Zomwe wayankhula Waxy Kay pa Maliro a Bambo ake a Bishop Kapenga ku Robins Park in Blantyre

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 1 июл 2024

Комментарии • 79

  • @JOHNOlesmasCosmas
    @JOHNOlesmasCosmas 3 дня назад +20

    imfa ya munthu olungama pamaso pa Yehova pamakhara chimwemwe zilibwino indeed
    waxy mzimu wa Yehova ukuyankhura iye wangokhara chotengera chake
    may His soul rest in internal peace 😭😭😭

  • @ListerMunthali
    @ListerMunthali 3 дня назад +10

    Ndikukumbuka mu ulaliki wina wake bishop kapenga ananena kuti ngati situation ndiyoti sungayisithe no matter what, osalira just say zikomo ambuye.
    Pachifukwa ichi nane ndikuti zili bwino ndi mzimu wawo for God has relieved him from all his pains🙏

  • @WellosMphonde-wd2cx
    @WellosMphonde-wd2cx 3 дня назад +5

    Munthu akamwalira kulira kumatanthauza kusowa chiyembekezo pamene mau ake a Mulengi amati tisalire pakuti mu zonse tidziti zilibwino nde mukati speech yolakwika nde kuti chani. Lolani akulimbika mtima akhale akulimbika mtima pakuti ndi mawu ndipo mwa mawu tidzachuta mwa mawu. Say Amen/Ameen

  • @user-pn7cj9hb3t
    @user-pn7cj9hb3t 3 дня назад +9

    Chomwe walakwitsa Waxy Kay ndi chani anthu inu? Kapena simudziwa mau simudawelenge?

  • @user-uo3lm5wl5j
    @user-uo3lm5wl5j 3 дня назад +6

    Ifa ya wamuthu olungama kumwamba kuli chimwemwe mwAna wazelu kwabassi ndiwochepa agazindikile mawu wayakhula mwanayu Kwa amene amakhululupila mulungu wava tathsuzo lake amen

    • @MaeCuinhane-gq7ub
      @MaeCuinhane-gq7ub 3 дня назад

      Ndipo imfa ya munthu oyera mtima imakhala yokoma chifukwa amakhala akudziwa za komwe akupita

  • @ALINAFEMKOMERA-cm1md
    @ALINAFEMKOMERA-cm1md 3 дня назад +4

    He got broken... He wrote a status he was comforted that he should be strong since the father is in a better place
    Now he is strong anthu muyakhulisaso
    Mumtima akuliratu munthuyu

  • @LeahNundwe-wh6vz
    @LeahNundwe-wh6vz День назад +1

    Today's children at their parents funeral leaves alot of questions really

  • @AnthonyChibwe-bf4de
    @AnthonyChibwe-bf4de 3 дня назад +4

    He has to say so,, there is no way kut azikhala akudandaula yet zinthunzo zachitika kale komaso sangathe kuzibweza pat. Mmalo moti azingodandaula wasankha kusangalala that's a good choice or adakayankhula zodandaula zidakasintha chan? Umenewo nde umunawo mesa,

  • @thokozanisukah6448
    @thokozanisukah6448 3 дня назад +1

    Indeed zili bwino aliyese azafa komano kuluza munthu sichithu chophweka nde kumankhala makolo ako

  • @mikheykaunda3540
    @mikheykaunda3540 День назад

    RIP Munthu wakulu Kapenga we shall miss u

  • @RedKoffii-gl2vx
    @RedKoffii-gl2vx 3 дня назад +6

    Mwana ulimba mtima

  • @samuelkapasula-mn6es
    @samuelkapasula-mn6es 2 дня назад

    Zoonadi.....Zili bwino mwa Yesu khristu.....

