Panopa mzukulu wanga ali ku prison ku Thyolo atamupanga transfer kumuchotsa ku Blantyre ndikumupititsa ku Thyolo nkhani yake amakatola nkhuni ku phiri lina lake ku Blantyre pamene anthu omwe akuzunza a Malawi ndikuba chuma cha boma khoti lomwelo silikuwamanga
Eya a chakwera anaba chimangadi nkiukagulitsa ku tanzania ndiponso iwo ndi nduna zao anaba mao za Sattar Gate koma kumgomugwira Saulosi klaus chilima yekha.!! Bwanji kodi ? Afiti inu
Mmmmmm koma abale kumangidwa chifukwa cha nkhuni koma Mcp nde mukusowa zochita tu kuchititsa manyazi munya simudzawina 2025,apolice sakuyidziwa ntchito yawo palibe chomwe akupanga
Ma jaji akumalawi.naonso ali ngati asilikali NDI a Police anasankha kugwira ntchito ndi chipani kusiya kulemekeza malamulo , komaso Ben longwe AMENEYU AZIYENDA mosamala timutchola nsagwada dziko si lamake kapena chakwera ,
Umakwana DJ uli ndi voice yabho ❤❤❤
😂😂😂😂 best dj munya nane and you got nice voice.
Zikunveka bho❤❤
Ndikanakonda ndithakona ngope amunyanae mundfikapo
Aaaaaa DJ munyanane apatu nde mwaing'aluratu zoonadi beni Longwe ndi satana kapolo wamunthu
Ben longwe amachinda ana ake yakumbuyo
Mwaswela bwanji,ngati muli bwino dzikomo,koma ineyo kuno ku Zambia muku mveka 10%
Sorry ninali EMBA 10% pepani pepani mukumveka 100%
Mavuto kumalawi kadziko kachepelanji koma nkhani dzomwe zikuchitika🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌 Komatu ndive tomwe tinkavotela chakwela chiyipa chizata Eni ake chipandakumvomela kumvota kawiri Kaja zibwesi Lero tiri chontchi koma aMalawi Ife ayi
watching from jhb loud n clear
✦✦✦♥︎♥︎♥︎♥︎♥︎✦✦✦
☆☆☆☆☆☆☆☆☆☆
Inu ndi akatundu
Malawi is a very had country to leave specially the citizens than visitors
Proud of u keep it up the great work ❤❤
Panopa mzukulu wanga ali ku prison ku Thyolo atamupanga transfer kumuchotsa ku Blantyre ndikumupititsa ku Thyolo nkhani yake amakatola nkhuni ku phiri lina lake ku Blantyre pamene anthu omwe akuzunza a Malawi ndikuba chuma cha boma khoti lomwelo silikuwamanga
❤❤❤❤ DJ munyanane nyimbo wabayayi imandiwaza ❤❤❤❤❤❤❤❤
Loud and clear. In Pretoria north west in south Africa, umakwana
Uli super Munyanane
Clear. From Zambia chakwela should go
Chautaaone
Kumenekoooooo timakunyadilani Mr Munyanane kuno Ku South Africa Box B Kuli bwino, Kuing'alula mosawona apongoziiiiii kkkkkkk
🔥🔥🔥🔥🔥
Exactly
Ziko lapasi limakomera anthuu oipa
Loud and clear from Mozambique.
Lound and clear from capetwon
Loud and clear @ Winnie Mandela, Pretoria
Eya a chakwera anaba chimangadi nkiukagulitsa ku tanzania ndiponso iwo ndi nduna zao anaba mao za Sattar Gate koma kumgomugwira Saulosi klaus chilima yekha.!! Bwanji kodi ? Afiti inu
Mmmmmm koma abale kumangidwa chifukwa cha nkhuni koma Mcp nde mukusowa zochita tu kuchititsa manyazi munya simudzawina 2025,apolice sakuyidziwa ntchito yawo palibe chomwe akupanga
Mulungu alowelelepo azimai amenewa ayenela kutulusidwe
Mmmmmm mwinatu ndi maaaa iiiiiiii sorry mr vp
OSAMANGA ANAGWESA NDEGE KU CHIKANGAWA BWANJI,ENA KU BUTI 3MTAR OSAMANGA BWANJI
DJ ❤❤❤❤❤💯💯💯💯💯
Ulemu upite kwa tv mulungu ntanyiwa ndi Dj munyanane
Kkkkkk uzibwelabwela
Satan's anali m'busa 😂😂😂 panoso akungokwera akazi a eni
😊😊😊😊😊
Ndimachedwatu
Munyanane woyeeeee!
Dj yomweyo ipase moto asakufuna akagone
🔥🔥🔥
Ng'alura
Moto dj
Ndipo ziko la pasi Lokomela achuma ndipo zoipa zimachitkila abwino zabwino zimachitikila zoipa koma tose ndi ake ndithu
Ma jaji akumalawi.naonso ali ngati asilikali NDI a Police anasankha kugwira ntchito ndi chipani kusiya kulemekeza malamulo , komaso Ben longwe AMENEYU AZIYENDA mosamala timutchola nsagwada dziko si lamake kapena chakwera ,
😂 koma ili madzi mcp 😂 komaso iwe ndimoto mr lomwe ukukwanilatu😂😂😂😂 owulule onse mr lomwe
Do ndipo live mukuveka bwin ndiripano kukusatirani benlongwe ndisatana uyu palibe omwe angachivere chimenechi dj mulibho
Tikukuvani kwambiri kuchokela kuno ku eastern cape mthatha
Uku kuli zabwino so chonchi
🎉🎉🎉🎉🎉
Mwanzi ugwila nchito
Achimwene tikumvani kuno kutanzania mukumveka ndipo mupitilize
Dj wabho uyu
DJ Munyanane,how can I get the instrumental playing
Sounds like Rex Rabanye songs
Thanks boss
Umakwana DJ Munyanane🔥🔥🔥
Tinya nawedi sure
Dj munyanane mballi yanji mulli iweyyo ullibho nanga ennawo allibwanj osawopha osavowonka ndive amalawi mtanyiwwa osawopha bakili muluzi TV osawopha mulungu adalise wina aliyese astaguffllal yha Allah tiutseni soona shonde
😂😂😂
Amasulidwe with immediate effect
Hiw can I get into Ur WhatsApp groups?