakakamile ku mcp acokako
Nzeru sabwelekana inuyo muganiza zanu
Inuyo mukati achokako ku mcp inu mudakhalapo wa mcp?
Sitikufunaso makadeti muno mmmalawi
Mzimayi wachikondi uyu