Ati TB Joshua Anali Njoka, Njonda, Chigawenga ndiponso Ogwirilira - BBC

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 4 фев 2025
  • Chenjera Malawi Chifukwa Onga Iye Akhera Kwa Iwe

Комментарии •

  • @dingiswayokatundu2696
    @dingiswayokatundu2696 Год назад +1

    I think you are right dear brother. There is alot of sense in what you are talking❤❤❤❤

  • @thulambale2836
    @thulambale2836 Год назад +3

    You are right my Dear brother

  • @PromiseKhenzo
    @PromiseKhenzo Год назад +2

    U R SAYING THE TRUTH 😅😂

  • @Dee-h7c
    @Dee-h7c Год назад +1

    🔥🔥Anthu amadana ndi chilungamo✳️✅️

  • @jameschiziwa
    @jameschiziwa Год назад +1

    This guy is absolutely right remember the book of Mathew 7vs 21-23.lets carefully with these so called man of God

  • @JUSSABNTAIBU
    @JUSSABNTAIBU Месяц назад

    Sense ❤

  • @ZephaniaBanda
    @ZephaniaBanda 9 месяцев назад

    Mulungu apseleleze kamwa yako mudzina la Yesu kristu

    • @staprickskilled
      @staprickskilled Месяц назад

      mulunguyo akanakhal alipodi ndikanamuswa mbama 🤣🤣🤣🤣

  • @stanleykaludzu-bm4pm
    @stanleykaludzu-bm4pm Год назад +1

    We are not moved by this....to us Who followed him we have testimonies of how genuine he was as Man of God...keep resting man of God TBJ...You fought a good fight.

  • @KassimRasheed
    @KassimRasheed 9 месяцев назад +1

    Azi prophet wa ndi njokazenizeni afiti achabechabe agalu enieni

  • @staprickskilled
    @staprickskilled Месяц назад

    prophet kaya m'busa aliyese ndiwabodza

  • @HarietMtambo
    @HarietMtambo Год назад +1

    Kuteloku mbuzi ndiwe bwanji sunkadzuka munthuyo alimoyo nde ukubwela apa nkumazalankhula zopanda nzelu ife sitimakuombela mmanja tangopeza zina zoti uzichita chifukwa olo uziti amalawi ndiopusa iwe nde wachenjela chani

  • @thabitiesulaiman6194
    @thabitiesulaiman6194 9 месяцев назад

    Mukunena zoona m.balewanga ngakhale ife ku shisilam sithikhulupilila miracles or pang.ono amene amapanga zimenezo timati ndi afiti chifukwa after Abraham mose yesu komaso Muhammad mtende wamulungu ukhale kwa osewo palibe amene angapange miracles never chifukwa izo zidapita kale munthu ya atumiki nde brother mulungu azikudalitsani

  • @BrianFrazeh
    @BrianFrazeh Год назад +1

    Tb Joshua anali mneneri wa Mulungu amene akumunyozawo Mulungu awakhululukre sakudziwa chomwe akunena😊

  • @SlyvastyMiti
    @SlyvastyMiti 8 месяцев назад

    22:34

  • @sungananigondwe2807
    @sungananigondwe2807 9 месяцев назад

    Kutero amene akuyankha ma msg obakila Joshua muzaone ndiwankazi agalu chabe chabe

  • @TabuGondwe
    @TabuGondwe Год назад

    Nthawi yomweyi munali kuti mwawona kuti church yikuyenda mwayamba kubwebweta Mulungu akuyendereni

  • @StanleyKaila
    @StanleyKaila 7 месяцев назад

    Ambuye akukhululukileni kwambiri

  • @RachellTembo
    @RachellTembo 8 месяцев назад +1

    Uyu akunena zoona

  • @MasausoHopuson
    @MasausoHopuson 2 месяца назад

    Aise umanena chilungamo upitilize kutiziwisa zambili timakunyadilani kwambili amwene mot

  • @NoahKalima
    @NoahKalima Год назад

    Koma ntumbuka iweyo ,,unachenjera mopusa,,paja ulimwana unagwela ntchimbuzi ulimwa eti,,

  • @godfreybiziweck1224
    @godfreybiziweck1224 Год назад +1

    Kod amwene mmakhala kuti mwasuta chamba kapena bwanji kwenikweni

  • @petroschigete2460
    @petroschigete2460 Год назад

    Tisaweluze woweluza ndimulungu mungochedwanazo mudziwa bwanji analapa bwanji simunabwelw poyela mwiniwakeyo alimoyo pezanizina zochita

  • @SlyvastyMiti
    @SlyvastyMiti 8 месяцев назад

    Iyo ndiyo bobza.umakamba.chilungamo.

  • @marthansaliwa7732
    @marthansaliwa7732 Год назад

    You can not change Okhulupirika Chauta. Dzikoli likutha chomwe lucifer akufuna ndi kutenga ake wochuluka ku mpando wake wachionongeko. Palibe mwakambapo apa dhala chogwira mtima. Azunguwa akupusitsani. New world order at its best. Ziwerengani Mau a Mulungu mupulumuke. TB Joshua is dead. Why are these people coming out now. Why not come out and talk when he was alive. Okhulupirira Chauta sasunthika ndi nyengo zabodza za satana. Tili munyengo zotsiriza izi.

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Год назад

    Ngondolo iwe wadya chamba kwambili mphuno yaikuluyo

  • @inutuinutu5573
    @inutuinutu5573 7 месяцев назад

    Zabodza.. watch out the things u speak.. God's judgement will be on you

  • @mathewschifya764
    @mathewschifya764 Год назад

    Mkwenda nkhuni uko?

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Год назад

    Mphuno yayikuluyo iwe ndindani satana

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Год назад

    Iweyo wazitenga kuti