BREAKING NEWS-MICHAEL USSI IS NOW a new MALAWI'S vice president replacing SKC MAGANIZO ANU NDIOTANI?

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 1 окт 2024

Комментарии • 188

  • @thomaskalima7379
    @thomaskalima7379 3 месяца назад +20

    Congratulations Dr Michael Usi

  • @Jayleezbond
    @Jayleezbond 3 месяца назад +14

    Wabakili muluzi ujah ndikatakwe amaona muthu for one time kudziwaso atuuza zambrii mawa bass

    • @yotamrealboth3058
      @yotamrealboth3058 3 месяца назад

      What ever wabakili uja akamalankula zoona

    • @yotamrealboth3058
      @yotamrealboth3058 3 месяца назад

      Manganya congratulations ask God for more wisdom ❤

  • @OwenTembo-xq6ug
    @OwenTembo-xq6ug 3 месяца назад +15

    Amanganya tamango kupangani zamasewelo osati zandale mufelapo chakwela ndiwakupha

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 3 месяца назад +5

    Chilima was vibrant koma he was pinned down until he was quite. Ussi can be above Chakwera?? Let's wait and see the motive.

  • @isaacbwanali4699
    @isaacbwanali4699 3 месяца назад +5

    Tiwafunile zabwino zonse a Dr Usi ngati wachiwiri kwamtsogoleri wadziko lino ❤

    • @StanleyChinsewu
      @StanleyChinsewu 3 месяца назад

      Congratulations that's wise decision chakwela

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад +7

    Congratulations usi, thanks Chakwera ndakukonda kwambiri

  • @LamieTiger-ff7cj
    @LamieTiger-ff7cj 3 месяца назад +5

    Ndimafuna mundifusile achakwera Kut ngat Malawi yonse osawavot era adzakhala owinabe ngat adzakhale owin😂abe ma vote adzachokera Kut chabwino achewa onse takupatsan ndiomwe amakudan omwe atengen kod tima vote taachewa tokha tingakuwinitsen? Inutu mpando wanon non muchosedwapo

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3di 3 месяца назад +3

    Ndiwawo kale ndipo usi ananena kale kuti Ali m'mimba mwa apule palibe kulemekeza apa

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 3 месяца назад +3

    The guy is white shirt thinks he is smarter than others. Brian is the king bro.

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 3 месяца назад

      Keep your useless analysis with yourself, don't create competition and sow divisions where it is not needed, you must be a fool.

  • @ChikumbutsoJohn-rs4tt
    @ChikumbutsoJohn-rs4tt 3 месяца назад +4

    What we knows is Mnzeru salowera chokolo, chilima never compared with Usi chilima was gentleman man of God and a humbleman so the leadership of Chilima is from God

    • @SamiahNyaulanda
      @SamiahNyaulanda 3 месяца назад

      buh chilima sangasankhe kape more over usi amapemphelaso kwambiri

  • @RivinessiRivinessierick
    @RivinessiRivinessierick 3 месяца назад +2

    Ngati nkufuna ndarama zanu akuru coz mukufa moyo sagura MCP imeneyo inu ndi madzi amodzakare chirimatu adari doro muripati inu

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 3 месяца назад +2

    Eya zoonadi pachoka mnzako pali malo, koma izinso Michael Usi hmm ayi mwaonjeza.

  • @domminicchikalenda
    @domminicchikalenda 3 месяца назад +2

    Usi has not come to fill in the shoes of Chilima but the shoes of the vice president. Let Usi be his own man

  • @ChfKhosolo
    @ChfKhosolo 3 месяца назад +2

    Obanda auze kuti Tinali ndi Magufuli ku Tanzania chisazo champhavu

  • @ChikondiMasina-s8e
    @ChikondiMasina-s8e 3 месяца назад +1

    Congratulations Dr Michael Usi

  • @geofreydzinyemba6107
    @geofreydzinyemba6107 3 месяца назад +3

    Congratulations Dr M B ussi the people are behind you

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe 3 месяца назад +3

    Chigawenga china icho

  • @YoungMwacho
    @YoungMwacho 3 месяца назад +2

    Ussi not suitable may be politically but as VP or a leader no. Such position needs people with high integrity and caliber.

    • @PraiseKadzitche
      @PraiseKadzitche 3 месяца назад

      But Chilima choosed Usi as his vice 2019 ija. Which means Chilima akadawina nthawi imene ija Usi akanakhalabe vice tu.

