'AMANDIYAMWISA MALISECHE DAILY '- MMWENYE AWUZA WA NTCHITO ADZIMUYAMWA MALISECHE
HTML-код
- Опубликовано: 19 окт 2024
- MMWENYE AWUMIRIZA WA NTCHITO KUTI AZIMUSEWERETSA MALISECHE
Kupeza ntchito ndi chinthu chokoma kwambiri kwa munthu aliyense makamaka uyo amene wakhala nthawi yayitali akuyisakasaka ndipo ali ndi anthu amene amadalira iyeyo monga makolo, ana komanso mkazi. Pamene munthu wapeza ntchito ndiye kuti amakhala ali ndi chiyembekezo chachikulu kuti zinthu zake zisintha ndipo amene amamudalirawa ayamba nawo kukondwa. Komatu zimenezi sizili motero kwa mkulu wina wochokera mu mzinda wa Lilongwe. Mkuluyu amene dzina lake sitilitchula anapeza ntchito yophika kwa mmwenye wina a Jayesh Kumar Dalwad amene anali wothandizira ntchito za mkulu wa kampani ya Shayona Cement Corporation ku Kanengo analibe malingaliro akuti chimwemwe chake chakuti wapeza ntchito chitha posachedwa ndikuyamba kukhala moyo wa mavuto.
Atakhala kwa nthawi yayitali asanapeze ntchito, mkuluyu amene amakhala kwa Mtsiriza mu mzindawu anali akukanika kusamalira ana ake atatu, koma mu mwezi wa January 2023, iye anapeza ntchito ngati wophika ku nyumba ya bwanayu imene ili ku malo amene kuli ma office a kampani ya Shayona yi ku Kanengo. Atangogwira ntchitoyo kwa mwezi umodzi, mwezi wotsatira wake umene ndi wa February zinthu zinayamba kusintha ndipo akuti abwana ake aja anayamba kumamawuza kuti adziwasisita bondo lawo.
Aaaa zanchamba bass
Iyeyoso anagwirizana nazo bwanjibosangosiya nchitoyo bwanji nonse machende anu 😂😂😂😂😂😂😂
Mumabweretsa nkhani zofunikira koma musinthe speed yamalankhulidwee
Ndipodi ife kuti tinve bwino bwino palitu ntchito 😂😂😂🤣🤗🤗
Mwina ndi manyado,ineso sizimandiwaza
Ndipo ndie zimanyasa
Muthu kwanu ndimulolela kupanga zimenezo zaziii zauchisili ngati zimenezo
It's bad!!!😢😢😢 plz amalawi munthu ameneyo amangidwe
Km guys kwathu komwe tizilandila nkhanza zoterez amalawi ena kumavomeleza km mmm 😢
God have mercy on us
Aaaaaa zauchitsiru basi,amangidwe ameneyo basi
Umphawiwo wakula bwanji mpaka kuvomeleza zimenezo bwanji osawulura kapena kusiyana ntchitoyo kuyamba zochita zina
Hahahaha ine olo zitavuta maka sindingapange zauve ngati zimenezo
Ayi wachitola chikwama
Nanga ma million onsewo pajatu ndalama zilimunyasi
Nseu wamangochi wu zikukhala bwanji?
,,,😂😂mzimaiyo akunama amafunanso nae amagwilidzana naeso akufuna chipepetso eti 😂😂😂😂🤸🤸🤸🤸🤸
Sinzimayitu
Eishhhhhh zosayenda bwanji
Koma ndikhani iyiyi boma lamalawi limayenera kumuitanitsa mwenye ameneyu kuonetsa kukwiya nazo
Boma lake litiro brother???😂😂😂😂😂
Mpaka Chaka kumalorera zimenezo mavuto ake amtundu wanji
Osamuluma nchilawakewo bwanji kkkkk ndikuluma maphwala akewo bs yesyes kkkk
Mmmmmm koma abale zina ukambva yohhh kukhwima kapena?
Channel ichi ndichonama
Eshiiii
Mchitsilunso bwanji ameneyo
Amalawi akaona nkhungu lofiira eish
Amangidwe mwenyeyu
Umphawi ndi mavuto
We shouldn't Allow this in Malawi, that's not acceptable here,..
Osaiwala kuti Chakwera ndi chilima nawonso ndiodanatu ndi chilungamo ndie izi zangoyenera kumachitika basi
Boma la Tonse Alliance ndilodana ndi chilungamo nalo ndie atha kukamumanganso bambo olakwilidwayi poti
Umfiti amabungwe loweleranipo chilungamo chichidwe basi
Kulakwa 😢
Koma amwenye sazatheka 😢
Ndipo kwambiri
Asaaaa 😂😂
Iiiiii shaaaaa!!!
Munthu ukuvutika kut ukufuna ntchito umapanga chitheka so I don't blame him ndipo iyeyo amkafuna kusamala ntchito komanso amkakukumbikila mavuto akwao koma munthuyi adangokhala oipa basi
Kupusa bwanji samakadandaula ku ma bungwe ndi opepera
Km ndye bola andicose ntcito
Mmmmmm 😢😢😢😢
Sad
Chanma lindimo umo😂
Why Malawian we allow such pple
Chitsiru ndiiyeyo vuto longochoka koweta ng'ombe 😒😒
Umphawi szinthu
Uchisiru bas
Mmmmmmm zotsayenda
Zopusa
Zovuta aaa
Amabungwe kuno changu
ma gay achimwenye🤨🤨🤨