  • @MDAmir-ku4lf
    @MDAmir-ku4lf 2 дня назад

    Waxy akunena zoona, mau a munthu okhulupilira ndi oti zilibwino. Abale amzanga munthu akamwalira sinthawi yoti ife tizilira ndi nthawi yosangalala chifukwa chani ndikuyankhula choncho, chisanzo munthu akamagwira ntchito kaya ndi pa company kaya m'boma amayembekezera kuti mwezi ukatha akuyenera kukalandira salary, ndiye funso nali, ndindani amene amapita kokalandira salary akulira tipeza kuti palibe wina aliyense amakhala osangalara kuti lero tikadyera nyama, ndi chimozimozi inu ndi ine mulungu anatisankha ndikutisiya pano pa dziko lampasi cholinga chimene anatisiila pa dziko la pansi ndi chani tizimugwadira nthawi ndi nthawi, ndiye tamugwadira mulungu, mwini wake emweyo yemwe timamutumikira uja watiitana tamwalira ndicholinga choti akatipase malipiro pa ntchito yomwe iye anatipasa takhala tikumugwilira tidakali ndi moyo abale amzanga sinthawi yomalira imene ija ayi ndinthawi yotchulusa kupempha kwa mulungu kumupemphelera m'bale wathu kuti ngati anali ochita ntchito zabwino mulungu amuonjezere zabwino zochuluka pa ntchito yomwe iye anali kugwira adakali ndi moyo komanso ngati anali ochita ntchito pena zoipa mulungu asachulukise kuyang'ana zoipa zake Ameen

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 2 дня назад

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤

  • @POker_On1.
    @POker_On1. 3 дня назад +1

    Zibwíno 🙏🏾

  • @ZaffboyYellows
    @ZaffboyYellows 3 дня назад

    I'm very sorry 😢Your highness young king. If you want to talk ' I'm here at any time

  • @FlorahBanda-fl4vf
    @FlorahBanda-fl4vf 3 дня назад +7

    Speech iyi ndiyofunika azungu koma ife tiziti mwatilawula😢

  • @WakisaPhiri-e1e
    @WakisaPhiri-e1e 3 дня назад

    RIP Pastor 😭 Anthu awa amkavana

  • @user-ly4ug6wm9k
    @user-ly4ug6wm9k День назад

    My grandma said when someone passed away within two days ,,,,,,, umawona ngat zocheza koma dikila pathe masiku nde akut zilibwino ??? Pamenepa😢

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e 3 дня назад

    Owooo chabwino

  • @nkosikhonasiphiwemdlalose227
    @nkosikhonasiphiwemdlalose227 3 дня назад +1

    Some of the tribes in Zim they celebrate when they lose someone zili bwino akapumule ali ndi Yesu wao

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 2 дня назад

    Mauabwino kwamunthu olungama❤❤
    0:11

  • @chemapa
    @chemapa 2 дня назад

    zabodzazo zosamvekazo Mulunguyo anamuuzira kuti? pamaliro sitchukira. tisamaseweretse dzina la Mulungu. kulowetsa chibwana pamaliro a mtumiki wamulungu.

  • @Queen-m6f
    @Queen-m6f День назад

    May His Soul Rest in Peace 😢

  • @kondwanibuleya-br9gr
    @kondwanibuleya-br9gr 3 дня назад

    😢 what a man up

  • @Choicemlw
    @Choicemlw 2 дня назад

    Yesu analira pa maliro a Lazaro

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 3 дня назад +1

    Osamamuchemerera mfanayu ndikape chisiru paumunthu speech umatulusa malingana ndimaro ache awa anali bambo ake osati ngt kanali kushow koziwonesera kt kaya akazi akafire zachamba

  • @jamesbowman-cw8ts
    @jamesbowman-cw8ts 3 дня назад

    Koma ndiye Kuli mixed bag of comments,... Waxy this Waxy that,... aMalawi musiyeni mwana, walimba mtima ndi chiyembekezo kuti bambo ake ali malo abwino opumula ndi Yesu wawo ndipo palibe chodandaula,... Ndiye mukuti chani anthu "abwino" komanso osunga "chikhalidwe" chachiMalawi inu??
    Pena ngati ndinene kuti dikirani abambo anu akazamwalira muzayankhule speech yanu yabwinoyo,....koma poti imfa si yabwinonso. So whatever,
    Rest well Bishop Kapenga. We knew as man of God and we're sure to God your soul has returned. Rest Bishop rest🕊️🕊️

  • @jelblinds2017
    @jelblinds2017 2 дня назад

    There is nothing wrong jst that we as malawians have poor and shallow minds

  • @unarinematshomo2841
    @unarinematshomo2841 3 дня назад

    Muthu akamwarila, timarila pa nthawi imeneyoyo, ndee waxy kay sanalakwitse moti speech yake ili bho ndithu.