    • @LeendaDeborah2005
      @LeendaDeborah2005 3 месяца назад

      @@PraiseKadzitcheeeeh nzoona

  • @FannieJubeck
    @FannieJubeck 3 месяца назад +2

    Congratulations Dr Michael Ussi, May our heavenly Father guide you

  • @tonythengo9294
    @tonythengo9294 3 месяца назад +2

    Pass my regards to Ndebvu zamwayi

  • @AishaChipande
    @AishaChipande 3 месяца назад +3

    Bamboo asikono😂😂😂😂😂😂😂

  • @yosxmw
    @yosxmw 3 месяца назад +3

    All the best my favourite actor

  • @Lesterkaundah
    @Lesterkaundah 3 месяца назад +3

    Nkhan yabwino Mr Michael Usi

  • @ElizahMadi
    @ElizahMadi 3 месяца назад

    Mr Usi ,sadalakwise kuvomera , tisayiwale Kuti MULUNGU ANAMUTSIMIKIZILA DAVIDE,KUTI MWANA WAKO SALMON NDI AMENE ADZANDIMANGIRE INE NYUMBA .So let's wait and see ,CHILIMA was fire fire fire ,but let's wait and seee

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 3 месяца назад +1

    Usi chiyengo uyu inu i 15:50 think think usi he knew something or angomuphimba ndipos sangamulemekeze ngati zikhale ng'oma samalemekeza chilima who are you

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 3 месяца назад +2

    That's an excellent move by MCP. You are playing your Cards very well. It might pay off. Bravo.

  • @SurprisedDriftwood-ef3lc
    @SurprisedDriftwood-ef3lc 3 месяца назад +1

    34:23 abambo asikono now Vice president republic of Malawi

  • @nedsonbanda8108
    @nedsonbanda8108 3 месяца назад +1

    Times Radio muli uphungu wabwino. DR. USSI, these men are guiding you in a friendly way. Congregations Dr. Ussi.

  • @LuciusMowa
    @LuciusMowa 3 месяца назад

    Micheal USI ndi wa MCP kale chifukwa iye samapezeka ku misonkhano ya UTM koma chenjerani akuphanso ukuonena kale kuti MCP samafuna kuwadzudula akamachita zoyipa akungokhalila Kumanga anthu popanda chifukwa MCP ndi chipani cha nkhaza zazwika chakwera amadana ndi chilima mpaka kuphedwa chifukwa amafuna kuyimilila pulezident mu 2025 lero Wafa nawenso chenjerani USi.

  • @FredrickBashir
    @FredrickBashir 3 месяца назад

    According to the agrement signed by the two officers on the one to be the 2025 presidential candidate for the Tonse Alliance. Will Ussi be the one

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 3 месяца назад +6

    We are not serious Michael Usi got that position just to cover the mess.

  • @FosterChilumba
    @FosterChilumba 3 месяца назад

    From Cape town Brian Banda and your team we know that you hv bn captured by MCP your are not the same as u were b4
    When money talks chilungamo chimakhala mtulo

  • @AyouMafuken
    @AyouMafuken 3 месяца назад

    Bryan ngt a USI avale sapato za malemu chilima nde kt 2025 azayimila ngt president WA tonse kapena sazakwanisa kutelo komaso ngt a MCP asanga a amanganya azapasa pata osogora mu 2025 ngt mwapangano mu 2020 ?

  • @HarrisoncharlesMbweza
    @HarrisoncharlesMbweza 3 месяца назад

    Michael ussi I'm happy to be a follower I am happy to be a follower of kindness. But open your eyes to the dunes. Open your eyes my sun

  • @ElizahMadi
    @ElizahMadi 3 месяца назад

    Avise Pule,tiwona kuti mupanga support yotaní ma artist anzanu ,woyimba ,azitsunzo, wosewera mpira yonse . Awoneni anthuwa kuwapatsanso support

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 3 месяца назад +1

    Ngat m tengo wawisi wakorela kulibwaji uyu? Nakhan chomwe chamuchosa achilima motelom kusogoloko kulibe? Mmm guys chat chubi sichinaolok

  • @lumbanimsiska8952
    @lumbanimsiska8952 3 месяца назад +2

    “Inutu Paja mumakonda ku Phuluza mawu” 😂😂🤣🤣

  • @NovemberMmangathayo
    @NovemberMmangathayo 3 месяца назад

    Brian ndikukuwuza kuti usi siwa utm and nthawiyomwechilima amapanga ma pres briefing usi amangokhala chete ndikuwonangati munthuyo ndiwa mcp

  • @peter..nyirenda4780
    @peter..nyirenda4780 3 месяца назад

    Kodi andalewa ngati amakonda dziko bwanji safuna kudula malipiro awo komanso kumagwilitsa ntchito galimoto zotchepa kuti azikwanutsa kupanga chitukuko chadziko kuposa kumazisangalatsa okha
    Komanso kumagulitsa companys aboma zomwe ndalama mzake boma sitinamve kuti zinapanga chiani? Nanga aja anatenga ngongole zaboma azabweza litilo? Ndiye mr usi ntchito yomwe akufunika kuchita

