What we knows is Mnzeru salowera chokolo, chilima never compared with Usi chilima was gentleman man of God and a humbleman so the leadership of Chilima is from God
Mr Usi ,sadalakwise kuvomera , tisayiwale Kuti MULUNGU ANAMUTSIMIKIZILA DAVIDE,KUTI MWANA WAKO SALMON NDI AMENE ADZANDIMANGIRE INE NYUMBA .So let's wait and see ,CHILIMA was fire fire fire ,but let's wait and seee
Usi chiyengo uyu inu i 15:50 think think usi he knew something or angomuphimba ndipos sangamulemekeze ngati zikhale ng'oma samalemekeza chilima who are you
Micheal USI ndi wa MCP kale chifukwa iye samapezeka ku misonkhano ya UTM koma chenjerani akuphanso ukuonena kale kuti MCP samafuna kuwadzudula akamachita zoyipa akungokhalila Kumanga anthu popanda chifukwa MCP ndi chipani cha nkhaza zazwika chakwera amadana ndi chilima mpaka kuphedwa chifukwa amafuna kuyimilila pulezident mu 2025 lero Wafa nawenso chenjerani USi.
From Cape town Brian Banda and your team we know that you hv bn captured by MCP your are not the same as u were b4 When money talks chilungamo chimakhala mtulo
Bryan ngt a USI avale sapato za malemu chilima nde kt 2025 azayimila ngt president WA tonse kapena sazakwanisa kutelo komaso ngt a MCP asanga a amanganya azapasa pata osogora mu 2025 ngt mwapangano mu 2020 ?
Congratulations Dr Michael Usi
Bull shit
Wabakili muluzi ujah ndikatakwe amaona muthu for one time kudziwaso atuuza zambrii mawa bass
What ever wabakili uja akamalankula zoona
Manganya congratulations ask God for more wisdom ❤
Amanganya tamango kupangani zamasewelo osati zandale mufelapo chakwela ndiwakupha
Very good analysis times
Chilima was vibrant koma he was pinned down until he was quite. Ussi can be above Chakwera?? Let's wait and see the motive.
Tiwafunile zabwino zonse a Dr Usi ngati wachiwiri kwamtsogoleri wadziko lino ❤
Congratulations that's wise decision chakwela
Congratulations usi, thanks Chakwera ndakukonda kwambiri
Congratulation bwana usi
Ndimafuna mundifusile achakwera Kut ngat Malawi yonse osawavot era adzakhala owinabe ngat adzakhale owin😂abe ma vote adzachokera Kut chabwino achewa onse takupatsan ndiomwe amakudan omwe atengen kod tima vote taachewa tokha tingakuwinitsen? Inutu mpando wanon non muchosedwapo
inabwera kuzakhalatu mcp.
Ndiwawo kale ndipo usi ananena kale kuti Ali m'mimba mwa apule palibe kulemekeza apa
The guy is white shirt thinks he is smarter than others. Brian is the king bro.
Keep your useless analysis with yourself, don't create competition and sow divisions where it is not needed, you must be a fool.
What we knows is Mnzeru salowera chokolo, chilima never compared with Usi chilima was gentleman man of God and a humbleman so the leadership of Chilima is from God
buh chilima sangasankhe kape more over usi amapemphelaso kwambiri
Ngati nkufuna ndarama zanu akuru coz mukufa moyo sagura MCP imeneyo inu ndi madzi amodzakare chirimatu adari doro muripati inu
Eya zoonadi pachoka mnzako pali malo, koma izinso Michael Usi hmm ayi mwaonjeza.
Usi has not come to fill in the shoes of Chilima but the shoes of the vice president. Let Usi be his own man
Obanda auze kuti Tinali ndi Magufuli ku Tanzania chisazo champhavu
Congratulations Dr Michael Usi
Congratulations Dr M B ussi the people are behind you
Chigawenga china icho
Ussi not suitable may be politically but as VP or a leader no. Such position needs people with high integrity and caliber.
