Even the MEC chair herself knows that things are not going fine but seems like she is just there as the name, the salary and allowances only.She is just doing and even said what she always told but in her head knows the truth. My God be with our Country, Amen
NRB chilungamo chikukuvutani ma guy 2018-2020 MEC and NRB amagwilira ntchito limodzi and applications form ija ya NRB sticker ija imatuluka pompo pompo 😅
I don't understand why Lilongwe mean ku BT anthu aliko omwewo basi kkkkkkkkk ayi sizoona ndekutu the hole Malawi anthu ambili amakhala ku Lilongwe zaboza iziiiiiiiii inu mwatani bravo times ❤❤❤❤❤
Afotokoze zoona aNRB akapanga zibwana 2025 atiziwa kuti ife sitifuna zibwana tiliononga ndi zipolowe ife si Ana am a 1940 ife ndi a ma 2000 aphunzira mcp sitikuyifuna yatizunza pakwana.
Where are the ID cards printed. Zokondera ndizaona, umboni ndili nawo Ndithu. Amaweruka 3 okoloko and I even called one of the Officer and all the people that came after 3 o'clock were referred to the district NRB head office
Best program forever Times Tv is the best 🔥
Even the MEC chair herself knows that things are not going fine but seems like she is just there as the name, the salary and allowances only.She is just doing and even said what she always told but in her head knows the truth.
My God be with our Country, Amen
Munatiyankhulira gyz keep it up ndipo mulibembali
andevu mumayamkhura moveka mogwira mtima mwachikond kmaso mwachilungmo
Ashibale ashinawanda amenewo akunama ndithu
Mmmm asaname sakumalemba zolongosoka anthu timangobwezedwa kuti chimatchini chaonongeka
Mphatso Sambo ukuzitenga ngati wochenjela kuposa Atimes Machendeako
Kodi jene ansa anali wadpp bwanji sananene kuti uyu ndi wadpp adpp mwachulusa zonena
NRB chilungamo chikukuvutani ma guy 2018-2020 MEC and NRB amagwilira ntchito limodzi and applications form ija ya NRB sticker ija imatuluka pompo pompo 😅
Nkhani ndiyoti winaaliyense akalembetse mu kaundula wa chisankho basi. Nkhani ndiyoti umboni ulionse ukagwile ntchito, ngakhake chikalata chakwamfumu .
DPP yaluza tisanavote😂😂😂😂
Kikikikik koma Brian amaziwa kutsila mchere😂😂😂😂
Inu kupoto ndikubwela kulibe athu ochuluka ndikubwela ndiye sitheka bwanj kuchuluka athu ku central ndikupoto 2m kumwela 8k koma mcp anjaila kwambili amec agulidwa ndj nrb agulidwa ndi mcp uyuyu wameyu wagulidwaso koma mcp isalowe boma mulungu yankhani pembezelo langa
BT anthu osakwana even 1 mita eti koma LL ndiye mpaka kuthamangira 2 mita eeeeeee kuli zinthu eti !!!!
I don't understand why Lilongwe mean ku BT anthu aliko omwewo basi kkkkkkkkk ayi sizoona ndekutu the hole Malawi anthu ambili amakhala ku Lilongwe zaboza iziiiiiiiii inu mwatani bravo times ❤❤❤❤❤
Akuphatikizatu ndi a 2020 aja
Sakuyankha mfunsolo amenewo abwanawo ayankhe momveka bwino
Afotokoze zoona aNRB akapanga zibwana 2025 atiziwa kuti ife sitifuna zibwana tiliononga ndi zipolowe ife si Ana am a 1940 ife ndi a ma 2000 aphunzira mcp sitikuyifuna yatizunza pakwana.
Ine ndinajambulitsa mu march up to date id sinatulukebe
In time of DPP mec and NRB were working hand in hand polembetsa chovotera opanda ID amapita kukalembetsa awa akufuna atisokoneze
Chifukwa chani ku Lilongwe analebesa ambiri more than ma boma ena even osakwana one million ma ndela ena
Aziwona RRB amayenda mbali
DPP ndi yakuba Jane assah komanso jean mathanga onsewa ndi a DPP panopa onsewa Ali ndi ma udindo kuchipaniko
😂😂😂😂😂😂
Iwe wa N R B bwanji kusalima sunabwele kuzalembetsa komaso tikalimbetsa sakumatuluka mukumawasiya kut inuyo
Agwirizana basi ndi boma kuti abele
Kumalawi munthu akawina u president amarephela kuyamba kupanga chitukuko amayamba kupanga ukampen mwalo momanga chitukuko saulosi chilima adalakwa chani inu achakwela kupanda saulosi chilima mukanawina inu relo mukurephela kufotokodza mkhani ya ndege why
Guys mumatiyimirira ndithu,
Tili ku Pretoria koma timadzitsata through Times
Zisiluzi zaonjeza kongoelekeza kubela nde aliyese azipanga zake Malawi muno
Kkkkkkk
Where are the ID cards printed. Zokondera ndizaona, umboni ndili nawo Ndithu. Amaweruka 3 okoloko and I even called one of the Officer and all the people that came after 3 o'clock were referred to the district NRB head office
Aaaa mcp kunena mwachuchu mcp tikufuna mubela ndithu
Ingovomelani kuluza basi
NRB ikugwira ntchito yawo mokondera nalembesa 2022 koma mpakana pano ID yanga sinabwere ndayendera kutopa akuti zinabwera koma anabwera kuzazitenga kukazisiya ku Lilongwe mwezi uliwonse ndikumayendera koma kumangobwerera phone ndaimba ndaimbaso
Kwqchematu
Kulilongwe ndikumene ali anthu ochuluka papenepo
Koma tisayiwale kuti tinapanga mademo kuti dpp yichoke,ndye palibepo wabwino apa
Pakufunikaso mademo
Sanalembe moenela
U r waisting