  • @SailotaSamuel
    @SailotaSamuel 3 месяца назад

    Andevu zamwai osamakonda kuperela zitsanzo za ku ntchito Kwanu , zikumatipatsa ma picture osakhala bwino amene mumakhalila ku times ko 😢😢

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh 3 месяца назад

    Congratulations Dr Usi keep it up, thanks Mr President we still love you our President

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 3 месяца назад +2

    Zabhobho

  • @GivenKitha
    @GivenKitha 3 месяца назад +2

    Am Happy God guide you vp.All members of utm Loves u

  • @tiwongehojaney5873
    @tiwongehojaney5873 3 месяца назад

    Onesani zisudzozanu Amanganya😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😢❤😊😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅😅

  • @InnocentMlowoka-ew4lo
    @InnocentMlowoka-ew4lo 3 месяца назад

    Kodi akanyama chiuma adasowa bwanji?😅😅😅 bakili tv tikatundu, mungotaya nthawi ndi chakwela wanu.

  • @NoreenNaituri
    @NoreenNaituri 3 месяца назад +1

    Ina nadabwa Ausi kudekha

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 3 месяца назад

    Koma zilikotu ife pheee pawindo kudikira amanga akusintha zinthu 😂😂😂

  • @MaideLester
    @MaideLester 3 месяца назад

    More fire Mr Usi VP of our country Malawi

  • @LouisKamanga-zb2ok
    @LouisKamanga-zb2ok 3 месяца назад +2

    Aluka kontinua

  • @MikeGama-j6j
    @MikeGama-j6j 3 месяца назад +2

    Bola asafeso

  • @LUCIUSChamwamba
    @LUCIUSChamwamba 3 месяца назад +1

    Congratulations bambo asikono😂😂😂

  • @fedsonjossam-fj8ri
    @fedsonjossam-fj8ri 3 месяца назад

    bwana presendent mwasankha bwino kwambili mulungu akudaliseni❤

  • @YusufuAnafi-e6v
    @YusufuAnafi-e6v 3 месяца назад +1

    Zofoila😮😮😢

  • @LemosBanda
    @LemosBanda 3 месяца назад

    Bola asakhale chikwangwani potseka mkwiyo wa anthu a Utm pa imfa yowawa ya Chirima.

  • @ElonBlack1999
    @ElonBlack1999 3 месяца назад

    Chakwera only appoints the chewa's that's not fair

  • @OsmanMsini-xo1wh
    @OsmanMsini-xo1wh 3 месяца назад

    Aliyense ndi Doctor kumalawi or opanda zoyenerela

  • @MalvenDzonga-x7h
    @MalvenDzonga-x7h 3 месяца назад +1

    Ndi dzachi bwana dzomwe dzachitikadzo

  • @ststephanosecschl4151
    @ststephanosecschl4151 3 месяца назад

    Chakwera simungamuthe..he is very intelligent

  • @NovemberMmangathayo
    @NovemberMmangathayo 3 месяца назад

    Zose zimachitikazija amadziwana kuti pakubwela usi

  • @OmarManjawira-up3ns
    @OmarManjawira-up3ns 3 месяца назад +1

    A comedian man having that postion like seriously ? 😢

    • @Maxwell-e2d
      @Maxwell-e2d 3 месяца назад +1

      Boss you only know manganya not Michael usi

  • @BittonRashid
    @BittonRashid 3 месяца назад

    Wayankhula ndikupeleka chitsanzo Brayan

  • @ElizahMadi
    @ElizahMadi 3 месяца назад

    Make sikono Kuli iwe KO ukumva bwanji😂😂😂😂

  • @ChisomoBisani
    @ChisomoBisani 3 месяца назад +1

    Zabwino zonse

  • @GiftRichard-b1o
    @GiftRichard-b1o 3 месяца назад +1

    Okay chabwin

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 3 месяца назад +1

    Zabhobho

  • @CosmasChikwindi
    @CosmasChikwindi 3 месяца назад +1

    Zabwinozonse Dr Usi.

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 3 месяца назад

    Chalaka Bakha, Nkhuku singatole ayi.
    Anyway congratulations to Dr Usi BUT things will never be the same.
    There was one Chilima.

  • @MacdonaldJosephMbewe
    @MacdonaldJosephMbewe 3 месяца назад +2

    Osayiwalatu Make a sikono akhaleso pambalipo 🎉

    • @Dorah-zl9uf
      @Dorah-zl9uf 3 месяца назад

      😂😂😂😂

    • @gladyschisomo4324
      @gladyschisomo4324 3 месяца назад

      Make sikono waiphula basi apa kkkkkkkkk mwina sikono uja atulukila tsopano kkkkkk

  • @LimbaniMunthali-r3o
    @LimbaniMunthali-r3o 3 месяца назад

    😂😂 ati paja Inu mmakonda kuphuluza mawu hahaha

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica 3 месяца назад +1

    Happyfor Usi

  • @jomochirwa
    @jomochirwa 3 месяца назад

    Enafe zotukwanazo sitipanganawo.ndi mmene zimakhalila ndithu for replacement imafunika.congradulation
    Dr .usi.