But Chilima choosed Usi as his vice 2019 ija. Which means Chilima akadawina nthawi imene ija Usi akanakhalabe vice tu.
@@PraiseKadzitcheeeeh nzoona
Congratulations Dr Michael Ussi, May our heavenly Father guide you
Pass my regards to Ndebvu zamwayi
Bamboo asikono😂😂😂😂😂😂😂
All the best my favourite actor
Nkhan yabwino Mr Michael Usi
Mr Usi ,sadalakwise kuvomera , tisayiwale Kuti MULUNGU ANAMUTSIMIKIZILA DAVIDE,KUTI MWANA WAKO SALMON NDI AMENE ADZANDIMANGIRE INE NYUMBA .So let's wait and see ,CHILIMA was fire fire fire ,but let's wait and seee
Usi chiyengo uyu inu i 15:50 think think usi he knew something or angomuphimba ndipos sangamulemekeze ngati zikhale ng'oma samalemekeza chilima who are you
That's an excellent move by MCP. You are playing your Cards very well. It might pay off. Bravo.
It will never pay off
34:23 abambo asikono now Vice president republic of Malawi
Times Radio muli uphungu wabwino. DR. USSI, these men are guiding you in a friendly way. Congregations Dr. Ussi.
Micheal USI ndi wa MCP kale chifukwa iye samapezeka ku misonkhano ya UTM koma chenjerani akuphanso ukuonena kale kuti MCP samafuna kuwadzudula akamachita zoyipa akungokhalila Kumanga anthu popanda chifukwa MCP ndi chipani cha nkhaza zazwika chakwera amadana ndi chilima mpaka kuphedwa chifukwa amafuna kuyimilila pulezident mu 2025 lero Wafa nawenso chenjerani USi.
According to the agrement signed by the two officers on the one to be the 2025 presidential candidate for the Tonse Alliance. Will Ussi be the one
We are not serious Michael Usi got that position just to cover the mess.
From Cape town Brian Banda and your team we know that you hv bn captured by MCP your are not the same as u were b4
When money talks chilungamo chimakhala mtulo
Bryan ngt a USI avale sapato za malemu chilima nde kt 2025 azayimila ngt president WA tonse kapena sazakwanisa kutelo komaso ngt a MCP asanga a amanganya azapasa pata osogora mu 2025 ngt mwapangano mu 2020 ?
Michael ussi I'm happy to be a follower I am happy to be a follower of kindness. But open your eyes to the dunes. Open your eyes my sun
Avise Pule,tiwona kuti mupanga support yotaní ma artist anzanu ,woyimba ,azitsunzo, wosewera mpira yonse . Awoneni anthuwa kuwapatsanso support
Ngat m tengo wawisi wakorela kulibwaji uyu? Nakhan chomwe chamuchosa achilima motelom kusogoloko kulibe? Mmm guys chat chubi sichinaolok
Dyera limupha
“Inutu Paja mumakonda ku Phuluza mawu” 😂😂🤣🤣
Brian ndikukuwuza kuti usi siwa utm and nthawiyomwechilima amapanga ma pres briefing usi amangokhala chete ndikuwonangati munthuyo ndiwa mcp
Kodi andalewa ngati amakonda dziko bwanji safuna kudula malipiro awo komanso kumagwilitsa ntchito galimoto zotchepa kuti azikwanutsa kupanga chitukuko chadziko kuposa kumazisangalatsa okha
Komanso kumagulitsa companys aboma zomwe ndalama mzake boma sitinamve kuti zinapanga chiani? Nanga aja anatenga ngongole zaboma azabweza litilo? Ndiye mr usi ntchito yomwe akufunika kuchita
Andevu zamwai osamakonda kuperela zitsanzo za ku ntchito Kwanu , zikumatipatsa ma picture osakhala bwino amene mumakhalila ku times ko 😢😢
Congratulations Dr Usi keep it up, thanks Mr President we still love you our President
Zabhobho
Am Happy God guide you vp.All members of utm Loves u
Mmmmmmkkkkkk
Onesani zisudzozanu Amanganya😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😢❤😊😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅
Kodi akanyama chiuma adasowa bwanji?😅😅😅 bakili tv tikatundu, mungotaya nthawi ndi chakwela wanu.
