Milandu Ya chilima Yatha | Kaliati Ndi khwimbi La UTM kusangalala ''Athyola dance''

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 6 май 2024
  • Patricia Kaliati Ndi khwimbi La UTM kusangalala ''Athyola dance''

Комментарии • 37

  • @GetrudeMkandawire2
    @GetrudeMkandawire2 2 месяца назад

    SKC Boma motooo buuu 🔥🔥🔥🔥

  • @HassanTayubu-li3tm
    @HassanTayubu-li3tm 2 месяца назад

    Amazing inu mulibe nzelu kwambili

  • @KaipaEmanuel
    @KaipaEmanuel 2 месяца назад +1

    Chilima keep it up bwana

  • @WalikoMsutu
    @WalikoMsutu 2 месяца назад

    Zikakunyasa uwone zochita UTM 🔥🔥🔥

  • @user-ve7rx7vj1g
    @user-ve7rx7vj1g 2 месяца назад +1

    Muyambeso kutinamiza...kulakwatu uku aMalawi

  • @Dorah-zl9uf
    @Dorah-zl9uf 2 месяца назад +1

    Kkkk koma kaliyati sazatheka😂😂

  • @QueenNhlema-sc3nh
    @QueenNhlema-sc3nh 2 месяца назад

    SKC my vote❤❤❤❤

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z 2 месяца назад +1

    Basi tu a zimayi 😂kumadikura 😅

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o 2 месяца назад

    Wakwiya ndi mfiti SKC 2025 BOMA ❤❤❤❤❤

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 2 месяца назад +1

    Komatu aMalawi kumachilapa chilima ndi chakwera nzawo ndi zimodz pls kumaganiza mwakuya popanga chisakho chanu mutipwetekesaq

  • @user-dd9yq9qk1k
    @user-dd9yq9qk1k 2 месяца назад +1

    Mwaiwala kale a Malawi ayi zikomo

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 2 месяца назад +1

    Ukukup sakokakoka kukala ngamti opandazelu kusangalila chakumba chilima ndi mbusi chkwera palukundu pao iya yausilu uweiyai chatap

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 2 месяца назад +1

    Aaaa agalu nokha nokha ndi ndi MCP yanuyo okuba okha okha zauchitsilu mene wathelano malawi pano kumanyadila idzi thembelelo chiyani amalawi

  • @user-qj3db4lu7c
    @user-qj3db4lu7c 2 месяца назад

    anthu amene akuononga dziko ndi azimayi amangokondwera zilizonse,Koma pamapeto pake amayambaso kulira ndiyiwowo

  • @ChifundoChiwanda-ru3pg
    @ChifundoChiwanda-ru3pg 2 месяца назад

    🔥🔥🔥🥳

  • @manasemaposa
    @manasemaposa 2 месяца назад

    Bravo

  • @ThomNkhoma-no5rt
    @ThomNkhoma-no5rt 2 месяца назад

    🔥🔥🔥

  • @HassanTayubu-li3tm
    @HassanTayubu-li3tm 2 месяца назад

    Anthony inu mukungovomeleza zosalongosoka mukafika kunyubako mukukangona ndi njala

  • @temwamfunejere
    @temwamfunejere 2 месяца назад

    SKC🎉🎉🎉❤❤

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 2 месяца назад

    A dpp akuwona nyekhwe kaye ku bagamoyo nyekhwe inatembenukira😂😂😂

  • @user-kr8th5oh7b
    @user-kr8th5oh7b 2 месяца назад +1

    Kusangalarila Muthu okuba a Malawi amaganiza mopeoera

  • @hopembendela
    @hopembendela 2 месяца назад +1

    Panyapanu agalu

  • @KaipaEmanuel
    @KaipaEmanuel 2 месяца назад

    Asowa nazo kolowa kd .?

  • @jahmanmakwinja-ef7zn
    @jahmanmakwinja-ef7zn 2 месяца назад

    UTM yabwera kudzakhala,, take it or leave it, afune asafune. Next government ndi UTM led by SKC

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 2 месяца назад

    Inu munawona okuba okha okha akumangana uchisilu mudzalowabe mundende bola moyo

  • @Hlehle719
    @Hlehle719 2 месяца назад

    😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 2 месяца назад

    Ayi zikomo anthu inu koma ndi chani???

  • @Abdul-xk8dq
    @Abdul-xk8dq 2 месяца назад +1

    Koma mukusowa zochita chosecho maluzi alitho

  • @louisbonongwe8537
    @louisbonongwe8537 2 месяца назад

    Koma campaign iyaka

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 2 месяца назад

    Ndikamaona anthu akumasapotabe chilima ndi tonse alliance ndimangot amalawife tilindivuto lalikulu.koma zoona anthu amenewa atipusisa kale 5 years for nothing still kumawaomberabe manja.agalu amenewa 2019 amabwebwetuka kut anzawo anali olephera lero iwo alowa mkat zero kwa 10 lero anthu akutengekabe nawobenso.amalawi ndife ofa kuzimu ndithu ndi thupi lomwe ndife osaganiza timangooneka ochenjera koma tulo lilindife Mmmm zosaoneka.timatengeka ndizazing'ono kwambili even tishirt imene sitichedwa kuiwala ndife agalu eni eni.atipusisenso kachikena makapewanso tiwaikenso pampando for 5 yrs again zoona?iwo alibwalo akulephera kumenya mpila pomwe ama bulema anzawo kumati olephera.timilomo tawoti tinabwebwetuka kwambili mu 2020 muja apatayambanso kunamiza anthu 😂😂😂😂 mayo I cry for my mother land Kaya nabadwilanji kumalawi ine ambuye tikhululukileni ndithu sitidziwa chomwe timatsatila ndife akhungu mmalawi muno.and sitidziwa chomwe timafuna ife pokavota timangopangila kupsa ntima basi osalingalira zamawa.

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 2 месяца назад

    MCP amatelo inu muli ku kenani anzanu kuwasiya kwa pilato zaka zonsezi, ulendo onyamukira limodzi.

  • @user-wi9pe2hz7e
    @user-wi9pe2hz7e 2 месяца назад

    Masanje eni,,eni,,kulephera kuimba njaratu imeneyo😢😅

  • @umalimaganga
    @umalimaganga 2 месяца назад

    CHIPANI musachichepetse ichi nchamoto

  • @CHAKUWALOMKANDAWIRE
    @CHAKUWALOMKANDAWIRE 2 месяца назад

    Nice