Zomwe ayankhura Mai Joyce Banda zokhunza Tonse Alliance kucha kwa Lero

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 16 окт 2024

Комментарии • 52

  • @PreciousKaliati-l6u
    @PreciousKaliati-l6u 3 месяца назад +3

    Your excellency,Dr banda, your charitable initiatives are reflection of your remarkable character and dedication to the betterment of society. Keep shining mama , kudana ndi inu ndi thembelero chabe.God bless you

  • @SanidaChirwa
    @SanidaChirwa 3 месяца назад +4

    Our excellent ngat mfuna mbiri yanu izakhale yabwino mkamwalira ,tulukani mu Tonse Alliance,mpakidwa magazi oyipa kwabas

  • @chelseajackson3200
    @chelseajackson3200 3 месяца назад +2

    Alipo women & girls oti anapindula ndi izi akamba awa?? Atchuleni. She could've mentored a girl or girls for presidency if she was sincere😢😢

  • @NatashaMakay-k5e
    @NatashaMakay-k5e 3 месяца назад +1

    Anthu omwe munapanga ngwilizano, mumafunika kutuluka kalekale. Mwaona zisankho zayandikila muzioneka ngati okonda anthu..antku munawatengela kumavuto.

  • @GilbetaMasamba-te8kp
    @GilbetaMasamba-te8kp 3 месяца назад +1

    God continue bless you your excellency ma, your such a blessing to malawi

  • @MphatsoMhoney-xn2ft
    @MphatsoMhoney-xn2ft 3 месяца назад +2

    Malawi leaders are always talk wisely when they are out of gavervent,give them charnceand see there performance

    • @mwale86
      @mwale86 3 месяца назад

      This one performed kungoti amalawi mpandila u can't appreciate because she is a woman,when she came in kunalube fuel kunalibe Forex anthu kuchipatala kumwalila because of magetsi after generator zinalibe fuel magetsi akuzima mwanyasi but she did it in just 100 days I feel that's something we need to acknowledge that she did good.

    • @chelseajackson3200
      @chelseajackson3200 3 месяца назад +1

      Performed where?? She is full of family politics. Look at her age kukakamila leadership in PP. I bet she was one of those voices calling for Chilima to join MCP! Fully knowing that she will get in through the backoffice.

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r 3 месяца назад

      @@mwale86why do you want to make women to look like they are the most hated beings for no reason?? Pali zinthu zina zake adachitadi bwino koma anapoilabe ndithu.

  • @chikondichanza9772
    @chikondichanza9772 3 месяца назад +1

    Mayiwa is one of the creams ku Malawi Kuno. Awawa ndi machine enieni. Kudana ndi mayi awa ndikudana ndi chitukuko. aMalawi amzanga alot of known countries are recognizing her as very important trustworthy and helpful woman , why not us . Lord should have mercy on us , so that we can how potential this woman is. aMalawi tinazolowera kutamikira munthu akamwalira.what a shame

    • @juntoiman
      @juntoiman 3 месяца назад

      Mmmmm Iwe wachibwana Eti Ameney Mesa ndimunthu Modzi adapusisa malawi

  • @FosterChakanga
    @FosterChakanga 3 месяца назад +1

    Tulukakoni masten,,asakupakeni nawo manyiwa pliz.Inu ndi mbambande

  • @AustinMhone-r3s
    @AustinMhone-r3s 3 месяца назад

    The best leader

  • @mkajikosya-uq5hs
    @mkajikosya-uq5hs 3 месяца назад

    God bless her excellence Dr Joyce Banda

  • @MaryMlomba
    @MaryMlomba 3 месяца назад +1

    Repent before it is late

  • @AlexBand-f4p
    @AlexBand-f4p 3 месяца назад +1

    Mwaganiza bwino kwambirimbiri tulukakoni kumeneko mwaganiza bwino kwambiri mayi zikomo zikomo

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 месяца назад +5

    Aaaa awa amayi adyela adzuzitsa malawi kutipatsa MCP yokupha komatsa yankhaza iiiiii tsitidzayiwala mayi banda anatipanga nkhadza dzedi chifukwa chofuna moyo wawo kukhale pabwino otsati amalawi akhala pabwini ayiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii mulape mulungu akhululukileni mwanatiyika pa dzuwa

    • @mkajikosya-uq5hs
      @mkajikosya-uq5hs 3 месяца назад

      Nanga malemu SKC apepesenso?