  • @esthelbanda782
    @esthelbanda782 3 месяца назад

    Congratulations Dr Ussi

  • @CharlesBanda-t9j
    @CharlesBanda-t9j 3 месяца назад

    Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.

  • @CharlesBanda-t9j
    @CharlesBanda-t9j 3 месяца назад

    Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.

  • @NovemberMmangathayo
    @NovemberMmangathayo 3 месяца назад

    Bakili muluzi tv akulu ndikatundu amafufuza

  • @CharlesBanda-t9j
    @CharlesBanda-t9j 3 месяца назад

    Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 3 месяца назад +1

    Eeeh 🤔

  • @BenjaminMnyenyembe-zy5mi
    @BenjaminMnyenyembe-zy5mi 3 месяца назад

    Congratulations mr usi

  • @gladyschisomo4324
    @gladyschisomo4324 3 месяца назад

    Ndipo malango ali apa akanati ma leader's amavetsela ndi kuwagwilitsa ntchito bwezi zinthu zikuyenda bwino

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll 3 месяца назад

    Congratulations to Mr usi

  • @AustinChiyembekezo-cx4mz
    @AustinChiyembekezo-cx4mz 3 месяца назад

    The problem is chakwela mulibe leader ship .... sizingatheke kukonza chilichonse

  • @franciscomkozomba
    @franciscomkozomba 3 месяца назад

    VERY CONGRATULATIONS DR MICHAEL BIZIWICK USI, YOU ARE A MAN AMONG MEN.........GOD BLESS YOU.....

  • @JohnNyirenda-pj4fb
    @JohnNyirenda-pj4fb 3 месяца назад

    A mtanyiwa mwagwatu apa avoid talking

  • @JamesPhiri-g3o
    @JamesPhiri-g3o 3 месяца назад

    Congregation mr usi tikufunilani kugwila ntchito yabwino nda president amr chakwera

  • @CharlesBanda-t9j
    @CharlesBanda-t9j 3 месяца назад

    Mr president l salute you for choosing Dr Ussi to be our new vice president. God bless you, God bless Dr Ussi and God bless Malawi.

  • @LamieTiger-ff7cj
    @LamieTiger-ff7cj 3 месяца назад +3

    Muthu yemwe satenga mbali ochenjeranso kwambili ndi Brian

  • @ELIDAMISOMALI
    @ELIDAMISOMALI 3 месяца назад

    Vp osatsuka nkamwa eti inu zithu zake

  • @TryceMagombo-sh7kb
    @TryceMagombo-sh7kb 3 месяца назад

    Congraturations Dr micheal usi the manganya ur the best geri kuchita kuposa wakusankhayo

  • @EmanuelMuotcha
    @EmanuelMuotcha 3 месяца назад

    Ausi mupange zaziko osati za chipani kapena zachakwela ayi uwu ndimwai omwe wafika munthawi yobvuta pa ndale pa tchuma

  • @MCAnthonyNdau
    @MCAnthonyNdau 3 месяца назад +1

    Obviously wish him all the best

  • @jollylunda4034
    @jollylunda4034 3 месяца назад

    I wish Mr Manganya Dr usi the best time in office may The Lord bless you with wisdom tolead Malawi to great heights

  • @mabetikadzuwa9445
    @mabetikadzuwa9445 3 месяца назад

    Live MBC malawi

  • @CardoJustin
    @CardoJustin 3 месяца назад

    Malamulo adziko lamalawi amapereka mphamvu kwa president kuti atero ndiye don't blame him

  • @NedMoyo
    @NedMoyo 3 месяца назад

    Congratulation times you inspire us very good and powerful counseling indeed we are hopping a lot from our new VP

  • @MeahKamanga-qy4ut
    @MeahKamanga-qy4ut 3 месяца назад

    Congrats Mr Usi. I know we lost a great leader but we need to move on. Mr President, we are behind you.

  • @BintonDzuwa-d3p
    @BintonDzuwa-d3p 3 месяца назад +1

    Good

  • @ELIDAMISOMALI
    @ELIDAMISOMALI 3 месяца назад

    😊😊

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 3 месяца назад

    Manganya zamaliro szmankhuza uja chidwi chake chinali cha vp mfiti

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 3 месяца назад

    Tili kumastandi ife😢

  • @mustafanaminga
    @mustafanaminga 3 месяца назад

    Nonse ndinu a mcp chokan apa