  • @OwenTembo-xq6ug
    @OwenTembo-xq6ug 3 дня назад

    Sizilibwino ndizolilitsa kwambili 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @Mphatsolikotima
    @Mphatsolikotima 3 дня назад

    Rip bishop kapenga 😢

  • @ShyreenKwisongole
    @ShyreenKwisongole 2 дня назад

    Emen

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 3 дня назад

    Wavala mzimuwamji mwanau

  • @GetrudeGama-gu5rb
    @GetrudeGama-gu5rb 3 дня назад +1

    Zowonadi ziribwino kwaiwo kwantha kwatsara kwaife

  • @user-wz1jy3uj8p
    @user-wz1jy3uj8p 3 дня назад

    ❤❤❤❤❤❤

  • @Tryness-wb6dj
    @Tryness-wb6dj 3 дня назад

    Rest well Bishop Kapenga

  • @JosephJosab
    @JosephJosab 3 дня назад

    Ku show kapena maliro

  • @eltonnankhwere3284
    @eltonnankhwere3284 3 дня назад

    Of course am satisfied with the speech it seems unakonzeka ngati ukupita
    ku show.i remember you wrote kuti tiyeni mawa tikakumane pa Robins Park ndikaimba nyimbo in other way its not fitting

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm 3 дня назад

    Mwana wamuna azikhara olimba mtima choncho waxy mbiri yako yabwno umakhara bwno ndi bambo ako ambuye akuze malire amoyo wako ndi abale ako😢

  • @AneesaMoosa-nv6bq
    @AneesaMoosa-nv6bq 3 дня назад

    Rest in peace bishop kapenga

  • @mikemakamo7360
    @mikemakamo7360 3 дня назад

    Koma mwana wakondwelatu 😂😂😂
    Zotindipamalilo wayiwala yoh mphamvu ziko likulowa bola

  • @SinyoroMoyo
    @SinyoroMoyo 3 дня назад

    Chitsiru chamwana ,nde chojowera-jowera ndichani .ngati zili bwino osangoyankhula bwino bwino kupereka ulemu kwa anthu ena bwanji.kufuna kutchuka ndi uchitsiru udzazindikira bwino patsogolo

  • @CatherineKumwendaCatherine
    @CatherineKumwendaCatherine 3 дня назад

    Kwa munthu oti amaziwa za kumwamba mwana wayakhura zomwe Mulungu amatilimbikisa pamavuto or pa Mtender tiziti zili bwno

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa 3 дня назад

    Sitinazolowele spech ngati izi kuno kwathu

  • @maxyfreeman9691
    @maxyfreeman9691 2 дня назад

    Kaya mwanayu sanasute koma

  • @MalawiSangano
    @MalawiSangano 2 дня назад

    Mau abwino kwa munthu olungam

  • @HussainGaffarOlaiza-hy9sg
    @HussainGaffarOlaiza-hy9sg 3 дня назад

    💔🕊

  • @rabeccadytone8772
    @rabeccadytone8772 3 дня назад

    Wakhutu la uximu wanva

  • @user-jn2oc3cn3q
    @user-jn2oc3cn3q 3 дня назад

    Km ine kaya ndi chimodzichi km speech yi sinandivekere mwaumunthu

  • @marryrobert7092
    @marryrobert7092 3 дня назад

    A malawi uziwa kurangiza mwana warakwa chani kod simuziwa kuti muthu akafa sibwino kurira mokweza ndemumatu iyi azirira

  • @FranckieDambah
    @FranckieDambah 3 дня назад

    Eeeeee waxy umatha kuyankhura

  • @billykamwendo6517
    @billykamwendo6517 3 дня назад +1

    Ife ndi a Malawi, izi nzachizungu ndipo naaa ine sindingayankhule chonchi ali oti ndi bambo anga.