    • @FosterChakanga
      @FosterChakanga 3 месяца назад

      ​@@mkajikosya-uq5hskumakhala ndi umunthu sometimes

  • @BlessingsBanda-nh7ur
    @BlessingsBanda-nh7ur 3 месяца назад

    Zilibwino koma zomayika background music instrumental ndizopoyila pama serious massages

  • @dianachabs
    @dianachabs 3 месяца назад +2

    Ambuye adzikudalitsani masten ntchito zachifundo ndiye mukuzichita

  • @BenardPhili-wp5jt
    @BenardPhili-wp5jt 3 месяца назад +1

    Amayi anthu timakukondani komanso Inu Mai mumatikonda amalawi munawamangira yumba anthu osauka ambirimbiri kuno kunkhamenya, anthu atavutika ndi ngozi za madzi munawathandiza powamangiranso nyumba kumwera

  • @AliceNaphiyo
    @AliceNaphiyo 3 месяца назад +1

    This woman is our Gem. Very good and we love you

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад +1

    Chipanda Dr Joyce Banda sitikanadziwa kuti mu Boma mukunedwa ndalama

    • @mwale86
      @mwale86 3 месяца назад

      Ndipo zowona no president has allowed an audit while in office it's only HE Dr Joyce Banda mayi awawa ndikatundu

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад

    Anamanga nyumba Kameme , Chisenga in Chitipa District..
    Chilumba and Khwawa in Karonga
    Chintheche, Bandawe, Vizara, Chisala in Nkhata Bay
    Mzimba Boma, Njuyu, Thunduwike, Nkhamenya in Mzimba
    Lula and Ng'onga in Rumphi list endless under Mudzi Transformation

  • @PreciousJames-fh1xs
    @PreciousJames-fh1xs 3 месяца назад +1

    Amai mumakwanila palipose zitukuko muno mudziko lamalawi mwapanga m, boma ririrose
    Tikanena zothandiza osowa nde ndikudya kwanu ndipo simuona khope kana mtundu
    Amai Banda Mulungu azikudaritsan thawi zonseeee eee

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 3 месяца назад +6

    Makhuluku akumalawi

    • @vitujames53
      @vitujames53 3 месяца назад

      Ukhuluku wakuti anasintha dzikoli with 100 days ukhuluku anapangila kuti

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 3 месяца назад

    Unakasiya Chilima mkamwa mwa Ng'ona.

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe 3 месяца назад +2

    Kkkk Ndàlqma za cash gate zao sadzatenga kumanda.ayi..kumwamba sikufuna cuma..nkhale awawa a mr Sattargate wa a mcp wa ndi zinduna zaozi.kwa Yehovah kuchiweruzo sadzatenga Sattargate chuma chaocho amenYoù honoüable Robbers of our nation just be awaiting to be thrown in ĥll fire by Jesus Cĥrist.for crime of Stealing or Robbing malawi nation.all the same .be blessed as you walk towards jesus christ to be judged

  • @DevisonHala
    @DevisonHala 3 месяца назад

    Inu mayi chilima mumanena kuti ndi mwana wanu ndiye munachilandila bwanji chipongwe chimenechi

  • @rightlombe380
    @rightlombe380 3 месяца назад +2

    Which youths do you assist?

    • @mwale86
      @mwale86 3 месяца назад

      Ambilimbili through her community Development initiative project people mainly youths benefitted kupeza chakudya in kasungu isn't that helping youths??

    • @mkajikosya-uq5hs
      @mkajikosya-uq5hs 3 месяца назад +1

      Ambiri anapindula anagawa njinga zamoto pano akulipilira ana ma school fees through Joyce Banda foundation

    • @mwale86
      @mwale86 3 месяца назад

      Ndipo zowona zake even she feeds over 15,000 children through her Joyce Banda foundation pajatu Amati mmela poyamba hence ana akakula bwino azakhala ma youth othandiza dziko lawo​@@mkajikosya-uq5hs

    • @vitujames53
      @vitujames53 3 месяца назад

      Kodi kabaza ku Malawi kuno anabwera ndindani

    • @vitujames53
      @vitujames53 3 месяца назад

      Tapitani ku ma secondary a Boma mdziko muno atsikana akupelekedwa ma fees..

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад

    Anthu amalandila nkhuku kumaweta mabanja kumapeza ndalama ndikumadya bwino panyumba pawo..
    Mbuzi, N'gombe

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 3 месяца назад

    Mmmmmm m'mai otapa tapa uyu uliboh mudzapita ndindalama amzathu

  • @SaeedHurzrut
    @SaeedHurzrut 3 месяца назад +1

    hule wachabe chabe

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад

    Nzeru zawo ndizopititsa patsogolo dziko maka maka anthu ovutika ammamidzi

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад

    Nthawi yawo mankhwala mzipatala samasowa..kunalibe basi kaguleni ku pharmacy

    • @mwale86
      @mwale86 3 месяца назад

      Ndipo zowona

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад

    Ambuye azikudalitsani ndikukupatsani moyo wautali

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 3 месяца назад

    Lankhurani chabe chichewa

  • @JusticeMpondaphili
    @JusticeMpondaphili 3 месяца назад +1

    Awa ndi mai amzelu sangakakamile ku mcp acokako

    • @DalitsoBoster
      @DalitsoBoster 3 месяца назад

      Nzeru sabwelekana inuyo muganiza zanu

    • @DalitsoBoster
      @DalitsoBoster 3 месяца назад

      Inuyo mukati achokako ku mcp inu mudakhalapo wa mcp?

    • @DalitsoBoster
      @DalitsoBoster 3 месяца назад

      Sitikufunaso makadeti muno mmmalawi

  • @vitujames53
    @vitujames53 3 месяца назад

    Mzimayi wachikondi uyu