Ina nadabwa Ausi kudekha
Koma zilikotu ife pheee pawindo kudikira amanga akusintha zinthu 😂😂😂
More fire Mr Usi VP of our country Malawi
Aluka kontinua
Bola asafeso
Aitu anapha nawo chilima
Congratulations bambo asikono😂😂😂
bwana presendent mwasankha bwino kwambili mulungu akudaliseni❤
Zofoila😮😮😢
Bola asakhale chikwangwani potseka mkwiyo wa anthu a Utm pa imfa yowawa ya Chirima.
Chakwera only appoints the chewa's that's not fair
Aliyense ndi Doctor kumalawi or opanda zoyenerela
Ndi dzachi bwana dzomwe dzachitikadzo
Chakwera simungamuthe..he is very intelligent
Zose zimachitikazija amadziwana kuti pakubwela usi
A comedian man having that postion like seriously ? 😢
Boss you only know manganya not Michael usi
Wayankhula ndikupeleka chitsanzo Brayan
Make sikono Kuli iwe KO ukumva bwanji😂😂😂😂
Zabwino zonse
Okay chabwin
Zabhobho
Zabwinozonse Dr Usi.
Chalaka Bakha, Nkhuku singatole ayi.
Anyway congratulations to Dr Usi BUT things will never be the same.
There was one Chilima.
Osayiwalatu Make a sikono akhaleso pambalipo 🎉
😂😂😂😂
Make sikono waiphula basi apa kkkkkkkkk mwina sikono uja atulukila tsopano kkkkkk
😂😂 ati paja Inu mmakonda kuphuluza mawu hahaha
Happyfor Usi
Enafe zotukwanazo sitipanganawo.ndi mmene zimakhalila ndithu for replacement imafunika.congradulation
Dr .usi.
Congratulations Dr Ussi
Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.
Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.
Bakili muluzi tv akulu ndikatundu amafufuza
Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.
Eeeh 🤔
Congratulations mr usi
Ndipo malango ali apa akanati ma leader's amavetsela ndi kuwagwilitsa ntchito bwezi zinthu zikuyenda bwino
Congratulations to Mr usi
The problem is chakwela mulibe leader ship .... sizingatheke kukonza chilichonse
VERY CONGRATULATIONS DR MICHAEL BIZIWICK USI, YOU ARE A MAN AMONG MEN.........GOD BLESS YOU.....
A mtanyiwa mwagwatu apa avoid talking
Congregation mr usi tikufunilani kugwila ntchito yabwino nda president amr chakwera
Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.
Muthu yemwe satenga mbali ochenjeranso kwambili ndi Brian
Vp osatsuka nkamwa eti inu zithu zake
Congraturations Dr micheal usi the manganya ur the best geri kuchita kuposa wakusankhayo
Ausi mupange zaziko osati za chipani kapena zachakwela ayi uwu ndimwai omwe wafika munthawi yobvuta pa ndale pa tchuma
Obviously wish him all the best
I wish Mr Manganya Dr usi the best time in office may The Lord bless you with wisdom tolead Malawi to great heights
Live MBC malawi
Malamulo adziko lamalawi amapereka mphamvu kwa president kuti atero ndiye don't blame him
Congratulation times you inspire us very good and powerful counseling indeed we are hopping a lot from our new VP
Congrats Mr Usi. I know we lost a great leader but we need to move on. Mr President, we are behind you.
Good
😊😊
Manganya zamaliro szmankhuza uja chidwi chake chinali cha vp mfiti
Tili kumastandi ife😢
Nonse ndinu a mcp chokan apa