    • @TadalaChithope-yg9fo
      @TadalaChithope-yg9fo 3 дня назад

      Azibambo nthawi zambili amakhala olimba mtim and uyuso panja mean oyamba ayenela kukhala strong komas tiyamike kut bambo ake amwalila waxy atatembenuka mtima komas kwaimayife zovuta kom kwa mamun ngt uyu akudziwa chomwe akuchita komas mwa okhulipilila izi zosavuta ngt munawon live yadzulo mayi ake okhala akaz awo anayimba nyimbo xa phamvuso coz ndi anthu okhulupilila and akudziwa kut akuyakhula mulungu wawo

  • @BestMtawali
    @BestMtawali 3 дня назад

    Ndalama unadya zacosoma zja nyimbo zake ndizit unaimba?????😩😩😩😩

  • @TadalaChithope-yg9fo
    @TadalaChithope-yg9fo 3 дня назад

    😭

  • @daziana2023
    @daziana2023 3 дня назад

    Zilibwino

  • @MarthaMfulusa-vj3xe
    @MarthaMfulusa-vj3xe 2 дня назад

    Strange

  • @DJcliffBandakhudzanga
    @DJcliffBandakhudzanga 3 дня назад

    Waxy ndi nfana olimba mwana wamamuna adzitelo

  • @YellowmanExen-nw1hy
    @YellowmanExen-nw1hy 15 часов назад

    I think this man waxy mutu wako sumakoka,ngati chili chamba mmmm.are sure bambo ako apita you can say this nonsense sure?

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 3 дня назад +1

    Iyi ndi lmfa osapanga zibwana kawonesa picture yanji kwa azukulu amipingo pamwambo wamaliro kakuti sharp wachani zachamba

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 3 дня назад

    Muzidyatu bwino ganjayo

  • @EmmanuelNgamuti
    @EmmanuelNgamuti 3 дня назад

    Young man where hv u taken the energy to make this non African speech on a day like this?

  • @DavieChangoima
    @DavieChangoima 3 дня назад

    Sorry rnp

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 3 дня назад +1

    Guys mwanai watani kodi
    Paribe muthu amasangalala pa ifa ai .
    Uyu wandikaikisa chabwino R.I.P pastor kapenga

    • @HannahChingwalu
      @HannahChingwalu 3 дня назад +1

      Chakaikitsa pamenepo ndichani?? Akuyenera kutero kumene chifukwaso zili mmalemba Mulungu ananena kuti kwaikika kwamunthu kufa,,chamoyo chilichonse chikuyembekeza imfa Ambuye alemekezeke chifukwa wakwanilitsa mau ake,,osati zanuzo apa

  • @SamsonChiwera
    @SamsonChiwera 3 дня назад

    Mmmm waxy Kay Kuno ndi kumalawi ndye yaaa kumbali Ina it's ok kuti zilibwino koma another side this speech is useless to me when you grow up that's when you will realize that l made silly speech RIP Mr kapenga

  • @Ampambachulu
    @Ampambachulu 3 дня назад

    Bro thought he killed

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 3 дня назад

    Waxy akanakhala ngati chija chinthubidwa cha chilima chija akanag'alura

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o 3 дня назад

    Kuyankhula kotani uku, mwana wachibwana

  • @BlessingsMangwaya-mk4fi
    @BlessingsMangwaya-mk4fi 3 дня назад +9

    This is not a fitting speech for the day your father passed away 😪😪

    • @lindamyaba
      @lindamyaba 3 дня назад

      Be serious man, waxy mwaonetsa maturity, zili bwino

    • @inessmsiyambiri8517
      @inessmsiyambiri8517 3 дня назад

      Sonotu anthu odziwa mawu zimaaiyana ndi osadziwa mau zili bwino basi ambuye walora

  • @Melinavituhs-tc8ys
    @Melinavituhs-tc8ys 3 дня назад

    Komatu for sure now irealize rhst crying during someone's daeth is for us poor imagine what is this speech 😭😭😭😭😭💔💔end with sure
    Anyway rest well pastor kapenga