BREAKING NEWS NKHANGA ZAWONA PA LIMPOPO FM NDI COMRADE NTANYIWA KWABWERA MA ISRAEL 11 pa 15 SEP 2024
HTML-код
- Опубликовано: 17 сен 2024
- NKHANGA ZAWONA PA LIMPOPO FM NDI COMRADE NTANYIWA CHIGAWO CHA USIKU,KWABWERA MA ISRAEL 11
Izi ndi zomwe wayakhula
Thanks Mr ntanyiwa God protect you all the time
Koma social media osazaiyiphweketsa guyz
Kodi asilikali ntchito yawo ndi chani,eeeee koma ngati nkulu wa asilikali wadya ndalama,akanangotula pansi udindo wake, mmmmu atipwetekesa galu ameneyi
Mcp zopha chilima,ma plan anayamba chaka chomwe tinavota coz nkati mwawo munali dyera ndi ugogodi.
Guys kodi tikudikila chani? Tatiyeni kumsewu chikangawa akufuna kuyambitsa nkhondo inu simuona? Mbuzi imeneyi akutiona a malawife kupusa
God protect you mr tanyiwa,why God
May ALMIGHTY ALLAH protect Mr Ntanyiwa 🙏
Thanks mr Ntanyiwa God bless you
Big Up brother ❤❤❤
Tiyeni pa nsewu basi chakwera wationjeza
Siteti house ija kwasanduka kosugirako zigawega basi
tiyeni marawi tidzuke tisango chonde chonde mandem chakwera wanjaira machendeake osadura
Mtanyiwa ndi #1🎉🎉🎉🎉🎉
Achoke uyu bas Chikangawaaaaa watikwana Panseu amalawi
If there are organizations that help countries, please, come and help Malawi. I don’t want to face this….war. We are tired of crying. We don’t want to cry again. God help us.
We have been waiting for this continue to give us the best analysis of what is happening around the world
Basitu I now believe that Ntanyiwa stays in heaven...
Mbambande boss
Limpopo FM ❤ nkhanga zaona
❤❤❤❤ tikadali maso sitinago
Tiyen pamsewu basi chakwera achoke
Apuresdent chepesan kubwelesa alendo ankhondo mudziko lamalawi sizabwino anthu amatopa mukakhala mukumbukile za kukenya chonde Mr puresdent
Big brother
Comrade ingondipatsa ineo ndivere that audio cfkw ndatopa ndi manyi akubiba cakwerawa
Umatiimilila comrady mtanyiwa
Panseu athu munafooka athu opangisa mademo anatha
Timakukondani❤❤❤❤❤
Tingangowotcha Start House 🏠🏠 Yoo bas iyah asatitopese Chikangawa pathako pache
Wel come
Zikachitik tivera kwa inu ❤❤
Koma zoona tidikile mbozi zilowe mmutu mwanu comrade??? Release the audio!
Alore alore akane akane welcome comdred mtanyiwa
Comryde ntanyiwa in,galuleni basi aziwe kut inuyo simuthu wamba
Akumatiwonjeza munthu uyu ateromo akufuna kupha anthu ena nde munthu uyu zufunika kukawotcha Stars House komweko aaaa atithano mmalawimu
Ndipo tiyeni
Aaà a MCP sakugona ndi notse mukuwulula dzotsisi za MCP nangao nyumba yaboma yasandika kolandikula dzigawenga KOMATU MA ISRAEL AWA KUTSAFE MUNTHU ONTCHUKA AMALAWI MWAWONA KUWAWA MASOKA ENAWA OTSAMAYAMBA DALA mwina abwela kuthandidza pa nkhani yobela chitsankho ngati dzili idzo nde amalawi mudzawadziwa 2025 kuti akachepa kayenda MCP tsamalani idzi mukupanga magadzi achaka chamawa
Umakhwwana heavy Comrade Nthanyiwa,usazafe ,uzangosowa like Enoch mu bible. Pliz audio imeneyo plizzzzzzzzzzz uyiphulise ,agalu amenewa akukoza osagwirira😂😂😂😂😂
Chifukwa chale awagenda kusanje
Antanyuwa mumatiyimilila mwa wa angaga uku ku nsika wanjala timenyele nkhondo amalawi
Chakwera the maphia
Iiiihhh sad
Antanyiwa tapangani za ma audio amundegewo kut tione kuti tichita motani
Eeeee koma chakwela
❤❤❤❤
Work up guys 🤔🤔
chakwera machende ake akufuna kubweresa khondo muno eti machendeake abambo ake
❤❤❤❤❤❤ ntanyiwa your my mfumu
koma Kodi kuribe anthu wotithandiza kuti atiyimire Kodi anthu wose agurika ndindarama koma ziko rathu rikupita kuti abare tose tiri ziii zinthu zikuwonengeka 😢😢
Vuto tilibe Atsilikiraki olimba mtima kuti ayambise kuukira,,anakayambitsa ife tili ready kuwathandiza kuti tithane ndi chikangawa
kod ntchit ya MDF ndichan 😂😂😂😂😂
Kuteteza mbava zikuluzikulu
Zopanda umboni izi
Ine aluya akamadana ndi dziko la Israel ndi ngati ndi anthu odzikonda koma panopa nazindikila chowoonadi kuti anthu amenewa ndi Haram
Tangoponyani asanaphenso anthu ena please maliro atikwana ife eeeeeee
Mmmmm koma malawi
Kodi ya ng'ombe ijah simunafufuze kuti zafa ndi chani chongo Kona iwowo
Zabwana issa zijah
Koma asilikali ah Malawi Defense Force akumva bwanji nkhani ngati idzi? Koma Chakwera galu wa munthu kwa basi
Chenene
Eeee koma chakwera
Mademo...akufunika a violence,ngati achina mtambo aja,ndipamene angature pansi udindo
tiyen pa msewu guys achoke chikangawa atipha kenako tonse
Uremu wanu❤❤❤❤
Kuankhula koma simu chitapo kanthu anthu oipa inu
Ndipo zoona zake nanga titani tikanva zimatiwawa
Kodi asilikali alikuti? Kuti azinthandiza dziko muno abale mulungu wanthu atinyhandize
Kidi asilikali a mw tchito yanu ndi chani mwangokhala ngati mwagon bwanji
Ndipo inu,,, tikungofuna silikali oti atilimbise mtima akhale kutsogolo kwathu ife tigwire ntchito
Tulutsani odio yo tive
Choka wa wa chamba